Ayi ndi pamene mudzadziwe kuti ndale ndi zovuta kuti amusankhe kabambe running mate ku dpp bdi zovuta cause kueme kuja kuli mikhala kale nde apite ku utm cholinga akazapanga alliance kabambe azamutwnga ngati running mate wake fro m utm nde ndale zimenezo
Musiyeni kabambe apite but still more DPP yiwinabe whether you like it or not
@user-og4oe5yp4wАй бұрын
Akabambe akufuna upulesidenti ku UTM
@ShabaniKuswereАй бұрын
Dyera kabambe koma akuluakulu anthu andale dyera kuteroku waona kuti ku DPP mpando wautsogoleri saupeza ndeapapa mpungwepungwe omwe uli Ku utm ndi Dr Usi iye watengerapo mwai ofuna kukatenga utsogoleri. Koma chipani cha DPP sikuti chipangidwa affect chifukwa kabambe tsogolo lake la ndale silinayambe kuoneka
@ExcitedBreakingWaves-oh3zbАй бұрын
Mbava zokha zokha.
@user-xo8ms5wh2sАй бұрын
Kabambe akuthamangira ku UTM akufunako akakhale President sakudziwa kuti President wa dziko lino ndi Mutharika
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Aaaaa iwe usavutike ndi ankhalamba yakoyo kagwere
@dondamissonchdziwe3958Ай бұрын
Iweyo Ndiye wasalira mu tonse alayansi, Nonse amene mwasala mu tonse alayansi musama lire,muphesanso a Malawi ena
@Musa1828-l5dАй бұрын
Ife a UTM tatuluka chifukwa Chakwera anapha Chilima
@user-fi7ko7bl6fАй бұрын
Munapha mesa Chilima nde a UTM atuluka musanamalize koma akusiyilani Kamanganya ka yudas😅
@AndrewSimakweliАй бұрын
Boma lilibe masompsenya
@Musa1828-l5dАй бұрын
Kabambe alibe chikoka
@eliffagondewe8214Ай бұрын
Phuma koma silabwino.
@UsenLashidАй бұрын
Anthu akutuluka mwa alliance chifukwa chakwela akutenga ngati mpandowu anawupeza mwa iye yekha 2 alliance sakupeza mmphindu la alliance chakwela wangopanila yenkha zabwino zonse ndichifukwa UTM yatuluka yawona kuti wina wake wa phangila zose