Ma kape a MCP munapha chilima mungatiuze chiyani mboleyanu a kunkuyu
@McshonWilliam6 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@ChrispineJonathan6 күн бұрын
Mwachedwa
@LimbaniSamueli7 күн бұрын
Dpp sakugona nayo tulo athu awa
@AlexanderTraffick6 күн бұрын
Mwayambano kufusana nokha nokha kkkkk zinthu zaipa basi
@henrychakachadza33577 күн бұрын
Chimanga chamasula(chafula) kale.
@AbdiBadiru-n9b6 күн бұрын
Tooooooooo much late 😮😮😮😮😮😮😂😂😂😂😂 mwalozedwa
@HassanChikumbe-jk5xc6 күн бұрын
Black box ilikt ?
@robertmchoncho6 күн бұрын
Koma imfa ya Chilima mukuipanga kusalemekezeka Zoona mpaka kutukwana ndinu Malawi wa mtundu Inu??
@MarySinjirani6 күн бұрын
Mosses upezelepo mwayi apa unene kumene kuli BLACK BOX iwe kodi ndi chani chikuku gwira pa kamwa ifetu tikudikila umboni wo chokera mu BLACK BOX izi mu kukamba apazi mwachedwa nthawi yanu yatha musati pusise a Malawi sitikukodwa nanu