Bayana akunena zoona pa za environment yaku malawi, imagwetsa mphwai munthu kulimbikira
@FisherAction8 күн бұрын
Good
@LeyvanSamuel-pe5tc7 күн бұрын
Good said 👍 guys always mumayima pa chilungamo
@MosesLeckson8 күн бұрын
Pena pake tiyeni tizivomereza kuti a Malawi ndi olimbikira.Palibe uyo amadalira boma.Timadya,kudzigulira zovala,kudzigulira mankhwala tikadwala ndi zina zotero patokha umoyo mkumayenda.Zosalimbikirazo akuzidziwa ndio malinga ndi anthu omwe amawadyetsao.Tikudandaula kukwera mtengo kwa zinthu ndiye titani ifeyo kulimbikirako kuti zitsike?Asaiwale kuti omweo amatipeza mkumadzatilinjeza ndiye zomwe amatilinjezazo kodi poti akhala pamipando chikhaleso chitonzo?
@peterchikwakwa84766 күн бұрын
True
@peterchikwakwa84766 күн бұрын
Boma ndilosalimbikira ndiye anthu alimbikira bwanji?? Pulezidenti kumangoyenda, malo momanga dziko, zomvetsa chisoni, look at what bingu did? Anali serious ndi Boma and anthu nso started doing things differently