BON KALINDO THE D.C 4 JULY 2024

  Рет қаралды 24,142

Club Junta

2 күн бұрын

Пікірлер: 106
@jamusnamwino-br2iz
@jamusnamwino-br2iz 2 күн бұрын
munthu amene amadana ndikalindo ndifiti kwambiri Kalindo amatiimirila ife amalawi
@ElasonAimon
@ElasonAimon 2 күн бұрын
Kuyankhura molikonda zdiko mowakonda a Malawi mulungu apitilize kupatani mphavu Komaso madalitso ochuluka
@ChristopherMadulira
@ChristopherMadulira 2 күн бұрын
The DC mwana oopsaaa kwambiri gwilan ntchito boss
@MosesKalenge
@MosesKalenge 2 күн бұрын
💔💔💔
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 2 күн бұрын
Kuyakhula mwatchutchu bon ❤
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 2 күн бұрын
Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
@joyahmedjoma4615
@joyahmedjoma4615 2 күн бұрын
Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
@user-wu8kp7ui5j
@user-wu8kp7ui5j 2 күн бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 2 күн бұрын
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting. Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
@lameckmajiga5426
@lameckmajiga5426 2 күн бұрын
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 2 күн бұрын
Mr pangolin tatulutsireni ndodo ija achinagwenembewa
@omanm2919
@omanm2919 2 күн бұрын
❤❤❤❤ The DC nthawi zonse kuima pa chilungamo. Ndipo chilungamotu sichimawopsa stand with u all the time
@chirpykachingwe6802
@chirpykachingwe6802 2 күн бұрын
Munthu uyu amenyela nkhondo Malawi it's up to you Malawians kukhala mene mulili olo kutengapo step
@JumaKachala
@JumaKachala 2 күн бұрын
Nkhaniyo ndiyowona
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 2 күн бұрын
I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi.
@joyahmedjoma4615
@joyahmedjoma4615 2 күн бұрын
Ndipo message ya apolice ndi iyi mukazagopezeka mukutenga bali ya chakwera uzazima sitikuchedza pa 10 ok we need change our Malawi 🇲🇼
@user-xc1gk6bw6m
@user-xc1gk6bw6m 2 күн бұрын
Powerful massenge fadah ❤❤
@DONOR265
@DONOR265 2 күн бұрын
Za ma hca zo ndee eeeeh zavuta zedi
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn 2 күн бұрын
Anabwelatu pa shop yanga ndi nfuti akuti kuzatolela ndalamaya nsongo kkkk mpaka mfuti tiziwopa zomwezi?
@twavysibale4751
@twavysibale4751 2 күн бұрын
The dc ..mwana owopsa kwambiri 🤣🤣
@AliciaMaphanga
@AliciaMaphanga 2 күн бұрын
❤❤❤❤❤ DC
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 2 күн бұрын
Ulemu wanu Malume ❤
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 2 күн бұрын
Nanga munthu oti anachita kukatengedwa ku Church angaziwe kulamulira dziko? Ndinkona amangolembana mbutuma zokha zokha
@FrancisGama-qb7ze
@FrancisGama-qb7ze 2 күн бұрын
Boma lokuba kwambri
@TecksonKaima-dr6er
@TecksonKaima-dr6er 2 күн бұрын
Oletsa zoyankhula zanu munthu wamkulu,ameneyo ndiye kuti ndi mfiti.mulungu akudalitseni bwana
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 2 күн бұрын
Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.
@user-pf5hu2pd2b
@user-pf5hu2pd2b 2 күн бұрын
Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 2 күн бұрын
Good Messnge my Bon Kalindo
@johnnyeliah4302
@johnnyeliah4302 2 күн бұрын
That's true Mr. D.C
@thomasbodo4099
@thomasbodo4099 2 күн бұрын
Boma la anthu opusa ma savage
@BashiluChimake
@BashiluChimake 2 күн бұрын
Ife2 tikudikila ndodo ituluke
@FrankFrancis-ch3xv
@FrankFrancis-ch3xv 2 күн бұрын
Yes!kodi izatuluka liti ndodo
@user-po6ir6eh4z
@user-po6ir6eh4z 2 күн бұрын
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
@user-ul1fb4yn5o
@user-ul1fb4yn5o 2 күн бұрын
The DC mwana woooopsa kwambiri
@MarthaJafali
@MarthaJafali 2 күн бұрын
Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti
@user-jw5rx9ze8k
@user-jw5rx9ze8k 2 күн бұрын
Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.
@MisheckSenga-q4i
@MisheckSenga-q4i 2 күн бұрын
Mmakwana boss mn
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel 2 күн бұрын
Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu
@lameckmajiga5426
@lameckmajiga5426 2 күн бұрын
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
@PatrickSamson-po7uy
@PatrickSamson-po7uy Күн бұрын
Umakwana
@VictoriaWilly
@VictoriaWilly 2 күн бұрын
Munthu wamkulu zedi, the DC
@dontreybanda278
@dontreybanda278 2 күн бұрын
Good massage boss
@McshonWilliam
@McshonWilliam 2 күн бұрын
Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯
@DanNzima
@DanNzima 2 күн бұрын
The DC!!!!
@MarthaJafali
@MarthaJafali 2 күн бұрын
Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele
@miraclekayira9613
@miraclekayira9613 2 күн бұрын
Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji
@BENSONRANGWANI
@BENSONRANGWANI 2 күн бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@Enock-c9l
@Enock-c9l 2 күн бұрын
A opposition afasa ngati Chilima
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 2 күн бұрын
The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 2 күн бұрын
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
@Leo-fj6gz
@Leo-fj6gz Күн бұрын
The Dc 👹👹👹👹
@GiftPhiri-tt7nn
@GiftPhiri-tt7nn 2 күн бұрын
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 2 күн бұрын
Nde nkhani zake
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 2 күн бұрын
Audio iyi yandikhudza kwambiri.
@user-ty4pq5ub3q
@user-ty4pq5ub3q 2 күн бұрын
The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.
@LazarusEvasonchafachaola
@LazarusEvasonchafachaola 2 күн бұрын
D.C ukhalise umatiimilila kwambil
@Pangolinimw
@Pangolinimw 2 күн бұрын
The DC
@GiftKananji
@GiftKananji 2 күн бұрын
Timakunyadiran bg
@user-ji4xn6me8d
@user-ji4xn6me8d Күн бұрын
Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 2 күн бұрын
Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen
@ZionekaMember
@ZionekaMember 2 күн бұрын
Iwetu akupasazo ukabweza
@dalitson3558
@dalitson3558 2 күн бұрын
Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 2 күн бұрын
The DC mwana olimba mtima
@rachidecaundealy8335
@rachidecaundealy8335 Күн бұрын
Assani,keti
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 2 күн бұрын
Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 2 күн бұрын
Amutuma kuti azasunzumile kuno Ha😅😅😅😅😅😂😂😂😂wanya nayo wadya ndalama zaulele
@JingaleMwafulirwa
@JingaleMwafulirwa 2 күн бұрын
Proud of DC
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 2 күн бұрын
Wi love you ❤❤ bon kalindo
@IsaacMusa-py2jm
@IsaacMusa-py2jm 2 күн бұрын
Powerful 👊
@lameckmajiga5426
@lameckmajiga5426 2 күн бұрын
Kod ma track ndi zida zoopya zomwe zinalowa m'muziko mwanthu zija zikuzatani! Kapena boma linagula zida zankhondo za M.D.F? Tatifufuzileni mr kalindo please! Otherwise chakwela atha kutigulisapo apa!!
@oscarchafulumira3127
@oscarchafulumira3127 2 күн бұрын
Dangerous child ❤
@YusufuKaifa-fr4wt
@YusufuKaifa-fr4wt 2 күн бұрын
❤❤❤❤❤ great full story poor DC
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 2 күн бұрын
Morning the DC
@AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
@AnnoyedFallingLeaves-zp8dy 2 күн бұрын
Nde mwati Yosefe anali wa number chani? Nanga Benjamin? Pilizi chonde!
@user-xt2ic5gg1g
@user-xt2ic5gg1g 2 күн бұрын
Joseph wa 11 Benjamin 12 walakwitsa pati munthu
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 2 күн бұрын
Timam'konda Dc,,,iwanawe ušamalimbane ndi Dc
@LimbikaniKadzongwe
@LimbikaniKadzongwe 2 күн бұрын
Amalawi tiyeni tikhale maso osalola zimenezo zoonadi ndikuba poyera
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni 2 күн бұрын
D c ❤️❤️❤️❤️❤️
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 2 күн бұрын
Powerful!!!!
@MartseMichael
@MartseMichael 2 күн бұрын
Mwana owopsa kwambili
@user-wb3us4pg4b
@user-wb3us4pg4b 2 күн бұрын
❤❤❤ The Dc
@user-eb2yo9bc9k
@user-eb2yo9bc9k 2 күн бұрын
Akudziwana onsewatu
@user-zg6mn8qr4m
@user-zg6mn8qr4m 2 күн бұрын
🔥🔥🔥
@macDonaldKuwani-zo3nv
@macDonaldKuwani-zo3nv 2 күн бұрын
💪💪💪💪💪 Bon K
@IssahTchakato
@IssahTchakato 2 күн бұрын
Ndipo Ine andikhomela pa shop akut ndisokhele 80
@user-nq7yv2lm6k
@user-nq7yv2lm6k 2 күн бұрын
❤❤❤❤❤
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 2 күн бұрын
Mcp boma lakuba kwambiri.
@Wellingtonphiri-op8pp
@Wellingtonphiri-op8pp 2 күн бұрын
❤❤
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 2 күн бұрын
Anganga
@kondwaniwhite2871
@kondwaniwhite2871 2 күн бұрын
Auzeni chilungamu
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn 2 күн бұрын
A DPP ADYA BANZI NDIIIIITHu!!?
@JunaKananji
@JunaKananji 2 күн бұрын
❤❤❤❤karido
@MasterHeadson-ki7ji
@MasterHeadson-ki7ji 2 күн бұрын
📌
@MussahSmart-wn5ue
@MussahSmart-wn5ue 2 күн бұрын
The DC umakwans
@user-uj9st8zp7v
@user-uj9st8zp7v 2 күн бұрын
Ndili pambuyo pako bon kalindo the D.C
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s 2 күн бұрын
Tingopita ku cort basi
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 2 күн бұрын
Dc
@AdamYas-ec9oc
@AdamYas-ec9oc 2 күн бұрын
Mumakwana kunena dzoona the dc
@homeremedys3748
@homeremedys3748 2 күн бұрын
Rest in peace Redson Munlo 😢😢😢😢😢. We love you the DC
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 күн бұрын
Boni kalindo watha basi
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 2 күн бұрын
Iwe usamalimakimbane ndi DC ukutaya thawi
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 2 күн бұрын
I stopped listening to this nonsense frm coz I don't see any profit
@MarthaJafali
@MarthaJafali 2 күн бұрын
Who told you to listen get out
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 2 күн бұрын
Iwe ndiwe chitsulu osangatuka bwanji ndani akukukamiza kuti uzimvela zomwe akunena bon kalindo musiyeni akutokota za nzelu zothandiza ife iwe unalandila ndalama kuti uzifowola anthu choka galu
@IsmailRahim-yy3yr
@IsmailRahim-yy3yr 2 күн бұрын
The DC
@GiftKananji
@GiftKananji 2 күн бұрын
Timakunyadiran bg
The day of the sea 🌊 🤣❤️ #demariki
00:22
Demariki
Рет қаралды 103 МЛН
Получилось у Вики?😂 #хабибка
00:14
ХАБИБ
Рет қаралды 7 МЛН
你们会选择哪一辆呢#short #angel #clown
00:20
Super Beauty team
Рет қаралды 10 МЛН
Nutella bro sis family Challenge 😋
00:31
Mr. Clabik
Рет қаралды 9 МЛН
Papa yeh dila do ajse mein aapki behen 😢😊 #shorts
0:30
Sikha shorts and vlogs
Рет қаралды 139 МЛН
Вор в законе заступился за официантку  ...
0:59
Сериалы 🍿
Рет қаралды 9 МЛН
Люди были шокированы от увиденного 🤯
0:29
Фильмы I Сериалы
Рет қаралды 3,1 МЛН
Sigma Kid Hair  #funny #viral #comedy
0:17
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 3 МЛН
Мама хитрая😂​⁠​⁠@ladymilanapap4610
0:16
МишАня
Рет қаралды 1,9 МЛН