Omwalira apezeka wa moyo

  Рет қаралды 76,263

Malawi Lovers 🇲🇼

Malawi Lovers 🇲🇼

Күн бұрын

Пікірлер: 71
@CatherineDesire
@CatherineDesire 3 ай бұрын
Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?
@Lloyd-gd6pu
@Lloyd-gd6pu Ай бұрын
Ine kwathu zidachitikako 2015 mwana wa uncle anga adamwalira ali ndizaka 9kubwera 2015 km pano adangosowa kma nayeso amkatchura mayina ya anthu tonse ndithu mmmm zokhumudwitsa
@RobertKBanda
@RobertKBanda Жыл бұрын
Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx Жыл бұрын
Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya 3 ай бұрын
Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya 3 ай бұрын
Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B
@JohnChibalo-wf8gr
@JohnChibalo-wf8gr Жыл бұрын
Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 10 ай бұрын
koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please
@EdinaKaonjola
@EdinaKaonjola 7 ай бұрын
Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏
@CatherineDesire
@CatherineDesire 3 ай бұрын
Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?
@Felix-ln4ql
@Felix-ln4ql 2 ай бұрын
Koma padziko pano pakuchitika zinthu eeh ndagoma
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Жыл бұрын
Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje
@peterbakuwo1249
@peterbakuwo1249 Жыл бұрын
🙆🙆🙆🙆
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 Жыл бұрын
Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk
@oliviaolivia4979
@oliviaolivia4979 Жыл бұрын
Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 Жыл бұрын
Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji
@florencebonga3211
@florencebonga3211 Жыл бұрын
Ambuye alandile ulemu 🙏
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 5 ай бұрын
Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni
@rachealphiri3416
@rachealphiri3416 Жыл бұрын
It happened in Zambia twice
@ephraimphiri5789
@ephraimphiri5789 Жыл бұрын
Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...
@chimwemwemaquesuwell5841
@chimwemwemaquesuwell5841 Жыл бұрын
Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 10 ай бұрын
ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh Жыл бұрын
Ukulu wa Mulungu tauona
@tonyteixeira2463
@tonyteixeira2463 2 ай бұрын
Tolo Thoko😅
@MoloiTeboho-x9f
@MoloiTeboho-x9f Жыл бұрын
Number ya abelo pls pls ol ya abusa
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 5 ай бұрын
Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo
@HawaMamo-q2v
@HawaMamo-q2v Жыл бұрын
Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya
@collinstrevor
@collinstrevor Жыл бұрын
Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo
@richsambakusi424
@richsambakusi424 Жыл бұрын
Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa
@Pungwe123
@Pungwe123 Жыл бұрын
Divine postmortem
@LenardCosmass
@LenardCosmass 16 күн бұрын
Koma ndietu mmmm
@esthermakwinja3207
@esthermakwinja3207 Жыл бұрын
Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke
@nimrodkapingatheu5475
@nimrodkapingatheu5475 2 ай бұрын
Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....
@IvvyMakuluni
@IvvyMakuluni Жыл бұрын
Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂
@PempheroNamacha
@PempheroNamacha Жыл бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka
@MadaGrant
@MadaGrant 11 ай бұрын
Great work prophet❤🎉
@JosophineSolobala-hp5ds
@JosophineSolobala-hp5ds 6 ай бұрын
So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢
@oswardmwale216
@oswardmwale216 11 ай бұрын
Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo
@MussaIbla
@MussaIbla Жыл бұрын
Eish zovesa chisoni kwambiri
@CostaCasimiro
@CostaCasimiro 10 ай бұрын
Blassa semanal agovati ndi agedo
@MADALITSOSNMNANJEE
@MADALITSOSNMNANJEE 2 ай бұрын
Amen agapezek ndi # ya mbusa ameney anditumizir
@mordecaikachale2497
@mordecaikachale2497 Жыл бұрын
Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi
@AriohChauluka-lm9oo
@AriohChauluka-lm9oo Жыл бұрын
M
@AmusedSakura-dx1nw
@AmusedSakura-dx1nw 8 ай бұрын
Lord have mercy
@BlessingsBanda-qn7xr
@BlessingsBanda-qn7xr Жыл бұрын
Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu
@marioRojas-j7c
@marioRojas-j7c 11 ай бұрын
chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 Жыл бұрын
Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 Жыл бұрын
Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.
@ChisomoKapanda-jg2uf
@ChisomoKapanda-jg2uf Жыл бұрын
Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku
@PempheroNamacha
@PempheroNamacha Жыл бұрын
Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮
@YusufMolesi-vr4pn
@YusufMolesi-vr4pn Жыл бұрын
Hy
@JusticeMakwinja
@JusticeMakwinja 5 ай бұрын
Tikufuna busayo ndithu
@marthacassam
@marthacassam Жыл бұрын
Zaulendo uno tiona zithu
@FobbieBanda
@FobbieBanda 10 ай бұрын
Too bad. The name of the Lord is a strong tower
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx Жыл бұрын
Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 11 ай бұрын
😂😂 Paja timafera ma jekete... Koma awawa voice yawo ikuchita kumveka kuti ndi a prophet di
@patriciacraiton-sf5vu
@patriciacraiton-sf5vu 10 ай бұрын
😂😂😂😂
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh Жыл бұрын
Abelo ukutiona kupusa
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn Жыл бұрын
Shame😢
@jamesjealous-p4v
@jamesjealous-p4v Жыл бұрын
Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga
@MadalitsoHope
@MadalitsoHope 11 ай бұрын
Zamphavu 🙏👏 prophet
@KINGMANMAKALA-hb9gs
@KINGMANMAKALA-hb9gs Жыл бұрын
😂😂😂😂
@AliAli.aliheassim
@AliAli.aliheassim Жыл бұрын
Taona nawo zikomo
@patrickjaenda8288
@patrickjaenda8288 Жыл бұрын
Zomvesa chisoni kwambili
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 Жыл бұрын
Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike
@Friday-h1s
@Friday-h1s Жыл бұрын
Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 11 ай бұрын
Ineso ndikuifuna ngati munaipeza please share
ZIKUCHITIKA - Anthu Awiri omwe anamwalira zaka zapitazo apezeka mu mb'oma la Balaka
51:27
Nastya and balloon challenge
00:23
Nastya
Рет қаралды 70 МЛН
小天使和小丑太会演了!#小丑#天使#家庭#搞笑
00:25
家庭搞笑日记
Рет қаралды 33 МЛН
KULONDOLOZA ZA IMFA YA AGNESS KATENGEZA...@MibawaStudios
18:50
Mpungwe-Pungwe mw
Рет қаралды 47 М.
kangaude
33:06
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 17 М.
Ankolo
14:08
Sleak Tetti
Рет қаралды 92 М.
CRUISE 5 WITH BLACK MISSIONARIES
1:05:27
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 84 М.
Ogulitsa Ziwalo Xa Anthu  Agwida Ku Thyolo.
1:27:49
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 214 М.
Amayi Tokotani
1:00:44
Mibawa Studios
Рет қаралды 2,9 М.