Yaphweka ndrama ya misonkho ya a Malawi pangani m'mene mungathere
@ElatonGwaza-k4hКүн бұрын
Koma Malawi akupita kuti kumangozira ngati nyumba
@johnkatapeh7182Күн бұрын
Chikangawa no more
@hamiltonsolomon3756Күн бұрын
Kkkkkkkkk
@UseniMailosiКүн бұрын
M 300 000 yapita pamenepo
@GeorgeMboma-e7jКүн бұрын
Kkkkkkk😅😅
@Halima-i4xКүн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂
@MercymithieMithieКүн бұрын
Akt akuika tala😂😂😂😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅😅
@rashidadan2533Күн бұрын
Amalawi kupusa mpaka kumazila mseu mukuona
@KingDavedNkhata19 сағат бұрын
Ndipo Ife anatilodzayo ayi dzikomo
@AndreaNgulubeКүн бұрын
Kunalembedwa aliyese alindi makweloake nanga aja anapwedwa kumuzuzu sanali athu 20 aja inu adpp
@rasheedjohn6956Күн бұрын
Atupule simunthu olakwa iyayi. amatiuza amalawi koma kumsava
@Joel-o3kКүн бұрын
Kulibe boma kumalawi ndi za drummer bs zikupanga atsogoleri . Kugula oyimba ndi anthu a maudindo otchuka mu zipani zina bac Chakwera alibe umuntthu wa umunthu satanic yamulowa kwambiri
@DONNEXKhama-bk1gyКүн бұрын
Bola pamenepo kmabe takhumudwa.nane
@WanangwaMfuneКүн бұрын
Achita bwino nawoso tidzaatsiya osatengako nduna ku UDF kkkkkkk
Bwana Atu. Bwino mukapitiliza kusemphana ndi ma sapota muchitha chipani. Anthu akwanu akudya chitedze inu mukupita kwa A Congress kkkkkkkk Ndale yosamveka bwana.
@RaphealKwelaniКүн бұрын
Ase mumakwana uli bho
@ArnoldKhandeyaКүн бұрын
a udf mukula mopusa , masewera mumachitawotu chipanicho chidzatheratu
@sabinaphiliКүн бұрын
antanyiwa mwadzuka bwanji mwasowatu Pauline pamakoma chifukwa cha inu