If Marry Chilima is to stand as UTM president I do see Dr Joyce Banda supporting her I do see 90 percent of candidates supporting her I do foresee a landslide and the rise of a new dawn. Vote Marry Chilima...... Ma Bishop please approach this woman please she's our last hope.
@edsonwolemba30119 күн бұрын
Cashgate leadership
@AllanaChiphazi9 күн бұрын
😮A Joyce Banda ayiwala cashgate hahaha
@MsondaBanda8 күн бұрын
Chaboza ichi
@billymhoni95278 күн бұрын
Mai mary is the Key for UTM malawi...
@MuhireDominic-rw4vf8 күн бұрын
That woman bolaninso m c p 😂
@MisheckAselo8 күн бұрын
Kkkkkk zoona Mr DC kungong'alura 🎉🎉🎉
@RaphiqueYusuf8 күн бұрын
Koma Bon Kalindo ndikuyamikireni mumatsatiradi,zowonadi mayiyu walankhula mopereka chiyembekezo kwa anthu osawuka.
@ChristinaMdeza9 күн бұрын
Bring moreee!!! ❤
@DickisonyusufChiwalo29 күн бұрын
Pls joyce banga send bus south Africa we are seafaring here boma lakuno likutigwila ndikumatibvutititsa chonde tumizani mabasi aboma pumani boma pls pls
@fortunekamdumli-xy5zn8 күн бұрын
Kamala Harris sangawine
@anthonynkhoma42659 күн бұрын
Kalindo is a confusionist. He can't tell you the truth. He hates the current leadership bcause he was not given minesteeial post. Kagwere uko ndi dpp yakooyo
@AhamaduKareem-x5y9 күн бұрын
Zoona bwana
@GospelSoldiers-sr7np9 күн бұрын
Komatu ndi Mai Joyce Banda yemweyo amachemelera chakwera
Cashgate,kugulisa ndege mai emwe anaononga dziko la Malawi kwa nthawi yochepa bola Chikangawa emweyu than Joyce Banda😂😂
@PrinceThom-pe6ie8 күн бұрын
Koma iwe ndi Nyani WA MUNTHU.
@hamissimdoka96658 күн бұрын
Kulepherako sikuti alephera onse iyeyo Joyce Banda sikuti anali mu tonse alliance momo. Ndiye lero akubwebweta chani misala eti
@AndrewChirombo9 күн бұрын
Mai amenewa simunthu wabwino akunama amenewa ndi nthila kuwili saziwa chimene akufuna
@Blessings-b7h9 күн бұрын
You're right ndi mmai oipa kwambiri.
@georgeraphael81988 күн бұрын
@@AndrewChirombo mai wakuba wakupha
@SteveZimba-e8s8 күн бұрын
Koma born karindo uku ukunena zoona ku utm ofunika kusogolera ndi Mary chilima chifukwa chilima sadasogolele dziko ndipo chipanichi chikhoza kumangidwa bwino imvani inu utm msamutaye Mary chilima ndi key wanu
@SlindiryLoveness8 күн бұрын
Iweso mutuwako sikuyenda bwino satana iwe bwanji uzingolimbana ndi dpp yakoyo zazii zimene ukuyankhura
@DeviLinya9 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤
@FebbieNjewa-g3k9 күн бұрын
Bola asdzalowensenso cashgate,,,codzadziwa mcipande poomola
@chadreckchibwithala14939 күн бұрын
u don't know ndale nayi banda ali ndi mcp u must know that. adpp munya akalindo ali busy pa ganyu wawo