Born kalindo ndi activiits okwanila keep it up more fire
@augustMag11 күн бұрын
Mr Bon Kalindo kuikunena zoona president Chakwera palibe chimene akuchita mdziko muno la Malawi lafika powawa popweteka Ambuye atimenyere nkhondoyi 2025 achoke vote yanthu Amalawi imuchose munthu osaganizira aphawi tchito kugawa ndalama Kwa anthu akwao kukasiya the DC Boooon Kalindo president wa aphawi ku Malawi the voice of Malawi 🔥🔥❤❤❤❤
@isaacchiwaula73111 күн бұрын
Muuzeni born kalindoyo kah adzaimire pa mpando wau president mudzamuvotere kut adzakuomboleni mavuto omwe muli nawowo tione ngat iyeyo adzakwanitse kulamurira anthu
Ndikanakhala ine mayi osiyidwayo ndikanapanga zoti president ndi gulu lake akanandidziwanso. Amalawi ndi opepera kwambiri kufasa kwa mtundu wanji? Uzimu chani?
@NancyBanda-g2j11 күн бұрын
Atha kuphedwa Mary ndie akuopa KUsia ana paumasiye src
@Kabwilachikangawa11 күн бұрын
Okufa saopa kuola
@dysonmasiye573610 күн бұрын
Ndikanakonda mai Chilima abwere poyera kuti akapikisana nawo ku convention. Koma ndithokoze kuti nthawi zonse mmawauza anthu zofunika koma makutu awo ndi ogontha.... Kunena zoona atangoti maiwo akapikisana nawo ndipo atha kuwina koopsa cos alibe mbiri zoipa ai and alinako kuthekera kupotitsa patsogolo dziko lino
@ishmaelsiffah990011 күн бұрын
Generation yathu ndiyomvetsa chisoni,mwina ndikusawerenga history,taonani achina Kamuzu,kwame Nkuruma,Nyerere,Mandela anamenyela ufulu wao alindizaka zochepa, remember 16 June ku South Africa inali ya achinyamata,ine ndimaona ngati achina Kamuzu anamenyera ufulu pothana ndi atsamunda,zimene zija zinatheka atsamunda amkatiphinja aja anathana nao,lero ikutiphinja ndi corruption ndimaona ngati tikanadzuka ndikuwauza atsogoleriwa kuti enough is enough katangale watizunza mokwanira watikwana kuyambira pano palibe apangenso zakatangale zakezo tithana naye tokha
Kodi mmalawi muno tiziikana mma udindo chifukwa cha chisoni? Aliyense akuziwa kuti UTM si chipani koma movement, ndipo movement singakhale ya kubanja kwamunthu. Komanso Mary Chilima sananenepo kuti ali interested ndi za ndale. Don't force her, azachite kupanga chiganizo mwiniwake. Kukhala mkazi wa munthu wa ndale sizitanthauza kuti nawe ndiwandale
@Kabwilachikangawa11 күн бұрын
😂😂😂😂 awanso
@ThomasMlowoka11 күн бұрын
More fire 🔥🔥🔥 The DC 💪💪
@CaptainNyenga11 күн бұрын
I get you DC😢 merry chilima should stand as UTM candidate
Apa zafikapa kungopita kusiteti house kuchotsa zake zomwe wazisiya popita ku chaina zo dziko likhale mwanja mwa ansilikali mpaka patsiku livota bas
@Kabwilachikangawa11 күн бұрын
Chokani apa mmangoyankhula tiyeni kunseu ntooo osatuluka
@Kabwilachikangawa11 күн бұрын
Asilikali ake ati? Oliza mikonono ndi masana omwa? Fools
@Martinmkapangakapanga11 күн бұрын
iwe born kalindo ine ndinanena kale kuti pamalilo achilima anthu ena ankayakhula mwa mphamvu koma pano kuli ziii atangoyika malilo dziko lamalawi lovesa chisoni
@MarkShuva-jq8iz11 күн бұрын
Phindu la chilima yomwe tikuziwa ife ndi campain yomwe anamuika pachulu Chakwera,
That's true Kalindo.mayi Chilima atengeko mbali ndi yogwira kwam6
@christinaguliguli9 күн бұрын
Kodi ndiposo mademo mmakapempha kaye kwa DC kuti chani amenewo si ma demo omwe tikufuna ife inu mukuona ngati angalore akudya ndalama zochokera konko? Tiyeni tichite mademo osaleletseka atiphe atiphe ineso zikundiwawa kosalekeza usiku ndikagona ndikungoganiza zaupandu,mundisamaletu mwamva anyani inu
@HevenChiwaya11 күн бұрын
Mr Kalindo inuyotu muyesese kuti muwapulumuse aMalawi chifukwa ndiinu nomwe munapangisa kuti a Malawi azikumana ndi mavuto omwe akukumana nawo lelolino popanga ma demo ndi Chakwela wanuyu...
@user-gp2zp2dj1w11 күн бұрын
Chakwera chitsiru Cha president
@JamesBhiwhymilanzi10 күн бұрын
It's nice ❤
@BrightNamoko11 күн бұрын
Kkkkk Nkhan nd way forward Tiuzen titan
@ChisomoPachanya11 күн бұрын
Tamuudzeniso DC kuti kuno ku South Africa amalawi ambili ali ma prison kumangidwa kamba ka mapepala please amalawi ambili akuvutika kwambili ma prison akuno atipemphele ma transport
@MACKDBandah11 күн бұрын
Amalawi azanga chonde mokupephani ndimafuna number ya Mr president Bon kalindo chonde tanditumiziren chonde kose komwe muliko amane ali ndi number ya a president anthuwa Mr bon kalindo ndithandizeni mopepha chonde
@BeatriceLilemba-ww6cb11 күн бұрын
The DC my vote🔥
@LucyEndmond11 күн бұрын
More fire 🔥🔥🔥🔥🔥 the. DC👂👂👂👂
@maryphiri240911 күн бұрын
Bodza lokha lokha ilo musamumvelele palibe iye cimene angakuchitileni zaboza
@johnkatapeh718211 күн бұрын
❤❤❤ the DC
@alicechinyama415511 күн бұрын
Pajatu African national parks ili mmanja MWA mdzukulu wa kwini kubmangalande
@HalimaMtewa11 күн бұрын
The DC more fire agalu amenewa akutizudza kwambiri
@EstherChimalizeni11 күн бұрын
Ing'alule fada
@DavidMsokera11 күн бұрын
Khani ya infa ya chilima ambiri mulungu odziwa za kumwamba ndi pansi akatiweluza chifukwa chokwelezera kusavana pakati pathu, chifukwa iye ndi amene alimwini chilungamo
@DavidKajawa11 күн бұрын
More fire baba kalindo
@MalitaKapesi11 күн бұрын
Abale tatiyeni tipange zoti chakwela asabweleso ku China kwake wapitako aaaaa tatopa naye uyu
Good messages the DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC bon kalindo 🇲🇼
@KosmasMunthali11 күн бұрын
Tichotse ng'ona gyz😂❤❤❤❤❤❤❤❤❤😂😂❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@rhodamaunge-uq5dz11 күн бұрын
Mcp angoizimisa isazapezekeso mmalawi A mary pamoz ndi akubanja tithandi zeni
@NormanMwale-g1i11 күн бұрын
More fire Bon!!
@DavidMsokera11 күн бұрын
Mh, infa ya chilima yapezetsa anthu zokamba, koma amalawi adzayankha zosezi kudzera mu voti yao, ndipo nkhani imenei mh yakwana guys, and only God knows
@ConlardNkhoma11 күн бұрын
Mkufuna kt akhale nkazi wanu? Kkkkkk
@sulleahmnyimbili136211 күн бұрын
Mmmmm koma the way mmene anafera Chilima I don't think angapange zandale izi
@aarondickson7011 күн бұрын
Bon talk about the truth of tea pluckers who are employed in two weeks contact, can they send their children to school with the cash of two weeks contract ?
@Danp-q4n11 күн бұрын
Big up a dc
@ShrenkieNgoni11 күн бұрын
Mary chilima 💙
@PartsonMdeza11 күн бұрын
akut muchira 😂😂😂
@VanessaHale-v7x11 күн бұрын
Zowona bwana
@yotamumahomed131311 күн бұрын
inenso ndikudabwat kut Mary chilima akupangapo chan pa imfa ya chilima
@Kabwilachikangawa11 күн бұрын
Ali duuu
@GladesMhango11 күн бұрын
Zoonadi the DC
@danielfaylosi266111 күн бұрын
komatu kufa samaferana bwana DC olo inu simugafere akazanu atamwalira