and those people are not UTM atengedwa kundilande bangwe and other areas. apasidwa ma 200 hands every one of them
@ConfusedAstronaut-qv6wqАй бұрын
Kodi inu chikuvuta ndichiyani kunena kuti ndi mcp or utmost palibe amene angakuvutitseni,athu akufuna kungodzowa bwana.
@Littlefair7Ай бұрын
Dr. Usi, in Democracy the rule is simple, majority rules, UTM yatuluka ku alliance inuyo mwatsala nokha simuzikwanitsa, chokani ku Tonse, yendani pamudzi ndi anzanu.
@DysonUmaliАй бұрын
If I were Usi I would chosen one lose the vice president post or lead UTM . USI can has no power to lead UTM as a party unless he resigns as vice president and not work with MCP government. If Usi was intelligent politically he wouldn't have accepted the vice president post that MCP new would weaken him politicallly .
@CyrusBanda-l5yАй бұрын
Powerful speech
@augustinechibbalazi8897Ай бұрын
Dr Usi you are a democratic leader
@user-sh6gi5uq3lАй бұрын
Mumafuna umboni? Zodana pa ndale ndizomwe zikuononga Malawi wanthu Political hatrage will not take us nowhere usi is the unifying factor
@chitanibenito1109Ай бұрын
Upange zomwe chilima amafuna kupanga ukudziwa kale kuti he was about to declare the separation for tonse alliance ndiye osatipusisa apa nthira kuwiri iweyo.
@billymhoni9527Ай бұрын
Ali yekha kumenekoko ..
@frezarphiri3480Ай бұрын
Iwe dyera bambo sikono chifukwa chani iwe ukulabadira za imfa ya chilima
@user-es4jt6ds8mАй бұрын
Ma sapota osewa ndi a MCP akowapatsa malaya awo🎉
@AlexKaunda-ny2egАй бұрын
Kodi a usi mukuvalabwinotu kodi ndi malaya achilima
@fulabanda2115Ай бұрын
Ndalama zoopsa kwambiri
@KinziWindasoni-h4b7 күн бұрын
Ulibe nthawi yobwezela pamenepo ukutani
@GiftKumbambeАй бұрын
Kkk kodi magalasiwo amakhala akuyabwa
@dysonfysonchifundo2284Ай бұрын
zoti UTM ili magulu angapo kod ndi zoonadi eti? 😂
@user-zw8ns7bk7sАй бұрын
Ndipo musakaike😂😂
@dysonfysonchifundo2284Ай бұрын
@@user-zw8ns7bk7s kkkkkk zovuta kwabas
@user-ol6uc7bj2wАй бұрын
Kkk usi ase ❤
@ChikondiAmosi-ue3jkАй бұрын
Koma kunena Zona umu muli mzeru kungot anthu timafuna kunyonzana koma ussi muli usogoleli
@DysonUmaliАй бұрын
Usi believes money buys favour in politics but he doesn't know what the voters who are true UTM wants and the pain they are have gone through in this bloody alliance . Undiwolose ndi kakutafune)
@HaliJanaАй бұрын
KOMA AMALAWI NDINUDI OVUTIKA KOBASI KUMASEKELELA ZIMENEZI ZOONA