A Malawi ofunika kulapa machimo Anu palebe mmalawi Amalankhula chilungamo
@user-vm7iz6oz6rАй бұрын
Chakwera azachoka mowawa musiyen even azayesere kuba kwakeko koman mulungu awakatha ndithuuuuu
@mitochilukas9170Ай бұрын
Solution chakwela walephera ndi boma lake
@ChifundoNinjeАй бұрын
Ndipo ineyo sindinaonepo muthu okuba ngati chakwera ndi nduna zake
@StiveKantikiАй бұрын
Kulibe akuziwa olo apulewo saziwa kanthu angoziwa Kuba basi
@Johnybegood260Ай бұрын
ndiye chitsiru china chiza votela MCP
@MalawianCameraАй бұрын
Big up
@JonesChingaya-yf4ggАй бұрын
Even akanakhala kut ndi a DPP okhaokha ndie inu ngat Boma muzingowayang'ana anthu akukhapana??? Mesa timati palibe Ali pa mwamba pa lamulo???? Stupid government ever.
@EstherPeter-cf1vfАй бұрын
Anthuwa onse ali cholinga choti adzabele ma vote chaka cha mawa
@clintonhodda9830Ай бұрын
Ndiye ife tikamati ulamulira ukulephera mkulakwa?
@user-rn7wv8ze3vАй бұрын
Zikhale ng'oma pamozi ndi Chakwera zeru alibe Kulibwino anthu awiri awa atule pasi udindo chifukwa palibe chimene akupanga
@homeremedys3748Ай бұрын
The DC Osachita Mantha Tabwelani ndima audio aja this is Democratic country, Mukuopa boma ili ladzitsilu
@Tawina0101Ай бұрын
Anamulanda Foni ku police,,,akuti akufufuzamo
@user-gd3jx7tr1pАй бұрын
Zosezo vuto NDI dpp ndiyomwe ikubweretsa mavuto Ku migration alowesa ndale Malo monthandiza zika zawo
Chakwera achotsedwe kumene 2025. So Immigration CEO ndindani kusachotsedwa timudzutsira Ayaya.
@user-oe1lg4xo7wАй бұрын
Guys matuvi Ali ku immigration adanyera ndi chakwera nchifukwachake akulephera Kosova mavutowa. Achakwera , azikhale ndi immigration officials atule pansies maudindo
@user-jl6sq3ph1bАй бұрын
Mai yolamuwo ndi MDF panopa ili ku mcp siyoziimilaso payokha ai panopa inagulidwa mpakana ndi mec yomweso fundo kachali ndi a mcp amenewo onsewo
@SymonNamalomba-sh3fuАй бұрын
Which A president are you talking about
@user-hy6gc6ld9wАй бұрын
Kalumo , zikhale onse anasankhidwatu ndi chakwera okubayi ndipo chakwera pakha sapanganso chiganizo ali ndi anzake komano kodi anzakewa ndiyekuiti amawawuza chani abwanawa chakera ndianzake onse ndi mbava anthu okuba mochitisa manyazi
@user-ev6bi7jr7gАй бұрын
MCP simalabadira kulira kwa amphawi bola iwowo zawo ziribwino tikayankhula chonchi aziti tikudananao
@user-pl8kw3dc9dАй бұрын
Chakwela ndi zikhale ng'oma ose ndakuba ndi zinkhumba ndi makape
@user-cb2cv9fz7mАй бұрын
Kkkkkkkkk ma big inuyo mumatha kuyankhula mwamzeru, mbuzi za anthu including chakwera mbava yaikulu apite uko,bodza basi
@kennedybandaАй бұрын
Kaku Immigration kaja nde kamapambuka mwano.
@petrooverton6643Ай бұрын
solushoni ndi chakela chifuka chakela ndiye bwana awo ngati sisitimu yaonongeka bwanji osagula ina
@nnmzakwachamzakwacha9405Ай бұрын
Chakwera has failed beyond. How do you believe in someone on retirement.
@user-nk5mj5ws8vАй бұрын
achakwela adziwa bwanji asakuyendela mene dzikuvutamo ango yangula ali kunyumba ndi nsogoleli ovensa chinsoni
@marryphili5419Ай бұрын
Vuto ndiloti boma la MCP silikufuna chilungamo alitenga dziko la Malawi ngati family yawo tiwonana 2025 Muli busy ndi kudya misonkho ya amalawi palibe Chimene mukupanga
@ChristopherBalutiАй бұрын
The president is wik
@dorcasmwale6328Ай бұрын
koma mukudziwa kuti anthu akutuluka atanyamula ma fake papers, anthu akutenga ma risk kuyenda opanda passport
@user-jn9tz3li3vАй бұрын
Mavuto ochita kufuna, tamuyitanani Timothy Mtambo kuti akufotokozeleni pa program yanu chifukwa ndi mmodzi amene atifikisa pamenepa ngati dziko.
@user-pl8kw3dc9dАй бұрын
Achakwela zoti anali abusa mmmmmmm linali dzina chabe kuba nkhaza many of God 😂😂😂😂😂😂 zaboza galu iwe walephela magilass ngati fulu
@user-ig7dv8rp7rАй бұрын
Makape a MCP azaziona
@user-nw6ie3xx8bАй бұрын
This hot current yinali yachongo no one was giving a space to talk
@AmusedDimSum-hd5ypАй бұрын
kalumo ubongo udauma kalekale
@user-ek7mv2vo4fАй бұрын
Kukhapakukhapa
@SynodAuditАй бұрын
kuteteza forex
@JonesChingaya-yf4ggАй бұрын
Chakwera ndi munthu wa bodza kwambiri, ngat amanena chilungamo ndie kut amakanena kwa IMF ndi world bank chifukwa kumeneko ndikumene kuli anthu omwe akuwatumikira.
@SynodAuditАй бұрын
kuteteza forex kkkkkkkkkkkkk
@mchipenguleАй бұрын
Tikamanena munthu tiziganizila kaye, chifukwa mwina zitsilu mukhoza kukhala inu anthu akuchikamwa. Sitikudabwa chifukwa chingakhale ana a Israel mchipululu amalankhula ngati mmene mukuchitila inu. Anthu mulibe pabwino mwinaso amene mumafuna kuba ndinu mukulankhulanu a Dpp nanga izi zinayamba zachitikapo? Asiyeni azanu agwire ntchito kufikila zitheka. Nanuso a Times mumaonjeza kwambiri mumaoneka ngati azeru kwambiri kapena mumafuna udindo? Tiphuzile kulemekeza a dindo enanu ndinu alaliki pamenepa. Kumbukilani ana a Israel mchipululu tikamayenda njira mumakhala zambiri. Dzisungileni ulemu please chonde.
@ZelinaKisswellАй бұрын
Ulemu umapita Ku ulemu uzake Mesa anayamba ndi kalumo kunyoza nde iwoso atopa zikanakhala KT Iwo amawayankha bwino professionally I don't think bwezi a times akulankhula chonchi
@user-gz9iy7sd7jАй бұрын
A Times akulankhula chilungamo asamanyengerere munthu.
@leveltrapper4322Ай бұрын
Zako izooo aseh koza TV yako uzilankhula mwa ulemu wakowo..
@user-cf9yz3ei5oАй бұрын
Gentlemen no .matter how much we can talk Malawi died sometime back economically
@user-hg6qp4hs2mАй бұрын
When sometime back you talking
@shupikayintuwaluwa-5899Ай бұрын
N then, as a citizen wat z ur responsibility on that matter
@mabvutochimkondenji910Ай бұрын
Chakwera 2030;woo
@user-hm9nc7lz6eАй бұрын
Mmm ukunama ngati dziko lili lake
@user-jl6sq3ph1bАй бұрын
Uzamuwinisa iweo 2030 chakwera basi 2025 mukapitilize kulima uko kuminda yanu ikukudikililani inu abyapapinu
@user-gz9iy7sd7jАй бұрын
Noway Chadwell is going 2025 no matter what come day come sunshine.
@douglastholo390Ай бұрын
Well researched topics and well analyzed with constructive arguments that intend to assist in building the nation.
@user-rn7wv8ze3vАй бұрын
Zikhale ng'oma pamozi ndi Chakwera zeru alibe Kulibwino anthu awiri awa atule pasi udindo chifukwa palibe chimene akupanga