Fog wapha Chilima ndi osakhalitsa. Amalawi akulira maliro a Vice president.

  Рет қаралды 18,311

Human Rights Consultants TV

Human Rights Consultants TV

13 күн бұрын

Пікірлер: 32
@augustMag
@augustMag 5 күн бұрын
Mulungu wamphamvuzonse landilani mizimu ya abalewa amene mwawayitana kuti abwere pamaso panu Ambuye chifukwa Cha ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha long live professor Arthur Peter Muthalika God is chosing you again ❤
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 11 күн бұрын
APM deserves a big credit, we love you adad long live.
@user-qb4pj5yy5b
@user-qb4pj5yy5b 11 күн бұрын
Its good that people have come back to their senses APM ali moyo unlike Bingu, timazindikira ubwino wake atapita, long live APM
@JackMvura-ik2td
@JackMvura-ik2td 10 күн бұрын
Kodi a pm alowa UTM kapena akangolowa ndimutu kufuna mavote
@DAMZYLINJE
@DAMZYLINJE 11 күн бұрын
❤❤❤❤❤Ayi ndalila ine motsozi tsikana iwe Mulungu akudalitseni ndiwo anse omwetso ine ali mu mtima mwanga
@spargomw
@spargomw 11 күн бұрын
😭😭😭😭 misozi yosatha m'maso mwanga 😭😭😭😭 Chilima, Chilima 😭 😭
@MestarBenson-nx1mo
@MestarBenson-nx1mo 11 күн бұрын
Rest in peace Mr. Chilima whole people we are cry for you.hour heart is broken.we will miss you .
@wilsonfelix6559
@wilsonfelix6559 11 күн бұрын
Apm respect zoonadi
@FrankKambwani
@FrankKambwani 10 күн бұрын
Aliyense akudziwa kuti Chakwera ndiyemwe wapha anthuwa basi😢😢😢
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 10 күн бұрын
Mopandanso kukayika Chakwera ali ndi mangazi mmanja mwake a anthu amenewa afera pa ndenge imeneyi kuphatikizapo olemekezeka Mr R Kasambara onsewa aphendwa ndi MCP anthu oyipa kwambiri
@FahadiFalaji
@FahadiFalaji 11 күн бұрын
Ameen
@user-lw9su5om5z
@user-lw9su5om5z 10 күн бұрын
Eeeesh zosayenda ay
@user-ol3ty1dj1u
@user-ol3ty1dj1u 11 күн бұрын
So bad😢😢😢😢😢😢😢😢😢
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 11 күн бұрын
Chilima anali chiyembekozo cha a Malawi and Peter adamupanga chipongwe chilima povera omuzungulira as result Dpp idagwa as kuthamangitsana otsala lack of democracy, bcoz mphatso ya utsogoleri inalipo mwa chilima that's why anali ndi value pa ndale sadaonetse kupupuluma kulikonse pano zapha legacy ya mcp which means mcp no more chance to win
@MebleNgulinga-hi6rg
@MebleNgulinga-hi6rg 11 күн бұрын
Amen the truth will come out
@MaxwellChiwaya-tv7kn
@MaxwellChiwaya-tv7kn 11 күн бұрын
Komadi ulemu upite kwa Peter eeeeeish
@augustMag
@augustMag 10 күн бұрын
Father Kimu you are true man of God may God bless you 🙏🙏
@user-ib6jc4es3s
@user-ib6jc4es3s 11 күн бұрын
Ndeno afana oganiza bhoo tsogolo alipezadi kwachakwela kumenza asanamalize kutafuna otsalanu phunzilani kulemekeza omwe akuchitilani zabwino.mwambi kamba anyelera pomwe wamtenga
@MaxwellChiwaya-tv7kn
@MaxwellChiwaya-tv7kn 11 күн бұрын
Misozi yanga sikutha daily ndikaganiza zomwe Peter anapanga lero Chilima wapita ngati bodza
@louismagongwa
@louismagongwa 11 күн бұрын
😢😢😢 mulungu asunge mzimu wachilima ndi ena
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 10 күн бұрын
Amen Father zudzavumbuluka ndithu
@InsideMalawi
@InsideMalawi 11 күн бұрын
Mafunso ayakhidwa posachedwapa
@AbitiFinala
@AbitiFinala 10 күн бұрын
APM my vote 💖
@juniortsegula3847
@juniortsegula3847 11 күн бұрын
Apm my vote ❤
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 10 күн бұрын
A Chakwera zakuvutani tulani pansi udindo.
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc 11 күн бұрын
Mbolo yako chakwera
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g 10 күн бұрын
Na munthu wa Catholic odzavotela Congress ndi opusa.
@worldfamous_23
@worldfamous_23 10 күн бұрын
APM woyee!!! Let me see if you delete this comment 🤣🤣🤣🤣
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 10 күн бұрын
Koma sadamuphe komanso peter sadamunyoze chilima paliponse
@JustinLipipa
@JustinLipipa 6 күн бұрын
Koma samaphatu anzake paja
@worldfamous_23
@worldfamous_23 6 күн бұрын
Maybe someone reading the comments is unable to interpret ( KZbin interplate gets it wrong sometimes). These 2 agree that it’s okay to steal, openly be corrupt, be nepotistic as long as you don’t say anything bad about your opponent, or try to kill somebody. These 2 people in my comments will vote on the next election. The biggest fight should be tackling ignorance, until then we will still be no where as a country.
@worldfamous_23
@worldfamous_23 6 күн бұрын
We’re deleting comments now, what happened to freedom of speech 🤣🤣
бесит старшая сестра!? #роблокс #анимация #мем
00:58
КРУТОЙ ПАПА на
Рет қаралды 2,9 МЛН
Just try to use a cool gadget 😍
00:33
123 GO! SHORTS
Рет қаралды 85 МЛН
Backstage 🤫 tutorial #elsarca #tiktok
00:13
Elsa Arca
Рет қаралды 48 МЛН
Homemade Professional Spy Trick To Unlock A Phone 🔍
00:55
Crafty Champions
Рет қаралды 57 МЛН
Was Putin zum Pakt mit Nordkorea treibt | ZDFheute live
12:35
ZDFheute Nachrichten
Рет қаралды 217 М.
Meet the Press NOW - June 19
50:11
NBC News
Рет қаралды 450 М.
Billionaire Jim Ratcliffe On Man Utd Players, Stadium & Strategy: Full Interview
37:35
бесит старшая сестра!? #роблокс #анимация #мем
00:58
КРУТОЙ ПАПА на
Рет қаралды 2,9 МЛН