Who should we trust? To answer you. Let's vote for dpp. Why? Dpp is much better than mcp. For example,there many areas where mcp is failing. First, nepotism. Second, corruption. Devaluation of kwacha which has led to high cost of living. Poor management resources. Lack of leadership skills. Thanks for your attention.
@user-ol7ly5in2f25 күн бұрын
Your right
@PrinceKachimanga27 күн бұрын
DPP IS what we need.....LAZARUS chakwera is not a litsening president...
10 Minutes 40 Sec......Wonder wafunsa funso lomwe yankho lake ndi limene lingathe kusintha Malawi for good......apa chofunika ndikusintha System yondetsera Boma....just like Chihana ananenera pa Times Xclusive ndi Brain Banda last year.....lets advocate za Federal System......munthu olo ophunzira bwanji kaya wanzeru ...System. iyiyo...its like ma variant. a COVID.....coz tinachoka pa DPP Gov 0.0 ......apa till pa DPP Gov 0.1
@andrewkawonga448728 күн бұрын
No longer about people but themselves. Greedy.i like this
@bristonmwenga528626 күн бұрын
That's what democracy means mwauponda,, 50 + 1 has come to stay to kick out tribalism, corruption, being egocentric, arrogance etc
@petermsamariamapira893329 күн бұрын
Mulungu wathu ndi okhulupilika atipatsa president wabwino mu 2025 ,inde president samptsa munthu ndalama ayi, Koma zinthu dziko tidzigulako better price, Anthu tikuvutika yoooo
@bristonmwenga528626 күн бұрын
Chunga said the best,, no need to vote due to party stronghold or tribal lines but to vote for Malawians With best qualifications regardless of where they come from❤
@AhmadumkomaTambala-lr9gp28 күн бұрын
DPP bola kulekana ndi MCP ikutphela ufulu chilichonse chovuta ld ikuvuta kut munthu upangitse ndy pamnepa zikuynda
@BenjaminTembo-el5md25 күн бұрын
Dpp moto zinazi ayi mcp must gooooooooo
@BethsiderTavares-ug4sv29 күн бұрын
Sutter has been pardoned and he is demanding compensation from Malawi.
@YusufuShaibu28 күн бұрын
Ndale xakwathu kn ndi zachamba xodwalitsa mutu
@WisikiBlack-gj4gu29 күн бұрын
Udf moto ndiyomwe ikufunika afa
@OfwaMwambila28 күн бұрын
It will take someone who truly loves malawi to convince me to go 🗳vote..am not the kind to be taken for granted(my vote)
@LongiMtimabii29 күн бұрын
Apm🔥🔥🔥🔥
@user-zk5nu5fh6l28 күн бұрын
APM ndi dilu ❤❤❤❤
@user-eh1gn1nj9d26 күн бұрын
Anthu Aku Malawi amadikira President akawapezere ndalama
@AnafiRGRajabu-me9ki29 күн бұрын
Peter ndi putin 2 from rasha😅😅😅😅😅
@andrewkawonga448728 күн бұрын
2025 is choosing the best devil .wow we have nice analyst.Politics in Malawi has no direction
@richardbanda386228 күн бұрын
Vuto amalawi timaombela mmanja zinthu zopusa
@user-jl6sq3ph1b25 күн бұрын
Chakwera ndi chilima basi iwowo akanika kuyendesa ziko iwowo km Kuba ndi nduna zizawozo achina chimwendo banda boma losangalala okha okho ali boma ndi family ya chakwera
@Trancy-xt4py28 күн бұрын
Yakho mukuliziwa kale Kuti Malawi winaliyese akusiyanisa boma la mcp ndi DPP Kuti thawi ya DPP zidaliko bwino alekeni amalawi Ali kunjaku Kuti asiyanisa bwanji pa 2025 Kuti WABWINO ndani Koma Ife tikuziwa
@innocentkapachika659129 күн бұрын
Komanso anthu Ake ambiri ndi akuluakulu. Promising ndithu
@AnafiRGRajabu-me9ki29 күн бұрын
Malamuro apange ena oti munthu akalonjeza ngati osachita dzimwe adalonjezaso if before 5 year's achosedwe. Komano ngati osatelo malawi sazasinhta
Vuto ndiloti kwathu kuno sikupezeka nsogoleli wabuino it's only later Bingu wamuthalika uja ndi yemwe anali wamasomphenya bas
@user-mj3ms4jt3b29 күн бұрын
Koma nkhani ndiyoti peter munthalika sangadzawine chisankho cha 2025 loko MEC chair person atakhala mwana wake wa peter munthalika
@isaacbwanali469929 күн бұрын
KuMalawi tidakali pamavuto amnanu- sindikuonapo chipani chomwe chingatiphule mugoli ili laumphawi- kokano ndiMulungu yekha yemwe angathandize aMalawi muukapolo uwu waTonse ❤. Jona, Wonder, Bayana, mumatiyimilra- keep the fire 🔥 burning
@StevenBwanausi26 күн бұрын
Guys musanamizane bingu ndi Boma
@ChiwamboThomas11 күн бұрын
Vote DPP
@TiyanjaneMkwate-we8gu28 күн бұрын
I like the word yot choose a better Devil.
@richardbanda386228 күн бұрын
More fire guys
@user-mx5cx3gl4h28 күн бұрын
DPP woyeee
@stevenbanda240929 күн бұрын
Zooona, Capitol Hill, kuli zisawawa,
@AnafiRGRajabu-me9ki29 күн бұрын
Ndikomwe kukumayambila usiluwu ngati amalawi akumasunzika kamba ka ulamuliro ndi kumeneko
@casilasjawadu158629 күн бұрын
UDF ndi yomwe tikudikira
@josephgrevaxio284728 күн бұрын
Vote
@KenChitete-pg3ws29 күн бұрын
Kutsowa chipani chabwino mudziko,,athu adzavotela DPP koma ngati chipani chabwino chilipo,,,, DPP ndi MCP onsewa ndi asatana oyenda ndi mwendo,,kwa ine bola ndikhale otsavota bola ndivotele afford.
@sidreckrashid932728 күн бұрын
Good am with u, tizangovotela popeza kulibe zina za mzeru.
@KenChitete-pg3ws29 күн бұрын
A Peter Mutharika anali muboma athu anali kulila kwambili mudziko pano abweleletso muboma???? Dziko likakhala losauka athu akasowa pogwila amakaombela manja ngakhale chili chigewanga kwambili,, Peter Mutharika anaononga Malawi kwambili apitaapita,,,,sikuti ndikufuna chakwela aii sikuti ndine wa MCP aii koma amalawi tiyeni tidzipita ku tsogolo titsabwelele mumbuyo.
@user-jn9tz3li3v28 күн бұрын
Vuto sunapeleke suggestion to appreciate your views. A Malawi awona kuti Peter was better than this useless Chakwela. If Chakwela performed APM could not have come back, even DPP as a party ikanatha ngati UDF.
@BethsiderTavares-ug4sv29 күн бұрын
They only know how to dikhulira!
@stevenbanda240929 күн бұрын
50+1,l choke kuononga mphamvu za chipani.
@WisikiBlack-gj4gu29 күн бұрын
Aaaaa bola tiese udf & aford
@TysonWaTysonKasukuwere29 күн бұрын
Wonder Msisa what type of a journalist? You did not do proper research. The last time Arthur Peter Mtharika held a rally at Njamba was on the 19th of December 2021.
@stanleykaludzu-bm4pm29 күн бұрын
Ana a Dad ife kumva ilovo sugar kukoma kukoma basi 2025 bomaaaaaa
@mother86628 күн бұрын
A Chunga atchende kufuna kulibeleka boma
@MirajLaja28 күн бұрын
Jona Manjawo muzawapweteka ochungatu. Manjawo muchepetse yambakata yambakata sizimaoneka bwinoo
@IvyMithi29 күн бұрын
Ma shirt ofanana ngat mwachita ku pangana
@eliffagondewe821429 күн бұрын
. Ndi uniform paja hotcurrent amavala ma uniform..
@edgarmsofi58928 күн бұрын
Uwone pa thumba Pali lable.
@NancyCharlie27 күн бұрын
Kaya amwene
@AlfredSomanje28 күн бұрын
Kodi mbiri yake iti
@EstherNgolleka-zs2fj29 күн бұрын
Linda madzi apite uziti ndadala
@EmmanuelMtchule28 күн бұрын
bora dpp is not mcp
@actuarialscience228328 күн бұрын
Atupele boma
@ashingsmvula335729 күн бұрын
Mumangodzikolakola anthuni. ACB us independent no influence of president and cabinet. But when ACB fails you say the president and cabinet is not fighting corruption.
@user-dk6yc8pl2m28 күн бұрын
Your very stupid
@RickySwartz-fp3fc28 күн бұрын
Mmmmmm izi ndiye ayi
@user-kq9gz3jh1m28 күн бұрын
Dpp muwusogoleri wa Apm ilibe maso mphenya ozasintha zinthu analephera 7yrs
All presidents v failed us let's forge ahead as malawians & choose new blood,,, never go back to Egypt, forge ahead,, dzuwa saloszerana❤
@simonchirwafoon829424 күн бұрын
Vuto ndi sankho basi lets vote for new party not mcp or dpp guy's Malawi will remain the same if we will vote for mcp / Dpp
@user-og4dg6kz5s28 күн бұрын
How can a normal person vote for someone who is 84yrs in 20 first century yet he failed his term ....DDP out.....MCP same Whatsapp group
@stellakaluluma824128 күн бұрын
You guys, one the panel, Mr Wanda, pamkuku and chunga, you seem also to be forgetful. We are after development nothing else, if we talk of DPP, it started with Bingu assess what Bingu did in Lilongwe, Mzuzu and Blantyre only within eight years, including silos and fuel reserviors, it was too much development within a short period of eight years. You confuse people the characters of individuals and DPP.