Ndipo I wish ndikanaonera live awawa udindo wawo akufuna anthu aziwaopa osat kutumikira anthu ndipo ahhh.....😊
@salimmkumakumakitombi-yc7pw Жыл бұрын
Kodi mlendo anali ndani pa Hot current imeneyi.... nduna yoonjedxera nkwiyo kwa A malawi
@KinziwindassoniKinzi3 ай бұрын
Nzeru ilibe ndunayo ubwino wake 2025 mbava zikuchoka
@SharmamontenJafalisharma2 ай бұрын
😢😢
@ancientnkhata1137Ай бұрын
Mbamva zinachoka kale 2020
@bi8942 Жыл бұрын
A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri. Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025. AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa
@eliffagondewe8214 Жыл бұрын
Kkkkkkk
@gavinpillay125310 ай бұрын
Galu wammpha dzikodi silingalongosoke ili nduna yaza chitetezo ikuyikiraso kumbuyo mbwererazi
@Extratremendouszeus3 ай бұрын
Chilbe nzeru chunkhumba chimenechi He uses his udindo wrongly
@BennettNjedza2 ай бұрын
😂
@AndsonAcd-j6iАй бұрын
Mumatha 😂😂😂
@MotivatedI Жыл бұрын
This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing
@Littlefair7 Жыл бұрын
He forgot we're in a democracy with his dictatorship mentality.
@mercythom586810 ай бұрын
Poyamba ndimaona ngat Times imadana ndi DPP koma now ,,,,,ndazindikira kut it's only times yomwe tingaipange trust❤❤❤❤❤
@Mbesa09 Жыл бұрын
I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.
@MADALITSOMISHEC Жыл бұрын
😂
@tadalarhostinchiphwanya7891 Жыл бұрын
Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.
@ezekielchihana2927 Жыл бұрын
@@tadalarhostinchiphwanya7891true
@stevekamangaFrancisАй бұрын
This is true these guys akhalitsa they need to change hosts otherwise akuzifila too big for Malawians akudzimva usukuluzi
@thondoyaenterprise3795 Жыл бұрын
Big up minister for taking these kids to school.
@moseskavalo3304 Жыл бұрын
The nduna himself doesn't know how to argue,,too much emotions ķkkkkkkkkkk hahaha MCP is dangerous party indeed
@fedson2050 Жыл бұрын
This Hot Current palibe chimene tatola ngat ife ma Listeners ndim'mene akuyakhira wakubayo
@g_deonm5793 Жыл бұрын
I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.
@rasulrayman4517 Жыл бұрын
Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..
@FranksonKennethChipande6 ай бұрын
2025 ndi Chaka chamawa Why panic with this thing Let's go and work for our better
@dellingsmunthali2669 Жыл бұрын
Nyama zikulu-zimulu dada zikhare munthu murara chomeneeee ntchindii zikumwenererani chomene pa yankho rakut president azakhara chakwera motoooo💥💥💥💥💥💥
@adonvingison4331Ай бұрын
Mukakhala pathunzi musaone ngati azanuso alipathunzi .aim speak with you boss
@moseskavalo3304 Жыл бұрын
We are sad Nation
@keithmlenga4657 Жыл бұрын
You, not we😅, I am not
@KennieChangs Жыл бұрын
I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk awiliwo angopanga zibwibwi
@BrownNamondweАй бұрын
Iwenso ndi mbuzi
@augustinechibbalazi88973 ай бұрын
Zinkhali Ng"oma is skilful at his work.Hon.Minister please,keep watch on illegal influx of immigrants here Malawi.
Abanda andunawo asakane kuno ku phalombe tinapereka ndalama 30 pin mpana pano ndalamazo zinapotera tinaberedwa bas aaaa
@JoshuaChizampeniАй бұрын
Ndipo uyuyu zikhaleyu NDi machine mafuso enawa NDi ambwerela
@jacquesnsabiyaremye3166 Жыл бұрын
Akuti zinthu zitsika😢! Koma Chimunthu chi ndi cha Pokoso bwanji!!
@precioussauli2887 Жыл бұрын
Honorable Minister is not able to take questions as asked. It is normal for AIP beneficiaries to increase as the population of the country is also growing extremely. And regardless of the increase of the beneficiaries, only a few out of the ones that were supposed to benefit this year benefited.
@confidencezunguya7552Ай бұрын
Zikhale amatha kuyankha guys
@PeterThawi-jc7zl Жыл бұрын
Guys let's gather here for comments😂🤣🤣🤣
@SautsoBandah-lf4so Жыл бұрын
Guys u r losing control of your interview
@JacksonMoyo-tm8dv2 ай бұрын
Zinthu zadula koopsa nthawi iyi ya Mcp
@languitoneelias9972 Жыл бұрын
Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de
@patricklimiton1023 Жыл бұрын
Inuyo kuzitenga kuzindikila ??
@ChristinaKachoka2 ай бұрын
😅😅😅@@patricklimiton1023
@stevekamangaFrancisАй бұрын
Program yanu mudzimpatsa munthu mpata kuti alongosolele mfundo zache kwa Malawi am not saying this for the minister in particular. Program yanu imaoneka kuti mumamuitana munthu kuti mudziputsitsa, osati akuyankheni, Inu timakumverani dairy. Hot current, editors chani chani. Pankuku learn to manage time,
@MphatsoSimiliwadi3 ай бұрын
Very wise minister
@AlexHenere-r6lАй бұрын
Muchedwa naye musiyen ndiwamakani ameneyo
@BrownNamondweАй бұрын
Makani ake opanda nawo nzeru
@MichaelChisenga-n4h2 ай бұрын
Ndiolotse ndi kakudye nde ameneyu
@BenissoneErnesto-kn9bd Жыл бұрын
Watching from mozambique
@MarkCropper-z2m Жыл бұрын
Mximm zautsiru anduna anuwo akuyankhula zichani😊
@madalitsoonale5338 Жыл бұрын
My Malawi 😭😭😭😭 y having useless minister like this one, useless government too😭😭😭😭😭
@YohannyMangulama2 ай бұрын
Amanjaila bulaan apa wakumana naxo
@AlexHenere-r6lАй бұрын
Musiyen wakan
@chikoko-uj2tt Жыл бұрын
Tell him mr Nanyon is a human being also
@PatrickKandulu-i6g Жыл бұрын
Komatu andunawa awachenjelera akanganyawa eee
@BarnettKaphukaАй бұрын
🔥
@James-uq6hv Жыл бұрын
Kkkkk kids are taken into a class, the kids have their sponsor, bravo to the minister Zikhale for the response trying to educate a bulutiwa
@ShakiraJackson-x8w3 ай бұрын
Nduna iyi ikhadzangolowatsa mboma it means dera lakero ladzaza zitsiru zokha zokha
@aronluka8086 Жыл бұрын
Duna imeneyi kodi imakhalira kuti zoti anthu adalandidwa ma 30 pn iyeyo sakuzidziwa koma ameneyi
@awesomechannel77523 ай бұрын
This guy need an evidenve from you guys but was he producing the the documentantion ya constitution yo?
@DavieJames Жыл бұрын
Let the minister answer questions not asking questions
@MaxwellBinauli2 ай бұрын
Koma boma la mcp Linangotengana zidepete zokha zokha ,Zikhale ndimunthu oti kumamutchula nduna zoona chitsiru ngati chimenechi
@BrownNamondweАй бұрын
Oyipa awa
@BrownNamondweАй бұрын
Awina akaba
@jeuzywandasigner49083 ай бұрын
This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾
@MburaChona Жыл бұрын
Nanga evidence go to agreement ya succession anasainira ena a mu alliance ili kuti? The minister should produce It, infact a nation is not led by more than one President, does not make sense.
@wakisawinga27443 ай бұрын
Now I know what he meant by being the strategist 😢😢😢😢
@charlespaulbanda8136 Жыл бұрын
I like how nduna imeneyi pays attention when someone is on the flow
@ancientnkhata11376 ай бұрын
He pays attention to details Eish
@LukaAfromad2 ай бұрын
Anduna mukukana zoti AIP sikuyenda bwino?
@BrownNamondweАй бұрын
Mr Brian mulipafupi ndi mbuli munthu oipa ameneyi
@MphangalaАй бұрын
Kodi mlendo ndi ndani mu Hot current imeneyi chifukwa tu apa sipakuoneka mlendo oyitanidwa pamalopa
@KumbukeniThomaschimbenje-hw2rcАй бұрын
Ku malawi ufulu kulibe zokamba za andunazo aaaaah zofunika ana a std 1
@Sabina-hw4js3 ай бұрын
People are sleeping for days without food yet them are having big stomachs
@Sabina-hw4js3 ай бұрын
Whether kukwera or not people are suffering.
@fredwchipatalaАй бұрын
Muwuzeni kuti koma asayiwala kuti kuti kuli bakili muluzi tv
@DanielZunguza14 күн бұрын
Awa ndi omwe anapha Biyeni muthuyi ndiwoyipa kwambiri.
@leonardmussah7902 Жыл бұрын
This has been one of the poorest interview so far, the minister has failed to take all the questions & frankly speaking he has acted as a football commentator