Limpopo FM khetchemu Ntanyiwa kutulukila tsopano ndipo amva kuning'ina ku bomako lero

  Рет қаралды 28,466

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

Ай бұрын

Пікірлер: 91
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Mr Ntanyiwa tiudzeni anapha chilima asanathawe tidulanepo dziwalo please fast
@user-ks3uw8gj8h
@user-ks3uw8gj8h Ай бұрын
Komatu a Chimwendo Bandawo Mulungu akuwawona , ndipo akapitiliza adzamfa imfa yowawa
@MerryWayson
@MerryWayson Ай бұрын
Mr Mtanyiwa mulungu akutetezeleni muzonse tili Pano chifukwa cha inu❤❤❤❤❤❤
@FisherAction
@FisherAction Ай бұрын
More fire big thus true
@DavieMasowo
@DavieMasowo Ай бұрын
Mulungu azikutetezani amtanyiwa
@MozzyBSaimon
@MozzyBSaimon Ай бұрын
Inenso ndilj ku Capetown ma polo ake ndimupitila komko adxiwe kuti ndithana naye asanabwele.kwa Comrade mtanyiwa
@leoleonard2103
@leoleonard2103 Ай бұрын
I love Limpopo fm because imakamba zowona, pls Malawi samala ukuyitana nkhondo mudziko Lako samala 👌🏽☝🏽🙌🏾
@donexmakande5979
@donexmakande5979 Ай бұрын
Ntanyiwa ndikatundu umatiyimilila go forward big Ulemu wanu
@IshuKatanga
@IshuKatanga Ай бұрын
he is staying at Sea point Cape town don't worry is just a small boy
@jesusminded3033
@jesusminded3033 Ай бұрын
No,he is not.He is a patriot.Belueve that and it is the people who love justice who can agree with him.Don't insult people simply because they don't think the way you think.If you have a different view criticize constructively my friend Good day.
@JusticeNyirenda
@JusticeNyirenda Ай бұрын
We don't need this 🥱🥱
@MphatsoIshmaeladam
@MphatsoIshmaeladam Ай бұрын
Truth always painful more 🔥 ntanyiwa chilungamo tikuchifuna infa ya chilima
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt Ай бұрын
Tili Tchelu kunvelela from Mozambique. Umayita big Ntanyiwa.
@user-artharkkadango
@user-artharkkadango Ай бұрын
Alibe manyaz mkomwe zoona kuba ndalama za nzika zoona km ku Malawi kuno aaah😅
@JOHNOlesmasCosmas
@JOHNOlesmasCosmas 29 күн бұрын
ndidasiya kumvera ma radio Aku Malawi coz alowetsa ndale koma inu a Comrade Ntanyiwa mmakwana simunyengelera pa Limpopo FM mmaitha man
@DanielJuwawo
@DanielJuwawo 7 күн бұрын
Mukhale bwino dzina la yesu
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 Ай бұрын
Mtanyiwa mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 Ай бұрын
Chakwera akutsegula mmimba ndi nduna zake komwe aliko mpdze pedze man😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 Ай бұрын
Tiuzeni ndithu comrade Ntanyiwa,, ayaluke amenewa 😂😂😂
@YasinMmadi
@YasinMmadi Ай бұрын
Ng'alulani a limpopo
@DysonNakhaphe-bo4dl
@DysonNakhaphe-bo4dl 21 күн бұрын
Mr comred tili nanu mapehelo mulungu ali mbiyanu muyimilila ntundu wonse pitilizani kugwila ntchito yotamandika
@user-zr7wk4oq2x
@user-zr7wk4oq2x Ай бұрын
Buddy Ntanyiwa‼️ Proud of you brother 🖤🔥🔥
@HalimaDamiano
@HalimaDamiano Ай бұрын
God bless you ntanyiwa
@SteviePatrick-g2p
@SteviePatrick-g2p 2 күн бұрын
Ayi akunama ameneo
@janemanyamba7201
@janemanyamba7201 Ай бұрын
Ulemu wanu bigger mumatiuza zoona zokhazokha palibe chinsisi padziko lapansi palibe wa muyaya
@johnmpatama1461
@johnmpatama1461 Ай бұрын
Tipatseni house number komanso street name. Tikamuchedzere galu ameneyi
@user-oy6dl1pv9e
@user-oy6dl1pv9e Ай бұрын
Ine phee mwachidwi ndi Limpopo ❤
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Chimwendo Banda mphono Ngati nkhumba😂😂
@TamalaMwamlima-gk5im
@TamalaMwamlima-gk5im Ай бұрын
Ingalule mr ntanyiwa nazoni
@SostenKuyeli
@SostenKuyeli Ай бұрын
You will be protected by the almighty God
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 Ай бұрын
Mtanyiwa agogo Anga akufuna akupaseni khunda mukaotche
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Iwe kalasonga ndi kudula machende pa two days wait and see
@EllenNamulu
@EllenNamulu Ай бұрын
Mulungu akhale nanu boss
@user-cy4pg1bo5o
@user-cy4pg1bo5o Ай бұрын
Ng'alura big umakwana kk
@davidwakhokamoto1124
@davidwakhokamoto1124 Ай бұрын
Number yagalu ameneyo pls aziwe kut tilipo ochuluka ambiri
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js Ай бұрын
Mbava
@amosnyongo6565
@amosnyongo6565 Ай бұрын
Sea point
@kasupeowenpaul
@kasupeowenpaul Ай бұрын
Sea point Baba
@JumaAlli-vf6jp
@JumaAlli-vf6jp Ай бұрын
Mumakwana abwana
@tlhalosozindlani4544
@tlhalosozindlani4544 Ай бұрын
Yes yes yes heeeeee we respect you ntanyiwa yomweyo galu iwe usampase ndimpasa kkkkkkkkkk
@MayamikoSambo
@MayamikoSambo Ай бұрын
God is in control
@viennasamuel2976
@viennasamuel2976 Ай бұрын
Sizachilendo kubedwa ndalama mu fon popanda pin abale tidzinena zoona ,palibe akudziwa zoti ena akumachotseledwa ndalama? Osamangotsutsa zilizonse
@MalinoChidzulo
@MalinoChidzulo Ай бұрын
Kaya amati social media kaya tizinva basi
@MphatsoIshmaeladam
@MphatsoIshmaeladam Ай бұрын
Ndipo please akatinamiza ndi report lawo inuyo bwelani ndizonse mwatisungira kut choona chioneke
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz Ай бұрын
Limpopo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@user-artharkkadango
@user-artharkkadango Ай бұрын
Be safe my bro.... God will save and can't found u
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Ай бұрын
Aaaaaa koma macadeti mulibe manyazi akutumani kuti muzitsutsana ndi COMLED ntanyiwa , inu mukuona ngati zibisika zimenezi ,moti chilima anachita kuphedwa SIMUKUDZIWA ,munya muona mwachita zaumbuli , Malawi wa pano si wakale mukhaula ndi mcp yanuyo
@benjaminjobo3525
@benjaminjobo3525 Ай бұрын
Munthuyu ndikumudziwa
@marygoza1205
@marygoza1205 Ай бұрын
Alandila zingati abale ake akuvutika ku Malawi uko shame
@clementchatepa
@clementchatepa Ай бұрын
Amalawi tinasukusula pano tiye nazo fada
@user-dt8nr1zx6e
@user-dt8nr1zx6e Ай бұрын
❤❤❤❤
@EliasJimmy-fv1wk
@EliasJimmy-fv1wk Ай бұрын
Ntanyiwa tikufuna nyimboyo chilima MMM
@ChikumbutsoTsalangu
@ChikumbutsoTsalangu Ай бұрын
Respect
@user-zx3pz2wy1j
@user-zx3pz2wy1j Ай бұрын
Koma nambala ya chisisi ayidziwa bwanji pochotsa ndalamazo?
@user-ym8rn5kd1s
@user-ym8rn5kd1s Ай бұрын
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Ай бұрын
WINAWE UCHITA MANYAZI CHIFUKWA CJIFUKWA ANTHU ANAFA AJA ASANAPHEDWE AMAYANKHULA NDI ACHIBALE AWO MCP INAPHA ANTHU OSALAKWA
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e Ай бұрын
Ntanyiwa ndiwe 1
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz Ай бұрын
Timpeza ndipo asowa
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi Ай бұрын
What is rong is rong...amalawi atopha ndi ulamuliro wangaza ndi kupha
@EllinaBitto
@EllinaBitto Ай бұрын
Mnthanyiwa❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭 A Chilimaaaaaaaa mayo ineeeeee
@wilsonali7890
@wilsonali7890 Ай бұрын
Guys Ku Cape town ko yekhayo just set out
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js Ай бұрын
Mbabane za boma
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Iwe usanamize anthu pano 25million ayitenga bwanji without pin.?
@JusticeNyirenda
@JusticeNyirenda Ай бұрын
You don't understand technology
@SandrahEsther
@SandrahEsther Ай бұрын
Okuba amaba bwanji mma foni aanthu pin amaitenga kuti?
@user-er7ub4ug7y
@user-er7ub4ug7y Ай бұрын
Comled mtanyiwa l proud of you 💪💪💪
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o Ай бұрын
Za ziii
@ThomasPeter-zt2ju
@ThomasPeter-zt2ju Ай бұрын
Mbolo yako
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o Ай бұрын
Boza ilo ndipo ndikuona kut pano wasanduka slave chifukwa ntendere ulibe ukungoyenda tchelutchelu paliponse ,zoona abale ako osawawona chifukwa chomenyera ufulu wa chipan cha dpp nkukhala wopanda ntendere koma kumalawi uzafika
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j Ай бұрын
Panyo pako ukuti boza
@bisweckchimphamba8497
@bisweckchimphamba8497 Ай бұрын
Ma cadet ena a MCP ndameneyu mutha nonse,am watching you where you're
@ThomasPeter-zt2ju
@ThomasPeter-zt2ju Ай бұрын
Machendeko
@dennisrobert4617
@dennisrobert4617 Ай бұрын
Kanyimbo munayambira kaja kamandikhudza ndingakapezs bwanji
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js Ай бұрын
God will punish them
@user-zv3cy2xj5p
@user-zv3cy2xj5p Ай бұрын
Bodza ili anakhapa bwanji anthu awo anali mu ndenge, ndiponso bwanji inuyo osangobwera ndikupangitsa msonkhano poyera kut tikudziwen mwina mungadzakhale vice wa dziko
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
Ndipo bwanji osangobwela poyela ali busy kulimbana ndi boma zimenezi zimafunika akubanja komaso kubisalako zikuwonekelatu kuti boza pali anthu amamugwirisa ntchito
@CatherineMbela
@CatherineMbela Ай бұрын
Inu inu anthu onsewa akuyakhula kumapeleka ma umboni nanga akhale Kuti sanaphe anthu akuwamangilanji anthu ose azingopeka achewa Pena pake kumavomeleza zinthu
@LucianoKapepuza-sy9wx
@LucianoKapepuza-sy9wx Ай бұрын
Wa MCP iwe kape chisilu chakumuzi
@GodfryMalishe
@GodfryMalishe Ай бұрын
Ndinu achisiru kwambili ndipo palibe chanzeru chomwe mwakambapo apa
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@CatherineMbela eya asisi anthu akuyankhula zinthu zambiri nanuso mumaziwa kuti chinthu chikachitika pamachuluka zoyankhula zoona komaso za boza koma limachuluka kwambiri ndiboza amati chilungamo chimamasula ngati iwowo akuziwapo kanthu kungopita live kukawawuza chilungamo koma za mu social media sizingatithandize anthu akuyenela kumangidwa chifukwa alibe umbo ena imakhala sanje koma zikuvesa chisoni dziko lathu mumalo mogwirana manja ndipomwe akapasula akuchulukila bible limati muzako akakuchitila choipa iweyo muchitile zabwino ndipo umupemphelele ndiye woyankhulafe ndifeso timawoneka ochimwa pamaso pamulungu mwawona
@OssmanAbubaker-st7pu
@OssmanAbubaker-st7pu Ай бұрын
Bwana please tatitumizileni phone number ya mnyamatayo inendikufuna ndimugwire chifukwa inendili ku Cape Town comwekuno Sakundiziwa bwino bwino mnyamata ameneyo
@Yahiya-wm8nd
@Yahiya-wm8nd Ай бұрын
tbwela komko cpt
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Mr Ntanyiwa tiudzeni anapha chilima asanathawe tidulanepo dziwalo please fast
@user-ct7jo8df6m
@user-ct7jo8df6m Ай бұрын
Sea point
LIMPOPO YOO NTANYIWA  WABWERA NDI NKHANGA ZAONA PROGRAM LERO PA 28 JULY 2024
17:21
КАК ДУМАЕТЕ КТО ВЫЙГРАЕТ😂
00:29
МЯТНАЯ ФАНТА
Рет қаралды 10 МЛН
Clowns abuse children#Short #Officer Rabbit #angel
00:51
兔子警官
Рет қаралды 77 МЛН
INTERVIEW YA MICHEAL USI PA TIMES NDIPO WAYANKHA ZA UTM KUTULUKA TONSE
1:29:52
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 108 М.
Nancy vs Che Nkope - Zikhale Ngoma Kapena Drums?
10:46
CHE NKOPE
Рет қаралды 34 М.
Chegutu : Ruvimbo wekuurairwa $100 onzi opfuka asati avigwa
1:03:06
HOT CURRENT PA TIMES 28 JULY 2024 NDI WONDER KOMASO JONA
56:21
Malawi Trends TV
Рет қаралды 3,4 М.