More Fire 🔥 🤧......Bon Kalindo....Auze amenewo amvetsese...Chakwera wationongera Mother Malawi... People are suffering tindikwera kwa zithu zofunika kwambiri.
@LaikaSaidi2 ай бұрын
Athilen mau anthu osaopa Mulungu amenewo
@Kabwilachikangawa2 ай бұрын
Just meet the DC outside my home. What an honor to meet him...🤝
@BruceChirambo-ly8jm2 ай бұрын
BOOOOOON KALINDO🔥🔥🔥🔥🔥💯💯💯
@Homeofpeace3212 ай бұрын
Ayi dzikoli ndilaiweyo kalindo, osamakhala ndi nsanje
@CalvinThomson-ys5zf2 ай бұрын
Uniform mpaka muisoka zikizaki 😂😂😂😂😂😂
@YassinAmbali2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂
@arthurkayuza2 ай бұрын
Ndiye mwati chani "ng'alulazation"😂
@OwamiSimeon2 ай бұрын
West of west president in the world 🌎
@ghamagift45912 ай бұрын
Lets go.....umati tsegula mutu
@GeraldChikalema2 ай бұрын
😂😂😂 Ng'alulazation yomweyo kuti wawawaaaaa
@JonaZimpita2 ай бұрын
Mbu🥵li iwe tang,aluluko chizungu
@MoeshahIbrahim2 ай бұрын
Alot is not going well amalawi tiziombela mmanja sitima 😂 ifeyo kodi aliyense amateurs galimoto aaah njala ndalama izipezeka
@GRACIOUSKENAN2 ай бұрын
Hello our president bbboooonnnn kalindoooooo
@loneymagwera9152 ай бұрын
Ng'alulasation🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@Mervic-vm8eo2 ай бұрын
Tilimu zimu wa chikangawa pano 🙌🙌🙌🤣🤣🤣🤣🤣
@AlinafeLinje2 ай бұрын
Mr DC mumakwana
@RitaKainga2 ай бұрын
Ng'alulaaaa!!!!!!! THE DC CCCCCV!!!!
@DavidJackson-ox4xm2 ай бұрын
A Malawi tili pa mavuto oopsa kwambiri MULUNGU atithandize kwambiri
@SamuelKulimah2 ай бұрын
Shallomo Malawi shallomo 😂😂
@EmmaculateChadambuka2 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤I love you Mr. DC
@inessmsiyambiri85172 ай бұрын
Koma DC ndimakhala ndi chidwi ndi apolicewa iiiiiii unifom eti mpaka kuisokasoka eti
Winawe olo manyazi ulibe, ukulimbana ndi Bon Kalindo apa , CHOTI udziwe Bon Kalindo ndi president waife osauka ndipo izi akuuza ife, iweyo abale ako nda a Chikangawa Party takudziwa shame on you! Our president please more 🔥🔥🔥 Tell them the truth, winawe uziluma pa mchombo, wekha- wekha- kunyoza Bon Kalindo yaaa , Useless boy
@dytonmoyo46292 ай бұрын
🔥🔥🔥🔥
@DixonChimanya2 ай бұрын
Kubwera kumeneko tawauza bwino
@SimonBanda-b1f2 ай бұрын
Ayiwala kuti ndalama zo agule fertilizer NDI mbewu za subsidy kuti mwina anthu alandile mwachangu komanso anthu ambiri Koma azapeleka mbewuzo February chaka chamawa
@DixonChimanya2 ай бұрын
Dyson @tasona mbolo yako sukukuoa kuti ku Malawi pano kwafika nyasi Pantumbo pako Ngati ukamadya za kape wakoyo chikangawa udzingodya
@Geraldmkwewu2 ай бұрын
Mumakwana madara chakwera chikangawa watikwana kd ndalamazo muzipatara mulibe makhwala katundu wadura nde atagure zake ndani bznesiyo chakwera akanafa km amanganya nanuso mungoyenga ngt wamisara muzayaruka nxt year
@prettytambala56872 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂
@JamesKhengemussa-t1d2 ай бұрын
Big man,asyene kunga'alula
@RemitterFlik11302 ай бұрын
Ndipo mutipase number yanu bwana tizikuuzani zambiri zomwe nguluwezi zikuchita
@MaryPanje2 ай бұрын
❤keep it up
@GeraldMustafa2 ай бұрын
The DC ❤❤❤
@EMILYKAWALANGA2 ай бұрын
Ndipo kukasiyako akuchita kulandila ma 1 milion koma chikhalikenicho kwinaku analemba kut anthu azilandila 150 paka pano ndalama anthu sanalandilebe koma kwao anthu akuva kukoma munthu woipa uyu akungoona kwao konkha