1st born wa Dzanja from MG 1 uli ndi umunthu coz pa dziko pano uli ndi brother wako mmodzi from MG 2 komanso ndi mwana musamalire, komano zolinga ZENIZENI za MG 2 PA mlandu wu aaaaaa chabwino tiyeni tione kuti MALAMULO akuti chiyani
@TabiahWisick16 күн бұрын
Fusolanga kod mayi akut chumachili mmanja mwa anaawo akuyendetsandi ana ngat chuma chawo,tsopano nanga bwanji mboniyoikutiso chuma chili mmanja mwamayi awo sangathe kugawa ?
@MwaleYankhoKatanga-k3e2 ай бұрын
She knows how to explain,this marriage issue
@ChrispoGawani2 ай бұрын
Mwanayu ndi wa m'ng'ono akuyenera kusamalidwa aphunzire school yabwino azigona pabwino chuma adzapanga yekha msogolo m'mayi wa mkuluyi wavuta sapereka gawo la chuma komanso bamboyu analakwitsa osalemba will iyeyo ndiyemwe anayenera kugawa chuma adakali ndi moyo azibambo anzanga tiphunzirepo apa nkhani izi always zimavuta kwambiri
Amen good wafunsa funso labwino mkazi wa mkulu mahule wa ndi anthu oyipa wake kunalibe
@MeltonMumba-rn9mf2 ай бұрын
Exactly
@patrisiobinalison84762 ай бұрын
Uyutu sihule ,mkazi wamkulu pomwe analakwila ndi kuvomeleza mitala
@GiftCMlangeni2 ай бұрын
Mind your tongue remember ngati pali hule ndi abambowo not mkaziyo. Am also aman how can idate wantchito wanga? Mesa amkagwirantchito nde amakapempha banja ngati? Wamkukuyo adavomeleza bwanji mitala nde chitavute nchani kungomugawirako kuti asathe nthawi yaboma? Kungoti ndikupatsa business imodzi or minibus imodzi basi nkhani yatha. Komaso akuiwalakuti chuma chimatha, dzina la abambowo lilindi wamwamunayo, enawo mawanja akakavuta adzamufuna nchimwene wawoyo?? Nanga mayiwa akadzakalamba akaziwa adzakwanitsa zonse zomwe zimafunika mamuna akhalepo?? Mmmmh kuipamtima kukuoneka apa
@McDonaldKanyinji2 ай бұрын
As long as the first wife accepted that they were on polygamy, the worth is suppose to be shared according to how many kids each wife has......... but not equal..... Court should observe this.❤
@AshleyMbewe-k5z2 ай бұрын
I second with you bro,the rulling is very important
@PaulBambe-m3tАй бұрын
Where is the ruling. I need it pliz. Give me a link 😂
@CeciliaPaulchidule27 күн бұрын
Km kuli zinthu😂😂😂....second wife is so courageous
@gracechingaresearch-b5v16 күн бұрын
Malemuwo asanamwalire anaenera kupangiratu kalikose pamwana wanuyo mesa mukuti anakugulirani kanyumba basi pangani za business sisi😂😂😂 muchedwa mukalilira chuma kubereka mtsikana sichifukwa iwe ungofuna chuma basi
@ShaibuMbwana-h2i6 күн бұрын
Shaibu mbwana 😂😂😂😂😂
@peterjoshua25952 ай бұрын
I just like the guy who’s sat behind the accused 😅
@hajikasaku605428 күн бұрын
I like second wife she had a good question to first wife
@FrankNyoni-pm3jz2 ай бұрын
What was the final judgment ?
@PamelaSumbuleta29 күн бұрын
Koma chigamulo ndie chikuchedwa bwanji kkkkk
@gremmerchris712 ай бұрын
Nkazi wachiwiri uziyamika kuti uyu woyambayu anakulola kulowa m'banja lawo komaso pokutenga kuti uzikamugwilila ntchito chokhacho uzimuyamika...usazitenge wapamwamba kwambili kuti wabeleka mwana wamamuna nzakoyo sikufuna koma zidangochitika.. Komaso iwe nkazi woyamba kuti ufike pomwe ulipo dzidatengela nzakoyo kukhetsa thukuta ndikudzichepetsa kwakwe kuti iweyo ukhale umoyo ofewawo muthokoze pomupatsa shop imodzi over time mudzapeza ina basi simple..mukutelo pokuti iye ndiyemwe wasunga nfunda wanu basi
Aah ine I think this is just acting why do I see the same faces on different cases or maybe it's only me 😂😂😂
@corretabanda76852 ай бұрын
Eyaka ndi acting. Akufuna kuti anthu adzipita ku khoti zikaavuta, komanso anthu tidzitengerapo phunziro.
@MilwardChanza-mr4yr2 ай бұрын
Mkazi wachiwiri anakakonda anamkagaila ma percentage angat?
@RemitterFlik11302 ай бұрын
Ndipo anthu musamangoti a agawe agawe muli inu mungapange zimenezo uyotu ndi hule apezaso bambo wina kuti abelekele mwana wa nkazi sinanga ali pa business yopangila ana kwa zibambo omwe akufuna ana osiyana m nyumba ine ndikuti asampase....
@owenlingwa10 күн бұрын
Mau ngat kaz chiphwanya 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@glorynkhomaАй бұрын
Mwanayo athandizidwe bas kms amayi wo ndiopusa kangoona kuti pomwe ndkugwira ntchito pano pari chuma bas ndavomera banja zaziii ndpo musamupase kanthu azikhala konko kumipando yofubwako
@vestarmkandawire61382 ай бұрын
Mkazi wa chigololo ameneyo ndi mbuzi,, banja ndi ndalama ndi zinthu ziwiri zosiyana. Mkazi woyamba ayankha bwino kuti adavomereza mwamunayi akhale awose osati chuma. Ndiye huleyo chuma chake ndimwana wamwamunayo. 1 Akumbukire kuti anali wa ntchito wa mayi wamkuluyo 2 wamulakwira kumulanda mwamuna wamwini. Apapa kunena zoona chuma asamugawire ndi wakuba mayiyu. Zikuonesa kuti wapha mwamuna ndiye kufuna chumacho.
@AwufWaria2 ай бұрын
Wolakwisa ndi mayi oyambayo povomereza mitala,chuma chiyenera kugawidwa basi
Vuto lowakhira nkhani pali za uhule apa mesa akuti unali mgwirizano oti ayese zida abambowo amafuna mwana wa mwamuna ndye atafunsidwa amayi akuluwo anavomera kuti vuto palibe atha kukhala pa mitala mwayi uwo mimba mkubwera akabadwe mwana chimphongo ndye kuti mdala Ku khosi mbeeee kuti mission yatheka mwana wa mwamuna wapezeka. Ndye chomuchulira kt ndi hule mumakhala chili chani....?????
@MwaleYankhoKatanga-k3e2 ай бұрын
The first daughter is coming with some juries and want to run away from this as solution
@HevenChiwaya2 ай бұрын
Nkadzi wa chiwiliyo chuma akanapasidwa ndi mamunawakeyo chifukwa chumacho ndi cha kubanja lalikululo mamuna wanzeru satenga wa kwa Nkazi winabkupitisa kwina akanapanga zawo nthawi imene amunawo Ali ndi moyo😢
@josephgondwe58292 ай бұрын
Nkhanizi ndi za kuMalawi konkuno, I like it kuti you are using Chichewa osati zokhala ndi interpreter.
@HaroonHaji-rp4if2 ай бұрын
Malamulo amatiuza momveka bwino zachuma chamasiye mwana wamng'ono komanso ndimwamuna akuyenera kupatsidwa gawo lake koma akharea ndimtsinkhu woyenera ndipo MG 2 sakulakwitsa sichifukwa MG 1 pamene amavomereza mitala anadziwa zoti ali ndi chuma chimene umwini waukulu umakhara kwa ana
@AgnessMaumbo2 ай бұрын
Akafukule amunache ankamuuza kuti amupatsa chuma adzamupatse,vuto la tsikana amasiya chomwe apitira maso muchanya kwa zimuna aeni ake kkkkk,akamaona nkazi akuoneka bwino amaona ngati akumusamala ndi mwamuna nde kumakhala kuti ndipite nane ndizikaoneka ngati amene aja,osadziwa kuti munthu wamayi amazilombikira yekha kkkkkkk,kuphunzitsa kwabwino amene akuonera atsikana aphunzirepo sure
Umfiti suposa pamenepo,kumakhala ndi umunthu palibe amadziwa za imfa kuti ingachitike mwachangu kwa bamboyo,ndili sure naye gawo lake lipezekapo akagamula.
@GibsonZunda2 ай бұрын
Agawe chumacho
@PociahMack2 ай бұрын
@@MikeMwale-bw1xw wina wazuzika naye wina kungochoka uko Ali agawe zosathekatu
@MikeMwale-bw1xw2 ай бұрын
@@PociahMack Ayi agawane anapangira limodzi,sikuti wangochoka uko nayeso anali mrs
@mphatsokauta63872 ай бұрын
@@MikeMwale-bw1xw kungoti kwanthu kuno ma banja samayenda mwadongosolo
@elsontmsukwa43562 ай бұрын
Ine ndimaganiza kuti chuma chisungike bwino chingokhara ndimunthu yumozi azichiyanganira kenako aziwapasako azake asowekera chinachake chifukwa akapupuluma kugawana mwana tava ndi wamungono nde mwina nikutheka awagawira koma koma mutu wa business alibe apeza chonse chathaso nde mwanayo azapezachani akakula 😢😢😢😢
Bwanji you don't fully finish your court trials... whats the point of not letting us know the judgement. I. USA they finish fully. We love watch such stuff
@HildaMachinjiri2 ай бұрын
😮😮😮 ati ana akazi alibe ntchito nkhani ija waiononga 😂😂
I think sanati akufuna chuma chonse, nkona akuti angowagayirako ka gawo chabe
@marianyirendaАй бұрын
Komano walembedwa ntchito mphaka kumasukilana ndi a bwana wosachita mantha mphaka kuvomeleza kuti mukwatilana yikhale mitala ndi mkazi wa bwana mmmmm koma azimayi muzikhala ndi mantha please
@AgnessMakuluni2 ай бұрын
Chuma ndi chamkazi wamkulu no matter kut ali ndi ana akazi okhaokha, wang'onoyo bwezi atamupangira chuma chake asanamwalire
@GiftMoyo-eh8pw2 ай бұрын
Ndipo wamkulu wandisangalatasa koposa asagaile Chuma icho cos mwachoka Patali Mamie hule linagwa mchikondi bcz Chuma I 😂😂😂😂😂😂😊
@NedsonKennedy2 ай бұрын
Sibwino kumangoti MG 2 ndioyipa ngati kuyipa sanakuwone bamboyo asanamwalile mukawone anthu wamba😂 chuma agawe basi, kuthandiza mwana it's not a big deal.
@DesireMphatsogama2 ай бұрын
Komatsu inu omwe mumapanga post muzimalizitsa mpaka kuchigamulo coz timaphunzilira momwemu
@starlonJames-qr4xl2 ай бұрын
yes
@ComfortChiombangoma2 ай бұрын
Zoonadi ndithu 😂
@JoaoLazaroMATABICHO2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂zowond
@CleJohn-v6z2 ай бұрын
Yes iwe😂😂
@KondwaniGumba2 ай бұрын
Ngati adali mkazi wa malemu ndikumuberekera mwana , akufunika kukhara ndi gawo la chuma Cha mamuna wawe. Ndikukhulupirira kuti pakutha pa khaniyi ikomera odandaula.
palibe kumugawila koma kugawana...100% ya assets yo then awona anthu oyenela kugawana ndangati then aliyense atenge percentage yake. community of property ijayo
Watchitoyo anafoira bamboo alimoyo,akanapempha zake zoti aziyendesa ekha abambowo asanamwalire koma pot mphuno salota
@graciousbwanali50792 ай бұрын
Gyz if i can have chance to coach people before the court ambiri sibwenzi akuluza milandu❤
@wittinessnkhokwe2 ай бұрын
Kodi anthuwa anangokhala amodzimodzi tiziti amangoyelekeza ndi zaku court?
@GilbertKuziona2 ай бұрын
Ngati mkazi wankulu akuziwa ndipo anavomeleza zamitala ndipo akudziwadi kut kuli mwana kwa mkazi wachiwiri akuyenera kumupasa gawo lake mwanayo
@StanleyChinsewu2 ай бұрын
When we are in that situatio n solve this problem before you die it's about money not marriages today
@dinnakabaghe42462 ай бұрын
Iyiyi imakhala Drama koma kuti tiphunzire mmene nkhani amaweluzira mma Court athu, moti muzionera pa MBC TV Monday 5:pm to 18:00. pamakhala nkhani zosiyanasiyana koma anthu ake otenga mbali ndi omwewa. Zikomo
@miryamkatundulu2 ай бұрын
Please men before you die, write your last testament and will so that life is not complicated.
@MikeMwale-bw1xw2 ай бұрын
Kodi bwanji programm yofunikila ngati iyiyi adayipatsa nthawi yosakwanira?Tikaonetsetsa chofunika kwambiri ndi chigamulo koma anthu tisanamve chigamulo akupezeka nthawi yatha amatero?konzani tikufuna tidzimva programm yonse bwino bwino osamatisiya mmalere.
@bonfacekantwanje62232 ай бұрын
Akuti akufuna chuma Cha chani? Koma guys😊
@zimmekapachika67842 ай бұрын
Kwakoma ndikuno😅😅😂😂😂😅😅
@binwellchunga49862 ай бұрын
Mai uyu wodandaula chuma apatsidwe sitikuti wagawane pakati koma chuma atengeko izi akulankhula Mayi wankulu izi ndizopusa kwambili mamuna wake ngati amatenga maliseche mkumalowetsa ku nyini kwa mzakeyu mpakana ubelekamo mwana sizoti wapusitse court kuti mwana wazimuthandiza Noooooooo uyu chuma apatsidwe basi
@henrymwale89942 ай бұрын
Kodi izizi zimakhala zenizeni kapena ndi mwa drama coz anthu ake ndimaona amodzimodzi
@SoniahMussah2 ай бұрын
Drama😅
@ChifundoBita2 ай бұрын
Ndi drama yomwe imaphuzitsa anthu zokhudza khothi, malamulo, kuweluza milandu
@PeterJafariАй бұрын
Kodi anagamula bwanji guys ine ndikusaka koma sikupezeka koma mkadzi wang,onoyi akuyenera amupase ngawo lake ndithu
@henrychikuse15432 ай бұрын
Uhule ulibe profit chemwali. Komaso kulibeko mau oti amuna athu koma amuna Anga. Mwana wanu ndiwakuchigololo ndiye mwana wakuchigololo sawerengedwa
@SteveriaNyalugwe2 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤
@DavidChapalala-i2g2 ай бұрын
Nkhan yabwino kwambiri 😂😂😂😂😂😂 Chumacho ndi cha onse ndipo akuyenera kugawa bas