Zoti Manganya ndi wa UTM amazidziwa yekha😢,ndipo asatinyasepo apa iiya,nthakati wachabechabe
@EsterManiyaСағат бұрын
Kkkkk bambo asikono kuteroko
@YousufuJohnСағат бұрын
Usi azanya manyi pa conversation ataluza chifukwa palibe uyo azamuvotele
@YousufuJohnСағат бұрын
Usi pantumbo pake azavota yekha ndimkazi wake
@RaphaelKatimba2 сағат бұрын
Manganya si president wa UTM ai Manganya ndi kazitape wa MCP ndipo ndi galu fisi nkhumba yeniyeni
@MusaLion-os1lxСағат бұрын
Ndikunenetsa kut izitu akuchita ndiyeyo guys ndani yemwe anagalore kut mwana wake wamagidwa otsapitako aaaaa atsatiputsitse ife serious
@S-rr1euСағат бұрын
Usi,,,, ndiwa MCP not UTM
@RiteRoderick2 сағат бұрын
Utsi ndioyipa zedi Koma guys let's fight strongly for our freedom
@stevenmwamadi30352 сағат бұрын
Usi ndi galu yamuthu ndi snake ameneyo anatengapo gawo pa khani ya dege ija koma thawi ndi nyengo ikubwera pompano muthawa kumalawi kuli kwanu pompano sikale
Mwaupeza kale umboni oti amafuna kupha usi?? Mesa dzulo mmati akufuna kupha chakwera lero mwasinthaso ndekt simukudziwa chomwe mukupanga mungofuna anthu aiware zakuvuta kwa mafuta ndi commission of inquiry ija ana anjoka inu
@YousufuJohn4 минут бұрын
iwe galu eti iwe siwukudziwa kuti mbuzi yakoyo ndiyakupha komaso ngakhale atamanga anthu sangawinebe ku conversation palibe angamuvotele manganya ayiwale azamuvotela mkazi wake ndi ana ake wamva kapolo iwe?
@StevenKupheka-k6b2 сағат бұрын
Usi ndi mbuzi and galu ya munthu
@NyirendaAndrew-w8q23 минут бұрын
Manganya otsamunenapo autsi ali chabe bwino
@CassimMbalaka15 минут бұрын
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxidwa pa ifa ya chilima