ZOMWE AYANKHULA ACHAKWERA DZUWA LIKUSWA MTENGO KU BLANTYRE 🙌🙌

  Рет қаралды 33,223

HOT 265

HOT 265

18 күн бұрын

Пікірлер: 536
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 16 күн бұрын
Amene sakufuna chakwela Ngati ine . Come here.akunamiza anthu uyu
@samsonmtumbati4855
@samsonmtumbati4855 17 күн бұрын
Mr pule mukuzinamiza zoti mupitiliza chaka chamawa mukunama kwambiri pa ground sipalichoncho baba muzakhumudwa kwambiri
@user-px9gd6fc6w
@user-px9gd6fc6w 17 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@charleslimbani8590
@charleslimbani8590 17 күн бұрын
Koma na Dpp yokha zoti ingazalowensooo mmmm tikunamizanaaa
@user-nx7yz4qo8f
@user-nx7yz4qo8f 17 күн бұрын
DPP boma chaka chamawa
@user-nx7yz4qo8f
@user-nx7yz4qo8f 17 күн бұрын
DPP boma chaka chamawa
@user-rd2td7bg4c
@user-rd2td7bg4c 17 күн бұрын
Dpp boma bas
@alfredbanda886
@alfredbanda886 17 күн бұрын
Mbuziiiii Yakumwa Madzi Ometela Ndevu Galuuuuuuuuu Chikwanteleeeeee
@user-px9gd6fc6w
@user-px9gd6fc6w 17 күн бұрын
😂😂😂😂 really😂
@user-yy8pi8zl9l
@user-yy8pi8zl9l 17 күн бұрын
Only God knows the 2025 leader... May God intervene
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr 16 күн бұрын
Yes God knows what will happen tomorrow....I dreamt that Peter will be president of MALAWI
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 17 күн бұрын
Chakwera ndi mbuzi yamuthu inu mwapanga chani mu 4 yrs ??? Ai lekani kunamiza amalawi
@LovelyBlini-cu3iu
@LovelyBlini-cu3iu 17 күн бұрын
Mlungu atimenyela nkhondo bwana ngati mkudalira kuba ziwani ichi ku mwamba kuli mlungu
@ThokohKalonga-je9rx
@ThokohKalonga-je9rx 17 күн бұрын
Kodi chifukwa chani amalawi timangopusisidwa apapa wbwera uyu ku blanttyre mukuombela manja ngati akupanga zinthu why!?
@user-zg7iw8kq4r
@user-zg7iw8kq4r 16 күн бұрын
Vuto dzikoli mbuli zachuluka
@user-oo1sx7fb4v
@user-oo1sx7fb4v 16 күн бұрын
Ndalama
@charleslimbani8590
@charleslimbani8590 16 күн бұрын
Ndiye muziwe kuti zokonda za inuyo c zokonda za awooo.....ngati inuyo mumakonda Dpp musayembekeze kuti awo akondanso Dpp ayiiii .....ngati mmaombera mmanja Peter ...panopa ena akuombera mmanja chakwera.....ngati mwagona ndi njara pa khomo panu musayembekezere kuti kwa Neba nakonso agona ndi njara .....umo ndi momwe moyo umakharira ......simungawapange anthu onse kuti akonde Dpp ......koma wanzeru amakwera Timu imene ikusogora pa ground nthawi zambiri yoluza .........
@AliSalimu-wl3vi
@AliSalimu-wl3vi 17 күн бұрын
Koma guys kod ku state house ku amasuta chamba eti nanga boza limeneli bwanji
@babranzima8120
@babranzima8120 17 күн бұрын
Akuzinamiza amenewo
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr 16 күн бұрын
MCP ikuzinamiza Peter is already chosen to be president of MALAWI
@CliveNdalama
@CliveNdalama 16 күн бұрын
😂😂😂😂
@samsonmtumbati4855
@samsonmtumbati4855 17 күн бұрын
Boma la mcp limatinamiza kwambiri kamuzu palibe chomwe adachita mdziko la Malawi chimene tikudziwa ndikuba ndalama za Malawi makolo athu amakagona kutchire chifukwa kamuzu amafuna misonkho ndiye kuti chiyani lero
@berthamigodi6529
@berthamigodi6529 17 күн бұрын
Ulibe manyazi komaso mwna umakomoka ma University, zipatara kkkkk Malawi tayani ndale
@FraserNamaona
@FraserNamaona 16 күн бұрын
Zoti ma University or zipatalazo amangozinsintha mayina simukuziwa? Even Kamuzu stadium ija, bunda college kungonena zochepa anamanga ndi asamunda.
@DeveliousMasinja
@DeveliousMasinja 16 күн бұрын
Tiziti Bingu uja adali ozungulira mutu akamati Kamuzu adapanga zinthu zambiri??
@wisdom20mkango49
@wisdom20mkango49 16 күн бұрын
Iwe ngodwala bwanji..... don't include kamuzu mukhani yako...he is the only guy that did good for Malawians ukafunse agogo ako...osati mbuzi zako Za dpp zo😂😂😂😂😂4get guys dpp will never come back muulamuliro
@bernardnyirenda7639
@bernardnyirenda7639 14 күн бұрын
K​@@wisdom20mkango49
@TrysonChimenya4-fm8nt
@TrysonChimenya4-fm8nt 17 күн бұрын
Malawi tikapusa tipitilira kuvutikabe President wanji wosapanga regret Mukamakavotera MCP kawiri zanu izo, Kodi bwanji sakutiuza percentage ya zomwe atipangila out of Promises????????? Time to vote for president based on region will no longer help us ....... Ine ndiye ayi Chakwera, Chilima akagwere ndi anthu onama zedi Komanso what we should know this is political battle, sangabwere poyera nkumatiuza kuti eya 2025 tizaluza that's why even those small small parties are promising that they will win come 2025. Uku nkulira kwanga ndatha ine wanu amalawi anzanga
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr
@LovelyAzaleaFlower-uc8vr 16 күн бұрын
Ndipo you have said the truth anthu awawa mukut a MCP waaa God will give them a severe punishment
@user-gk3bb8dx1m
@user-gk3bb8dx1m 17 күн бұрын
Apm my vote
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y 16 күн бұрын
Your president is another Bola Tinubu of Malawi, sorry he has pasted his sell by date, u can even ask Namalomba.
@EmmanuelChiweza
@EmmanuelChiweza 15 күн бұрын
Chabwino
@VincentChikondano
@VincentChikondano 17 күн бұрын
Stadium sinadzadze or half nde simungadabwe?
@user-vh1cq5gs5u
@user-vh1cq5gs5u 17 күн бұрын
Koma mmene akumuyang'anira Anthu ake amene wabwera nawo kuchoka ku lilongwekowo akuwawona chifukwa akumuysuysatu zoti akhoza kuwinaso
@user-xv5pr3ji6w
@user-xv5pr3ji6w 17 күн бұрын
Inu nde ayi ndithu za ziiii!!
@josephchitsulo5882
@josephchitsulo5882 17 күн бұрын
Kodi mukulota kapena kubwebweta? Nayensotu Kamuzu wanuyo ankatelo
@user-nl5rq9to2s
@user-nl5rq9to2s 17 күн бұрын
mwayambilatu kulila pack and go
@IshmealSaidi-kw6pd
@IshmealSaidi-kw6pd 17 күн бұрын
Zaziiiiiiii president osadziwa chimene akuyankhula
@louischitete1076
@louischitete1076 15 күн бұрын
Chakwela my vote kulibe opikisana naye uyo ndi owina basi
@JonathanDube-vc5qp
@JonathanDube-vc5qp 13 күн бұрын
I support, chakwera is going to win❤
@khumalonyirenda4437
@khumalonyirenda4437 16 күн бұрын
Chakwera boma ,salute
@user-vh1cq5gs5u
@user-vh1cq5gs5u 17 күн бұрын
Koma ukudalira chani galu wamunthu iwe zakudya ukunenazo waziwona kuti ukuwona ngati Anthu angakwanise kugula fertilizer pa ntengo was 108,000 kwacha? mbava, mbala, chiphe munthu oyipa ngati njala
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 17 күн бұрын
Kufuna osafuna iwe utuluka galu
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 16 күн бұрын
Kodi Mnyamata woganiza bhooo basi amuchita tame????
@Malawinews1
@Malawinews1 17 күн бұрын
Cant you memorize the script and present as you not just reading...
@FrankBanda-js1zr
@FrankBanda-js1zr 16 күн бұрын
Abwana awo!!!!!!! 2025 woooooo
@MacdonaldMushaya
@MacdonaldMushaya 17 күн бұрын
Ndiye anachoseranji ma office ku Blantyre kuunjika ku Lilongwe? Waziwa liti kuti Blantyre ndi Malawinso? Wadabwa chani Lazalo, Nyanja Nyanja ua Zana?
@gomezthera535
@gomezthera535 17 күн бұрын
Boma ilooo❤❤❤
@AjeliMw
@AjeliMw 17 күн бұрын
😂🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣😂😂😂😂 mawu ake ndi onvetsa chisoni kwambiri 🤣 apule 🙌🙌🙌🙌
@elizamaster2168
@elizamaster2168 17 күн бұрын
Achakwela musamathe mawu kumbukilani kt ovota ndife Malawi amene tikukumana nd mazuto muulamulilo wanuwu
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 17 күн бұрын
Eti eti
@MwambakuluKamwambasa
@MwambakuluKamwambasa 17 күн бұрын
Am a boy who belong to both two sides Lomwe and Chemwa because my dad from kasungu in Santhe and mom in thyolo Thomas .u like it or not .am a solution.
@user-rl8xs2kf1o
@user-rl8xs2kf1o 17 күн бұрын
Kodi Ali ku kapeni 😂 ayiwala zomwe apitira mbuzi za anthu
@user-cq1wv9nq4y
@user-cq1wv9nq4y 16 күн бұрын
Aaaaa ine mmene ndanvera ma speech awo kumeneku nduona kuti uyu unali mnsonkhano wa ndale wa mcp not mwambo okumbukila Kamuzu asamatinamizepo apa olo aja akuti achimwendo aja kulakhula kwanji kumenekuja ati akutchula Peter Munthalika ati sangatenge boma aaaaa zugwirizana chani ndi mwambo okumbukila malemu Kamuzu??? Eeeee koma guys ku Malawi mmm ayi zikomo
@petertaulo8014
@petertaulo8014 17 күн бұрын
Mbuzi ya munthu sitha kuyankhula
@davidmalasa9912
@davidmalasa9912 13 күн бұрын
Kamuzu sadamange stedium iyi ndi sir geofry cobby
@DannielOnions-fy3dc
@DannielOnions-fy3dc 15 күн бұрын
God knows what comes next
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 17 күн бұрын
Apule kuyesera kubayibitsa anthu ku Kamuzu Stadium, eti anthu kumangoyang'ana osabwezera kkkkkk! Koma m'Malawi anakonza ndithu.
@JackMvura-ik2td
@JackMvura-ik2td 17 күн бұрын
Sanje akulu ndinu afiti eti mumadya matewera kwanu eti demeti or pitala angafike gulu limeneli mbuzi
@LamseyLazarous-dl5qd
@LamseyLazarous-dl5qd 17 күн бұрын
Anthu akeso ndiwomwewa anali zulo ku DPP
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 17 күн бұрын
Izitu sizinali za chipani
@user-mh9se5to6k
@user-mh9se5to6k 16 күн бұрын
Kkkkkkkk zoonadi big
@user-jw5rx9ze8k
@user-jw5rx9ze8k 16 күн бұрын
Koma chakwera mwati ali ndi nzeru? Ndikuona ngati chomwe akuyankhula sakuchidziwa.
@ElvisSpesho
@ElvisSpesho 16 күн бұрын
Makamaka chisilamAchakwera amadana nacho limodzi nd anthu akulilongwe,bas zingo khala zamutundu,tsopano msilam ndye ali paliponse,azichemwali anu onse anakwatiwapo ndi msilamu tili ndi anatu mwa kabudulamu, kuphiri la njudz,kwamasumba,ndye nkhondoyo ife tingo ona kucheedwa,kt tikuonetsen
@spargomw
@spargomw 17 күн бұрын
Kwasonkhana zipani 9😂😂😂😂 Peter dzana lija aliyekha koma kunali chiguluuuuuuu❤❤❤❤❤
@user-jr7bq8sw6t
@user-jr7bq8sw6t 16 күн бұрын
Ndipo ine utu sindimamva mfundo zzomwe amayankhula Koma mukuti olo ulaliki wake unali omveka bwino bwino?
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 17 күн бұрын
Ameneyo akuona ngat mchalichi eeeeeee kupitiliza kunama
@GreshamDaniel-hu5ht
@GreshamDaniel-hu5ht 16 күн бұрын
Galuyii achoka bas afune asafune
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 17 күн бұрын
Achabale akeo akwiyatu
@MphatsoMannet-uf5nm
@MphatsoMannet-uf5nm 16 күн бұрын
apm.my vote baba palibe ncanzelu ndikunva.mwainu.sakho.hvy
@LovelyBlini-cu3iu
@LovelyBlini-cu3iu 17 күн бұрын
Akudalira kuba awa
@user-xi2jz8ru1w
@user-xi2jz8ru1w 17 күн бұрын
Komasotu big wa samata kusanga or wa kazi awowatu kungo kala ngati nyapapitu
@YohanePatrick-lc2lq
@YohanePatrick-lc2lq 17 күн бұрын
Bt niya azungu
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 16 күн бұрын
Ndipo atakuvotere ndan
@user-lk8kj9zv6x
@user-lk8kj9zv6x 17 күн бұрын
Nyawu razalo
@geoffreykankhomba
@geoffreykankhomba 15 күн бұрын
Ovota ndi anthufe kulankhula uku its like ma vote muli nawo mnyumba mwanu ,sitinaiwale ñjala ,kukwera kwa zinthu kubvuta kwa chakudya ,kukwera kwa chimanga mpaka 60 000 zomwe sizinachitikepo mu History ya Malawi ,ziwani kuti anthu ada nanu kukhosi kuyambira ku primary school mpaka ku collage ,ma civil servants ndi Ena onse ,aphunzitsi ndi ena onse ,kufikira munthu wakumuzi sakufunanso kumva dzina la tonse alliance and MCP tionana September 2025 ndipamene mudzaziwe kuti Amalawi anatopa nanu
@BaldwinBanda-gd9zo
@BaldwinBanda-gd9zo 11 күн бұрын
Chakwera ndiwe mbuzi yamano pasi
@user-xs3nj1es1r
@user-xs3nj1es1r 16 күн бұрын
Peter Mutharika awinaso🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@yassinmpangiwa
@yassinmpangiwa 17 күн бұрын
Apm my vote 😂😂
@mussahkachere2332
@mussahkachere2332 17 күн бұрын
Kom amalawi nd anthu onvesa chison kwambil 😂😂😂..anthu tikuvutika km still kuiimbila mmanja zinthu zopanda sogolo..
@preciousthafungaunje6631
@preciousthafungaunje6631 17 күн бұрын
Osaiwala kut amalawi Fe Tu tangofuma kumudyela munthu kma awa antha
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 17 күн бұрын
Eti makamaka azimayi chosecho usiku azikagona nd njala
@Hastings-on9is
@Hastings-on9is 17 күн бұрын
Sindikuziwa kut anthufe timaganiza Chan,, mpaka kululutira garu ija koma😢
@MavutoNgoma-kk6lq
@MavutoNgoma-kk6lq 17 күн бұрын
Garu yamuthu çhakwera
@patrickscott9086
@patrickscott9086 16 күн бұрын
Ndizona tizivutikabe bas muziba ndalama muzilemba job aku banja lanu
@DevisChikapa
@DevisChikapa 17 күн бұрын
Ameneyi ndi galu kwabas
@davidkadyakapita8836
@davidkadyakapita8836 16 күн бұрын
Zaziiiii Chakwera ndi chitsiru kwambiri
@ChrispinJohnson-py5ie
@ChrispinJohnson-py5ie 17 күн бұрын
madala mukunama mwalaphela mulibe nzeru olo mfundo mulibe
@ChrispinJohnson-py5ie
@ChrispinJohnson-py5ie 17 күн бұрын
kape chilichonse choyankhula kulemba basi kupanda nzeru galuu
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 17 күн бұрын
Kodi ameneyu amalembela ndani
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo 16 күн бұрын
Ukunama ase ng'ooo udye ndalamazo komaliza wopusa iwe
@user-lv4qd4pm1e
@user-lv4qd4pm1e 17 күн бұрын
Chakwera my vote wina afune or asafune mcp pachiongolero
@giftjamali8204
@giftjamali8204 16 күн бұрын
Muthu ukamati nkazi uyu ndimukwatila umakhapa kuti madongosolo onse ofunikira manja wapanga Apure akukunaminzani pls konzani nyumba yanu yokapumila
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo 16 күн бұрын
Mulungu atithandize munthu uyu woipa mtima
@user-tr2gp5vt8o
@user-tr2gp5vt8o 16 күн бұрын
Mutu owuma chakwera
@user-pf5er7gc9s
@user-pf5er7gc9s 17 күн бұрын
Ndikufuna passport yanga mkulu zonamizana apa ai. Zinazo mukumanga kumalawi komwekuno?
@CharlesmakveliNyirenda
@CharlesmakveliNyirenda 17 күн бұрын
Kkkkkkkkkk
@christophersmunthali5348
@christophersmunthali5348 17 күн бұрын
Zoona mulungu ayenda
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 17 күн бұрын
Akufuna kubela agalu awa
@EmanuelPaul-io2hk
@EmanuelPaul-io2hk 2 күн бұрын
Ine zandale simbali yanga,chakwera samaopa Mlengi mwachidule mkulu wasanaki.
@user-nk5mj5ws8v
@user-nk5mj5ws8v 16 күн бұрын
achakwela mudziyangula momalidza udindowo mwiniwake a kubwela bola yiweyo walawa nawo koma adzanu achilima eeee wauponda
@user-rd2td7bg4c
@user-rd2td7bg4c 17 күн бұрын
Palibe angavotele ameneu wapenga
@alexsumani6823
@alexsumani6823 17 күн бұрын
Maloto achumba
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 17 күн бұрын
Ndiye iye wapanga chan ,zongoone likasa
@KumbukaniZgambo-xd9tm
@KumbukaniZgambo-xd9tm 15 күн бұрын
Kwachematu kkk
@DannielOnions-fy3dc
@DannielOnions-fy3dc 15 күн бұрын
God can not do that much TO M.C.P again
@bigthellamwechande8641
@bigthellamwechande8641 15 күн бұрын
Boma ilooooooo
@user-et3il7pi7t
@user-et3il7pi7t 16 күн бұрын
Nanga kuthesa katangale muthandizapo bwanji pamenepo
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd 17 күн бұрын
Ukochooooka!!!!!!
@MAYESO-ub9dm
@MAYESO-ub9dm 8 күн бұрын
Pulezidenti opanda mfundo zogwilika
@ElizabethMajiga
@ElizabethMajiga 17 күн бұрын
Mulungu amamva mapemphelo ana akee
@mathewskapinga5227
@mathewskapinga5227 17 күн бұрын
Chakwera my vote
@DavidKalumo
@DavidKalumo 16 күн бұрын
Nonse otsutsa tikuti nonse yiwalani mwamva kodi ?
@GloryRudraksh
@GloryRudraksh 11 күн бұрын
Funso ndiloti mukazawina 2025 muzapanga chani
@AbuOsman-ts6ef
@AbuOsman-ts6ef 17 күн бұрын
Chigawenga chija nanu
@usumanidaudi
@usumanidaudi 17 күн бұрын
This man is mede
@innocentissah2636
@innocentissah2636 17 күн бұрын
Mr President mukulankhula zakumapwa........ mwamva
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 17 күн бұрын
Kkkkkk
@user-px9gd6fc6w
@user-px9gd6fc6w 17 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂zitsilu ooyeee kkkkkkkkk 🤣🤣🤣😂
@harrymicah6140
@harrymicah6140 16 күн бұрын
😂😂😂😂 zoti anhaeinenso akuluwa mmm mwina kumaloto
@user-zm9nl8zn2b
@user-zm9nl8zn2b 17 күн бұрын
Akhwangwala inu osowa nzeru
@KondwaniJ.Nkhoma-wt5zo
@KondwaniJ.Nkhoma-wt5zo 16 күн бұрын
Awaso koma akodzera bulangete sanayanike. Ayiwala kuti usiku ukubweraso
@JohnPoul-lk5yq
@JohnPoul-lk5yq 17 күн бұрын
Chakwera woyeee
@MadaChinkhombe
@MadaChinkhombe 9 күн бұрын
Boma lakukanikani sir
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 16 күн бұрын
Wandikweza bp sindikwanisa kumaliza video iyi , zausiru
@ChifundoChingwalu
@ChifundoChingwalu 16 күн бұрын
Ngati tili ovota ndiiyeyo Sadzadzitha
@PeterThawi-jc7zl
@PeterThawi-jc7zl 4 күн бұрын
,😂😂😂😂ambuye atiyendele...awawa nde ahyi...mmmmhhh
@user-hq6dq7zr1e
@user-hq6dq7zr1e 17 күн бұрын
Adad omwewo moto buuuuu💥
@patrickmenyauti4876
@patrickmenyauti4876 17 күн бұрын
Awa ndi achisiru ndithu
@PhillipKashot
@PhillipKashot 17 күн бұрын
Ngwape iwe 😂
@KhumboKawelama
@KhumboKawelama 16 күн бұрын
Chakwera 2025 my vote
@DionKumilayi
@DionKumilayi 17 күн бұрын
Pantumbopawo ndithu
2024 Elections | EFF, Rise Mzansi satisfied with votes received
10:59
UTM Musapusitse A Malawi Lero   Bon Kalindo
17:09
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 36 М.
100😭🎉 #thankyou
00:28
はじめしゃちょー(hajime)
Рет қаралды 23 МЛН
Miracle Doctor Saves Blind Girl ❤️
00:59
Alan Chikin Chow
Рет қаралды 36 МЛН
Pray For Palestine 😢🇵🇸|
00:23
Ak Ultra
Рет қаралды 27 МЛН
Did you find it?! 🤔✨✍️ #funnyart
00:11
Artistomg
Рет қаралды 121 МЛН
Namadingo - Kondabe [Visualizer]
3:23
NAMADINGO
Рет қаралды 268 М.
Izindaba zesiZulu @13H00 | 31 May 2024
23:27
SABC Izindaba
Рет қаралды 39 М.
BON KALINDO WAKANG'ALULA YA ACHILIMA 31 May 2024
15:56
HOT 265
Рет қаралды 6 М.
Cruise 5 with Prophet Habakkuk Stanford Sinyangwe
1:06:02
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 89 М.
100😭🎉 #thankyou
00:28
はじめしゃちょー(hajime)
Рет қаралды 23 МЛН