Gulukunyinda the big nyau Chakwera alinso komweko,tamugendani galuyo.Mmutu mwake muli magawo 2.Gawo loyamba kuli zoipa zokhazokha gawo linalo kulibeko kanthu😢😢😢😢😢
@eliaskhofielias81523 ай бұрын
KuMalawi kulibedi international legend ndaonela pa lucius banda.anali chabe legend wa malawi mokha basi.akanakhla wa international akanamuika ngakhale news zakinja achina BBC,even pa south africa pomwe atisiya iyepa akanamulengeza pa SABC News ngat anachitila Oliver ntukudzi. anafera kunja ku USA koma news break down news everywhere the whole world including SABC NEWS.mpaka kumpangila programme yake yomukumbukila pa morning live.koma banda not..
Iweso billy usaname apa iwe ndi soja panalibe ubwezi soja anali mbava anadya ndalama dzose dza Paul chaphuka anadya ndiye akatibulana konko
@AlexKaunda-ny2eg3 ай бұрын
😂😂 Chimwendo Banda mphuno Ngati nkhumba munthu akafa mbili siyimaipa ndinu a MCP mwamupha😢😢
@CharlesmakveliNyirenda3 ай бұрын
Kkkk chimwendo ndi wa usilu 😂😂 chi mutu kukula ngati matako a Monica chakwela ku chepaso😊😂
@Magamax-qc4jg3 ай бұрын
Tizamusowa mr BANDA 😢
@MalekanoChikaonda3 ай бұрын
😢
@IqraKandulu3 ай бұрын
Bily asaname amamunyoza
@MikeMerecah3 ай бұрын
Ena kuchita kupha bora licias anavutika akapume ngati mkotheka,,,,,,,
@marthamusukwa79353 ай бұрын
Rest in peace Soja
@PreciousMkomo-yn6ge3 ай бұрын
Rest in peace Soja
@BENSONRANGWANI3 ай бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@AlexSilence-p3l3 ай бұрын
Rest in peace soja
@CharityChirwa-t1e3 ай бұрын
Tizakusowani Abanda zambili tilibe pachifukwa choti amalawi mukanyengo kochepa taluza athu ofunika kwambili zimuwanu uwuse ntendele osayiwala moni kwachilima moni kwa matafale moni kwakasambala moni kwa po champhuka wina kwa chibade wina kwa atoti manje wins kwa katelele wina kwa matse 💔💔😭😭😭😭
@VungaQueen3 ай бұрын
Amen Moni ukawafike ndinthu anthu awa muzimu yawo iziutsa mumutendere