Population ku north inali bwanjii Who called dead North Infrastructure inalibwanjii Why many people martyred? All these development you are saying North could have been better than central and southern Even Chilembwe did before kamuzu 60yrs of independence gravel road,are you serious? How much have you pocketed?
@KenChitete-pg3ws3 ай бұрын
Kamuzu Banda anali bwino chifukwa,kunali Admark ku Malawi kunali maphunzilo apamwamba kunali chithandidzo mwana akakeelela ku university amatengapo mbali ya school fees,,,zonsedzi pa ma president tsopano awa anapangapo chiyani?????
@KenChitete-pg3ws3 ай бұрын
Aliyense president amakhala ndi ubwino ndi kuipa,,,bakili muluzi anapha oyimba wathu wapamwamba kwambili,, Mr evison matafale,,,,abingo anapha mwana wa school,,,a Robert chasowa analakwa chiyani?????? A Peter Mutharika anaononga Malawi kwambili,,potisithila school yathu ya bwino chifukwa cha nsanje yake ya muntima chimuthu choyipa kwambili ndi brother wake anapanga kota sisitimu kuti aphe maphunzilo kumpoto ndikanva zina loti DPP ndimanyasidwa kwambili.