Boma lililonse anthu amaphedwa momvesa chisoni kwambiri koma ili lanyanya kwambiri Kodi anthu simukuo a nokha ozawina 2025 akudziwa ndi Mulungu yekha basi
@Littlefair72 ай бұрын
Atolankhani aku malawi ndi mbola zokha zokha, amafunsa mafunso ngati akupanga malumbilo a ubatizo. Ndinaonera atolankhani atamupanikiza president ku Kenya kumufunsa mafunso okhwima osati izi, za ziiii. Mafunso opusa ngati awa even mwana wa kindergarten akhoza kuyankha.
@Chancykwalingana2 ай бұрын
atopa kale campaign asanayambe kma magogo party 😂😂😂😂😀😀😀😀😀😀
@edsonnyasulu53942 ай бұрын
Anthu a nzeru onse mwawathamangisa kale asalako ndi anthu A dyela
Padzana mudaononga ndinu... apa tikuona zotsatira zakuonongako... Zimene awononga a Tonse zidzaoneka akadzachoka .. ngati angachoke.
@edsonnyasulu53942 ай бұрын
Koma anthu ena alibe nzeru zoona munganene kuti Peter athandiza dziko pomwe analephela kale komaso mukufuna azafere pa mupando ngati ku malawi kulibe anthu A nzeru zachamba basi
@KondwaniGumba2 ай бұрын
Muuponda ife agogowo ndi anu ife ai, .
@MrAhmidu2 ай бұрын
So you mean that when in government you have corrupt ways to raise funds and since you are in opposition and those means aren't there, you decided to just do with the non-lucrative means you have? Iyayi, tamva nawo.
@dumbokadaluka57592 ай бұрын
I felt that was stupidest answer as a response to a qn
@yasitafuphiri-nw2he2 ай бұрын
Budget yonse ikalowa zingati ,yankhani funso osadzilumaluma lilime apo
@GanduBondu2 ай бұрын
Guys trying to put youth to be reader please people is tried where is young youth of Malawi to give power 😢guys one day we gonna done with government like Kenya Nigeria bec kind of reader who done long Malawi future we can't allow them to take advantage with our country no to them same people who kill our Malawi bt we still gives long time dream no matter what let's say no this people again again take Malawi give power to our young youth team to build Malawi
@DoYouKnow38382 ай бұрын
English yabwanji iyi 👆😂😂😂❓❓❓
@PiliraniDanielDaniel2 ай бұрын
Sitikufuna mgogo ife kulamulilaso Malawi
@MaritaBanda-p4z2 ай бұрын
choka malawi muno ifes sitikufuna kulamulilidwa ndi chakwera
@charleskayamba-s7c2 ай бұрын
kodi inu nkhalambaiyi yuti chani taniuzn gays
@JamesSaidi-rw6ek2 ай бұрын
Dziko lawonongeka ndi chikangawa party
@PeterRabson-z3w2 ай бұрын
Mbambande namalomba APM woyeeee
@VeraVermaak2 ай бұрын
First president of Dpp wos Dr Bingu wamutharika and second president of Dpp Professor Peter mutharika it's family property not National zawo zakubanja
@MarthaBango2 ай бұрын
Inde asiyeni azanu Chala cha mulungu chinaloza iwe,chakwera inuyo ndi akubanja kwanu anthu akuvoteleni
@PatrickMangochi2 ай бұрын
Madala team😂😂😂 Koma anthu mulibe manyazi,a Chaponda akulephera kuyankhula apa chifukwa cha ukalamba
@charleskayamba-s7c2 ай бұрын
palibe uwina ninkhalamba yakoyo
@EliSMpuka2 ай бұрын
Komatu Zinazi asiyileni achinyamata
@JoelKacheche-x6i2 ай бұрын
MCP Yatengaso boma mosa Kanyika,Dpp yasogoza okalamba,chibwana chachikuru ku voteraso peter mutarika azizango gona mbava zikutenga misonkho ya A malawi.
@JamesSaidi-rw6ek2 ай бұрын
Ife tikwera dpp mcp ikagwere
@ChifundoZimba-jh7dh2 ай бұрын
Namalomba kape
@yasitafuphiri-nw2he2 ай бұрын
Chaponda mweya unatha 😢
@hassammaulana45292 ай бұрын
Ai koma sindlama zake koma za amalawi osati zakuyumba kwake
Kodi George Chaponda mchimangayu mwamutenga ku museum?
@LawrenSonga2 ай бұрын
Zinakuvutani kare inu mthawi yanu inamtha basi
@EllemiaChaduka2 ай бұрын
Mwabwita kale inu a Dpp convention ya chipani chanu mukathana a zipani zina kkkkkk anamalomba kanganizani popanga zinthu
@TamUs-u2h2 ай бұрын
Namalomba kuchikamwa
@MaritaBanda-p4z2 ай бұрын
iwey ndiye uli ndikuchani
@anthonynkhoma42652 ай бұрын
Anthu womwe ankafuna kupikisana ndi agogo ndi womwe munawathamangitsa aja. Za misewu musatinamize. Iwo aja anangokumba pa area 18 round about paja basi. Ma 6 lane roads musatinamize. Mufuna kunamiza anthu. Komanso za agogonndi mombera University yomwe aphunzitsi ake ndi achina Dan lu. Kkkkkk cementgate simukutchula bwanji?
Anthuwa akalamba inu kulephera kuyankha mafunso moyenerako ndikukalamba. Dzikoli likufunika anthu a nzeru za tsopano koma anyamata. Amene akutha kuyenda ndi dziko osati nkhalambazi ayi.
@MuhammadBAKILI-kl2mj2 ай бұрын
Chimanga chikugulidwa 45pin not 35pin
@WachiyawoWangalusa2 ай бұрын
Chikangawa.sangawine.ndiwakupha.
@EagerChicken-qj6xu2 ай бұрын
Izi ndizopandanso demokarase ndi chimodzi modzi nthawi yakamuzu,
@WinerdShadreck2 ай бұрын
Muzingoika nyimbozo
@WachiyawoWangalusa2 ай бұрын
Imfa.yachilima.ndiimene.imugwese.chakwela.
@ChrisyMbewe2 ай бұрын
DPP..yomweyo
@johnkambala6922 ай бұрын
Bodza lankhkhuniza. Muona the next five years.
@CosmasChikwindi2 ай бұрын
PDP woooooooyeeee❤❤❤❤
@EllahChikwatu2 ай бұрын
Kkkkkkkkkk kom ndaseka
@FunnyKalimwayi2 ай бұрын
chikangawa sawina
@RafnikMaida2 ай бұрын
❤😮😅
@JACKSONHULUWA-j2n2 ай бұрын
Opposition woyee, mcp ichoke basi
@MjombaMjuba2 ай бұрын
Munya muwona, mudzakomoka, dikilani
@WachiyawoWangalusa2 ай бұрын
Chakwela.sakumuziwa.mmalawi
@BlessingsSimbi-s2d2 ай бұрын
Dpp my vote tikuchedwa kovota adadi omwewo🎉
@DanielPeterson-k5o2 ай бұрын
Sindingabetse vote yanga ine kupatsanso peter bola akanayimira wina koma chakwera ndi peter dzikalima adyera nonkhanonkha
@MLWPhiri2 ай бұрын
Nde voti yako ife tisegule nayo mmimba kagwele uko
@DanielPeterson-k5o2 ай бұрын
@@MLWPhiri khalambanso la lero? Shame on you bro look at chaponda kkkkk koma guys ndizoona tikufuna kusitha koma team yankhalamayi ikagwere
@MLWPhiri2 ай бұрын
@@DanielPeterson-k5o shame on you too by the way am not your bro mwina iweyo umatamba nkuona chilichonse chili bwino bwino kma ukanakhala wanzelu sukanatengela Za kukula Kwa Munthu kma kuganizila amalawi
@DanielPeterson-k5o2 ай бұрын
@@MLWPhiri iwe chisankho changa sichako panga chisankho chako but for me l will follow my heart ndipo sindingavotere peter ineyo anthu ambiri apanga macomment why target yako ilipaine?Peter akanapatsa wina ku ddp ndikanawapatsa vote yanga chifukwa l need charge koma peter himself bolanso chakwera emweyu