Iyiyi ndi move akufuna asakayime nawo pa President adziyenda ndi Bello mu thumba... 🙆♀️🙆♀️🙆♀️
@JoycieMbayaКүн бұрын
Eeeh Koma! There is just too much evil happening in this country. May the Almighty God come to our rescue.
@JosephMkuzi16 сағат бұрын
Ine Joseph Mkuziwaduka Osadanda masten Sweet for sweat keep it up
@S-rr1euКүн бұрын
BomA la MCP ,,, mwatasa kwambili... Kufuna kubisa imafa ya SKC
@MillieMalakamКүн бұрын
From Cape Town mitchells plain town centre. Chakwela ukufuna chiyani. Iweyo manganya ndimbuzi yamuthu kwambili ukuziwa kt upule sungatenge ndichingangawa wakoyo
@mabvutomichaelpanagona194923 сағат бұрын
Iyi ndi pulani kuti asaime pa koveshoni ndi Michael usi wagwirizana ndi chikangawa
@DoreenZuze-r1n22 сағат бұрын
Zoona akutiopa
@Isakaymw2 сағат бұрын
Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
Politics yo dyetsana Manyi.. .We ready to die for this flag Zachimizi .Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
@RonnMtafyaКүн бұрын
Muja Paulos amanzunzira osatira Yesu ndi pamene Chikhristu chinafalikira kwambiri.Mungoonjejera mkwiyo wa pa 29 ndi 30 OCTOBER.
@EddahKaunda18 сағат бұрын
History is best teacher koma kusanva anthu
@GraceKamanga-k8v22 сағат бұрын
Ku Malawi timayankhula Chichewa,chitumbuka atinthandauzire mlandu wake timve bwino bwino
@AshimayeGamaКүн бұрын
Basi manyodza dpp ameneyo lelo adziwona okha kuti boma ndi dpp chipani cha ulemu
@ShanifaMustaferКүн бұрын
Our country now is more 𝕎𝕠𝕣𝕤𝕖 𝕥𝕙𝕒𝕟 𝕓𝕖𝕗𝕠𝕣𝕖
@victoriasamarthankhata8 сағат бұрын
Ndingoziwa nawwo kuti azukako bwanji amai lero kuchitokolosi,ndadzuka ndi matha zedi😢😢😢,so God help us
@MerryBiyela2 сағат бұрын
Good make it truth on one life
@SameBanda-q5q18 сағат бұрын
Ngat walakwa amangidwe basi bcoz nobody is above the law
@FanessayassinFanessayassin17 сағат бұрын
Mbuzi yamunthu iwe
@Lee-lee-w1r4 сағат бұрын
@@FanessayassinFanessayassinakuti ngati walakwatu. Nde mukufulumila kutukwana bwa
@SitithanaSonani23 сағат бұрын
God deliver our beloved country whr r we going
@SostenPiyoКүн бұрын
Manganya akudziwa za kumangidwaku, Mulungu akuona, opposition be careful about
@EliaSiska-n6rКүн бұрын
Inka Malawian politics very few women speak out. Kaliati is a voice for women.
@thomluciouss73607 сағат бұрын
Politics in Malawi is cleartivity that dazzles
@EdsonchilongoSitoe20 сағат бұрын
Iri si boma ayi akufuna kuti kumbutsa nthawi ya kamuzu banda from mocambique
@AllanGonthi23 сағат бұрын
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
@shayrafernandeslatif955619 сағат бұрын
Michael Usi amadziwa kuti sangakhale president, Akweni for President,we are praying for you Akweni and our country Malawi
Akufuna manganya kuti atenge chipani kuti chibwerere ku mcp a kunama tu manganya anthu savoteratu
@JohnmarkNazombe-hi9xd21 сағат бұрын
AMUCHITA BWINO HIM AND CHILIMA AMAYELEKEDWA KUMANYODZA MUNTHALI KA...IN SUPPORT OF CHIKWERA...LERO WADZIWONAH!!!!!!
@horacechera6978Күн бұрын
Timaona ngati muzitifotokozera nokhatu nanga mukuwerenganso zomwe alanda anzanu ku page kwawo Ife tingopita ku page konko kaa
@LouisKuyeliКүн бұрын
Pora moto
@PercivalKalua9 сағат бұрын
Uku ndi kuwonjezela nkwiyo wa chikangawa airport.
@PatrickKondowe-f7o20 сағат бұрын
It's normal ngati walakwa amangidwa ndithu. It's not politics but normal.
@BrightZionga9 сағат бұрын
Chilikwamzako mudzaziona man
@AugrinNgunga23 сағат бұрын
Boma ili mulibemo democracy
@judithphiri348Күн бұрын
Awa atitha onse😢
@EneyaManda-r1p20 сағат бұрын
Malawi Wachpka pamaso pa Mulungu Tikuyeñda ndi zeru zathu sitinati.
@SamuzZimba21 сағат бұрын
Sanalakwitse adziwe kupeleka ulemu Kwa akulu akhale zaka 3
@rodgerskampira941219 сағат бұрын
Adziwe akulu ake ati? There is no way MCP can stop Malawians from seeking justice. Awa akupita kumapeto a nthawi yawo. Apa Amalawi taphunzirapo kuti MCP siinasinthe.
Aaaa adzi ndidzimene kaliyati ndi malemu chilima amafuna onena analipo koma kutsamva MCP yoyipa koma kakaka idzi anthu ambili omangidwa pa dzifukwa dziiiii kufuna kuti MCP itsachoke boma koma dzilikotu
@LuciousMulipo17 сағат бұрын
As MCP tries to kill UTM and entire opposition using Kape manganya,, shame
@AdamusuwediMandela18 сағат бұрын
Kunzuza azimayi ndi mavuto akulu kwambili kaliati amatukwana bakili muluzi koma sanammange boma la chakwela ndi lolephela atetezeni azimayi onse nzdiko muno kusaziwa ndale ndi matenda
@KelevraKatesa-g3z22 сағат бұрын
Strong we stand,free up PK
@IsaacBauti23 сағат бұрын
Ubwino wake bon kalido the dc mwama owooopsa kwambiri ananena kale Ndie sidzachilendo ai chikangawa paty
@JacobVictor-z7rКүн бұрын
Munamutenga nokha Lazalo ku chipiku kuti akhale president wanu lero akumangansoni mukhaula naye Chikangawayo
@HappinessSauzande-h3rКүн бұрын
Zirikotu 🙌
@HarrsoniКүн бұрын
Mulandu waukulu oponsa wakugwa kwa ndege ?
@YankhoRumwila57 минут бұрын
Akudziwana awa ndi momwe amadyera. Anthu a ndale zawo ndi zimodzi.
@patesnkajenda425819 сағат бұрын
Malawi is more fire apa ndeeeeeeee zativuta basssss
Manganya plan akufuna akweni asakayime ku convention 😢
@mikekaliza-bw4yg21 сағат бұрын
amalawi sisamapange chochi zosezi wapanga ndi usi pofuna kumulepere kuti asamenyere ufulu wa malawi basi tiwuzeni chomwe a mcp mukufuna chencheni
@LuciusPatrick-f2cКүн бұрын
Koma apolice amene mikugwirisidwa ntchito achipan tizaona boma likadzasintha ntchito za mcp ndizimenezo chipani chakupha iweso jezebelo ziwa kt paudindo umenewo uzachokapo
@TameeraInglis21 сағат бұрын
Izi wapanga. Ndi manganya kuti asazaime. Pampando wa upresident pajanso ndi yemwe adampeleka malemu. Chilima.
@supa4dupa22 сағат бұрын
Dictatorship ya Chakwera ndi Usi,zabodza zones akufuna ku opyeza opposition,MCP ya bodza,kuba,kupha,kuyambira Kuma 1960s.Ma International Human Rights ,IMF,UN,World Bank ,EU,stop donating to Dictatorship Chakwera who has crippled Malawi and it's citizens,fuel crisis,poverty,no maize ,no fertilizer, and they killed VP Chilima and others,they are abusing Malawians.Free HON Kaliati,HON Navitcha and opposition.
The Elect the worst to lead us,kodi akuwona ngati dzikoli la ambuye awo
@JulietNyondoКүн бұрын
Kma boma iyiii zosakhala bwino Kodi apa tikupita KU zisakho tizingomangana Kodi zikhala bwanji mwatilakwira kwambiri
@ShareefAlli-m4l21 сағат бұрын
Kufuna kuwononga UTM uku, Eshhhh koma kumalawi amwene
@ChikwawaКүн бұрын
Mayi a Kaliati munakatenga mfiti ku church kuti adzazunze anthu osaoka, onani akumakumangani komanso kumadyanso ena mwa inu. Munatenga zosayenela kuzibweretsa ku dziko.
@stephenchavula116222 сағат бұрын
kenaka mumva kuti winwa atenga injuction yolepheretsa convetion,so that rumour is true,shame we are becoming a lawless nation