Pot amalawi ena apangisa kale ma I'd akumozambiq kut akavote kumeneko mu October,anthu amenewo amalowa bwanji mdziko muno kod chimenechi sichikhala chipeleganyu?
@user-xn3lq1hj1r16 күн бұрын
Ndakuso kotsera nkulinga utamva mawu ndiye apita patali ndipo alankhulidea mopanda kudzungulira straight and directly to the point. APM my vote✔️
@user-un6qv6sj3h16 күн бұрын
Ndipo ayankhula mchichewa ❤
@HawardKalipande17 күн бұрын
Simunati apaka Inu bola mwaziwonera komanso kudzimvela iweyo kumkuyu ndi mzakoyo mwapanga chian??munya simunati APM yemweyo
Kunoko ku chinsapo ku Kakule primary school akulembesa nd ana azaka 12 omwe mmmmm kma boma ili. Akulemba ndi mzika za Mozambique zomwe. Ndye Nick chakwela wakapangisa ma ID kunja ozabela zisankho kma
@user-zk7jw9up6m16 күн бұрын
Nkunkuyu ndiwe chisilu ndi chakwela wakoyo tazingobani
@mcdonaldgerard970714 күн бұрын
Zimene walankhura muthalika kwamunthu wanzelu zake palibe cholakwika ayi, koma kuti maloto achumba amakhala ofoira ndiye zimene akunena chakwera yo!!!!!
@user-lk8kj9zv6x17 күн бұрын
Zitsilu inu galu wanu chakwerayo mmesa ndi wankulu wampingo
@user-mj2te7vl6p17 күн бұрын
Y only that sentence
@BysonMakalani13 күн бұрын
Nyekhwe
@HassanJameskananjie16 күн бұрын
Aganiza bwino bwino mmene mukubela anyapapi inu munya next year
@alfrednazombe15 күн бұрын
Tili kwaeni kom zikutheka salary kulandilisa apolisi 5 komnso kuwalipilila magesi madzi ndi rent kkkkk mcp out kunkuyu tazingophuza long life pills bs unyanya kugagadaa kkkk
@laymanchirwa802616 күн бұрын
Kunkuyu nthongo lako
@user-nn7sv5yb8h14 күн бұрын
Ndichifukwa chiani mukunamiza a Malawi mopusa chotere ngati amalawi ndi opusa
@jamusnamwino-br2iz16 күн бұрын
simunati mulila akhukuyu koma akunama palibe chimene mungalankhule chazelu
Eeee Kom Sana name jt mufuna mubele muchoke bas zopusa zanuzo mukasak kopangila agalu inu iwe ukulakhul we ukulakhul izi fukwa chandler komas kuopa imfa