Kuti nkhoswe ameneyu Kuti achoke pakufunika inuyo dpp utm and aford pangani gwirizano ufd Atupele pawekha sungachite kathu chifukwa simungawathe amalawi tooonse ambiri tiri ku dpp ni APM basi and utm, aford and udf iri ni percentage tochepa ngati 1.5%
@DesireMoyo-y8x7 күн бұрын
Mkuchita kulilila migwilizano
@BlessingsNgomba7 күн бұрын
I pray musamayankhule kwambiri. Let us hear from the mouth of a horse
@HalisonSolomon7 күн бұрын
NDIPO SAKUNAMA CHAKWERA CHIMUNTHU CHOIPA CHIKUKHALIRA LIPOTI KOMA AKACHOKA MBOMA NDI POMWE PADZADZIWIKE CHILUNGAMO
@PollyLysonLutepo7 күн бұрын
Anthu omwe safuna kuti Imfa ya Chilima Ifufudzidwe ndi a UTM asatinamidze. Ndicho chifukwa amakakamila kuti aima pa Wokha. Amadziwa kuti akapanga m'gwilizano MCP Yiluza. Omwe anapha Chilima adziwika. Ndiye ndibwino tiime pa tokha kuti MCP yiwine Kafukufuku wa Chilima asachitike. Koma takudziwani chomwe m'makanira m'gwilizano.