BASITU NKHANI IJA YANG’ALULIDWA PA TIMES PAMENE AMAWERENGA NKHANI ZOMWE ZACHITIKA LERO KWACHEMA

  Рет қаралды 31,993

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 97
@JohnfosterNkusengwa
@JohnfosterNkusengwa 36 минут бұрын
Good and l hope everything it will be fine Jfk all the way from cape Town pa boma ❤❤
@JohnJohn-og8rt
@JohnJohn-og8rt 4 сағат бұрын
Is good nice now Zikom mulungu asikudalisapo chakwera achoke 2025
@PatrickTimothyh
@PatrickTimothyh Сағат бұрын
Free Malawi, free Malawians. Freedom thou art a foot....
@EsetaGerate
@EsetaGerate 2 сағат бұрын
💃💃💃wanyera chikangawa kkkkkkk umati ungatani machende ako
@abgi.doctor.august
@abgi.doctor.august 2 сағат бұрын
Ili ndi dziko la Mulungu zikomo Ambuye ndinu Mokha mumakhala ndi mayankho anthu anu a Malawi ❤❤❤
@MariamAlabi-t3n
@MariamAlabi-t3n 3 сағат бұрын
Democracy woyeee Mizimu ya anthu 9 aja uwuse mumtendere not forgetting Ralph Kasambala ,chonde timenyereni nkondo ,
@MjombaMoosa
@MjombaMoosa 3 сағат бұрын
Amen nthawi ija yakwana yochoka pa pando Mr chikangawa wagwa nayo keasala nkumapita ku Court every week ya 2025 nyiiii
@PeacefulBackpacker-mn2gi
@PeacefulBackpacker-mn2gi 2 сағат бұрын
Chakwela ndi mbuzi yopanda zelu
@MfipaKapwera
@MfipaKapwera 4 сағат бұрын
Very good every body must register inorder to exercise his or her to vote.
@PatriciaChiwerenga
@PatriciaChiwerenga 4 сағат бұрын
Hallelujah 🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🙏🙏🙏
@ThocoThawan
@ThocoThawan Сағат бұрын
Ambuye musatisiyire pomwepo
@MariusChiumya
@MariusChiumya Сағат бұрын
NRB isamakanamizireso net work kumalemba aliyense kuchoka apo kulembesa ku mec
@WysonAdamu
@WysonAdamu 2 сағат бұрын
Mulungu sichakwela kapene chimwendo ayi dzikoli ndilamuthu Wina aliye sidzimene amafuna makape enawa
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 34 минут бұрын
Ndipo chikangawa mmm ndigalu kwabasi
@JanaJovian
@JanaJovian 2 сағат бұрын
Mulungu mutiyankhe tilimuwulamulilo asatana mcp yikutizuza amalawi
@Alice-z7t4z
@Alice-z7t4z 3 сағат бұрын
Wagwa nayo Anabel izoooo usova 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@MakabaBauleni-c2i
@MakabaBauleni-c2i 2 сағат бұрын
Kma yesu ameneyu aaaaa watimenyera nkhondo ife tili chete
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 3 сағат бұрын
Kungopanga zoti ena azidziwe basi ❤❤❤
@CathleenMsaya
@CathleenMsaya 2 сағат бұрын
Osaopa amalawi dzikoli ndilathu
@DennisTobias-b4r
@DennisTobias-b4r 3 сағат бұрын
Khoti layamba kuopa lawyer uja kuti awaulula
@ChisomoChigaga
@ChisomoChigaga 3 сағат бұрын
😂😂😂😂
@benjaminjobo3525
@benjaminjobo3525 4 сағат бұрын
Amen kumwamba kuli mulungu
@MauriceMukona
@MauriceMukona 2 сағат бұрын
MCP yomwe ikulamula panoyi ndi yomwe ijayi ya ku Ghana ya kamuzu banda.Chakwerayu wangokhalapo ngati chukwangwani chabe.🐊🐊🐊🐊🤦🤦
@martinsailesi1731
@martinsailesi1731 2 сағат бұрын
Passports and driving licences belong to the government please.
@SifatiMoses
@SifatiMoses 4 сағат бұрын
Mayi Joyce banda amamupotsa chalakwe poganiza.
@gift-y4k
@gift-y4k 2 сағат бұрын
Chakwela wamisala akufuna kuyesa kapena Kuti kuphuzila kubela Ngati chilima komat sizitheka
@HarrisonMwanga-xy4sc
@HarrisonMwanga-xy4sc 4 сағат бұрын
Nkhani, yabwino kwa amalawi okonda ziko lawo salute
@ChristinaMdeza
@ChristinaMdeza 3 сағат бұрын
Amen mwatimenyele nkhondo ife tli chete chi satanacho chichite manyazi
@Alice-z7t4z
@Alice-z7t4z 3 сағат бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@jollyfriday1892
@jollyfriday1892 3 сағат бұрын
UTM vote yangaaaaaa
@GradinaNgalande
@GradinaNgalande 3 сағат бұрын
Chilima musagone mwachangu paka tizavote chifukwa tizasowa zimu wanu pathawi yovota chakwela mazi basi
@ADAMSONGONDWE
@ADAMSONGONDWE 3 сағат бұрын
Smartmatic isagwiritsidwe ntchito
@TiwongeChikhoza
@TiwongeChikhoza 3 сағат бұрын
Ndipo watsalanso nzimai uja mtali manja atule pasi usindo hule ameneyo
@RuthBeyala
@RuthBeyala 4 сағат бұрын
Ambuye musasiile pomwepa chonde tioneni ife ana anu
@PeterMorgen-k4b
@PeterMorgen-k4b 3 сағат бұрын
The smoldering charcal👐👐👐
@JustinLipipa
@JustinLipipa 3 сағат бұрын
Kodi ndingalipeze kuti Buku la smoldering Charcoal 😂😂😂, nchere, Bota aaaaa you just reminding me in those good old days
@PeterMorgen-k4b
@PeterMorgen-k4b 3 сағат бұрын
@@JustinLipipa Tafufuzani mma book-shop Blantyre ko
@MaryNgola
@MaryNgola 4 сағат бұрын
Aleluya
@violetkamfose6693
@violetkamfose6693 2 сағат бұрын
An assessment need to be done on condition known as dyslexia
@khasimMusa-d3w
@khasimMusa-d3w 3 сағат бұрын
Amen
@Kabwilachikangawa
@Kabwilachikangawa 4 сағат бұрын
MULUNGU SI JEMUSI!!!!!! KUMENYA KUGWETSA BASI
@ChisomoBanda-jo4ix
@ChisomoBanda-jo4ix 4 сағат бұрын
Murungu aremekezeke ndizo timafuna zimenez
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 2 сағат бұрын
😂😂😂😂mbuzi za amalawi..... How do you recognise the citizen without ID..... MCP inawina musavutike.... The entire mec is MCP family
@ClementMinyanga
@ClementMinyanga 4 сағат бұрын
Tikavota bas🤣
@HenryChiwaya-g4d
@HenryChiwaya-g4d 4 сағат бұрын
Zochitika kuno ku malawi ndingoti Dzuka MALAWI
@ShazidaAlfred
@ShazidaAlfred 3 сағат бұрын
Amen ambuye zikomo mwatiyakha pepho lanthu
@JasonMailos
@JasonMailos 3 сағат бұрын
❤❤❤❤yaah
@DennisTobias-b4r
@DennisTobias-b4r 3 сағат бұрын
Mcp ija pa ulendo basi ma plan anu aduka,
@InnocentChauwa
@InnocentChauwa 3 сағат бұрын
Ameen
@thomasmakata8861
@thomasmakata8861 4 сағат бұрын
Kumwamba kulandire ulemu
@elizasingano
@elizasingano 4 сағат бұрын
Nkhani kma imeneyo
@RaffickAllie
@RaffickAllie 3 сағат бұрын
Apa mudzi onse wakwathu tikavota basni kkkkk Moto kuti buuuui
@RaymondKaumba
@RaymondKaumba 3 сағат бұрын
Wagwa nayo.ndani Chiletso sichintheke
@CathleenMsaya
@CathleenMsaya 2 сағат бұрын
This woman has lost her senses Joyce
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 3 сағат бұрын
Atsogoleli athu simuchita manyadzi ponamiza anthu awo.
@HarryMwakimeme
@HarryMwakimeme 4 сағат бұрын
Zoona masten
@LeyvanSamuel-pe5tc
@LeyvanSamuel-pe5tc 3 сағат бұрын
Sono Za smartmatic zija zilipat guys 🤔
@JimmyAlfred-p1y
@JimmyAlfred-p1y 3 сағат бұрын
Ambuye tipatseni munthu ozatiimila 2025 popeza munthu tilibe
@JulietLizziePhiri
@JulietLizziePhiri 4 сағат бұрын
I can forsee the Rise and Fall of Eid Amin part 2, ahead 😅
@innobashirbernard7853
@innobashirbernard7853 3 сағат бұрын
Tipatseni ife chakudya chathu chalelo
@RichardChathyoka
@RichardChathyoka 3 сағат бұрын
Wina alila kkkk😂😂😂😂😂
@DanielJuwawo-s5n
@DanielJuwawo-s5n 3 сағат бұрын
Wina alira chaka chake nchino
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 3 сағат бұрын
Vuto ndi kaphunzisidwe sikali bwino.
@McshonWilliam
@McshonWilliam 4 сағат бұрын
on my way going to the shop kukagula mowa kut ndiufile y annabera amandipwetekesa mutu heve any question from joab chakhaza kumangot malamulo athu sakulora relo alikut 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@Alice-z7t4z
@Alice-z7t4z 3 сағат бұрын
Ali mmadzi ameneyo 😂😂😂😂😂😂
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin 3 сағат бұрын
❤❤
@MikeChitambe
@MikeChitambe 4 сағат бұрын
Tili komweko bas 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@MercyKutentha
@MercyKutentha 3 сағат бұрын
God and God alone😅😅😅
@RebeccaChikalenda
@RebeccaChikalenda 3 сағат бұрын
Ndubwera lne ndzarembetse lme
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 3 сағат бұрын
Kuyambila inuyo.
@chimwemwechikwawa
@chimwemwechikwawa 4 сағат бұрын
Hahahah izi ndazikonda, odi nkalembese ine
@HasheemSalade
@HasheemSalade 3 сағат бұрын
Ndazkonda zimenez
@KentWilliam-r2v
@KentWilliam-r2v 3 сағат бұрын
Pamenepa zili bwino kwambiri
@KassimJumah-s8b
@KassimJumah-s8b 3 сағат бұрын
Zopusa basi makape inu
@RajabAssan
@RajabAssan 3 сағат бұрын
Ndipo live
@RobertGoliat-gt2qh
@RobertGoliat-gt2qh 4 сағат бұрын
Apa ndye zilibwino tsopano
@kondwanimunthali7401
@kondwanimunthali7401 4 сағат бұрын
MEC chair finally defeated
@Kabwilachikangawa
@Kabwilachikangawa 4 сағат бұрын
CHITSIRU CHIJA CHI TONKHWE-TONKHWE
@Alice-z7t4z
@Alice-z7t4z 3 сағат бұрын
​@@Kabwilachikangawakkkkkkkkkk 😂😂😂😂😂😂🎉
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 4 сағат бұрын
Nkhani yabwino kwambili
@DakaValilani
@DakaValilani 3 сағат бұрын
Indendizona
@BrightonKamwendo-db1ci
@BrightonKamwendo-db1ci 4 сағат бұрын
Moto kuti buuuu
@GeoffreyWatchipa
@GeoffreyWatchipa 4 сағат бұрын
Koma kumeneko 😅😅😅😅
@FunnyKatchenga
@FunnyKatchenga 4 сағат бұрын
Agwa nao akanganya amenewa
@YUNGBRÔÔKLYÑ-w1t
@YUNGBRÔÔKLYÑ-w1t 4 сағат бұрын
Kumwamba kudyele nyama
@johnjoachim3820
@johnjoachim3820 2 сағат бұрын
Zilibwino
@johnjoachim3820
@johnjoachim3820 2 сағат бұрын
Milandu yaku Malawi ikukhala bwanji this my first kumva kuti muthu wamangidwa kamba koti amafuna kuphwanya lamulo 😊 ma judge mulipo koma where did you get this power mudziwaletsako a mcp kuti malamulo anu samatelo👣🔊
@BrightonKamwendo-db1ci
@BrightonKamwendo-db1ci 4 сағат бұрын
Nthawani tidusa inu
@jamemagalasi8190
@jamemagalasi8190 4 сағат бұрын
Dusani bwana 😂
@MaryNyirenda-nq3mh
@MaryNyirenda-nq3mh 4 сағат бұрын
Hluuuuuuu ulemu wanu dutsani😂😂😂😂😂😂😂
@BrunoChakukuma
@BrunoChakukuma 3 сағат бұрын
Anabel 😂😂😂😂😂😂😂 dweku
@Edithmchinza
@Edithmchinza 4 сағат бұрын
Tikavota 😂😂
@JACKSONHULUWA-j2n
@JACKSONHULUWA-j2n 4 сағат бұрын
Deal
@DorothySangala
@DorothySangala 4 сағат бұрын
Ndetika votela ndani umuvotela akusowa osewa zaozimozi
@hendricksmlendo6192
@hendricksmlendo6192 4 сағат бұрын
Iwe sukuona, sukumwa , kapena political blindness
@RuthBeyala
@RuthBeyala 4 сағат бұрын
Political blindness
Will A Basketball Boat Hold My Weight?
00:30
MrBeast
Рет қаралды 114 МЛН
啊?就这么水灵灵的穿上了?
00:18
一航1
Рет қаралды 85 МЛН
Mom had to stand up for the whole family!❤️😍😁
00:39
Всё пошло не по плану 😮
00:36
Miracle
Рет қаралды 3,8 МЛН
Izindaba zesiZulu @19H00 l 25 October 2024
21:17
SABC Izindaba
Рет қаралды 10 М.
COMRADE FRANK -TAMVANI ZENI ZENI ZOMWE AMUMANGIRA KALIATI UJA AMALAWI.
9:04
Will A Basketball Boat Hold My Weight?
00:30
MrBeast
Рет қаралды 114 МЛН