Dan lu, amadedwa kwambili ndi anthu amene sankafuna kut DPP ikhale pa mpando ... Popedza kut ambili amene sankafuna DPP anali anyamata ... Dan lu pokhala mnyamata anadana ndi anthu ambuli maka achinyama .... Dan lu ndioimba wabwino amene sankayenera kusikidwa ... . Zikanakhala kut dan lu ... Ankasapota UTM bwenz zisanachite affect music career yake ... Sindikut career ya Dan inaonongedwa ndi DPP ai koma kut panali kusiyana ndithu ... .. I come in peace
@tariroJinya2 ай бұрын
Palibe amene amamuda Dan lu
@GeorgePhiri-ub2of2 ай бұрын
answer Dan lufan amaimbila chipani choti anthu ambili kuchokwela pasi pa mitima yawo chipanicho amadadanacho mmodzi mwaiwo ndi ineyo basi khani yamala
@AeeshurQuenjieАй бұрын
Dan lu u r still my fav artist osadandaula kut ukudedwa ndi anthu worry when God abandon you coz I biliv God loves you more
@eusterkalunguАй бұрын
I like you Dan since I was 5 years yuh are my best musician
@hannahsitimandau91072 ай бұрын
Amamuchitira nsanje nyimbo zake ndi zobeba
@FloridaOssy192 ай бұрын
Zoonadi ❤❤
@ShamimuWilliameАй бұрын
My vote brother Dan lu Amamuda shifukwa shachilungamo amayimba saumboni dzoka dzoka love you Dan lu God bless you 🙏 amen
@emmanuelkennedy6389Ай бұрын
Khani nayi amakonda kuyimba nyimbo zoraura atasiya kuyimba nyimbo zaraurazi kubwerera chuni chake chakare zose zitha kubwerera chumake umatha kuyimba iweyo ndiwe number one osagonja ili ndi luso lomwe anakupasa mulungu pitiliza
@MtolaMbalaso2 ай бұрын
Amadele,chifukwa chakuti,Dan luu, amata, OK tangowona nyimbo dzimene anathulusa dzachipanidzo winandan angamakwe, palibe kumalawi kuno km Dan,yemwewo
@MussaMbota2 ай бұрын
Man dan luu ndimwana wabwino kwambili amadana nayeyo angokhala ansanje
@EuniseMasuku2 ай бұрын
Dan lu tandiponyeleko kanyimbo ka sanje ndiye mandigwilane imandimvesa🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@MaupoMhango2 ай бұрын
Koma enafe Dan lu sitikumuda ayi. Komaso nyimbo zake zimatisangalasa koopya akamati kuyamba nyimbo zake nkumati Malawian music Dan lu❤❤❤❤❤❤
@FloridaOssy192 ай бұрын
Ine ndimamukonda Dan lu ndip ndazamukondabe mpaka kale ❤❤❤
@BunayaSalanje2 ай бұрын
ine ndimakhonda kwambili ❤kupoza winaaliyese oyimba ku malawi ko 🇲🇼 achalume wachiyao wangalusa brother
@AdeelMusaahАй бұрын
I love u Dan no matter how people hate u I will be there for u 😥😥
@DeodataKachapiraАй бұрын
Mnyamatuyu amaimba bwino asavutike ndi anthu all days are not Sundays. Komanso akati mpikisano ndi umenewo. Ajetuwo alibe nthawi, go ahead vuto achinyamata ambiri ngakhale aziimba zoimbidwazo samamva
@DoresChisale2 ай бұрын
Ine nde ndmakonda mpaka Pano ndpo nyimbo zake ndmazikondaso Maka Maka ija ya Tulani pasi udindo ija eeee anapha 😊😊
@MaryBanda-n3h2 ай бұрын
Ine Maka ija yoti winaso ai eee ndimaikonda
@blessingkamanga17812 ай бұрын
I don't know that people hate Dan Lu myself I love him.
Kaoneni KZbin views ya nyimbo zake mupeza kuti Sam akukamba zoona muziitsata music paliponse not m'ma benning centre koma pa social media
@rainJCMw2 ай бұрын
Umangomuda ndiwe ine simamuona vuto ayi
@ChristopherKawilam2 ай бұрын
Ndat boza Ada Sam uyu Ali ndi sanje kwambilil
@AgnesMwale2 ай бұрын
Mungoti chili chose chili ndi season... Nanga rashly wakhala zii apa???
@HappyAbyssinianCat-xt2bm2 ай бұрын
Dan luuuu amamuda chifukwa ndi munthu ozindkira kunena zoona dpp ndi boma labwno alibe zambiri ngat mcp chipan chamagazi manja nde Dan luuu ndi nyamata oganiza bho❤
@sharifujoe76332 ай бұрын
All most amakhala oyimba amnzizawo ife kwatu kuyamikira any one amapanga bwino pa music industry
@DONNEXKhama-bk1gy2 ай бұрын
Dan Lu amaswa koopsa athu amachita .naye nsanje ali ngt mfumu payekha ... nyimbo zake Za chipan anaswa
@YoungScott-p7e2 ай бұрын
How about malemu Lucius Banda poti nayeso wakhala akuimba nyimbo zandale
@HypeGallery-ur9xd2 ай бұрын
Umamuda ndi inuyo ife timamukonda😊❤
@ApsChap2 ай бұрын
Sam Malvitha tikusika akapitiriza kuda Dan Lu
@GraciousBayard2 ай бұрын
Umboni ndi KZbin views ya nyimbo zake
@GraciousBayard2 ай бұрын
@@ApsChapSam mavitha akukamba chilungamo ngati simusata music ndi bwino kukhala chete
@BonomaliIman2 ай бұрын
Ngati dziko la malawi emwe anayimba nyimbo zabwi nzachipani ndi Dan lu bs nde tingamudele nji ife ma citizens iwe umamuda siife ayi
@KelvinChitwanga2 ай бұрын
Umamuda ndiweyo nde ukanati ndichifukwa chan munthu amamuda dan lu osat anthu! Wamva iwe
@JacksonNamalumbe2 ай бұрын
Alipo wakutuma kuti uziyakhula zopusazi ? Ife ukuziwa mene timakondela Dan Lu ( lozani zanu ife tiwone)❤
@SandikondaIsaac2 ай бұрын
Ilove danlufani and his music
@JusticeFriday-q1j2 ай бұрын
Muthu sakondedwaandi athu ose kom kwaenafe tiribe naye murandu amatisangarasq kuno
@MoosaSame2 ай бұрын
Ur first person to say that bro no one hates Dan lu
@LailoguntherElickАй бұрын
Amamuda kaya chifukwachan nanensosinziwa koma Dan lu ali fantastic 2 mach
Uja anaimba yoti tiyende pamodzi ndi mtima umodzi timayikonda mpaka lero. Kuna koipa kuimba nyimbo ya Peter panthawi yoti dzithu zikubvuta iye kumanjoya. Iyeyo amasapota Muthu amene amaszunza anthu ndipo anthu amamuda Peter amapanga mademo kusamfuna Peter munthalika.
@GraceMaida2 ай бұрын
Done ndimfana oti amatha ndiye timuda bwanji iweyo ndiye usamamuwonela kukondwa koma Done ndimbambande moooo fire Done we love you so much ❤❤❤❤❤❤
@Randy-er2xo2 ай бұрын
Ndimfana wabho ndilibe naye bvuto
@CASSIMDinala-z7e2 ай бұрын
Amatha nfanayu broskie
@shukurajaaffarie-cr2nm2 ай бұрын
Umamuda ndi iweyo osati ifeyo iwe sudziwa kut Dan ndi mu yao ? Ndie sundiwaso kut mchewa ndiwa sankho?
Dan Lu anakwera chipani cha anthu oipa osayamika komanso ozikonda. Vuto ndi limeneri. Muziwe kuti DPP inayamba bwanji nanga zonse zomwe zinachitika kwa anthu omwe anaononga chuma chawo nthawi yawo kuti bingu akhale pammpando zinawawa bwanji nanga abwenzi awo. Ndiye wina akaimbire nyimbo anthu awa avina? Amavina ndi kusekerera ndi omwewo a DPP chosatila chake Dan Lu ali mmazi. Olo nyimbo zake kukubwera kuno anthu adzasiya kumvera azamvere ndi okhawo akuwatamandawo
@mayesojameskatete2 ай бұрын
Ineyo ndimamukonda dan lu ❤❤❤ APM uja osazamuphwekesa
@Ghama-k4i2 ай бұрын
I don't know if there are people who hate dan lu coz us we love him
@IshumeilHaroon2 ай бұрын
Dan lu is the best
@RICHARDMAGWIRAАй бұрын
Iwe nawe Muthu sakondedwa ndi onse osangonena kt umamuda iwe bwanji
@PreviousStanley2 ай бұрын
Guys Moyo ndichoncho munthu amankhala ndi anthu omukonda komaso odana naye sizingantheke kukondedwa ndi anthu onse olo utankhala wabwino
Ada awawa amakamba chilungamo komnso kuima pa chilungamo so pajatu amalawi amadana ndichilungamo amakonda boza bas
@HappyBotha2 ай бұрын
Dan luu ndimunyamata oyimba bwino,,,that's y amamuda
@hanffyamizy27062 ай бұрын
Unayamba wapitako ku sho yake ngat
@GraciousBayard2 ай бұрын
Umboni ndi KZbin views ya nyimbo zake
@Hassanianusa-go9wv2 ай бұрын
Aaaa iwe choka kape iwe
@falliotphiri6882 ай бұрын
Dan Lufani Ali ndi Magazi a Blue, ndipo palibe oyimba amene Ali wa DPP. Kuposa Dan. Choncho amene amadana naye ndi adaninso a DPP
@Chiwaya-v6h2 ай бұрын
lne ndimakonda Dan lu ndip ndazamukondabe mpaka khale😊😊😊
@AliNtolera2 ай бұрын
Malawi amadana ndichilungamo komanso jealous chifukwa Dan lu amatha komanso ndiokongola samaoneka ngati mbuli za kumalawi
@DavieLosani2 ай бұрын
It's my first time kunva kuti Dan Lu amadedwa
@andrewchirwa21932 ай бұрын
Dan Lu ndiwoyimba wakulu so sakuyenela kuyamika andale aziyimba nyimbo zake woyimba akwathu ndale zikuwabwezelesambuyo🤷
@SmilingBurger-qm4oh2 ай бұрын
Dan lu amasapota andale amene anyamata akudana nao koma chosecho iye amayimba nyimbo zachinyamata mwachitsazo ulamulilovwa DPP umadana ndiachinyata ambiri koma iye akhayimba zochemelera chipanicho ndichifukwa ambiri adangomutulaka
@SamsonNyoma2 ай бұрын
Amamuda coz ol yandareyo Imakhala hit
@YusufDyton2 ай бұрын
Ngani ndiyakuti dan lu amawada anthu chifukwa choti ndi muyawoo ukaunika ku malawi ndi zikho losalana mituthu kuli monga D20, Dan lu,Bandera,ndi ayaoo ena km zakhondedwa ndi anthu akumalawi ayi
@DavieLosani2 ай бұрын
Iweyo udzinvela kwambili nyimbo ya Dan ,msanje.
@stevietungama97752 ай бұрын
Amamudela Zina ameneyo bwanji nkasa samadedwa
@edsonnyasulu5394Ай бұрын
Oimba ena sadedwa ndi anthu chifukwa alibe mbali ya chipan pomwe Dan lu akuwonesela kuti ndiwa dpp
@tamandanimaliro75192 ай бұрын
Umafotokoza zosaveka iwe ungosiya bola bakili tv
@JoevsJohn-fg6wz2 ай бұрын
Mmwe Ali Tongo sam malvitha mkulimana nazibambotu mwasene gakwiona,mufune Muthu Wina osati Dan Lu mungoyalukapo apa
@InnocentMaganga-gd6kn2 ай бұрын
Anthu amamuda chfkw nd oimba amene anaimba za ndale ndkupindula nawo pamene oimba ena onse mwanenewo palibe chomwe anapindula kuposa Dan lu😢😢😂😂
@SamboRuphan2 ай бұрын
Anyamata anyemba yemba (saymon and Kendall bwanji amayimba ya MCP,,,ndiye kuti mwangoeonapo Dan lu yekha 😂😂😂 zanu izo wakwiya akakolope nyanja😅
@owenmaseya69362 ай бұрын
Ndinu zitsiru kwambiri zifukwazo nde mwanena?
@ChikondiSabe2 ай бұрын
Amamuda chifukwa Dan lu ndi number one sangafane nawo, sanje ndiyowe yakula basi
@TheresaKuluwemba2 ай бұрын
Inetu ndye I love him kwambiri enawo ndizawonso!
@MikeAlabi-w2g2 ай бұрын
Iweyo Sam nddi amene umamuda Dan lu osati anthu enawo enafe timamukonda kwambiri ndiye siya uchitsilu wakowo
@muhammadisaid39682 ай бұрын
Komaso oyimba ambiri monga Billy , Banda bwanji samawaba , ndiye kuti anthuwo ndidzsilu
@MosesPinto2 ай бұрын
Anthu amachita mantha ndi dpp nde kuwawidwa ntima kwake mchifukwa amadana ndi dan lu
@MussaMalon2 ай бұрын
Kwayineyo dan lu ndi super power osamutuluka.
@EmmanuelGasiten-fo5dr2 ай бұрын
Ukakhala pa top, umakhala topic. Ndiye nkhani yaketu
@IvyMkhura2 ай бұрын
Amamuda Dan Lu ndiweyo, ife amatiwaza ndi kwambiri, amatha kuimba heavy
@SelemaniFred-rg9tt2 ай бұрын
Ine ndiye amandiwaza Dan lulu mnyamata wa kwathu kumangochi !!!! Kwa amene amamuda Dani Lulu ndiye kt amamuposa pachilichonse osamalimbana ndi ana osamba monga aku Mangochi ana olimbikira
@SmartMasauli2 ай бұрын
Ife timafila Dan Lu🔥🔥🔥
@OsmanRatbu2 ай бұрын
Yathu ija amalawi munthu zikamamuyendera sitisangarara imakura nd sanje dan lu amatha man ndpo kwambliiiso
@LaynaAdam2 ай бұрын
Akulu inuyo mukumana amene amamuda ali ndi zifukwa zawo osati chifukwa choti anaimbira dpp nkasa waimbira zipani zingati
@AsimaAndiwochi2 ай бұрын
Ine ndimamukonda dan ru
@CannyMpehla-d1s2 ай бұрын
vuto ndiuphawi kumalawi amamuda coz the man how is handsome komaso kuchimake kwa khutsa
@lacksonmanyewu36152 ай бұрын
Zoti Dan lu anthu amamuda ndi bodza lankunkhunidza
@InnocentChauwa2 ай бұрын
Tachoka naye patali Koma zomudazo mukuziwa ndinu kapena anakuuzani yekha
@MillyKachepa2 ай бұрын
Anthu akamakuda akuona zabwno za iwe kumangoyamika osamazitengera amakhala akukubersa madalitso ako
@JoevsJohn-fg6wz2 ай бұрын
Athu amaziwa Kut iweyo umamuda Dan Lu ndikuziwa munamufananidza ndi Dala wanu uja jetu iwe ndikaphe
@MatridaChikaphonya2 ай бұрын
Mtengo womwe ulindidzipatso ndumene umagendedwa don't worry Dan luu