Musalimbane ndi peter komanso Atupele ...pakampeni paja amaneneratu poyera kut MUSAVOTERE MCP ...nde anthu sanamve akut umafuna change...This is the change..the change can be positive or negative....asiyeni a MCP alamulire chifukwa ndie zimene munavotera...tichimine kaye a malawi...Pena Mulungu amapanga zoti anthu aphunzire kwambiri
Koma boss ndiiwe ozindikira koopsa keep it up, mavutowa tinachita kubwelesa tokha. Anatiuza ndipo anatilangiza koma kusanva ndipo ananena Peter Muntharika kuti mukupanga inuzi akubwerawo muona Nyekhwe. Lero ndiizi kaaah
@DanielZitande-y1d2 ай бұрын
Zoona brother uyu walankhura odiyo iyi ndi mbudzi ya Mano kunsi, ndipo samadziwa chomwe amanena. I love you u ndipo mau anga mwandinenera ndinu❤❤
@JohnAsendi2 ай бұрын
Zikomo amwene papani Mr pita ndi Tupele muzitikhululukila zoona vuto ndi ife ndithu🙏🙏🙏🙏🙏
@LeonardChinomba2 ай бұрын
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi
@macrinenduna10242 ай бұрын
Good comment. Truly these two Gentlemen are real country men.
@MonicaSteve-t5p2 ай бұрын
Good correction sir ❤❤
@WayneWinterbottom-y6s2 ай бұрын
More fire mr D takunyadilani kwambiri mwalankhulabwino
@PetroMatias2 ай бұрын
Ase wayankhura bwino mmanja mwako 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🤝🤝🤝🤝🤝🤝
@JohnJohn-og8rt2 ай бұрын
Ameen Iweyo mulungu akudalisene moyo ukuyangula zabwino mau amuna asitero amavuna dala athuwo
@LovemoreSalima2 ай бұрын
Thanks D phiri Auzeni ana amahurewa, Ndiomwe atifikitsa pa manyiwa. Bu shit, anthu amanyi amenewa. Azimuloza Chala ntambo.
@EdsonKamwendo2 ай бұрын
Mai woputsa iwe umafuna azingoyenda wamba iweyo siukuziwa kuti mcp ili ndi chiwembu chachikulu kodi mcp yakutuma ? Ugaluwako
@chifundocharles23482 ай бұрын
This is true boss,, atupere or munthalika asiyeni mavutowa ndiifeyo amalawi kusamva lero ndi izi
@FisherAction2 ай бұрын
Ndiye ngati akutero kut samatengapo gawo nkwabwino asayime asiye omwe angamathandizire kumamenyanawo nkhondo bcz we are in democracy no words kupembezana
Ndipo Apm ndi atupele 2025 anatisiya tikhaule tinapanga chipongwe tokha
@ElizahMadi2 ай бұрын
Malawi ngakhale wuyifele ,aaa ,chilima anapita ,nkhani yake kufera Malawi . Malawi si woufela
@MoosaDawood-l5c2 ай бұрын
Musiyeni uyo wadya banzi walandila ndalama.Mangochi singavotele mcp ai
@HUMPHREYBALANGWE2 ай бұрын
Tiyeni tingoyang'ana kutsogolo Munthu amadikira chopereka church kuti akhale ndi ndalama ndie mumaganiza kuti angalamulire dziko Lero ndi izi dziko latsala masanza okhaokha
@IsaacMusa-py2jm2 ай бұрын
Powerful 👊
@gracemkandawire87692 ай бұрын
Tinalakwisa tinavotela ena ndiyekuti tisadzudzule? Usanena kuti musakonze ayi ,,wa Aodio sanalakwise,,,tisawagwadile Oro kuwachonderela,,Iwo nde azamwe mkaka,,
@MiddayDeleza2 ай бұрын
Sanayankhule di bwino bambo amene aja Peter ndi atupere komanso former president Bakili Muluzi anayankhula po za mcp koma anthu kusambva lero ndi izi nde akamayankhula aziyamba aganuza kaye osamangobwebwetuka
Alomwe muli patchito chakwela ndukuzani pano simungamuchotse mulakhula mutopa chitsazo ma by election mukungoluza daily
@CassimMbalaka2 ай бұрын
Walandira ndarama za mcp amenyo
@SellinaSanena2 ай бұрын
Kusamva kwathu. Don't put the blame on Peter and Atupele. Tinavota tokha
@MarthaMbewe-uk5nn2 ай бұрын
Iyeyo akuona ngati a opposition angokhala? A Peter ndi atupele TU siopusa akumuwelenga kaye chakwela yu AKUFUNA amlize kaye uchitsiru wakewo kenako adzuke koditu campaign sinayambe kukhala zinthu a opposition mukuwanyozawo simuwafuna
@GeorgePhiri-ub2of2 ай бұрын
Tsono mukuona ngati mcp ingachoke boma ndi kutukwana kwa ma akitivisinu anthu muli ndichibwana kwabwasi tiye nazoni mukhala ku kotsutsa konko
Kma ndiye akuchita kuonekadi kuti awapatsa kenakake chifukwa nde akulubwalubwatu
@JusticeKawilira2 ай бұрын
Mwayankhula bwino kwambiri
@AshanAlexx2 ай бұрын
Watiyakhulila mwene
@AlliSaiti2 ай бұрын
Uku nde kuyakhura mopanda nzeru😅😅😅😅😅😅 kod adpp abalalika eti
@thulanimpphiri68732 ай бұрын
Zoona Peter atupele si ozikonda vuto ndife amalawi ovota mitu inawuma mtanyiwa kalindo bakili TV Peter atupere ndi ena ofunila Malawi zabwino alankhula za mcp koma sitinave. Panopa mukuona mcp ikugwirisa ngongole and ikugawa ndala and amalawi tawona mumene wafera chilima ndi abale athu koma still tikusapota bomalo amalawi tili ndivuto loganiza bwino. Munthu kuti mumuziwe kuti zeru alibe boma kuyakhula mwamatama kuzikona kupereka ndalama kuti anthu amuvotere
Tinawakana amapha ma albino amenewo asiye akalamba panopa sitikumvako kuti agwira ziwaro za anthu boma la peter linalibe security ndiposo wakalamba wapume zina mumangonama mulizambiri mu malawi panopa tikuwona zachilendo kale kunalibe ngati ndikukwera kwazinthu si malawi yekha ife tikufuna chitukuko basi zimene mukulankhurazo sizikumveka bora chakwera ndi anthu anuwo
@MohammedAriesa-j4x2 ай бұрын
Opusa
@LovemoreSalima2 ай бұрын
Gulu la mahure opanda mzeru ndimanena aja ndi m'modzi mwaiwo ndiweyo. Hule
@yotamumahomed13132 ай бұрын
Komanso umuuze kut watikwana
@shazirahJafali2 ай бұрын
Izi nde ndizoonad osapanga complain pa anthu awa ayi vuto ndamene anachotsa dpp kukavotela mcp
Ndipo big amai amenewa ndi chimbuzidi zedi Amai opanda nzeru
@yassinn56342 ай бұрын
Zaka 84 angathamange.? Anthu osazindikira inu Peter akanangotuluka tsiku limodzi mukuganiza khansala wa DPP akanaluza? Tulo basi
@JACKSONHULUWA-j2n2 ай бұрын
Nzeru ulibe
@yassinn56342 ай бұрын
Iwe ukuyankhulawe ndi Peter muthalika kapena Atupele akupatsa chani chitsiru iwe kagwade wekha kupepera eti kuzolowera kunyambita nsapato .Khala pansi asiyire anthu ozindikira aziyankhula. IWE SINNENERI WA ANTHU AWIRIWA
@yassinn56342 ай бұрын
Asiye ayankhe okha
@KestonNGUBO2 ай бұрын
A dpp mbuzi yagalu iwe ukuyakha
@JackMvura-ik2td2 ай бұрын
Tsono iwe wadya banzi ya pitala munthu wadyewa uku one kuziro 2025 mukunya chakwera bomaaa iwe mulomwe mwachepa achewa ndayao atumbuka simuwatha komaso ozindikila alomwe ena Asari Ngati iwe samuvotera pitila DPP yatha Palibe akuifuna tanganizani Mangochi zikumvekanso Kuti mwina pitala akhoza Ku votela chakwera😂😂😂😂😂😂
@LeonardChinomba2 ай бұрын
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi