Oimba omwe ananyozapo Bushiri

  Рет қаралды 498,401

Sam Malvitha

Sam Malvitha

Күн бұрын

anthu omwe anaimbapo nyimbo zonyoza bushiri

Пікірлер: 248
@sammalvitha
@sammalvitha Жыл бұрын
Zikomo poonera, chonde Ngat simunachite subscribe.. kumbukiran kutero ... Muchite like ...video iyi .... Zikomo
@muyabasamson
@muyabasamson Жыл бұрын
Akupanga sanjechabe
@starlonjamus
@starlonjamus Жыл бұрын
👍
@gordonmatsagopane
@gordonmatsagopane Жыл бұрын
1qq
@Dyson.chibaloh
@Dyson.chibaloh Жыл бұрын
​@@starlonjamusHy Hy hyhy
@bahatichirwa7601
@bahatichirwa7601 Жыл бұрын
😊😊😊😊😊😊😊
@gracephiri1203
@gracephiri1203 Жыл бұрын
Mwaitha bro muzibwelabwela
@jaymilazi2937
@jaymilazi2937 Жыл бұрын
Muzibwezerabwera ndi nkhani ngat izi
@IsaiasIsaias-yq7zg
@IsaiasIsaias-yq7zg Күн бұрын
Aaa Tilibe não mchito chifukwa sitingapezepo phindu
@amontchuwa6876
@amontchuwa6876 Жыл бұрын
Nanga iwe ukt bwanji Ine ai akuziwa ndi Yahweh
@JemabinGonani
@JemabinGonani 2 ай бұрын
But is wrong, kunyoza mtumiki wamulungu.
@harryhara6217
@harryhara6217 Жыл бұрын
Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.
@greshammshelera5344
@greshammshelera5344 Жыл бұрын
True bro
@RahmahMussa
@RahmahMussa 27 күн бұрын
Kodi bwanji mumazimva kuzindikira bigy kungofuna basi kulimbana ndi oyimbawa muungofuna kuwalakwitsa aaaaaàh
@ashraffmidu7837
@ashraffmidu7837 Жыл бұрын
Piksy didn't liar he only says the truth moreover that song of him it's my favorite song....akutithera mtundu m'malawi ameneyo...#MartseKeepRip😥
@NIDYBANDA-iz7xz
@NIDYBANDA-iz7xz Жыл бұрын
Pakut tilibe mphavu zopangila judge km mmmmmm
@judywilliams2349
@judywilliams2349 Жыл бұрын
That’s true, blood money. Magician full time.
@judywilliams2349
@judywilliams2349 Жыл бұрын
That’s true, Bushiri is a magician and I can’t understand how people are so brainwashed.
@keniekaipa1997
@keniekaipa1997 Жыл бұрын
Mbuzi iwe umanama......usiye kupanga za anthu
@EnockNyirenda-nr2uj
@EnockNyirenda-nr2uj 3 ай бұрын
Ayizikomo
@FauvorJohn-kp7yh
@FauvorJohn-kp7yh Жыл бұрын
Athu ena samakodwera akamachita zabwino padziko rapasi mzawo. BUSHILI NDI MUNTHU WABWINO KWA MBIKI OK
@DeOffice-zz7rb
@DeOffice-zz7rb Жыл бұрын
Like
@Ishriss1999
@Ishriss1999 Жыл бұрын
Koma Mthuzi ija simaseweratu 😂🙌
@sammalvitha
@sammalvitha Жыл бұрын
Anaswa
@hanifrego2744
@hanifrego2744 Жыл бұрын
True chilugamo akuchiziwa iye urendo wa kumwamba ndi one one so let God be God
@twarichissah4222
@twarichissah4222 Жыл бұрын
Nyimbo ya namadingo ya wabwela muli uthenga wabwino kwambiri ndipo kwa munthu wawumunthu pamenepo Palibe vuto lililonse 🤔🤔
@stevinmuhone877
@stevinmuhone877 Жыл бұрын
Machitidwe awo abushiri ndi amene tikuti samapemhphera mlungu ndipo ine sindizawakhulupirirapo ata
@hanabrighton9903
@hanabrighton9903 Жыл бұрын
Alandililatu pasipano ameneyo kumwamba kulibe mark my words
@hanabrighton9903
@hanabrighton9903 Жыл бұрын
Ineso chimodzimodzi alikuti Gracy Chinga cz of him ulemuumene mukuunenawo ndiyekuti mphotoyake
@NIDYBANDA-iz7xz
@NIDYBANDA-iz7xz Жыл бұрын
Km mwatzindkilisa zambili man sam
@rhodrickchingoli3636
@rhodrickchingoli3636 Жыл бұрын
aMalawi timakodwa wina akamavutika
@musicoftheviolinstudios.1109
@musicoftheviolinstudios.1109 Жыл бұрын
zofotokoza zanu zili bwino,ndizosakolana zachindunji bwino bwino.mulipo awiri ndi big mani enake samazitchula dzina lake .
@yassinrashid7012
@yassinrashid7012 Жыл бұрын
Mkulu wa bakili Muluzi tv
@bunayatambala310
@bunayatambala310 Жыл бұрын
This is true 💯💯💯💯 There is no way to like him this is Deval stan blood money God will fire him 🤞🤞🤞🤞🤞 he must repent en come back to Islam the truth he knows en Islam is straight way to go pradise plz plz bushir come back to Islam before judgement
@Littlefair7
@Littlefair7 Жыл бұрын
Kkkkkkk ma prophet a fake amanyozedwa kumene komanso kunyozetsa the entire Christianity, nanenso ndiyambitsa mpingo wanga basi. Ndiponso usamatchule kuti mtumiki wa Mulungu kumanena achina bushiri. Ma prophet a fake ndi amene akubweretsa ulesi komanso umphawi ku Africa.
@kalunguhelias
@kalunguhelias 6 ай бұрын
I've ukutiuza za bushir KT titaninaye
@noorwilly4710
@noorwilly4710 Жыл бұрын
Are you lying everything what you talking don't blame the people from Malawi musician you lying please you must talk no sense what you talking about please my friend you know the new 🤔🤔
@MercyMachipisaMunthali
@MercyMachipisaMunthali 5 ай бұрын
I will not like u because u promote evil satana pala wachita chithu muchikomenge not kuchikokomezga yaye
@DavidOdala-h3g
@DavidOdala-h3g 7 ай бұрын
Adha pasanapako ndwe galu kwambili Kod kusowa nthito ndkomwe kukuchititsa eti
@jayvidrah
@jayvidrah Жыл бұрын
ᎿᏟᏲᎥᎿ𐒀 ꂵꀎꀘꀎꀤꂚꁅꅏꀤ꒒ꍏ ᏴᎡᎪᏃᏃᎪᎻ
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Moses Makawa anavomereza kuti amatamba pa radio. Pamenepo wasatanic ndi ndani? Bushiri sindimamutsata koma Bushiri sananene kuti iyeyo ndi otamba.
@daviechannel8603
@daviechannel8603 18 күн бұрын
Koma gooti Amen Amen zilizonse bhushili ndisatanadi ndie poti mumagooziwa kuobela manja zilizonse koma bhushili ndimagazimazi bs mauthenga onse amatumiza mafoniw
@JuniorAbasi-eb5ce
@JuniorAbasi-eb5ce 11 ай бұрын
A Malawi ife tilibe ulemu Mr Bushiri zawo dzidayela khale chofunika ndi ulemu basi monga ine ndikuti ulemu wanu mr Bushiri .kodi A Malawi tinakhala bwanji munthu aliyitse akalemela.ali ndi vuto
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Atapempha ndalama ndikuwakaniza amangotukwana. Moses makawa anavomera kuti ndi mfiti pa radio.
@BlessingsZulu-q7i
@BlessingsZulu-q7i Жыл бұрын
Be careful with a word of God and don't make a mistake to follow wrong things that you will know that this is a wrong. read jobs 13 verse 14
@MatiasRaphael-dl7yu
@MatiasRaphael-dl7yu 4 ай бұрын
Anthu timakhulupilila ma prophet omwe anamwalila koma munthu yemwe timamuona zimakhala zovuta kukhulupilila komabe Pali mau Oti munthu sachuka Dela la kwao anthu azakhulupilila kuti bushiri analidi munthu wamulungu atamwalila ambili omwe Amati bushili simunthu WA mulungu sawelenga malembo oyela ngati ndioipa mulungu ndiyemwe angaone kuti akuchita choipa osati inu AI
@JohnPhiri-ki1zf
@JohnPhiri-ki1zf Жыл бұрын
All the people who is fighting Shepard Bushiri are Demons cos there are human demons. These pipo are casing themselves so let's watch these pipo are going nowhere with their music.
@JohnPhiri-ki1zf
@JohnPhiri-ki1zf Жыл бұрын
They can say, We're all pipo of God but I want to tell you that, There is pipo of God and the children of God now listen very carefully; The children of God are going to the internal life for ever and ever while The people of God are going to the hell then If you can not understand this, then you are a human demon.
@LEONARD-l5v
@LEONARD-l5v Жыл бұрын
Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.
@rachealjosephs7544
@rachealjosephs7544 Жыл бұрын
No matter what I can't be a member of bushiris church 😪😂 never cause he is not the real man of God
@MercyMachipisaMunthali
@MercyMachipisaMunthali 5 ай бұрын
Bushiri is man of God why God created us on his image don't judge. Just saying is not man of God 1. Ur selfish 2.wachokapo pamaso pamulungu Only God will justify us let love one another don't trust a man trust in God.
@daviechannel8603
@daviechannel8603 18 күн бұрын
Koma bhuchili amaulukadi koma kuli zinthu dziko lino koma chilungamo chimawawa bhuchili amatumiza mauthenga oti anthu akalowe chalichi chake ndie akunena zoona bhuchili ndiwasataniki
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@dhaoudhiabedinegomaseko2363 Жыл бұрын
Adzabwera ngati akhristu koma kuti adzanyenge ochuluka.Mawu awa ali mu bible koma anthu eti kakakakaka
@BornfaceMbewe-dr8id
@BornfaceMbewe-dr8id 3 ай бұрын
zikomo mupitize kusokola nkhani zotele nizofunika koposa
@AmosNephan
@AmosNephan 5 ай бұрын
Bushili ndinthu wabwino kwambiri
@RichardKachingwe-p8h
@RichardKachingwe-p8h 6 ай бұрын
Piksy ndi mfauna oziwika ndi bouma😂
@eliasleonard9448
@eliasleonard9448 Жыл бұрын
Moyo ndikamozi ndagwirana ndinamdingo
@DorisThambo
@DorisThambo Ай бұрын
Prophet bushili is not a true prophet wether like or not
@fradahmakwinja3835
@fradahmakwinja3835 Жыл бұрын
Major one is Great
@BlessingspMponda
@BlessingspMponda Ай бұрын
Kodi ndindan amene samaziwa zot namadingo ndi bushir amadana
@DorisThambo
@DorisThambo Ай бұрын
Nambululuka, mwaiwala kuti amambululuka koma alibemapikp .
@lysonkumbwezaabdullah6075
@lysonkumbwezaabdullah6075 Жыл бұрын
pamenepo zoyamikila zake ndi ziti
@BlessingsWakhutamoyo
@BlessingsWakhutamoyo 3 ай бұрын
If today mulungu says iam whom i
@judywilliams2349
@judywilliams2349 Жыл бұрын
I have no respect for the magicians. I can’t understand how people are so brainwashed. God help us.
@hendrixhendrickse1608
@hendrixhendrickse1608 Жыл бұрын
me too .
@SIDDHARTPATRICK
@SIDDHARTPATRICK 7 ай бұрын
Sure
@ipyanamwanyongo4169
@ipyanamwanyongo4169 Жыл бұрын
hey I will not fear any personality in the world,bushiri is not following Jesus Christ they just pretending like Christianity but not bro
@ChippieBetha
@ChippieBetha Жыл бұрын
Only God knows
@NjabuloMKhize501pro
@NjabuloMKhize501pro 3 ай бұрын
Pwedo
@chrissjunior8342
@chrissjunior8342 Жыл бұрын
Proudly you my brother " nd nkhan ngat zmenez 🤟
@ElizaNyirongo
@ElizaNyirongo Жыл бұрын
Love it
@AuthenticV
@AuthenticV Жыл бұрын
Pastor David Kalirani Amayenera kukhala pa number 1
@yusufelliotanalidodoloooma9685
@yusufelliotanalidodoloooma9685 Жыл бұрын
Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino
@mastersubiri7934
@mastersubiri7934 Жыл бұрын
Mulungu wake utii nanu kutengeka ndi zili zonse
@tichezechitukula5352
@tichezechitukula5352 Жыл бұрын
@@mastersubiri7934 Mwandifusilako boss!!
@MauriceKalira
@MauriceKalira 11 ай бұрын
TNM super rige malawi
@ChesterBanda-qm8fh
@ChesterBanda-qm8fh Жыл бұрын
Fire up otsogoleri
@DanielPatrick-u1g
@DanielPatrick-u1g 6 ай бұрын
Simungapezemo ndalama
@Frederick-s4h
@Frederick-s4h 16 күн бұрын
Wayawe Sadowa namiwa ndi uliminat
@KHOSWE
@KHOSWE 6 ай бұрын
Bushiri is not a christian
@JohnnyRafaelagustinho
@JohnnyRafaelagustinho Жыл бұрын
Besf
@MercyMachipisaMunthali
@MercyMachipisaMunthali 5 ай бұрын
God have mercy on you
@shotsfired588
@shotsfired588 Жыл бұрын
Wasatanic uyu, ngozi mmene zikuchitikira ku malawi mukuyesa ndi chani, ngozi zoopsya zikuchitikazi chibwerere bushiri kumalawi, magazi akuwukha mwakathithi anthu akufa moopsya and tinanena bushiri atangobwera ku malawi, kuzichitika ngozi zoopsya munthu Wasatanic ameneyi akabwera.
@mastersubiri7934
@mastersubiri7934 Жыл бұрын
True that brother
@ipyanamwanyongo4169
@ipyanamwanyongo4169 Жыл бұрын
Yes was satanic uyo too since Ali ku Malawi everyday I hear accident why her please bro don't defense him hey,but follow Jesus Christ not men
@daviechannel8603
@daviechannel8603 18 күн бұрын
Ndipo ndichoncho amatumizatso yekha mautenga kt anthu alowe sataniki mafonim mauthenga amatipeza amene akumuikila kumbuyoyo aliliimodzi
@lovemhango4051
@lovemhango4051 Жыл бұрын
Like
@AgnessNkosi
@AgnessNkosi 9 ай бұрын
Only God knows
@KondwaniGrey
@KondwaniGrey Жыл бұрын
Zilibwino kwambili
@HusseinCassimRajeef
@HusseinCassimRajeef 11 ай бұрын
zikomo awulusi
@JaelChilima-wn5qf
@JaelChilima-wn5qf 10 ай бұрын
hy
@membermussa9343
@membermussa9343 Жыл бұрын
Kkkk😮🎉🎉🎉
@LaurentAmbassador
@LaurentAmbassador Жыл бұрын
Last days
@ayamijackson1443
@ayamijackson1443 Жыл бұрын
Very much Best bro please ceep it up good job bro
@sammalvitha
@sammalvitha Жыл бұрын
I will try my best
@Alimoyo-km2ps
@Alimoyo-km2ps 6 ай бұрын
Following
@RaimundoMuquiale-yc7lf
@RaimundoMuquiale-yc7lf 9 ай бұрын
Koma ndiye
@LukaSaulula-kt7bu
@LukaSaulula-kt7bu 6 ай бұрын
Oooh okay
@SamMajawa
@SamMajawa 6 ай бұрын
Thanks
@IsaiahKamanga-e7n
@IsaiahKamanga-e7n 6 ай бұрын
Like
@frankleeliwonde6221
@frankleeliwonde6221 Жыл бұрын
Namadingo sanalengezepo kuti wasiya kuyimba nyimbo zauzimu
@sammalvitha
@sammalvitha Жыл бұрын
Watch my next video
@kennedykamoto5068
@kennedykamoto5068 7 ай бұрын
Umakwana sam
@tamarachipokosa9633
@tamarachipokosa9633 Жыл бұрын
Muchedwa nazo limbikirani ntchito
@PatsonSaiwala
@PatsonSaiwala 24 күн бұрын
😂😂😂 kodi zotelo
@osmanbeyadi
@osmanbeyadi Жыл бұрын
Mumaitha
@AffectionateFoliage-gh6bf
@AffectionateFoliage-gh6bf 8 ай бұрын
Keep it up
@DidaNfunsa-zj5es
@DidaNfunsa-zj5es 10 ай бұрын
Zoona
@renardnguluwe7914
@renardnguluwe7914 2 ай бұрын
Ndazkonda❤
@jimmuyaba9513
@jimmuyaba9513 Жыл бұрын
Muli ndi ntchito yopanda kulipilidwa
@JenniferRonnex
@JenniferRonnex 5 ай бұрын
Haji❤
@HAWAHANDRWE
@HAWAHANDRWE Жыл бұрын
Zikomo kwambili sam malvitha zaveka bwino
@kennethkaunda3636
@kennethkaunda3636 Жыл бұрын
Ndi zoona bro
@SelemaniSabiti
@SelemaniSabiti Жыл бұрын
❤❤
@MercyMachipisaMunthali
@MercyMachipisaMunthali 5 ай бұрын
Tose tapachalu chapasi ndise wakuchimwa Bushiri nayo wali ngat lwee pala wamanya lchi suzapanga zamuthu uzamukonda kwa mbiri. God bless Bushiri so that forex yisamasowe lfeso tikapulumusike
@SunnyWyson
@SunnyWyson Жыл бұрын
That's very gorgeous
@DavidThirani
@DavidThirani Жыл бұрын
ATHU AMAMUNYOZA BUSHIRI CZ CHUMA CHAKE CHOCHOKERADI KWAMULUNGU (ziwan kuti Dziko lapasi limadana ndizochokera kwayehova}
@ShadMuhammadWillard
@ShadMuhammadWillard Жыл бұрын
😂😂
@godfreybiziweck1224
@godfreybiziweck1224 Жыл бұрын
Ndizoonadi anamunyoza prophet shepherd bushiri
@RahmahMussa
@RahmahMussa 27 күн бұрын
Iweso uyambe kumunyozako
@MercyMachipisaMunthali
@MercyMachipisaMunthali 5 ай бұрын
Ndimamukonda Bushiri chifukwa samanyoza munthu sayakhula mau opusa kwa munthu. Inu muli Holly lnu mukumaimba nyimbo atsikana atavula ndee oipisisa lnu mwawalimbikisa athu kut God will bless them kapena mwawatengerathu kwasatana
@PastorDivaEPCInternatiolMinist
@PastorDivaEPCInternatiolMinist Жыл бұрын
Idon't know we need to learn and to respect men of God,their prophecy and their calling remember what happened to Mirrium belittled MOSSes the saint tooked for granted because he was their own biological brother.
@StarchJonas
@StarchJonas 10 ай бұрын
Don't put bad words in the mouth of the musicians pliz. Am not agreeing with your conversations
What Uebert Angel Said to prophet shepherd Bushiri on his Birthday feb 2024
9:04
Mbili komanso chiyambi cha Driemo
10:28
Sam Malvitha
Рет қаралды 117 М.
💩Поу и Поулина ☠️МОЧАТ 😖Хмурых Тварей?!
00:34
Ной Анимация
Рет қаралды 2 МЛН
Which One Is The Best - From Small To Giant #katebrush #shorts
00:17
Kucheza ndi wa Sataniki Mpakana Waziwulula Yekha
20:20
Morton Baghaya
Рет қаралды 168 М.
Ching'aning'ani comedy, ft Ngiringande
6:53
Malawi Page
Рет қаралды 324 М.
49 BILLIONS USD PROJECT😱PROPHET SHEPHERD BUSHIRI NARRATES THE WHOLE STORY
12:49
Goshen City,Mangochi
1:15
Ngwazitech PN
Рет қаралды 86 М.
Grace chinga analosera kale Za Tonse alliance
10:49
Sam Malvitha
Рет қаралды 7 М.
Report La Chilima Labwela - Ntanyiwa Kufotokoza
31:53
Malawi Extra
Рет қаралды 149 М.
REPORT LA NDEGE MU CHICHEWA NDIKUYANKHA MAFUSO ATOLANKHANI
47:28
Top 6 Most Protected Presidents in East Africa 2024
8:57
African Informant
Рет қаралды 415 М.
Chifukwa chimene a Malawi ambili amamudera Namadingo
10:36
Sam Malvitha
Рет қаралды 78 М.