Basi mdani wathu Ndi Njala Ndi maluzi very good speaking and special word anthu awadi alibe uchi,oladi is like a hunting dog amango kumba pamene Pali fungo za kanyama kamene kaditsa njira kumene akupita sakukuziwa Munthu wadyera zonse mzake Dzina lake Likhale Zaine
@ChristopherKadawati-k5d8 ай бұрын
Mwayankhula zoona okha zokha. Namayenda wina ndi Brown Mpinganji.
Andale ena ndi awa : Ken Msonda, Nicholas Dausi, Patricia Kaliati, Mai Chilenje, Saulosi Chilima ndi ena otelo ziwanthu ivivi sizikukufuninso mu ndale za Malawi iwowa ndi amodzi akusokonedza zinthu
@ChisomoChikafa-dd3sj8 ай бұрын
In politics every vote counts so let's undermine his influence. He has family members who will follow him and add more votes to mcp.
@AbdulIbrahim-b6v7 ай бұрын
Za Bakiri wanama Nena zauladi musa basi ndipo munthu uyu ndi wolephe na iwe bwanji osayima kuti uthandi ze Malawi PANO ngati ufuna kuthandi Malawi koma tuma inmy in boxi ine since from 1994 am a UDF member who can we put as our president a part from Atupele
@OsmanMailosi8 ай бұрын
I salute you man, those people who did not know about him, we now know. He a jealousy and greedy person. How can he contribute or give votes to MCP when he is just a mere person? MCP keep that empty tin and assure you, in all those villages that are mentioned in the audio where uladi mussa comes from, people will never give votes to MCP. A MCP mukuoneka kuti muli ndi ndalama zosowa nazo zochita, zidyetsani ameneyo alibe kalikonse msilamu ameneyo. Tsiku likudikira kummwamba akayankhe milandu.
@ivychithyoka15518 ай бұрын
Uladi ndi Ken Msonda alibe self direction in politics.
@TwaibSalim8 ай бұрын
Panga Zako iweee uyang'ane ma comment udziwe kuti ndiwe wabodza
@ivychithyoka15518 ай бұрын
A Msonda ndi a Uladi amangozidyesa Mumba zawo osati a Malawi
@KhonzoBlose-wq7zm8 ай бұрын
Kulankhula kumeneko a bro ,keep it up.
@peterphir22508 ай бұрын
Mukuti bwanji za Nankhumwa?
@TwaibSalim8 ай бұрын
Ukulankhula bodza ife tapeza kuti Ulad anamanga ma xool komaso amalipilira a nthu fees moti iweyo ndi munthu oipa
@superiormoses48028 ай бұрын
Waswa iyi ase kugagada mosanyengerela Ai bg up
@frezargamah34388 ай бұрын
Uladii Musa ndi dausi ndimbuzi maganidzo
@TwaibSalim8 ай бұрын
Panga Zako iweee
@PaulDaka-dc3re8 ай бұрын
Sibwino kutenga munthu amene analimu chipani china azingozungulira .ndale zotani mukupanga ku Malawi?
@rashidsaid22328 ай бұрын
Mahule pa ndale opanda chitukuko ongofuna kuti azingolemelerabe mbava zimezo
@GiftGift-d6u8 ай бұрын
Uladi madeya mussa, alibe chabwino angatipangile
@greychizaka40888 ай бұрын
Ang'aluleni makape bigman. Mukawakhutire kaye😂😂😂😂
@CyprianoSandalamu8 ай бұрын
That's true big,mr uladi want to benefit from the government of mcp yet he was speaking nonsense during the time of ruring udf ,dpp ,he said mcp will not enter into government,now ge has come to the same mcp very sharm.
@KapepuzaFernandos-bd6nv8 ай бұрын
MCP sikulamulila ikulamulila ndi tonse alliance Kofi a MCP mukuiwala zimenezi chifukwa choti mwamuimisa chilima kumudekhesa NDE mukuona ngati mukulamulila ndi inu a MCP mukunamatu
@FrynessMoyo-to2du8 ай бұрын
Chakwera Ali busy kugwesa anthu ose oziwika chakwera amapanga ndale zodanisa
@abdulrafiquekalembo4698 ай бұрын
Uladi Musa, Dausi, Patricia kaliati and Ken Msonda are the most useless politicians Malawi has ever had.You cannot show to anyone what they did to Malawians except jumping from one party to the other for their financial gains
@PatrickNampota8 ай бұрын
Ndipo ulad musayo sazimvera chisoni ndithu eeesh manyaka a munthu
@binalidjeyshabahzombamalawi8 ай бұрын
Powerful words big boss
@ConfusedAtv-bs4gc8 ай бұрын
Munasowa munthu wankulu izi ndizowowa Kuno kudowa tikudandaula kwambiri pakuona zimene zikuvhitikazi enafe takhala tikudzola mpaka matope timati kuifela mwina Kuti nafenso tizagwileko ntchito Koma lelo tikuona abwana akutenga anthu oti anaola kale kale pankhani zandale nkumati uladi tikumudziwa Kodi ndichani chimene anachita mudziko lino chooneka manga ndizaka zingati wakhala akugwila ntchito ndiboma manga wakhala maboma angati pempho Kuno kudowa abwana tisafele malebo owola kale ifenso tikudikila ntchito tachokela patali Mene tinkapha gwapeyi uladi Musa kudalibeko asamakonde nyama yoti azake APHA kale ayi
@faithkamlongera51288 ай бұрын
Big up brother, titsukeni mitu
@OsmanMailosi8 ай бұрын
Msilamu ameneyu ndiwadyera, ulendo uno saputsitsa a mmalawi, wakuba, mbuzi yamunthu, mcp ndiye yolowa munthu msilamu weniweni chitsiru Cha munthu