Zomwe wayankhula Michael Usi Lero atangofika mu Mzinda wa Blantyre

  Рет қаралды 21,512

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 125
@benardisaac1986
@benardisaac1986 2 ай бұрын
Nyengo ndizosintha manvuto sankha moyo wose wamunthu koma Dr usi all the best
@SadrackMalola
@SadrackMalola 2 ай бұрын
We all know kut anthu omwe avala makaka a UTM nd a MCP. Eni eni a UTM sitikupanga nawo zopusazo.
@JonesSiliya
@JonesSiliya 2 ай бұрын
Zoona akufuna kupusitsa
@JonesSiliya
@JonesSiliya 2 ай бұрын
Chilima nzake amane amakambilana naye ndi ndani nanga nthawi imene amakusekani pakamwa ndindani
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 2 ай бұрын
Ndimaona ngati adziyankhula zogwira mtima
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 2 ай бұрын
Michael usi is a matured intellectual who doesn't entertain nosense.
@giftmasenti5732
@giftmasenti5732 2 ай бұрын
Manganya ndi wa MCP kuchokera kalekale
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 2 ай бұрын
Wachepa nao u vice president.waiwala imfa ya skc.
@LukeKalima
@LukeKalima 2 ай бұрын
@@paulnyondo7572 aaaaaaaaaaa imfa ya skc ndiyotani anthu samamwalira kodi kapena munamuphera dala kuti muzipangira ndale imfa yake, kodi maliro akwanzanutu amaphweka chomchi akadzakhala akwanu zidzakuwawa kuti anthu azidzaseweretsa dzina la malemuwo
@johnbakali27
@johnbakali27 2 ай бұрын
Kodi iwe ukumenyera kampeni ya mco kapena UTM?
@LukeKalima
@LukeKalima 2 ай бұрын
Wandisangalatsa usi sakupanga nawo za mtopola ena achita manyanzi kumeneko ndiye kulankhulatu ambuye akudalitseni dr usi
@LeviBlackson
@LeviBlackson 2 ай бұрын
Anthu sakumudziwa Kodi ku Blantyre kapana amapanga sewero
@LeniaJosophat
@LeniaJosophat 2 ай бұрын
Mukutipatsirazi ndizabwino zeedi koma you need to fix the sound kuti zizikomabe( this is the VP)
@hastingskalambo8502
@hastingskalambo8502 2 ай бұрын
Ndekuti zoti UTM yatuluka ku alliance iyeyo sakudziwa
@joeldaniel-pc3ij
@joeldaniel-pc3ij 2 ай бұрын
Mwapatsa anthu a MCP ma uniform a UTM kuti aziti chani?
@Jane-qb5qf
@Jane-qb5qf 2 ай бұрын
Amalawi look sharp amalawi tilindivuto akati uku komweko uku komweko lekani timapemphera kukhala ndi chiganizo chokhazikika zimandimvesa chisoni kwambiri tisinthe mindset plz plz tizagwa chagada ndikati ndione amazayesa zida kuti kuli bwanji uku aaaa kaya Malawi
@sanddaniweck2703
@sanddaniweck2703 2 ай бұрын
Zangongole ife tilibenazo ntchito nkhani musise zinthu zakwela kwambili coz za Neef zo anthu ena akumamizi kwina salandila koma mukasisa zinthu anthu onse athandizika
@SydneyMwale-u9w
@SydneyMwale-u9w 2 ай бұрын
Ngongole imeneyi udzabweza ndiwe . Fataleza udula konseko
@samchibenene4458
@samchibenene4458 2 ай бұрын
Seriously
@moyowrobert3331
@moyowrobert3331 2 ай бұрын
zoti akumanga thumba ngati Mphaka sukuziwa
@JacobKasalika
@JacobKasalika 2 ай бұрын
UTM ndimaikonda komano tikudzibalalitsa yokhatu.Uyu ndinthu ndinyamata wa SCK
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o 2 ай бұрын
Mbuz yamunthu iyi yudasi ife a Utm zopusazo ayi sitikupanga nawo
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 2 ай бұрын
Missing Chilima Already😢
@RossanaMitha-tl9in
@RossanaMitha-tl9in 2 ай бұрын
Kodi akuti kwabwela ndani ?😂😂😂😂
@SifatiMoses
@SifatiMoses 2 ай бұрын
Muli mbali iti kodi Fada
@JonesSiliya
@JonesSiliya 2 ай бұрын
Mwachedwa ndi chilima simunapange chifukwa chiyani
@FrankidEugenio
@FrankidEugenio 2 ай бұрын
Ndale zayambika,Malawi ayiwale zambuyo.😂
@macdonaldchaonekera834
@macdonaldchaonekera834 2 ай бұрын
Kodi akupanga sewero la tikuferanji et?
@CosmasChikwindi
@CosmasChikwindi 2 ай бұрын
Palibe azalande m'dalitso wamunthu, Dr usi ndiodalitsika muzonse komanso olimbika.
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 2 ай бұрын
Koma bwanji sanavale makaka
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 2 ай бұрын
​@@FrancisNyayiamugula a MCP
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 2 ай бұрын
​@@FrancisNyayitikufuna chitukuko osati makaka
@SindisiweMendu
@SindisiweMendu 2 ай бұрын
Kusangalalila imfa ya mzawo
@JuniorKalipinde-gy7dx
@JuniorKalipinde-gy7dx 2 ай бұрын
Usaone ngati ndi bugwe LA adla limenelo akupweteka
@enockharry8039
@enockharry8039 2 ай бұрын
koma izi wina aziona
@NkosDysonNkosDyson
@NkosDysonNkosDyson 2 ай бұрын
Tangotsitsani fertilizer muonanso mudzawina mosavuta ife amalawi sititichedwa kuiwala
@RabsonGonondo
@RabsonGonondo 2 ай бұрын
Enafe tisayankhire
@VeronicaYohane
@VeronicaYohane 2 ай бұрын
Mudyelen bambo wasikono akabwela osadziwa kuyankhula odvala madiresiyo
@ShukuraniChitanganya
@ShukuraniChitanganya 2 ай бұрын
Mwschedwa nayo ngongoleyo bwana kkkkkkk nyimbo ikhale ya mpaka malilo vinyo watha
@MlecheFatch
@MlecheFatch 2 ай бұрын
A manganya mmmh
@MpapiParadise
@MpapiParadise 2 ай бұрын
Dziko la Malawi lafika pa uchitsiru weni weni
@JuniorKalipinde-gy7dx
@JuniorKalipinde-gy7dx 2 ай бұрын
Ndipo live
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 2 ай бұрын
Ayakhura ali pat?
@ChimwemweMuhelliwah
@ChimwemweMuhelliwah 2 ай бұрын
Kodi Usi ulimbali iti?. Koma umphawi luMalawi ukupepeletsa azibambo...
@JoycieMbaya
@JoycieMbaya 2 ай бұрын
Basi tizingokhalira ma handouts mpaka liti abale?
@ChrisjuZiyaya
@ChrisjuZiyaya 2 ай бұрын
Chizindikiro choti Usi siwa utm onani zomwe zavalidwazo , zomwe Malemu Sks sadapangepo. Tikufuna m'tsogoleri wa serious not this gys.
@jedoforsure2842
@jedoforsure2842 2 ай бұрын
Umakwana us
@genesismbewe
@genesismbewe 2 ай бұрын
genius
@SindisiweMendu
@SindisiweMendu 2 ай бұрын
Umbuli suzatha anthu munayambila kunamizidwa muja zilero changamukani
@lumbaninyirenda8223
@lumbaninyirenda8223 2 ай бұрын
tamangopitani muzikapanga ma drama,mfundo palibe apa
@EdwardChimwaza
@EdwardChimwaza 2 ай бұрын
Anamizana zokuti akope Southern Region
@KassimWilson-o8h
@KassimWilson-o8h 2 ай бұрын
Lelo akunamizila chilima lelo ndi mbuzi yamunthu
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 2 ай бұрын
Iweyo ukuti ukufuna ulongo sole, ndimaesa UTM yatuluka mungwirizano ukufuna kupusisanso Wanthu
@elizabethnkhata3438
@elizabethnkhata3438 2 ай бұрын
It's lik people are not happy
@frankwilliam9844
@frankwilliam9844 2 ай бұрын
There's contradictory in his mind,chomwe amalawi akufuna singongole,tsitsani zinthu,chepetsani kudalira ngongole za IMF...koma ndithu 60yrs independent Malawi yukanikabe kudalira payokha pa nkhani ya zachuma? so sad...Kodi maiko amzathuwa amatani Kodi ..adatukuka bwanji atalandila ufulu???
@CHRISSYBALALIKA
@CHRISSYBALALIKA 2 ай бұрын
Tasisani fertilizer zinthu zisike agalu inu muona muwina mosavuta
@ellahmvula
@ellahmvula 2 ай бұрын
Hahaha awa a mcp achina Eliza avala za utm
@constancemkandawire7378
@constancemkandawire7378 2 ай бұрын
You can't say that you love God if you don't love your nearby that's a total lie.You have failed to come together with your fellow utm members mukuti phala lomwe likudumpha mu mpoto lidumphe meaning you don't care ,ayi zikomo
@JoycieMbaya
@JoycieMbaya 2 ай бұрын
Koma zimenezi zitithandiza izi????
@KondwaniNdobvie-f4v
@KondwaniNdobvie-f4v 2 ай бұрын
Komatu adzake afanazo
@florenceharawa519
@florenceharawa519 2 ай бұрын
Uku wapita uku wapita punsi anagwa chada😂😂😂😂
@chikondiyovita7210
@chikondiyovita7210 2 ай бұрын
My data hu!
@MarthaChintolo
@MarthaChintolo 2 ай бұрын
Aaaaaa chifukwa chani Chilima unalakwitsa ee
@MerySaid-uw3cm
@MerySaid-uw3cm 2 ай бұрын
Tikufelanji
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 2 ай бұрын
Wakupha iwe manganya
@AbdullCassim
@AbdullCassim 2 ай бұрын
Iweso ndiye kayatu
@jeymulima9664
@jeymulima9664 2 ай бұрын
Kkkkk ngabule moyo,thetsa,uthetsa suthetsa kkk yathayi kkk
@LottiAffati
@LottiAffati 2 ай бұрын
kod akuyankhula kut chan apa guys aaaaaa, komanso amalawi ngoputsadi ndithu
@NathanMaunda-dz8gc
@NathanMaunda-dz8gc 2 ай бұрын
Awa sakuyankhula zotigwira mtima kodi nd wa chipani chanji ameneyi
@RahimYusufu-u2b
@RahimYusufu-u2b 2 ай бұрын
Sakudziwa zomwe a makawi akukumana nazo ....,
@RighteousMhone
@RighteousMhone 2 ай бұрын
Shimeyi atukwane😂😂😂
@RobertChisenga-ci2mq
@RobertChisenga-ci2mq 2 ай бұрын
BT chitsilu2 paja
@joma5327
@joma5327 2 ай бұрын
champhamvu kopasa kale kuthanthauza chani
@KassimWilson-o8h
@KassimWilson-o8h 2 ай бұрын
Anthu 4 okha bs
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm 2 ай бұрын
Km malawi ndfe anthu opusa kwambiri tinakali kuvutika
@MECChiona
@MECChiona 2 ай бұрын
wamisara uyu 😂😂
@SifatiMoses
@SifatiMoses 2 ай бұрын
Palibe kunyengelerana ndi ngongore nbuzi za anthu.
@MorexyMorry
@MorexyMorry 2 ай бұрын
Sizikuveka ai komas sizikugwilizana ayi
@jeymulima9664
@jeymulima9664 2 ай бұрын
Zaziiiiii
@QuotienieMw
@QuotienieMw 2 ай бұрын
Tikufilanji episode 10
@LACKSONJULIUS
@LACKSONJULIUS 2 ай бұрын
Nde ku MCP' ko akuti chani kkkk 😂😂😂
@Michaelchimwala-c6l
@Michaelchimwala-c6l 2 ай бұрын
Palibe chanzeru waywnkhula
@MuhammadNyambalo
@MuhammadNyambalo 2 ай бұрын
😅😮😢😅😅😅😅😂 patumbo pako iwe nyo
@ElizabethMwakamogho-x7j
@ElizabethMwakamogho-x7j 2 ай бұрын
Sukuziwa make awo find alimbe
@joekamphulusa4767
@joekamphulusa4767 2 ай бұрын
Chitsilu chenicheni ichi watenga athu a mcp kumati a utm 🚮🚮🚮
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh 2 ай бұрын
Ndimwana uyu alibe fundo
@TsuzenThomas
@TsuzenThomas 2 ай бұрын
Amalawi mitu sigwiradi sure
@charlesmasauko4651
@charlesmasauko4651 2 ай бұрын
Akufuna kugulitsa UTM KU MCP
@SydneyMwale-u9w
@SydneyMwale-u9w 2 ай бұрын
Emeneyi si dyera koma
@NELSONMULIMAH-fv6ub
@NELSONMULIMAH-fv6ub 2 ай бұрын
Zauchisilu zaziii
@momuumro
@momuumro 2 ай бұрын
Situfuna kunva zimenezo Ife tufuna nkhani yotuluka mu tonse alliance
@NATASHAChimtolo
@NATASHAChimtolo 2 ай бұрын
Opepela uyu malemu amavala makaka achipani chake
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm 2 ай бұрын
Nsogoleri anamwalira ka nanu inu mwatan kd
@charlesmasauko4651
@charlesmasauko4651 2 ай бұрын
Wosokoneza uyu
@FysonKaliba
@FysonKaliba 2 ай бұрын
Kod ati Ali Mbali iti??????????
@DavidPeter-e2o
@DavidPeter-e2o 2 ай бұрын
Aaaa zazi bas
@thokofodya1583
@thokofodya1583 2 ай бұрын
😢
@SmithLikoswe
@SmithLikoswe 2 ай бұрын
Zamasewelo bac
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh 2 ай бұрын
Kupusa
@ShelingtonMtemula
@ShelingtonMtemula 2 ай бұрын
Mbuzi yamuthu ameneyu dyela basi
@Vascomw
@Vascomw 2 ай бұрын
Hhhhhhh
@AbdulrahimoMassamba
@AbdulrahimoMassamba 2 ай бұрын
Satan ndiyemwe ali kutsogolo kwakoyo
@Michaelchimwala-c6l
@Michaelchimwala-c6l 2 ай бұрын
Aaaaaaaaaaaaaaaaaaa chitsiru mbuzi garu nyani mfiti iwe
@ShentrycChinoko
@ShentrycChinoko 2 ай бұрын
Sanje bac amalawi eeee
@FlorenceKamtema-kw5ru
@FlorenceKamtema-kw5ru 2 ай бұрын
Jealousy siumuna
@ChrisNkhoma-i8m
@ChrisNkhoma-i8m 2 ай бұрын
Mcp BOMA labwino kwamunthu woganiza mwazelu tiwone komwe tachoka .
@DalitsoBoster
@DalitsoBoster 2 ай бұрын
Yes
@Vascomw
@Vascomw 2 ай бұрын
Ïn̈ë n̈d̈ïm̈än̈g̈än̈ïz̈ä k̈üẗ äÿäk̈ḧür̈ä z̈äz̈ël̈üüü k̈m̈ ääää b̈ün̈d̈l̈ë ÿän̈g̈ä amayo
@sonkieleymanni6312
@sonkieleymanni6312 2 ай бұрын
ndiopusatu awawa,,,,,,,,,,,,,,,palibepo chanzeru anena apa
@LukeKalima
@LukeKalima 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu
@LukeKalima
@LukeKalima 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 mumafuna akanamanyonza kuteroko mwakhaula mindset change ikufunika ndithu
@SiphiweTonnyChidumayo
@SiphiweTonnyChidumayo 2 ай бұрын
Anthu sakusangalaratu😂😂
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 2 ай бұрын
Ndizawo zimenezo komanso musawapangire Zochita anthuwo . ngati inuyo simukusangalala basi
@SiphiweTonnyChidumayo
@SiphiweTonnyChidumayo 2 ай бұрын
@@ancientnkhata1137 eh eh iwe im commenting according ndimmene zuonekera nsiye ine
@MphatsobandaWilliam
@MphatsobandaWilliam 2 ай бұрын
Nice
ДЕНЬ УЧИТЕЛЯ В ШКОЛЕ
01:00
SIDELNIKOVVV
Рет қаралды 3,8 МЛН
Worst flight ever
00:55
Adam W
Рет қаралды 53 МЛН
Flipping Robot vs Heavier And Heavier Objects
00:34
Mark Rober
Рет қаралды 12 МЛН
MICHAEL USI WAYANKHA ZOMWE ANANENA A FELIX NJAWALA KU MZUZU.
8:04
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 25 М.
ДЕНЬ УЧИТЕЛЯ В ШКОЛЕ
01:00
SIDELNIKOVVV
Рет қаралды 3,8 МЛН