BON KALINDO LERO PA 29 JANUARY WAIPHEDULA NKHANI IJA NDIPO ENA APA NDIYE BASI AYALUKA

  Рет қаралды 41,459

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 56
@abgi.doctor.august
@abgi.doctor.august 8 күн бұрын
The DC Boooon Kalindo mukamati makape mukuwalekeza komano muziti ife a Malawi ndife amasikini ma street kids ndiye ifeyo president mwanthu ndi ochitisa manyazi kwambiri tipemphere Kwa Mulungu kuti president amene akutenga boma pa 16 September 2025 azatikonzere mavuto osanenekawa
@ChisomoYosefe
@ChisomoYosefe 8 күн бұрын
exactly
@ChrispineMuzungu-l8h
@ChrispineMuzungu-l8h 8 күн бұрын
First comment I come in peace the DC 🎉🎉🎉
@chirwaellace1093
@chirwaellace1093 7 күн бұрын
Keep it up vitu
@GabrielKbanda
@GabrielKbanda 7 күн бұрын
Olaruwa,,,,,,,VA mcp this is my Malawi amene amagwira mbendera ya Malawi SAOPA TIDZAFERA MBENDERA IYI
@akilaentertainment1993
@akilaentertainment1993 7 күн бұрын
Timakutsatani daily I hope tsiku lina malawi azakhala okomela tonse
@JamesPhilimon-h2w
@JamesPhilimon-h2w 7 күн бұрын
Inetso l appreciate Vitumbiko Mumba for everything he is doing
@user-hh8eu8dr4u
@user-hh8eu8dr4u 8 күн бұрын
We lucky to have you brother, you stand on justice, you fight for the people
@SmeldoBlack
@SmeldoBlack 7 күн бұрын
Mwana oophwya kwambiri 😂😂😂😂😂
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi 7 күн бұрын
Good job Minister vitumbiko mumba
@NellieChikuse
@NellieChikuse 7 күн бұрын
Ambuye bwerani mudzaweruze dzikoli😢
@GraceShaibu-i9d
@GraceShaibu-i9d 4 күн бұрын
Makape a MCP 😂😂😂😂😂
@MathewsMakalan-l6v
@MathewsMakalan-l6v 8 күн бұрын
The dc mwana oipa kwambili auzeni anthu awa osava aphaso wao yemwe kuntyolo anthu opanda chisoni awa auze born kalindo the dc
@SanudiMeleka-b2j
@SanudiMeleka-b2j 7 күн бұрын
We're on your back bra Umakwana ❤
@JimmyMzozoma-c7q
@JimmyMzozoma-c7q 7 күн бұрын
Zooona ADC
@MartinMajola
@MartinMajola 7 күн бұрын
Auze makape mcp mbava Zoka zoka
@Stankioiddrissah
@Stankioiddrissah 7 күн бұрын
Siumatipasa mayskho amavuto athu ndiye utibalalisa tiuze zochita titan
@MussWalasi
@MussWalasi 7 күн бұрын
❤❤❤❤🎉🎉🎉
@AlexanderBaluti
@AlexanderBaluti 8 күн бұрын
Chikangawa akukatenga balance ya nyanja..kodi munthu angakulande nyanja ndikumapita konko🤔🤔
@ElediyaWatch
@ElediyaWatch 7 күн бұрын
Ulemu wanu the DC
@Bbbbwesgtcjoug
@Bbbbwesgtcjoug 7 күн бұрын
Bola Inu olemeranu simupempha koma kunyoza mwezi ukatha kulandila bola mimatha man koma lapani msanga yesu amakukondani ndale sitidya ndipo ndale mulibemo chipulumutso sorry 😅😅😅
@ChimwemweMathyola-q7w
@ChimwemweMathyola-q7w 7 күн бұрын
Siku lililose timakusani ulemu
@MastonChabwera
@MastonChabwera 7 күн бұрын
Ndipo Vitumbiko ndinduna yokhayo ikugwirantchito yokomera amalawi
@RaphaelChiwisa-c4u
@RaphaelChiwisa-c4u 7 күн бұрын
Power to the people 💪
@ChifundoFrazer
@ChifundoFrazer 7 күн бұрын
Auze chilungamo agalu okuba amenewo 😂
@AlexKaudzu-l9k
@AlexKaudzu-l9k 7 күн бұрын
Koma zomwe akupangira achakwera wa akufuna kuwongogeratu dzikoli kuti obwerayo adzakhaule chani
@GeofreyChintabwa-ed8sk
@GeofreyChintabwa-ed8sk 7 күн бұрын
Gang gang
@TamandaSoko
@TamandaSoko 7 күн бұрын
Kaimeni a kalindo pa dpp compagn mwaipangira kokwana
@rittakawiriza
@rittakawiriza 8 күн бұрын
Kmanso zikhale chitsaznzo chachikulu Kwa anzathu otsutsa boma Kuti akalowa m'boma adzagwire ntchito mmene minister Vitumbiko Mumba akugwira ntchito yapamwamba Ambuye Mulungu okha azimudalitsa nthawi zonse ndipo azimutetedza
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 8 күн бұрын
Of course ndi zabwino zomwe akupanga V_Mumba,, koma tiganizilenso anthu omwe akuchotsedwa ntchito chifukwa cha kutsekedwa kwa ma Company,, Zisankho zayandikira tiona ma busy,,, MCP yapanikizika.
@BenitoCazota-q6u
@BenitoCazota-q6u 8 күн бұрын
Kodi ndalama zopitila ku Tanzania ko chakwera wazitenga kuti pakuti ku malawi kuno dollars kulibe?
@jameskatola4522
@jameskatola4522 8 күн бұрын
Ku reserve bank ziliko
@Vincent-x6m5n
@Vincent-x6m5n 8 күн бұрын
Mumba akuigwila
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 7 күн бұрын
Maudindo akufunika anthu achinyamata osati achizikhale ng'oma that why vitumbiko Mumbai akuchita bwino, generation iliyonse imazilamulila yokha
@LenadiMthandi
@LenadiMthandi 7 күн бұрын
Ai tiona kumene kupite Malawi chifukwa tafika potopa nazo
@ShamimuBisani
@ShamimuBisani 8 күн бұрын
Let me laugh in Swahil any way Kalindo our freedom fighter
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 8 күн бұрын
Kalindo mumatiyankhulila osaukafe ..mcp no more in 2025: anthu oipa zedi
@BysonPhiri-gu4io
@BysonPhiri-gu4io 8 күн бұрын
The DC 😅 mwana oopsa kwambili
@MathewsThugho
@MathewsThugho 8 күн бұрын
Winana wachita kumanga nyumba ku airwing ngati nyumba zaziphuzisi koma zilinyumba zake kom kumalawi
@judithStuwart
@judithStuwart 8 күн бұрын
Anthu aku mpoto ndi anzeru or simmawasankha kukhala president
@LetshaChirwa
@LetshaChirwa 7 күн бұрын
Kkkk km yaaa kukhalila kupepha bambo wamutundu wanji
@MissCaddy-yh7wd
@MissCaddy-yh7wd 7 күн бұрын
I really hate the mayor of Lilongwe, a very fake woman nde okonda ndalama. Anthu ambiri amawadandaula both okuda ndi amwenye omwe, sindinaoneko munthu wadyera ngati mzimai amene uja. Eish!!!!
@morgankaponda3945
@morgankaponda3945 7 күн бұрын
Nonsense! Ma pensioners akuvutika mu boma la congress. No gratuities. Akungofuna kubera ma company basi.
@ChingotopeJailos
@ChingotopeJailos 8 күн бұрын
Ine ndimafuna ndimve Yama ARVs ndye mwat tramp wait bwanji
@tungwaprecious
@tungwaprecious 8 күн бұрын
BAKILI MULUZI TV
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 7 күн бұрын
Akufuna anthu timwalire......chifukwa cha ulamuliro opusa wa Chakwera
@RichardAlick-o8k
@RichardAlick-o8k 8 күн бұрын
The DC
@BlessingsMuhaliwa
@BlessingsMuhaliwa 7 күн бұрын
5 years popanda chochitika
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 8 күн бұрын
What benefit acrues we , Malawians if our political and religious leaders are viliacos and cupidity diehards ???
@StigaraAfick-o2x
@StigaraAfick-o2x 8 күн бұрын
bon ku mcp kulibe wazeru kupatikiza ndi chakwela emweyo wazeru aliko ndi nduna ya zatchjto vitombiko basi
@greemynkhoma8886
@greemynkhoma8886 7 күн бұрын
Akalindo tinatopa nao ndikape weni weni uyu
@ChikoMasapula
@ChikoMasapula 8 күн бұрын
Chatsala Ku state House ndi chigololo😂😂😂 EEE zoopsa
@MathewTizze
@MathewTizze 7 күн бұрын
The DC
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 7 күн бұрын
The DC
@ISAACZOWAN
@ISAACZOWAN 7 күн бұрын
The DC
BON KALINDO LERO PA 06 FEBRUARY
19:03
Makosana
Рет қаралды 6 М.
Quando A Diferença De Altura É Muito Grande 😲😂
00:12
Mari Maria
Рет қаралды 45 МЛН
coco在求救? #小丑 #天使 #shorts
00:29
好人小丑
Рет қаралды 120 МЛН
BON KALINDO LERO PA 05 FEBRUARY
16:56
Makosana
Рет қаралды 27 М.
Ben Longwe Kuyankhula Za Ku Chikangawa - Part 3
21:04
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 11 М.
BON KALINDO LERO PA 04 FEBRUARY
16:12
Makosana
Рет қаралды 35 М.
Quando A Diferença De Altura É Muito Grande 😲😂
00:12
Mari Maria
Рет қаралды 45 МЛН