Booooooniiiiiiiiiii kaliiiiiindooooooo! Katundu osamangia unyolo koma chulungamo 😅😅😅
@LysonMtalika-tb6fk17 күн бұрын
That's our beloved president, president for the poor always guided and protected by the living God, long live our president, we poor citizens loves you more, the Dddddd Cccccc!!!!, the senior pangolin 🔥🔥🔥🔥
@KimJime-d9k17 күн бұрын
Zoonadi ine ndi mboni kundende kuli anthu osalakwa
@capsozmaulana366518 күн бұрын
😂😂😂 koma ichi,,, akuti pa convoy yanga pazikhalanso akasinja
@MaryMary-dz2th17 күн бұрын
Akuti mademo tsopano tizipanga bwino....The DC ✊
@williamdyton749817 күн бұрын
Theeee DC iweyo ndi one zomwe umanena zimachitika🇲🇼✊
@yuzzykamwendo393717 күн бұрын
This guys, is a strong man, he hasn't any fear and all time he fights for Malawians.Lets fight hand on hand guys Dzikoli ndilathu ndithu tisaope.
Bon Kalindo The DC ofunika azikhala ku State House ndipo tikamuthamangitse Satana Ali kumenekoyo
@christopherpetro-pen367818 күн бұрын
Akut koma chino sichimakpa kumangidwa😜🤪🤪🤪 ochatsika siyani kuononga ndalama zathu pa nkuluyu mungoziyipisila mbili
@christopherpetro-pen367818 күн бұрын
Sichimaopa
@pemphoashani461918 күн бұрын
Komano Kodi anthu osawukawo mukumawauza kuti azipangako chani kuti mu umphawimo adzachokemo. Chifukwatu kulimbana ndi BOMA sizingasinthe status ya osawukawo koma zitha kusintha status yanu. Mukalimbana nalo BOMA chonde tilimbikitseniso kuchita ma business chifukwa chete chete sautsa nyama
@Boystarpluss17 күн бұрын
Men ma business wo mupangira kutiko?dZiko silikuyenda bhoo amayenera kumadzuzula kut amalawi wo azikhala pabwino...ngongole Zama business mutenga kut?Amati mukonze chapansi kut chapamwamba chikhale bhoo...
@ChipiliroLungu17 күн бұрын
Vuto umaphatikiza za zelu ndi zofoila zomwe nde makhala kaye ndi zofoila zakozo
@GilbertKuchipinda17 күн бұрын
Pa ma china pokhapo nde wabayatu driver, operator gad zose zikugwilidwa ndi ma china lebala wawo ndi bwana wa anthu aku malawi.
@UmarMasame18 күн бұрын
Booooooon kalindo the comred💥💥💥🇲🇼🇲🇼🇲🇼
@DalitsoMatope17 күн бұрын
Ngati Satan simumuziwa melowere ku state house Satan amakhala kumeneko pamodzi ndi Angelo ake azikhale ng'oma ,,kunkuyu ,,,mkaka ,,Monica,,chityola ,,nick amenewa nde Angelo asatana
@AuspiciousKalambula-hp7gj17 күн бұрын
Ati ine ndiye ndi "kusendendani" uyuyu sakuwopa eeesh 😂
@user-qy9xf4rw4e18 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkk koma amalume😅😅😅😅😅😅
@NichorusKaimira17 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂🙌
@Machemba-b7s16 күн бұрын
Born kalindo is my eff
@awaliwilliam647218 күн бұрын
Makosana nanu mwati mudyele ma views pa speech ya nzanu nanu yakhulan yanu mupange post bas Khan ya straight
@Yamikie-yamikie17 күн бұрын
😂😂😂
@OWENROBERTS-hf7xd17 күн бұрын
Salute my homie 🔥
@bridgetmajor364617 күн бұрын
Inuyo ndi 1. More 🔥🔥🔥🔥🔥
@wilisonbornface428217 күн бұрын
Live from south Africa cape town
@johnussenu284817 күн бұрын
You are welcome in mangochi bon kalindo
@user-zr7wk4oq2x17 күн бұрын
Uyu ndi woopsaaa kwambiri ‼️🤣😂
@AlickSquare17 күн бұрын
Koma boma muthu uyu kungomusiya basi sidzoona paka apolisi 200 kuononga misomkho ya anthu
@georgefungulan664817 күн бұрын
Joab tachezaniko ndi bodyguard wa kalindo bwa?
@ozziehenderson997717 күн бұрын
Akut atamangidwe ndamako😂😂😂
@innocentsathasteven409317 күн бұрын
Iwe ndi nyooo ndikukudziwa bwino bwino
@StanleyChirwa-d6b17 күн бұрын
Chi booooniiiiii kalindo 🤣🤣
@Yamikie-yamikie17 күн бұрын
Ka instrumental kabpansiko kaksomoneza olo mukatsitse kwambiri😅
@rodricklanjesi243017 күн бұрын
Ma background music wo akuononga zinthu fix that guys ... almost ma videos Anu got the same prob
@MadalitsoJackson-ns3vu17 күн бұрын
Uyuuuuuu ase ati chiboni kalindo😂😂😂😂
@PempheroKachande18 күн бұрын
Koma yh ,,,ichi nde Kaya😂💔🤣🤣😳
@KENETHMAJASA-ud5ee17 күн бұрын
Kutchaya kugwetsa, shatapuuu!
@TrizerDoller17 күн бұрын
Number one kalindo
@UTHMAN-WAYA17 күн бұрын
T/A MABUKA 😂🔥 AND THE LAST MAN STANDING ✊🌹
@samuelazumah105017 күн бұрын
Munyengo ya ku ng'alula
@blessingschiwaya-zn8is17 күн бұрын
Koma Kalindooo
@user-cy9zp4fb2m16 күн бұрын
Oipayo alephera yekha
@kennedyfaraimulilo407417 күн бұрын
Ine ndine nyooo,too much drama.
@amonprincegenamu720318 күн бұрын
Booooonnn Kalindoooooo 🔥
@AnabandaMasauli-rk3lg18 күн бұрын
Ndalama zolipira Lawyer ndilibe ine
@yusufdaud966317 күн бұрын
Koma ichichi eeeeh 🙌😂
@Ntchindinkhwazi17 күн бұрын
Eeeeh !!! Uyuyu anatopa
@TimothyJobe-jc1ti18 күн бұрын
Akuti pa mdipiti okamutenga kalindo mudziikaposo kasinja😂😂😂
@CathyKatsokamalanda18 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@LzkayLzkay17 күн бұрын
Ife timakukonda bon Kalindo
@FestonJuwawo-dn4lp17 күн бұрын
Uyuyu ndi makina😃😆😃😆😃😆
@TitusShumba17 күн бұрын
Kalindoooo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@marychavula69817 күн бұрын
Inu ndi one😂
@JonathanChimwaza17 күн бұрын
Chilungamo sichimabisika
@JonesMalingaMalinga-nr6jc18 күн бұрын
Uyuyu mmmmm koma yeah
@user-zr7wk4oq2x17 күн бұрын
Inu makosana stop kuika ma instrumental si nyimbo izi mixieew tonse ndi oimba?
@RichardJackson-p9z17 күн бұрын
Zaphavu zmenez
@moyo7777717 күн бұрын
Boma lopusa
@AustinBanda-wg5pw17 күн бұрын
Bon Kalindo the DC
@user-jr6fe2gi4b17 күн бұрын
Musatitopese
@MaxWell-d7o17 күн бұрын
The DC mumakwana inyo
@captainsisitomalawi154817 күн бұрын
Chatokotatu ichochi ndichooopsa🤣🤣🤣
@Humphrey26517 күн бұрын
😂😂😂Kalindo
@SamsonMedson-oz7rq17 күн бұрын
Cd2d❤
@euccotechs174417 күн бұрын
Umakwana bale
@user-qc1yv3zk7i18 күн бұрын
Dc nkatundu uyuuuu
@ZiporahThiezy18 күн бұрын
Koma ziliko 😹😹🏃
@ShalomShine17 күн бұрын
Kasunja woyeeeeeee!!!!!!
@user-ch1jf9zk6g18 күн бұрын
Kma. Ichi🤣🤣
@lindamankhanamba758017 күн бұрын
Kuli zinthu ku 🇲🇼😂😂😂😂💔
@PeterNamphwanya17 күн бұрын
Chibooooon kalindooo
@ChimwemweFredrick17 күн бұрын
Kom ichiii inu 😂😂😂
@VeroNica-tp5vp18 күн бұрын
Eeeh kom ichi
@Fahadimalopa17 күн бұрын
this is born kalindo 😂😂😂🎉
@AaronMaganga-rj1pp18 күн бұрын
Koma ichi 😂😂😂😂😂
@ThokiezMw17 күн бұрын
Koma akulu awa
@Martha-m6e17 күн бұрын
Zowonadi tikudikira za ifa zimene zija.
@user-xg5dg7jj4d18 күн бұрын
UTM president
@ShadreckMtepuka-sj8ue17 күн бұрын
Komatu nde watokotatu
@uzacarolinakaime77217 күн бұрын
Inde Nyo!!!!... lol
@kha606817 күн бұрын
What's with the useless background songs ?
@user-hq5wh3pn5b17 күн бұрын
Kkkkk koma the DC
@user-mx5cx3gl4h17 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣kasinja
@TamandaniGawan17 күн бұрын
kuyaka
@Praise-u8f17 күн бұрын
W
@BeautyYona-vc7jp17 күн бұрын
The DC
@user-eh1gn1nj9d17 күн бұрын
A Kalindo mukuimira ndani bwenzi mutapita kwanu ku Mulanje muzikapanga campaign muzaimire DPP yomwe ija muzapeze chochita panopa sizikuthandizani izi muzafa osauka ndithu