Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤
@yowasschitsosa5348Ай бұрын
@@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba
Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi
@yowasschitsosa5348Ай бұрын
@@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,
@ExtratremendouszeusАй бұрын
@@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe Chikhulupiliro sagula Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu Mark 14:48 (Yesu sanamugwire ) Mark 15:21 (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo) Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka
@EdwinHowardmkandawireАй бұрын
Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?
@EdwinHowardmkandawireАй бұрын
@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa
@ExtratremendouszeusАй бұрын
@@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools
Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.
@SolomonNjolomoleАй бұрын
100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.
@PIYASSFKGCHIWAYAАй бұрын
Ulemu wanu brother
@MeriaMasingaАй бұрын
Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima
@AdamYas-ec9ocАй бұрын
Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha
@AjibuTwalibuАй бұрын
Mmmm man mwalankhura zoona ok
@bamusmajawa1619Ай бұрын
Iye uja mpaka azafa akuzuzika
@yowasschitsosa5348Ай бұрын
@@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,
Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi
@hamiltonsolomon3756Ай бұрын
Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha
@user-yv3jp3it2tАй бұрын
Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi
@RobertLuka-wy9clАй бұрын
Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa
Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.
@Mervic-vm8eoАй бұрын
Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise
@user-hm9nc7lz6eАй бұрын
Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima
@StevoZimbaАй бұрын
Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊
@WilliamLimwalwoАй бұрын
Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.
@JowasiMasina-fy8jiАй бұрын
Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi
@Lingstone-r3zАй бұрын
To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤
@peterlowole7841Ай бұрын
Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen
Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi
@user-vu4cz1mt4fАй бұрын
Chakwera wakupha tonse tikuzwa
@lysonkaselema7321Ай бұрын
Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi
@SandlessWakhuluma-ns1ioАй бұрын
Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.
@LouisAndrew-jr1yjАй бұрын
Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏
@user-my4gr1pv8hАй бұрын
Tizamusinja amweneo big ngamo
@KennedyPhiri-h9hАй бұрын
Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake
amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera
@FelixBoss-yn9peАй бұрын
Palibe zandale apa Koma choonadi
@isaaczuzeАй бұрын
Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima
@AiameAdamo-su1ntАй бұрын
Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.
@SimeonAbraham-u2jАй бұрын
Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva
@patassonelucaszovuta3431Ай бұрын
Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto
@RitaKaingaАй бұрын
Komanso ndege inagwera poyeratu eehh
@UsenLashidАй бұрын
Zaphabvu brother
@MarymahendraАй бұрын
That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .
@chipiesato-ut7hxАй бұрын
Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona
@user-ec4jo9cu4dАй бұрын
Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔
@spargomwАй бұрын
😭😭😭😭😭😭😭
@user-ww9rj2wx8dАй бұрын
Zowonadi brother
@AndrewMagomboАй бұрын
Zoona anthu a mcp okumpha
@AlexPhiri-in1reАй бұрын
Zoona bro
@moseskapelekeza8849Ай бұрын
Kodi muli joz
@ELLENKANJEREАй бұрын
Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni