Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
@joyahmedjoma46152 күн бұрын
Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
@user-wu8kp7ui5j2 күн бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@ChimwemweKondowe-nj4lx2 күн бұрын
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting. Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
@lameckmajiga54262 күн бұрын
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.
@user-pf5hu2pd2b2 күн бұрын
Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake
@user-nf3ik3ff6y2 күн бұрын
Good Messnge my Bon Kalindo
@johnnyeliah43022 күн бұрын
That's true Mr. D.C
@thomasbodo40992 күн бұрын
Boma la anthu opusa ma savage
@BashiluChimake2 күн бұрын
Ife2 tikudikila ndodo ituluke
@FrankFrancis-ch3xv2 күн бұрын
Yes!kodi izatuluka liti ndodo
@user-po6ir6eh4z2 күн бұрын
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
@user-ul1fb4yn5o2 күн бұрын
The DC mwana woooopsa kwambiri
@MarthaJafali2 күн бұрын
Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti
@user-jw5rx9ze8k2 күн бұрын
Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.
@MisheckSenga-q4i2 күн бұрын
Mmakwana boss mn
@ChrifordBiziel2 күн бұрын
Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu
@lameckmajiga54262 күн бұрын
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
@PatrickSamson-po7uyКүн бұрын
Umakwana
@VictoriaWilly2 күн бұрын
Munthu wamkulu zedi, the DC
@dontreybanda2782 күн бұрын
Good massage boss
@McshonWilliam2 күн бұрын
Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯
@DanNzima2 күн бұрын
The DC!!!!
@MarthaJafali2 күн бұрын
Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele
@miraclekayira96132 күн бұрын
Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji
@BENSONRANGWANI2 күн бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@Enock-c9l2 күн бұрын
A opposition afasa ngati Chilima
@user-fi7ko7bl6f2 күн бұрын
The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅
@hanifahmponda87112 күн бұрын
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
@Leo-fj6gzКүн бұрын
The Dc 👹👹👹👹
@GiftPhiri-tt7nn2 күн бұрын
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
@Extratremendouszeus2 күн бұрын
Nde nkhani zake
@SolomonNjolomole2 күн бұрын
Audio iyi yandikhudza kwambiri.
@user-ty4pq5ub3q2 күн бұрын
The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.
@LazarusEvasonchafachaola2 күн бұрын
D.C ukhalise umatiimilila kwambil
@Pangolinimw2 күн бұрын
The DC
@GiftKananji2 күн бұрын
Timakunyadiran bg
@user-ji4xn6me8dКүн бұрын
Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula
@user-gj4li2gc8o2 күн бұрын
Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen
@ZionekaMember2 күн бұрын
Iwetu akupasazo ukabweza
@dalitson35582 күн бұрын
Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku
@clintonhodda98302 күн бұрын
The DC mwana olimba mtima
@rachidecaundealy8335Күн бұрын
Assani,keti
@EllenPhiri-xt8pt2 күн бұрын
Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂