A day is never complete for me if I do not listen to what the DC has to say. I always look forward to hear his talking points, views, suggestions and general advice.
@HappinessKapombeza-ut9mo10 күн бұрын
That is really truth.....BIG UP BRAZA....!!!!
@sollomavenda82839 күн бұрын
Yoh right brother
@user-yt8lv6cq3k10 күн бұрын
Mufune musafunee born kalindo asakhara president believe me this is our future president if you like it or not born kalindo is going to be president one day 🤞🏽🤞🏽🤞🏽
@alexandermeke699410 күн бұрын
Mbuzi ya anthu opusa ndi opanda mzeru nzanu ndi ameneyi
@JoyceBanda-k8t10 күн бұрын
Or atakhala mbuzi its better than crocodile yemwe akungodziwa kupha anthu kuba komanso kuononga
@Okalekale9 күн бұрын
Kkkk,Koma Malawi analowadi mphepo,Uyuyu akhale president zoona?,anthu anzeru zawo ophunziranso ali kuti,Malawi si pamajigatu?.Komanso awa ndi antchito a Peter Muthalika.Ikadzawina DPP adzapatsidwa udindo m'boma
@alexandermeke69949 күн бұрын
@@Okalekale misala imeneyi chamba chili thooooooooooo
@Memoryphiri-rm2gl10 күн бұрын
The real freedom fighter
@Drmuhammadchiwona10 күн бұрын
Komatu mr plezident mukunenepa sopano we malawias we love you plezident
@alexandermeke699410 күн бұрын
President wa ma bodza ngati abambo ake satana plus APM wopha malubino😅😅😅😅
@AlexGomani-ss5nj10 күн бұрын
You are the true fighter mr DC!! your our Samson here in Malawi,. May God continue protecting you until we have rescued from this crockdile's mouth...
@user-pz4py6ew6z10 күн бұрын
Watching from SA the freedom fighter Indeed ❤❤❤ mulungu akutetezeni boss
Am agree kt report anatulutsali ndi lopanda pake and pamwamba pakuti it's istupit ine mkuti ndizamanyi ndibwino akangokhala chete chabe,a pule kumwambaku ku Mulungu yemwe dzina lake ndi YEHOVA analenga diso lanulo sangalephere kukuonani.
@RhodneyBwa38 күн бұрын
BON KALINDO NDI MUNTHU WABWINO KWAMBIRI KEEP IT UP MY PRESIDENT
@JohnfosterNkusengwa8 күн бұрын
We need people like mr b kalindo in this country ❤❤ l really like the way this guy is doing and l wish if we can choose mr kalindo as a president in our country All the way from cape Town pa boma ❤❤❤❤❤❤
Tsiku la lero fees ya Ku secondary school kuchokera pa 7500 mpaka 40,000 school free
@user-cd4df3vg4y10 күн бұрын
Uyuyu ndi kamuna 😅
@Lazarus-qo1sl9 күн бұрын
Our president boooorn kalindo 🔥 sazatheka
@YusufuKaifa-r2y9 күн бұрын
I'm proud on you Mr president of born to suffer of Malawian people's
@LottiAffati7 күн бұрын
bigman tsopano bwana kalindo the dc mumatiimirira biggy
@HassaniKhenge10 күн бұрын
Mr DC timenyereni khondo kuipulumutsa Malawi
@joyahmedjoma461510 күн бұрын
0 pa 10 😂😂😂 anali wovesa chison chakwera ndi nkazi wache 😂😂😂😂😂chikangawa woyooooo😂😂😂
@FREZERMICHAELBANDA9 күн бұрын
Bon Kalindo following from Zambia
@GibohKatema8 күн бұрын
Fire bwanaa
@AbdulrazaqHussain9 күн бұрын
If we know the difference between politics and economics, we will enjoy as a country, our politicians they mix the two together, that's why we are in this situation
@ChristinaMdeza10 күн бұрын
The DC mumayima pa chilungamo inu ❤❤❤❤ Good bless you true story
@AngolanChinga10 күн бұрын
Munthu wamkulu ameneyo the DC
@Okalekale9 күн бұрын
Iwe usatinamizepo apa iwe Kalindo,zolinga za gulu lanuli ndi zolinga za amene amakupangani sponsor,amakupangani sponsor ndi ndani?
@GeraldMustafa10 күн бұрын
🤣🤣🤣 Dzaka 10 pa u president koma ziliko the DC!!!!!!!
@SamukLungu-zg7fl10 күн бұрын
Kuyankhura kwa zeru kumeneko
@AbdulrazaqHussain9 күн бұрын
All in all, the DC is right, politicians think politics is a self riches garden
@IshmaelMkwanda9 күн бұрын
Kuyankha mwandiiiiii DC ❤
@pauljosephmakaula683510 күн бұрын
Munthu wa nzeru zachibadwidwe
@Andrew-mr5kp10 күн бұрын
The nyonyolido mwana wakwathu umakwana
@Abdulla-y9t10 күн бұрын
God bless the DC
@paulinekayuni162110 күн бұрын
Ndipo zodabwitsa ndege inyamuka bwanji opanda zipangizo ngati zimenezo President amayenera kufusa responsible people zimene akufusa Kalindo
@MrThomas-j9d9 күн бұрын
More 🔥 fire Mr BK ngaluleni Ameneyo
@CassimWasotso10 күн бұрын
😂😂😂😂😂 DC mumandiwaza
@SolomonNjolomole10 күн бұрын
The DC pangoline our representatives and freedom fighter ❤❤❤
@HendersonDziwa10 күн бұрын
Aborn ambuye akutetezelen kwambili mumati imilila
@user-nd7hy6st4j9 күн бұрын
A Kalindo andikumbutsa nzathu wina wake apolice anamugwira atangofika kumene kuno ku South Africa anatuluka kundende after 2 months anakabwera qanenepa anthu osamamudziwanso kkkkk pano amangoti mukunena uja ananenepera ku ndende uja? Kkkkk😂😂😂😂
@WillmotChiuimia-vr6ou9 күн бұрын
Yes Mr DC bon kalindo❤❤❤❤
@GreatConqueror-xx3vi7 күн бұрын
Mwayankhura bwino ndipo zanzeru kwambiri
@gkay-striker9 күн бұрын
The only thing I love about this guy chimayankhura without fear keep telling them the fact
@PempheroMoleni10 күн бұрын
Ameni born kalindo mulungu atimenyela nkhon 🙏🙏🙏🙏
@CharlesSelemani400008 күн бұрын
akulu bola musadzasithetu kukhala ngati mtambo uja.Enafe timakunyadirani ndithu muli ndi fundo za bwino.
@MercyMfune-dc3rq10 күн бұрын
Watching from S.A.
@user-jd9yz5hp7y10 күн бұрын
The one and only the Dc💪🏼💪🏼💪🏼
@MsondaBanda10 күн бұрын
Kkkkk Simbi zikulu
@ThomasStephan-tg6ng10 күн бұрын
the DC umakwana
@GodfreyMzembe-b3n10 күн бұрын
Kodi bwana kalindo sumungayimireko u president
@alexandermeke699410 күн бұрын
Aaaaa a alibe mzeru awa chamba chili thooooooooooo 😅😅
@user-iw6cz5ft2l10 күн бұрын
machine opangira machine amzake more 🔥🔥🔥
@AmonNgoma-c4h10 күн бұрын
Mutiyimile mr Born Kalindo as "PREZIDENTI",2025 .coz nzanuyu mmmm😢
@user-mv1wg2qd6i9 күн бұрын
Kaswiri kwambili DC
@user-yj8ez7dd3o9 күн бұрын
Mbala iyi wachita kunenena ekha kut akufuna kuthandizila zipani zina ndiwa bodza uyu akumatinamiza kwambir,ungadyese anthu osauka chisiru iwee nyapapi iyi ndi mtambo sakusiyana zao ndi zimozi
@mayesojameskatete9 күн бұрын
MCP inapha chilima ndianthu ena Aja basi palibeso umboni wina tikuufuna apa
0/10 is not a fair judgement. Attacking the president as a person does not help anyone including anthu ngati ife who will vote not for a political party but capable leadership with sound developmental policies. Abale we need not be misled by people who are promising us heaven so that they can get in on our ticket then to further their political growth . This is home to all of us . These drama issues will not build a nation.
@WarriorKB-u3k9 күн бұрын
Chikangawa lipoti limeneli ukawuze abambo ako iwe ndichisilu kwambiri ukutitenga ngati Amalawife makape eti? Uchoke gwape iwe 2025 A.P.M boma osati iwe,gyz ku Malawi kuno kulibe pulezidenti ichi ndi chisilu timuchotse