Mr Mtanyiwa mulungu akutetezeleni muzonse tili Pano chifukwa cha inu❤❤❤❤❤❤
@FisherActionАй бұрын
More fire big thus true
@DavieMasowoАй бұрын
Mulungu azikutetezani amtanyiwa
@MozzyBSaimonАй бұрын
Inenso ndilj ku Capetown ma polo ake ndimupitila komko adxiwe kuti ndithana naye asanabwele.kwa Comrade mtanyiwa
@leoleonard2103Ай бұрын
I love Limpopo fm because imakamba zowona, pls Malawi samala ukuyitana nkhondo mudziko Lako samala 👌🏽☝🏽🙌🏾
@donexmakande5979Ай бұрын
Ntanyiwa ndikatundu umatiyimilila go forward big Ulemu wanu
@IshuKatangaАй бұрын
he is staying at Sea point Cape town don't worry is just a small boy
@jesusminded3033Ай бұрын
No,he is not.He is a patriot.Belueve that and it is the people who love justice who can agree with him.Don't insult people simply because they don't think the way you think.If you have a different view criticize constructively my friend Good day.
@JusticeNyirendaАй бұрын
We don't need this 🥱🥱
@MphatsoIshmaeladamАй бұрын
Truth always painful more 🔥 ntanyiwa chilungamo tikuchifuna infa ya chilima
@AiameAdamo-su1ntАй бұрын
Tili Tchelu kunvelela from Mozambique. Umayita big Ntanyiwa.
@user-artharkkadangoАй бұрын
Alibe manyaz mkomwe zoona kuba ndalama za nzika zoona km ku Malawi kuno aaah😅
@JOHNOlesmasCosmas29 күн бұрын
ndidasiya kumvera ma radio Aku Malawi coz alowetsa ndale koma inu a Comrade Ntanyiwa mmakwana simunyengelera pa Limpopo FM mmaitha man
Ndinu achisiru kwambili ndipo palibe chanzeru chomwe mwakambapo apa
@user-nv3rf7bl7rАй бұрын
@@CatherineMbela eya asisi anthu akuyankhula zinthu zambiri nanuso mumaziwa kuti chinthu chikachitika pamachuluka zoyankhula zoona komaso za boza koma limachuluka kwambiri ndiboza amati chilungamo chimamasula ngati iwowo akuziwapo kanthu kungopita live kukawawuza chilungamo koma za mu social media sizingatithandize anthu akuyenela kumangidwa chifukwa alibe umbo ena imakhala sanje koma zikuvesa chisoni dziko lathu mumalo mogwirana manja ndipomwe akapasula akuchulukila bible limati muzako akakuchitila choipa iweyo muchitile zabwino ndipo umupemphelele ndiye woyankhulafe ndifeso timawoneka ochimwa pamaso pamulungu mwawona
@OssmanAbubaker-st7puАй бұрын
Bwana please tatitumizileni phone number ya mnyamatayo inendikufuna ndimugwire chifukwa inendili ku Cape Town comwekuno Sakundiziwa bwino bwino mnyamata ameneyo
@Yahiya-wm8ndАй бұрын
tbwela komko cpt
@AlexKaunda-ny2egАй бұрын
Mr Ntanyiwa tiudzeni anapha chilima asanathawe tidulanepo dziwalo please fast