HOT CURRENT - 28 JULY 2019

  Рет қаралды 9,747

Times 360 Malawi

Times 360 Malawi

4 жыл бұрын

Because of arrogance and big-headedness, Malawi is being ripped apart. Brian Banda and George Kasakula discuss this in this week’s edition of Hot Current.

Пікірлер: 38
@chriskaidi6871
@chriskaidi6871 4 жыл бұрын
I like you guys your really fight us ndimakunyadilani here in cape town South Africa
@stanleydamalekani7113
@stanleydamalekani7113 4 жыл бұрын
Grt! izi ndizo timafuna osati zinazi .
@dyelekalokoku7193
@dyelekalokoku7193 4 жыл бұрын
Thanks alot guys ndinudi mzika za Malawi
@liki-likiladies---lilongwe6963
@liki-likiladies---lilongwe6963 4 жыл бұрын
Kkkk koma guys u r making it... Big up guys... This is the only malawi we shall ever have
@williamsbanda9225
@williamsbanda9225 4 жыл бұрын
Yes Mr.Brian you are indeed for the poor citizens of Malwians, anthuwa ndi amodzi akudziwani,nkhani apa so amai away ayi nkhani ndi DPP party with few greedy individuals, koma Mulungu shall take over very very soon,instead of loosing job it shall be something else.
@roxtonmbawa8012
@roxtonmbawa8012 4 жыл бұрын
No point of correction main Jane Ansah ali nchiwanda not chiwindi matsulani nkhani ofunika deliverance mai uyu
@alexpeteribrameja1819
@alexpeteribrameja1819 4 жыл бұрын
Alex is back in Town
@johanpieterse194
@johanpieterse194 4 жыл бұрын
Munakatokota mpaka 2024 hahahaaaa
@amosmbuka6945
@amosmbuka6945 4 жыл бұрын
Amalawi amzanga ziwani izi. Jane is a judge, then onani mmene wakhumudwisira fuko la Malawi. ziwani kuti paziko la pansi palibe judge oposera mwini wake Jahova. she must stepdown. Ngakhale Peter nthawi yake yatha he must stepdown as well.
@williammkhalipi5143
@williammkhalipi5143 4 жыл бұрын
Mtambo is playing with u guys and he uses u mtambo tripecee Must fall,if U refuse why others , must,we,re sick and tired of,ur playing dirt, games,, , of politics working with, MCP utm,, we know they gave U better offers
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 4 жыл бұрын
Kkkkkkk safinyika kodi Brian ? Yes asafinyike aliyense
@moyo77777
@moyo77777 4 жыл бұрын
timakunyadiran ma big.....man mumayakuraq chilungamo
@dysonmukhuna6428
@dysonmukhuna6428 4 жыл бұрын
Ma demo anuwo mukuti peaceful yet mukamachita katundu akubedwa mukaba mukamanga ma nyumba magalimoto mwagula ndiye muzilemba thank God zachani mpila osewela wina mumachuluka nzeru ndipo chili kwa mzako
@danielmpombera9962
@danielmpombera9962 4 жыл бұрын
Ndimakutsan akulu akulu kuno ku south africa
@chebedi
@chebedi 4 жыл бұрын
Ndipinde shirt😝😛😝
@davismchenga3363
@davismchenga3363 4 жыл бұрын
Kkkk true.
@fikiremariwa7252
@fikiremariwa7252 4 жыл бұрын
Achokepo Jane pampando plz plz aboma
@nambelasilungwe5314
@nambelasilungwe5314 4 жыл бұрын
Chomwe akuopa a boma ,akawachotsa a mayiwo or akatulapasi ndekuti avomeleza Kuti chitsakho sichinayende bwino,
@dysonmukhuna6428
@dysonmukhuna6428 4 жыл бұрын
Mwaswa Japan embassy anthu oipa inu vuto simuatuluka kunja mukati muzituluka mukanaziwa kufunika kwake kwa embassy ndipo simukanaswa
@yamiechikhola6705
@yamiechikhola6705 4 жыл бұрын
Jane Ansar mmmmm ndiochimwisa kwambir
@edisonnyasulu9568
@edisonnyasulu9568 4 жыл бұрын
Kunena zoona muli pa njanji kungoti mulungu alinanu
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 4 жыл бұрын
The damage that is happening in the country is bcoz of one innocent Jane ansah.
@princenoah4390
@princenoah4390 4 жыл бұрын
Amayiyo akuopa chani kuusiya udindo. Palibe chimene angaluze akasiya. Koma akupanga mantha ndi a Peter munthalika kuti mwina adzafuna zawo
@sillahnyali5401
@sillahnyali5401 4 жыл бұрын
Apa nde timvera bwino kwambiri a munthalika alibe maso autsogoleri anangokhalapo kufuna kutchuka koma maso mphweya nde mmmmm alibe,Jane ansaah apite akapume ife tione zina
@zamcatahmed4949
@zamcatahmed4949 4 жыл бұрын
Koma B B ndi Kasakula ndinu madolo
@louismayiwakuphaameneyorob9736
@louismayiwakuphaameneyorob9736 4 жыл бұрын
B b ndinu olimbadi mtima chifukwa thawi iliyose akhoza kukuphani ocz panja safuna muthu onena chilungamo
@yufufmapata1470
@yufufmapata1470 4 жыл бұрын
Musamuyikile kumbuyo mp amene uja certificate yogula Vuto lake ndilimenelo
@conductorhlongo8960
@conductorhlongo8960 4 жыл бұрын
Jane Ansa ndiokula mtima akakhala wina akanachoka kale kale.Mademosration apitilire ngati katundu akuonongeka akafunse Janeyo ndi amene waononga zinthu.
@stewartkamwendo735
@stewartkamwendo735 4 жыл бұрын
Kumenyana komenyana njovu ovutika ndi udzu......... muzaziwa choona cheni cheni chikuononga malawi onani kachikena malamulowo America ndi dziko lalikulu koma zipani ziwili koma ndikomwe kunachokela kadzina koti ufu ndiye mumuone Malawi wantuyo ndimomwe timautengela ufuluwo ngati zimagwilizana zachisoni kwaife omwe sitinganiza zamawa
@dysonmukhuna6428
@dysonmukhuna6428 4 жыл бұрын
Stewart Kamwendo zoona izi anthu akuononga ka ziko kosauka aka
@dysonmukhuna6428
@dysonmukhuna6428 4 жыл бұрын
Eya anyamata inu mukukwanisa ntchito za satana bambo wanu ndi wambanda kuchokela pachiyambi kwake kupha kulanda ndi kuononga zimuonongani Malawi osauka kale
@ComfortNoahJofilisi
@ComfortNoahJofilisi 4 жыл бұрын
Ma guys mmatha inu!
@molanaahmad861
@molanaahmad861 4 жыл бұрын
Tingogawana dzikoli kumwela presdent wanu ndi paetarayo , pakati pano ndi kumpoto presdent wathu ndi chakwela . Zitatelo phokoso litha
@innocentbvumbwe5075
@innocentbvumbwe5075 4 жыл бұрын
Guys what you have said is very true if this people can understand your points you have raised here I think zikhoza kuchitira ubwino Kwa a Malawi ochuluka amene akuvutika chifukwa cha Jane
@dysonmukhuna6428
@dysonmukhuna6428 4 жыл бұрын
Noah Comfort Jofilisi samatha awa brother ma satanic awa
@simonchitenje6575
@simonchitenje6575 4 жыл бұрын
Zowona zake nzakuti Mai ameneyu chiwandachake akufuna kuphesa anthu ambiri ndi mzimai wosabeleka she is satanic woman.we can even see by her face.kunyasa ngati muleme.
@dyelekalokoku7193
@dyelekalokoku7193 4 жыл бұрын
Thanks alot guys ndinudi mzika za Malawi
MK Party leader Jacob Zuma addresses supporters
54:16
Newzroom Afrika
Рет қаралды 55 М.
[ICYMI] 'We won't work with ANC under Ramaphosa' - MK's Nhlamulo Ndhlela
21:22
ПООСТЕРЕГИСЬ🙊🙊🙊
00:39
Chapitosiki
Рет қаралды 14 МЛН
Black Magic 🪄 by Petkit Pura Max #cat #cats
00:38
Sonyakisa8 TT
Рет қаралды 33 МЛН
100❤️ #shorts #construction #mizumayuuki
00:18
MY💝No War🤝
Рет қаралды 20 МЛН
How many pencils can hold me up?
00:40
A4
Рет қаралды 18 МЛН
Times Exclusive featuring Davie Maunde - 1 June 2024
1:01:02
Times 360 Malawi
Рет қаралды 14 М.
Sports Arena on Flames game against Sao Tome - 3 June 2024
23:35
Times 360 Malawi
Рет қаралды 1,2 М.
2024 Elections | 'I have accepted the results'| Maimane
15:40
SABC News
Рет қаралды 105 М.
2024 Elections | uMkhonto weSizwe Party media briefing
14:05
SABC News
Рет қаралды 91 М.
Izindaba zesiZulu @19H00 | 31 May 2024
28:02
SABC Izindaba
Рет қаралды 39 М.
ПООСТЕРЕГИСЬ🙊🙊🙊
00:39
Chapitosiki
Рет қаралды 14 МЛН