Aaaah nde mukuona ngati mukagaea zinthu zanuzi tivotera inu zamanyi
@isaaczuze24 күн бұрын
My vote is for Apm in any way.....mcp the party of darkness
@RichardKuden26 күн бұрын
Chakwela my vote 😂😂😂
@augustMag26 күн бұрын
Musegula naye mmimba APM 2025 Booooomaaaa ❤❤❤❤❤
@tasmania52726 күн бұрын
APM ngoluzaluza iwe khala chete
@augustMag26 күн бұрын
@@tasmania527 Sindikhala chete mpaka anthu a MCP Bpp yanu itakwera mu 2025 Chifukwa Cha kuluza kumene muluze Our APM akunyada ulendo okalowa ku state house kuziona inuyo muzizinamiza kuti mupitirira kulamulla mpaka 2030 Mulungu wake utiyo kuti akatitaye mkumangomphulabe njerwa Zamoto? Siwa Abraham ayi
@tasmania52726 күн бұрын
@augustMag Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk. If wishes were horses, beggers would ride. Do you think pamene munampinda JB in 2014 then zikhalaso choncho ndi Dr. Laz? Mwauponda.
@Alexkalonga-t9s26 күн бұрын
Uzilakhula zoti akutame km amalawi apanga chiganizo mbuzi iwe
Mmmmmmm zikuyakhulidwa apapa anthuwa a kuopa Peter basi malo motulusa fundo akulimbana ndi kuti Peter sanakhare nawo PA convention za ziiiiiiiii
@HendersonNambera26 күн бұрын
Ndy ona comment ngati pali mcp yakoy😂😂😂 APM my vote wamv galu iwe
@JoelMwenegamba26 күн бұрын
Koma anthu muwanamiza awo adya???????? God is watching you mana.
@Mustapher-fb4qp24 күн бұрын
Amarawi honani má komenti kuyambila muntunda kufukira komenti ❤dpp yawina di mavoti 95 MCP 5 dpp moto moto
@ChikumbutsoChomali26 күн бұрын
Inu musatinyanse apa mai munawina chifukwa cha chilima inu muyambe kutenga masaza anu muzipita mmakwanu ndi chakwera wanuyo Peter sanaluzepo dpp ndiyomwe imaziwa kutsogolela ndikudziwa kuchengeta wanthu sizanuzo mbalame za anthu
@shadreckjumah26 күн бұрын
Mayi mbuzi yamunthu uchisilu pa mwamba pa uchisilu
@DalitsoMatope26 күн бұрын
Kodi ngati mulungu sakusangalala nawo utsogoleri wako mulungu amakutumizira matenda,cyclone ndi ifa njala chifukwa cha utsogoleri opusa nde zomwe zina bwera zinja ndi chifukwa choti mulungu sakusangalala ndi ufumu wanu