HOT CURRENT..12/05/2024..TTV's Content.

  Рет қаралды 16,371

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

19 күн бұрын

Пікірлер: 48
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 17 күн бұрын
Guy you are speaking openly and truly watching you live at SA Pretoria
@badanidube8315
@badanidube8315 17 күн бұрын
Ulemu ku times, komanso chakwera ngati our president wathu koma tikasiyanisa 8yrs kuchoka 2014 to Pano aaaaah Chakwera and his government has failed us Malawian Pano walandisa immigration ku zigawenga chaka chamawa alandizanso intelligence agency tizitenge bwino izi si za ndale koma ma fact / Chakwera his 4yrs in Office scores 13% out of 100 Peter his 4yrs in Office scores 47% out of 100
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 15 күн бұрын
Ndipo Zoonadi uyu akuwonga dziko mwamva inu..
@JedidiahChangantuwa
@JedidiahChangantuwa 16 күн бұрын
😮Vuto la anthu amene akulamula ndiloti akangotenga ulamuliro amayamba kudziona ngati madolo omwe otsogoleredwafe singatsutsane nawo pamfundo zomwe akuzitsatira paulamuliro wao. Mwaichi amayamba kutenga maganizo awo ngati opamba kuposa a aliyense, ndipo satsutsika, satenga nthawi yodziunika okha pamomwe akulamulira, ambiri mwaiwo maso awo amakhala pakudyerera zipatso za kutinyengera kuti tiwavotere_ kuyiwala kuti mawa adzatifunanso.
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 17 күн бұрын
Akalowa mboma amakasandulila kukakhala ziwanda za pansi pa nyanja samamva chisomi kwan anthu osauka
@albertkwizombe988
@albertkwizombe988 17 күн бұрын
This team add Brian Banda it will shake the whole national
@SameKaposa
@SameKaposa 16 күн бұрын
Exactly brother
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 17 күн бұрын
Guys mm bola dpp basi siawa atabwaliwa ayi mcp kubin ikafik and asazazukeso
@EllenaJames
@EllenaJames 17 күн бұрын
Dpp is better than mcp ndipo dpp imamva zomwe anthu akunena apapa mcp yafika potopesa chilichonse chili high
@Yousef-td7ux
@Yousef-td7ux 17 күн бұрын
Program imeneyi yandtegula maso
@yohanemakhawe502
@yohanemakhawe502 16 күн бұрын
I do agree kuti ma civil servants ndio amasithisa adale
@gaddiemkandawire6436
@gaddiemkandawire6436 17 күн бұрын
Sstana ndi satana ma guys palibe kusiyana
@KonzaniZinthu
@KonzaniZinthu 17 күн бұрын
Kuona dzaka dza mbuyomo Malawi alibwino panopa. Ena aja anaononga kwambiri. Awawa mwina angophunzitsidwa kalembedwe ka malipoti a bodza kwa azungu.
@ChitaloAbbas-fw2ed
@ChitaloAbbas-fw2ed 16 күн бұрын
Kodi zipani zilipo kumalawi ndi dpp and mcp bwanji osayakhula za udf ,afd and etc thawi yabakili bwanji
@JustinPhiri-kq2bb
@JustinPhiri-kq2bb 17 күн бұрын
mutharika sazayima angopanga testing amene akufuna kuwawona ma presidents cadets
@reubenchilongo4883
@reubenchilongo4883 17 күн бұрын
Welcome back
@TroubleGalimotoBanda
@TroubleGalimotoBanda 15 күн бұрын
zitsiru izi takanyere uko mapwala anu
@geofreydzinyemba6107
@geofreydzinyemba6107 17 күн бұрын
You guys I just want to ask you this question, These politicians they can transform the country or they love their own country what's there are in power only, if so how can we believe them that they can do better yet nothing they did in their country
@user-ux9ik4zr5x
@user-ux9ik4zr5x 17 күн бұрын
According to the bible no matter how hard it was for the Israelites on their way to Canaan,they didn't go back to Pharaoh
@Moses51
@Moses51 17 күн бұрын
Keep up 💯
@chinthowaphiri3336
@chinthowaphiri3336 17 күн бұрын
Unless Boyz..
@godfreymopiwa-yj5zv
@godfreymopiwa-yj5zv 17 күн бұрын
mmati atsukuluza akuwoneka otopatu Mjamba rally imeneyo eti
@ishmaeldama8906
@ishmaeldama8906 17 күн бұрын
He was talking about Singapore in 12years not one, even u yourself u can see, so don't talk like u don't stay ing in Malawi, every one is crying in Malawi, so don't talk about Peter munthalika, he didn't take his son to give him any contract, so who's doing nepotism in Malawi right,be very careful. From johannesburg
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 15 күн бұрын
Chakwera is worse hummm
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn 17 күн бұрын
Choosing a better devil indee
@Yousef-td7ux
@Yousef-td7ux 17 күн бұрын
DPP is the better devil is me from Soweto
@WilfredMathews-yl6ij
@WilfredMathews-yl6ij 17 күн бұрын
Komatu fusolo nde ndilovutadi kms mwafusa bwn kuti titseguke nawo mmaso ndipo kuti tsono titha kutani fukwatu ndie nchilungamo nayo dpp idabowaso kanthawi kenakake
@MuhireDominic-rw4vf
@MuhireDominic-rw4vf 17 күн бұрын
Hot current 😂😂🔥🔥❤
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v 17 күн бұрын
Inu ndinu madoro
@LOPEZFBINALI-wk1hn
@LOPEZFBINALI-wk1hn 17 күн бұрын
These guys eeee mbambande
@GeorgeKasuza
@GeorgeKasuza 17 күн бұрын
Achunga magalasi bwanj😂
@user-vb8ht5kr6z
@user-vb8ht5kr6z 17 күн бұрын
Kikikikkkikiki choising the better devil
@PeterPhiri-nd6op
@PeterPhiri-nd6op 17 күн бұрын
Dpp ndiyabwino kusiyana ndi mcp koma iwe wakhala pakati ndiwe galu ndiwe wa mcp chisilu iwe
@user-gb2sl1jt4s
@user-gb2sl1jt4s 17 күн бұрын
Ndipo live achisilu amenewo asiyen ziwavuta DPP is my vote
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 17 күн бұрын
Dpp is better than mcp
@user-nz9ty3ih1v
@user-nz9ty3ih1v 17 күн бұрын
kkkkk wamutukwanatu akuwona ngati MCP ingawineso aja azikalima fodya basi
@lillianmwanza4218
@lillianmwanza4218 17 күн бұрын
Mbwitu mbwitu
@KnowxySainet
@KnowxySainet 17 күн бұрын
Komano vuto mbuli zaanthu safuna kusiyanitsa apa Chilima sakulamula muno aliyetse akudziwa maudindo kunchonsa sono bwanji until pano kukamba zachilima nonsense...
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 17 күн бұрын
Iweyo ndi mbudzi chilima Sali mboma bwanji sakudzudzula bomalawoli
@KnowxySainet
@KnowxySainet 17 күн бұрын
Ayambe kuyankha muzit ayamba kuwukilana onkhaonkha Chilima oganidzabho tasiyeni a dpp aziyambana ife mulibemo
@Yousef-td7ux
@Yousef-td7ux 17 күн бұрын
Cinyengo cimatha ndi Yesu yekha osati bungwe
@Yousef-td7ux
@Yousef-td7ux 17 күн бұрын
Amene sanacimwepo ayambe agenda mkaziyu
@user-gb2sl1jt4s
@user-gb2sl1jt4s 17 күн бұрын
Koma mcp singafane ndi dpp ndichipan.chabwino peter muthalika woyeeeeeeee
@ishmaeldama8906
@ishmaeldama8906 17 күн бұрын
Dpp is going to run the country again, from johannesburg cbd, DPP woyeee ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@JedidiahChangantuwa
@JedidiahChangantuwa 16 күн бұрын
😮Vuto la anthu amene akulamula ndiloti akangotenga ulamuliro amayamba kudziona ngati madolo omwe otsogoleredwafe singatsutsane nawo pamfundo zomwe akuzitsatira paulamuliro wao. Mwaichi amayamba kutenga maganizo awo ngati opamba kuposa a aliyense, ndipo satsutsika, satenga nthawi yodziunika okha pamomwe akulamulira, ambiri mwaiwo maso awo amakhala pakudyerera zipatso za kutinyengera kuti tiwavotere_ kuyiwala kuti mawa adzatifunanso.
@Yousef-td7ux
@Yousef-td7ux 17 күн бұрын
DPP is the better devil is me from Soweto
UTM Musapusitse A Malawi Lero   Bon Kalindo
17:09
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 35 М.
DPP ndi UTM alliance itha kukhala yamphamvu bwanji?..HOT CURRENT 26/05/2024.
1:30:35
[Vowel]물고기는 물에서 살아야 해🐟🤣Fish have to live in the water #funny
00:53
Ну Лилит))) прода в онк: завидные котики
00:51
格斗裁判暴力执法!#fighting #shorts
00:15
武林之巅
Рет қаралды 80 МЛН
ZOCHITIKA ZA BRIAN BANDA 🙌🙌🙌🙌
22:25
HOT 265
Рет қаралды 23 М.
HOT CURRENT..28/04/2024..TTV's Content.
1:03:48
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 7 М.
MOSES KUNKUYU EXCLUSIVE INTERVIEW
56:13
Zodiak Malawi
Рет қаралды 23 М.
MR NKHOMBORI - MWAMUZGOLA - MALAWI OFFICIAL GOSPEL MUSIC VIDEO
4:36
MALAWI MUSIC TV
Рет қаралды 9 М.
A CHIMWENDO  BANDA  NDA PETER MUTHALIKA ATHANA NDITHU |
37:51
BEST MALAWIAN CATHOLIC SONGS 2022
1:02:58
Malawi Music Hub
Рет қаралды 168 М.
[Vowel]물고기는 물에서 살아야 해🐟🤣Fish have to live in the water #funny
00:53