BON KALINDO WABWERANSO NDIIZI TAMVERANI 05/09/2024

  Рет қаралды 34,023

Mpungwe-Pungwe mw

Mpungwe-Pungwe mw

Күн бұрын

Пікірлер: 56
@ChristinaMdeza
@ChristinaMdeza 11 күн бұрын
The DC nenani chilungamo bas chiyende ngati madzi koma zonse tasiya manja mwa Mulungu bas ❤❤❤❤
@RobertPhiri-gt2cr
@RobertPhiri-gt2cr 10 күн бұрын
Bon kalindo umatiimilira Mbava zichoke 2025 muome mseu wa mugabe hiway mmene uliri zomvetsa chisoni ngati kulibe boma 111st ❤
@MariamJaffali
@MariamJaffali 11 күн бұрын
❤❤❤❤ boniiiiiiiiiiii kalindooooooooo the DC
@ThomasMwandila-tn7cf
@ThomasMwandila-tn7cf 11 күн бұрын
Wamisara akufuna chipani choti aroweuyu,siuyu wayamba kuyendandi U.D.F
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 11 күн бұрын
Mmmm!!!!!
@Outi-p7d
@Outi-p7d 9 күн бұрын
Palibe zokuti zonse tisiyile mulungu . Koma action can help so much . Chondechonde tatiyeni tionese mbanvu kuwanthu.
@KelvinJpchimphepo-sh6nc
@KelvinJpchimphepo-sh6nc 10 күн бұрын
Ada amenewa asapangeso ndale chifukwa one day akazapanga ndale azagendedwa
@KondaniPhiri
@KondaniPhiri 11 күн бұрын
Talankhulani bwana DC malawi ikugonabe apa. Timuphe naye anthu onse ndende akagwire
@ChimsyUlemu
@ChimsyUlemu 11 күн бұрын
Ndipo ndiye ndizoonadi Malawi anthu anapusa kwambiriiii aphedwenso nawo iyaaaa these duckies
@IsaacKamanga-cv8ec
@IsaacKamanga-cv8ec 10 күн бұрын
Ati kusowa nkhondo 😂😂
@RobertPhiri-gt2cr
@RobertPhiri-gt2cr 10 күн бұрын
Koma ndyetu tikuberedwa kumalawi
@user-ux3ed3ni1p
@user-ux3ed3ni1p 11 күн бұрын
Acommanda and chief akanika kuti teteza.
@KelvinJpchimphepo-sh6nc
@KelvinJpchimphepo-sh6nc 10 күн бұрын
Mgwilizano tilibe, vuto osogolera palibe kut anthuwa amangidwe komaso akubanja ndamene afookesa amalawi sakulakhura kut anthu akhare ndi mphavu anthuwa akana choka, akanayimisidwa kaye ntchito awonese chilungamo
@HaliJana
@HaliJana 11 күн бұрын
Kusachosako ndipomwe muziwe kuti ndi plan oseo anaphela limodzi sangachosani tichosa 2025 ndikuonanao zochita
@MustafarBridon
@MustafarBridon 11 күн бұрын
Dc boniiiiiiiiiiii kalindoooooooo
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 11 күн бұрын
Munanena mawu a DC kuti amalawi siwowafera ndi chifukwa chake ziko lamalawi likupita aliyense akungoyang, ana tizionerani limodzi popeza tonse tili momwemu
@KelvinJpchimphepo-sh6nc
@KelvinJpchimphepo-sh6nc 10 күн бұрын
Basi khani ikhare tiwadikire 2025 Mesa kupusa ko tikunena ko anthuwa chaka chino akanayimisidwa akanayitanidwa ku bwalo lamilandu
@UthumanMwangala
@UthumanMwangala 11 күн бұрын
Amalawi ife tulo chomwe tkuzwa ndikudikila kut bakili tv kapena bon kalindo ayankhulalit pa social media tipange coment bas
@JoyceBanda-k8t
@JoyceBanda-k8t 11 күн бұрын
Pepani aprezdent anthu osauka pp asakhale mawo pa mgwirizano chifukwa ndi joyce Banda mmmmmm timamuopa
@Mustapher-fb4qp
@Mustapher-fb4qp 11 күн бұрын
Boni karindo warowa udf
@paulvan9306
@paulvan9306 10 күн бұрын
Zoona
@RobertPhiri-gt2cr
@RobertPhiri-gt2cr 10 күн бұрын
The Dccccc❤❤❤
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 11 күн бұрын
Pangani gwilizano nonse mwatchulidwa apawa ma udindo oyamba akulu akulu muzapereke mofanana pozasata ndi m, mene chipanicho chizapezere ma percent ake
@SamuelLiwonde
@SamuelLiwonde 11 күн бұрын
surely ma guys aku defence ndye anayenera kuimitsidwa
@ChimsyUlemu
@ChimsyUlemu 11 күн бұрын
Kkkkkkkkk akakomoka kumangowathila acid basi Malo mwa madzi
@user-ps5tv4hq3c
@user-ps5tv4hq3c 10 күн бұрын
Yes ❤❤❤❤❤❤
@RobertPhiri-gt2cr
@RobertPhiri-gt2cr 10 күн бұрын
Malavi onfire
@Cubotenterprise
@Cubotenterprise 11 күн бұрын
Amangidweee onseeewa
@Biath-m4b
@Biath-m4b 11 күн бұрын
Koma iwe wayankhula bwino bwanj mpake tikuti ndizopangana bwanj sanamangepo olo mmodzi apa zikumveka koma so akuthawa chian mdziko muno kukakhala ku china akusowa mtendere uyo
@ChisomoBanda-g5s
@ChisomoBanda-g5s 11 күн бұрын
🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉😢😢😢😢
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 11 күн бұрын
President chipani China vice chipani China secretary chipani China ndimaudindo ena zipani Zina mwina malawi angazaoneke kusintha
@williamlyton8016
@williamlyton8016 11 күн бұрын
the DC mwana owopsa kwambiri
@violetpotani
@violetpotani 11 күн бұрын
Uyuyu muti president yu asatiphwanyitse mutu tingoonda nazo izi
@mlimipatsogolo7323
@mlimipatsogolo7323 11 күн бұрын
Zikuti pweteketsa mutu tasakani mfundo zina zowawuza amalawi
@KingstonMahamba
@KingstonMahamba 11 күн бұрын
Likiliki nanuso nda opposition kani
@UthumanMwangala
@UthumanMwangala 11 күн бұрын
At wina azangokomoka😂😂😂😂😂😅
@user-cp4qt9hs8w
@user-cp4qt9hs8w 10 күн бұрын
Anthu nde mwayankhula km sizikusintha pangofunika kumukolaso mdege yakeyo chakwela
@DalitsoTanganyika
@DalitsoTanganyika 7 күн бұрын
Nkhondo yathu tayisiya mmanja mwa Mulungu
@FrancisKamwendo-p2i
@FrancisKamwendo-p2i 11 күн бұрын
Go deeper.ang'alulidwe basi
@NeemaMatewere
@NeemaMatewere 11 күн бұрын
@jamesjolichi2026
@jamesjolichi2026 11 күн бұрын
Bornnn kalindoooooooo
@Cubotenterprise
@Cubotenterprise 11 күн бұрын
Pagan comment smnuye
@Cubotenterprise
@Cubotenterprise 11 күн бұрын
Agalu a MCP
@AuphieBannet
@AuphieBannet 11 күн бұрын
Diiiiiiiiiiiisiiiiiiiiiiiiiiiiii
@BarnettKathumba
@BarnettKathumba 9 күн бұрын
imfa ya chilima siizaiwalika
@AlickChima
@AlickChima 10 күн бұрын
Kodi a born kalindowa anaphunzirapo za ndegeso?? Anahwiraposo ku army¿? Aaaaa zili zonse komenti. Asiyeni ma xpert azikamba zinazi za sewero la ADRAzi sizikuthandiza atah
@EmmanuelZiba-qz6ug
@EmmanuelZiba-qz6ug 10 күн бұрын
😢😢😢😢😢
@SalahMhone
@SalahMhone 8 күн бұрын
Vuto lake chilungamo chimawawa
@LidyaGoodson-fb4tt
@LidyaGoodson-fb4tt 11 күн бұрын
Kkkkkkkkkk
@HendrickBanda
@HendrickBanda 11 күн бұрын
🔥🔥🔥🔥
@VincentAndrew-p8l
@VincentAndrew-p8l 7 күн бұрын
Panyopako
@humphreyskasonde7096
@humphreyskasonde7096 9 күн бұрын
Iweyo ukazangopeza anzako ena atatu olimba ntima ngat iwe dziko lizasitha
@BICHALIDAYSON
@BICHALIDAYSON 10 күн бұрын
😂,
@AbgirlChinheya
@AbgirlChinheya 11 күн бұрын
🎉
@ClementWellos
@ClementWellos 11 күн бұрын
The DCccccccccccccccccccccc
@CHIFUNDOVINTULA
@CHIFUNDOVINTULA 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
BON KALINDO - 15/09/2024
16:38
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 5 М.
The FASTEST way to PASS SNACKS! #shorts #mingweirocks
00:36
mingweirocks
Рет қаралды 17 МЛН
Bend The Impossible Bar Win $1,000
00:57
Stokes Twins
Рет қаралды 47 МЛН
COMRADE NTANYIWA PA LIMPOPO FM - AMAFUNA ANDIPHE KOMA ZAKANIKA.
32:39
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 13 М.
COMRADE MTANYIWA PA LIMPOMPO FM
15:57
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 29 М.
KONDWANI NANKHUMWA WAYANKHULA IZI LERO PA 14/09/2024.
50:23
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 2,9 М.
TIKUDZIWENI - 25 FEBRUARY 2019
33:12
Times 360 Malawi
Рет қаралды 107 М.
BRENDA KOSAMU, LOST & FEARED DEAD
19:12
Rodwell Lumbe
Рет қаралды 28 М.
نبوءات المسيرى تتحقق بعد 25 عاما .. 7 أكتوبر موعد زوال دولة الكيـ،ـان
55:04
القناة الرسمية للإعلامي محمد ناصر
Рет қаралды 238 М.