BOMA LAMANGA MAYI PATRICIA KALIATI NDIPO ZASIMIKIZIKA KUTI CHIFUKWA CHOMWE AWAMANGIRA NDI ICHI

  Рет қаралды 101,071

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 544
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Күн бұрын
Iyiyi ndi move akufuna asakayime nawo pa President adziyenda ndi Bello mu thumba... 🙆‍♀️🙆‍♀️🙆‍♀️
@JoycieMbaya
@JoycieMbaya Күн бұрын
Eeeh Koma! There is just too much evil happening in this country. May the Almighty God come to our rescue.
@JosephMkuzi
@JosephMkuzi 16 сағат бұрын
Ine Joseph Mkuziwaduka Osadanda masten Sweet for sweat keep it up
@S-rr1eu
@S-rr1eu Күн бұрын
BomA la MCP ,,, mwatasa kwambili... Kufuna kubisa imafa ya SKC
@MillieMalakam
@MillieMalakam Күн бұрын
From Cape Town mitchells plain town centre. Chakwela ukufuna chiyani. Iweyo manganya ndimbuzi yamuthu kwambili ukuziwa kt upule sungatenge ndichingangawa wakoyo
@mabvutomichaelpanagona1949
@mabvutomichaelpanagona1949 23 сағат бұрын
Iyi ndi pulani kuti asaime pa koveshoni ndi Michael usi wagwirizana ndi chikangawa
@DoreenZuze-r1n
@DoreenZuze-r1n 22 сағат бұрын
Zoona akutiopa
@Isakaymw
@Isakaymw 2 сағат бұрын
Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
@AKMASEKO
@AKMASEKO 17 сағат бұрын
Komatu utsi sufuka opanda moto dziko lonseli sangangoma Mayi Kaliyati! Akulu anati kang'oma kolilitsa sikachedwa kung'ambika osangoti poti ndimzimayi koma ngati alakwa afunika akumane m'chigamulo osamangonyoza boma.
@IbrahimUseni-p8f
@IbrahimUseni-p8f Күн бұрын
Manganya ameneyo,,mafuta kulibe kummanga munthu wa utm akulira maliro achirima
@KhadijahMuhammadah-my7lc
@KhadijahMuhammadah-my7lc 16 сағат бұрын
Never give up pk
@ChimwemweSamson-l5s
@ChimwemweSamson-l5s 18 сағат бұрын
Ndale zaku Malawi
@DesireMjojo
@DesireMjojo Күн бұрын
Kalindo adanena kale izi ,sizodabwitsa
@dalitson3558
@dalitson3558 20 сағат бұрын
Kalindo ndi Katundu he never disappoints
@cuthbertjafali6059
@cuthbertjafali6059 Күн бұрын
Koma ndi chani makamaka, God have mercy on us
@JoelMwenegamba
@JoelMwenegamba Күн бұрын
Angofuna kuti kweni asapedze ku convention it's like government want to finish U T M. But God is watching.
@blessingbanda6206
@blessingbanda6206 19 сағат бұрын
But why mukumayika zithuzi nkhope yamagazi ngati munthuyo wakhapi propaganda
@MarryNyilongo-s5x
@MarryNyilongo-s5x 23 сағат бұрын
Mulungu si James pemphero mulungu amutetezere mai a kweni ndipo mzimu wa chilima uwakanthe anthuwo
@OmarMakawa
@OmarMakawa 19 сағат бұрын
Mayi ameneyu nayeso ndiosokoneza achita bwno kumutapa mesa ndi amene anathandiza bomali kt likhale pa pando eya uliziwe ziko zomwevlimapanga mwina uleka
@EnockLichenya
@EnockLichenya Күн бұрын
Masiku atha kale awa tionana this coming year, kutha nzeru kwa Boma uku😢😢😢😢
@AubreyShaba-b5d
@AubreyShaba-b5d Күн бұрын
Perekani chifukwa chomangira ...kungoti felony...timve zifukwa... felony sichifukwa..mukutisokoneza...
@FebbieNjewa-g3k
@FebbieNjewa-g3k Күн бұрын
Tru,,God z watching,,Mulungu awamenyera Mai kaliati nkhondo Ali cete
@JafaliAdams-l5k
@JafaliAdams-l5k 17 сағат бұрын
Amawonjeza kma kupanga ndale sanyozana mayi uyu akhale nd displin
@davidbulla5128
@davidbulla5128 19 сағат бұрын
Politics yo dyetsana Manyi.. .We ready to die for this flag Zachimizi .Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
@RonnMtafya
@RonnMtafya Күн бұрын
Muja Paulos amanzunzira osatira Yesu ndi pamene Chikhristu chinafalikira kwambiri.Mungoonjejera mkwiyo wa pa 29 ndi 30 OCTOBER.
@EddahKaunda
@EddahKaunda 18 сағат бұрын
History is best teacher koma kusanva anthu
@GraceKamanga-k8v
@GraceKamanga-k8v 22 сағат бұрын
Ku Malawi timayankhula Chichewa,chitumbuka atinthandauzire mlandu wake timve bwino bwino
@AshimayeGama
@AshimayeGama Күн бұрын
Basi manyodza dpp ameneyo lelo adziwona okha kuti boma ndi dpp chipani cha ulemu
@ShanifaMustafer
@ShanifaMustafer Күн бұрын
Our country now is more 𝕎𝕠𝕣𝕤𝕖 𝕥𝕙𝕒𝕟 𝕓𝕖𝕗𝕠𝕣𝕖
@victoriasamarthankhata
@victoriasamarthankhata 8 сағат бұрын
Ndingoziwa nawwo kuti azukako bwanji amai lero kuchitokolosi,ndadzuka ndi matha zedi😢😢😢,so God help us
@MerryBiyela
@MerryBiyela 2 сағат бұрын
Good make it truth on one life
@SameBanda-q5q
@SameBanda-q5q 18 сағат бұрын
Ngat walakwa amangidwe basi bcoz nobody is above the law
@FanessayassinFanessayassin
@FanessayassinFanessayassin 17 сағат бұрын
Mbuzi yamunthu iwe
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 4 сағат бұрын
@@FanessayassinFanessayassinakuti ngati walakwatu. Nde mukufulumila kutukwana bwa
@SitithanaSonani
@SitithanaSonani 23 сағат бұрын
God deliver our beloved country whr r we going
@SostenPiyo
@SostenPiyo Күн бұрын
Manganya akudziwa za kumangidwaku, Mulungu akuona, opposition be careful about
@EliaSiska-n6r
@EliaSiska-n6r Күн бұрын
Inka Malawian politics very few women speak out. Kaliati is a voice for women.
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 7 сағат бұрын
Politics in Malawi is cleartivity that dazzles
@EdsonchilongoSitoe
@EdsonchilongoSitoe 20 сағат бұрын
Iri si boma ayi akufuna kuti kumbutsa nthawi ya kamuzu banda from mocambique
@AllanGonthi
@AllanGonthi 23 сағат бұрын
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 19 сағат бұрын
Michael Usi amadziwa kuti sangakhale president, Akweni for President,we are praying for you Akweni and our country Malawi
@PreciousElijahKayinga-li3cn
@PreciousElijahKayinga-li3cn 22 сағат бұрын
Mukamabweretsa nkhani zanuzo timaona ngati mwafufuza nkupeza chimene wamangidwira koma inunso muli mbuli pankhaniyiii moti mkumakasaka mma comments aanthu
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 4 сағат бұрын
Eti eti
@TinaKazembe-l7d
@TinaKazembe-l7d 18 сағат бұрын
Akaliyat amaonjeza kunyonza
@MiracleRose-f9x
@MiracleRose-f9x 23 сағат бұрын
Kodi akufuna kumpha athu angati chifukwa chani m dima umadana ndikuujika bas tikufunabe commission of equrery
@victoriasamarthankhata
@victoriasamarthankhata 8 сағат бұрын
JESUS JESUS INTERVINE IN THIS SITUATION 😢😢
@CassimMbalaka
@CassimMbalaka Күн бұрын
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxidwa pa ifa ya chilima
@lawrencedanielmandauka
@lawrencedanielmandauka 22 сағат бұрын
Nde mukanangokhala chete osabwera ndi nkhani zossmveka spa mudziyamba mwafufuza kuti anthu adziwe chenicheni
@ruthkundwe7448
@ruthkundwe7448 Күн бұрын
No good,no rest for the wicked
@AlfredJuliusTemboh
@AlfredJuliusTemboh 6 сағат бұрын
Bwana Chakwera zomwe akupangazi adzafa ngati mwana ndipo sikale chifukwa pano anthu atopa nazo. Inu muzigona ndithu
@GreysonChilongo
@GreysonChilongo 18 сағат бұрын
MCP yikuopa chisankho ndichifukwa ayamba musokoneza mwapha chilima mwayamba kaliati nikufuna kusokoneza UTM afiti imwe a satanic imwe ba MCP agalu inu from Zambia 🇿🇲
@SamuelMponda-y3d
@SamuelMponda-y3d Күн бұрын
Angofuna kupeza mpata osokoneza nsonkhano waukulu wa UTM pa 17 Nov. 2024
@ConlardNkhoma
@ConlardNkhoma Күн бұрын
Ukayenda usasiye mlomo amayiwa amazitenga ngati adzao alibe pakamwa
@MikeMoris-zp6yg
@MikeMoris-zp6yg Күн бұрын
That's indeed
@MissiPhiri-h3w
@MissiPhiri-h3w 19 сағат бұрын
mulungu chonde chonde munarenga malawi ndiinu kodi dziko ra malawi muritetedze kuti anthu anu amene munawarenga akudzuzana okhaokha inu ndi chikondi kodi munarenga ndarama ndiinu chonde chotsani choipa ku malawi ko ngati mvuto ndiifeyo chonde tikhululukireni pomupanga chakwera kuti ariramurire mumava kurira kwa aphawi yakhani mulungu mwadongosoro ranu amen
@JohnJohn-og8rt
@JohnJohn-og8rt 19 сағат бұрын
Tupere ananena komaso phiter adadi wofa athu inu chaka chamawa uphusezo akumfunika tupere uzogoleri wabwino ❤
@WelosChifunga
@WelosChifunga Күн бұрын
Boma limeneli ndi loipa kwambili tionetsana 2025
@rashirdbanda8204
@rashirdbanda8204 Күн бұрын
Manganya panga manyazi ulibe umunthu Chocho kumati muzakhale president
@ShemjuniorMweramkulu
@ShemjuniorMweramkulu 17 сағат бұрын
This is what we expected from Mcp with it's president too bad
@James-w6j8z
@James-w6j8z 4 сағат бұрын
Boma ili ndiloyipa kwambili don't warry amalawi tiligwesa popanopopano Muthu sumaluma Chala chimene chimakudyesa phala
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx Күн бұрын
Akufuna manganya kuti atenge chipani kuti chibwerere ku mcp a kunama tu manganya anthu savoteratu
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd 21 сағат бұрын
AMUCHITA BWINO HIM AND CHILIMA AMAYELEKEDWA KUMANYODZA MUNTHALI KA...IN SUPPORT OF CHIKWERA...LERO WADZIWONAH!!!!!!
@horacechera6978
@horacechera6978 Күн бұрын
Timaona ngati muzitifotokozera nokhatu nanga mukuwerenganso zomwe alanda anzanu ku page kwawo Ife tingopita ku page konko kaa
@LouisKuyeli
@LouisKuyeli Күн бұрын
Pora moto
@PercivalKalua
@PercivalKalua 9 сағат бұрын
Uku ndi kuwonjezela nkwiyo wa chikangawa airport.
@PatrickKondowe-f7o
@PatrickKondowe-f7o 20 сағат бұрын
It's normal ngati walakwa amangidwa ndithu. It's not politics but normal.
@BrightZionga
@BrightZionga 9 сағат бұрын
Chilikwamzako mudzaziona man
@AugrinNgunga
@AugrinNgunga 23 сағат бұрын
Boma ili mulibemo democracy
@judithphiri348
@judithphiri348 Күн бұрын
Awa atitha onse😢
@EneyaManda-r1p
@EneyaManda-r1p 20 сағат бұрын
Malawi Wachpka pamaso pa Mulungu Tikuyeñda ndi zeru zathu sitinati.
@SamuzZimba
@SamuzZimba 21 сағат бұрын
Sanalakwitse adziwe kupeleka ulemu Kwa akulu akhale zaka 3
@rodgerskampira9412
@rodgerskampira9412 19 сағат бұрын
Adziwe akulu ake ati? There is no way MCP can stop Malawians from seeking justice. Awa akupita kumapeto a nthawi yawo. Apa Amalawi taphunzirapo kuti MCP siinasinthe.
@MussaMbota
@MussaMbota Күн бұрын
Azimai musanamizane zosayenda mbulanda coz mukangoziyalutsako
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Күн бұрын
Aaaa adzi ndidzimene kaliyati ndi malemu chilima amafuna onena analipo koma kutsamva MCP yoyipa koma kakaka idzi anthu ambili omangidwa pa dzifukwa dziiiii kufuna kuti MCP itsachoke boma koma dzilikotu
@LuciousMulipo
@LuciousMulipo 17 сағат бұрын
As MCP tries to kill UTM and entire opposition using Kape manganya,, shame
@AdamusuwediMandela
@AdamusuwediMandela 18 сағат бұрын
Kunzuza azimayi ndi mavuto akulu kwambili kaliati amatukwana bakili muluzi koma sanammange boma la chakwela ndi lolephela atetezeni azimayi onse nzdiko muno kusaziwa ndale ndi matenda
@KelevraKatesa-g3z
@KelevraKatesa-g3z 22 сағат бұрын
Strong we stand,free up PK
@IsaacBauti
@IsaacBauti 23 сағат бұрын
Ubwino wake bon kalido the dc mwama owooopsa kwambiri ananena kale Ndie sidzachilendo ai chikangawa paty
@JacobVictor-z7r
@JacobVictor-z7r Күн бұрын
Munamutenga nokha Lazalo ku chipiku kuti akhale president wanu lero akumangansoni mukhaula naye Chikangawayo
@HappinessSauzande-h3r
@HappinessSauzande-h3r Күн бұрын
Zirikotu 🙌
@Harrsoni
@Harrsoni Күн бұрын
Mulandu waukulu oponsa wakugwa kwa ndege ?
@YankhoRumwila
@YankhoRumwila 57 минут бұрын
Akudziwana awa ndi momwe amadyera. Anthu a ndale zawo ndi zimodzi.
@patesnkajenda4258
@patesnkajenda4258 19 сағат бұрын
Malawi is more fire apa ndeeeeeeee zativuta basssss
@HashrouYassin
@HashrouYassin 18 сағат бұрын
Awamanga chifukwa Choti anawakana chibwenzi apule,zoona mungamalimbane ndi mzimai mukufuna muzikhala busy kumugwilira kumeneko
@esterechamba9343
@esterechamba9343 Күн бұрын
Azimai tiyeni tikayende mbulanda Ku mnsewu zanyanya
@ChisomoLester-h7x
@ChisomoLester-h7x Күн бұрын
Ndi za ndale izi muzingovutika ndinu anthu ovutika, olo kaliyatiyo akuziwa chikuchitika
@FeliaNgunga
@FeliaNgunga Күн бұрын
Mwatero? Mwinadi
@CharityMhone-uk9ym
@CharityMhone-uk9ym Күн бұрын
Iwe kayaka tanena chifukwa chomwe mwawamangila sukunena bwanji...iwe ndi mnzako chikangawa matsiku anu awelengedwa mwazitenga ngati ndnu mashasha, daily kukacha tizimva nyasi za MCP ndi chikangawa mmmm mwanyanya😮😮😮😮
@EmmanuelSteve-q7b
@EmmanuelSteve-q7b 18 сағат бұрын
Izo ndindare manganya ndichikangawa afuna kuzunza azawo mmalo mosakha njira zotesera mavuto mmalawi muli bize kukorezer mukwiyo amalawi
@RonnMtafya
@RonnMtafya Күн бұрын
Can delay Change but cannot deny it.
@OmarMakawa
@OmarMakawa 19 сағат бұрын
Azimai boza osayenda maliseche muzangoyaluka musiyen ngat mukuona mavuto gulu lake ndilomweli lomwe linalimhlbikisa zisokonezo nthaw ya pita
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza Күн бұрын
Zonse zikuchitikazi akufuna anthu azikhala busy ndi kuyankhula za Mai kaliyat kufuna kuwayiwalitsa anthu za commission of enquiry
@ZungeniBanet
@ZungeniBanet Күн бұрын
Mmmm Kodi a MCP icho wakupenga nivichi
@isaaczuze
@isaaczuze 21 сағат бұрын
Boma loyendesedwa ndi zigawenga komanso mbava chonchi tikavotere anthu okuti akumanga anthu popanda zifukwa zenizeni
@CrispineBetha
@CrispineBetha 19 сағат бұрын
Manganya plan akufuna akweni asakayime ku convention 😢
@mikekaliza-bw4yg
@mikekaliza-bw4yg 21 сағат бұрын
amalawi sisamapange chochi zosezi wapanga ndi usi pofuna kumulepere kuti asamenyere ufulu wa malawi basi tiwuzeni chomwe a mcp mukufuna chencheni
@LuciusPatrick-f2c
@LuciusPatrick-f2c Күн бұрын
Koma apolice amene mikugwirisidwa ntchito achipan tizaona boma likadzasintha ntchito za mcp ndizimenezo chipani chakupha iweso jezebelo ziwa kt paudindo umenewo uzachokapo
@TameeraInglis
@TameeraInglis 21 сағат бұрын
Izi wapanga. Ndi manganya kuti asazaime. Pampando wa upresident pajanso ndi yemwe adampeleka malemu. Chilima.
@supa4dupa
@supa4dupa 22 сағат бұрын
Dictatorship ya Chakwera ndi Usi,zabodza zones akufuna ku opyeza opposition,MCP ya bodza,kuba,kupha,kuyambira Kuma 1960s.Ma International Human Rights ,IMF,UN,World Bank ,EU,stop donating to Dictatorship Chakwera who has crippled Malawi and it's citizens,fuel crisis,poverty,no maize ,no fertilizer, and they killed VP Chilima and others,they are abusing Malawians.Free HON Kaliati,HON Navitcha and opposition.
@PingeniChigwenembe
@PingeniChigwenembe 20 сағат бұрын
Muthu aliyense niwofunika osamawonjeza malakhulidwe
@HaziwellLameck
@HaziwellLameck 23 сағат бұрын
Cholinga chawo akufuna asakayime nawo PA u president
@ChoopsyaLloyd
@ChoopsyaLloyd 22 сағат бұрын
Ngati alakwisa amangidwe basi palibe zoti ndi mzimayi LAMULO LIGWIRE NTCHITO
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer 23 сағат бұрын
Bwanji osamanga anthu omwe anapha chilima nd anthu Ena aja Zinaz ndy ai srs please forgive God tichitiren chifundo mcp tatopa nay srs
@embersonmaonga1569
@embersonmaonga1569 Күн бұрын
🤣🤣🤣 10 ago ndamuona akuchoka kunyumba kwake amumanga nThawi yanji 🥺😂
@Yungjoe786
@Yungjoe786 Күн бұрын
The Elect the worst to lead us,kodi akuwona ngati dzikoli la ambuye awo
@JulietNyondo
@JulietNyondo Күн бұрын
Kma boma iyiii zosakhala bwino Kodi apa tikupita KU zisakho tizingomangana Kodi zikhala bwanji mwatilakwira kwambiri
@ShareefAlli-m4l
@ShareefAlli-m4l 21 сағат бұрын
Kufuna kuwononga UTM uku, Eshhhh koma kumalawi amwene
@Chikwawa
@Chikwawa Күн бұрын
Mayi a Kaliati munakatenga mfiti ku church kuti adzazunze anthu osaoka, onani akumakumangani komanso kumadyanso ena mwa inu. Munatenga zosayenela kuzibweretsa ku dziko.
@stephenchavula1162
@stephenchavula1162 22 сағат бұрын
kenaka mumva kuti winwa atenga injuction yolepheretsa convetion,so that rumour is true,shame we are becoming a lawless nation
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Күн бұрын
Kd boma losaunka nkalle ankufunna liposse phamene lilipha shinkangawaw samalani 225 muphita nnayyo bp
@juliussamson6212
@juliussamson6212 20 сағат бұрын
YAA NDIZOWONA CHAKWERA MANGANYA NDI PLAN YOCHITA KUKOZA MISANA YANU MBUZI WHY OSAMANGA AMENE ANAPHA CHILIMA MUKUMANGA ANTHU OSALAKWA OSACHITA MANYAZI KUNKUYU ANAPHA MUNTHU BWANJI SIMUKUMANGA APOLICE IZI MUKUCHITAZI MADZAYIVA KUWAWA
🕊️Valera🕊️
00:34
DO$HIK
Рет қаралды 13 МЛН
Ouch.. 🤕⚽️
00:25
Celine Dept
Рет қаралды 25 МЛН
"كان عليّ أكل بقايا الطعام قبل هذا اليوم 🥹"
00:40
Holly Wolly Bow Arabic
Рет қаралды 15 МЛН
COMRADE FRANK -TAMVANI ZENI ZENI ZOMWE AMUMANGIRA KALIATI UJA AMALAWI.
9:04
🕊️Valera🕊️
00:34
DO$HIK
Рет қаралды 13 МЛН