Oswald Jumani Kukamba Za Uladi Mussa

  Рет қаралды 13,620

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

Күн бұрын

Пікірлер: 42
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 8 ай бұрын
Basi mdani wathu Ndi Njala Ndi maluzi very good speaking and special word anthu awadi alibe uchi,oladi is like a hunting dog amango kumba pamene Pali fungo za kanyama kamene kaditsa njira kumene akupita sakukuziwa Munthu wadyera zonse mzake Dzina lake Likhale Zaine
@ChristopherKadawati-k5d
@ChristopherKadawati-k5d 8 ай бұрын
Mwayankhula zoona okha zokha. Namayenda wina ndi Brown Mpinganji.
@AlickMDayi
@AlickMDayi 8 ай бұрын
Ubwino wakenso MCP simuwinanso ataa Mumuyamike Chilima anakupangitsani kuti muwine komano ulendo uno iwalani brother Jumani
@masterkachingwe7448
@masterkachingwe7448 8 ай бұрын
Well articulated
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 8 ай бұрын
Andale ena ndi awa : Ken Msonda, Nicholas Dausi, Patricia Kaliati, Mai Chilenje, Saulosi Chilima ndi ena otelo ziwanthu ivivi sizikukufuninso mu ndale za Malawi iwowa ndi amodzi akusokonedza zinthu
@ChisomoChikafa-dd3sj
@ChisomoChikafa-dd3sj 8 ай бұрын
In politics every vote counts so let's undermine his influence. He has family members who will follow him and add more votes to mcp.
@AbdulIbrahim-b6v
@AbdulIbrahim-b6v 7 ай бұрын
Za Bakiri wanama Nena zauladi musa basi ndipo munthu uyu ndi wolephe na iwe bwanji osayima kuti uthandi ze Malawi PANO ngati ufuna kuthandi Malawi koma tuma inmy in boxi ine since from 1994 am a UDF member who can we put as our president a part from Atupele
@OsmanMailosi
@OsmanMailosi 8 ай бұрын
I salute you man, those people who did not know about him, we now know. He a jealousy and greedy person. How can he contribute or give votes to MCP when he is just a mere person? MCP keep that empty tin and assure you, in all those villages that are mentioned in the audio where uladi mussa comes from, people will never give votes to MCP. A MCP mukuoneka kuti muli ndi ndalama zosowa nazo zochita, zidyetsani ameneyo alibe kalikonse msilamu ameneyo. Tsiku likudikira kummwamba akayankhe milandu.
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 8 ай бұрын
Uladi ndi Ken Msonda alibe self direction in politics.
@TwaibSalim
@TwaibSalim 8 ай бұрын
Panga Zako iweee uyang'ane ma comment udziwe kuti ndiwe wabodza
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 8 ай бұрын
A Msonda ndi a Uladi amangozidyesa Mumba zawo osati a Malawi
@KhonzoBlose-wq7zm
@KhonzoBlose-wq7zm 8 ай бұрын
Kulankhula kumeneko a bro ,keep it up.
@peterphir2250
@peterphir2250 8 ай бұрын
Mukuti bwanji za Nankhumwa?
@TwaibSalim
@TwaibSalim 8 ай бұрын
Ukulankhula bodza ife tapeza kuti Ulad anamanga ma xool komaso amalipilira a nthu fees moti iweyo ndi munthu oipa
@superiormoses4802
@superiormoses4802 8 ай бұрын
Waswa iyi ase kugagada mosanyengerela Ai bg up
@frezargamah3438
@frezargamah3438 8 ай бұрын
Uladii Musa ndi dausi ndimbuzi maganidzo
@TwaibSalim
@TwaibSalim 8 ай бұрын
Panga Zako iweee
@PaulDaka-dc3re
@PaulDaka-dc3re 8 ай бұрын
Sibwino kutenga munthu amene analimu chipani china azingozungulira .ndale zotani mukupanga ku Malawi?
@rashidsaid2232
@rashidsaid2232 8 ай бұрын
Mahule pa ndale opanda chitukuko ongofuna kuti azingolemelerabe mbava zimezo
@GiftGift-d6u
@GiftGift-d6u 8 ай бұрын
Uladi madeya mussa, alibe chabwino angatipangile
@greychizaka4088
@greychizaka4088 8 ай бұрын
Ang'aluleni makape bigman. Mukawakhutire kaye😂😂😂😂
@CyprianoSandalamu
@CyprianoSandalamu 8 ай бұрын
That's true big,mr uladi want to benefit from the government of mcp yet he was speaking nonsense during the time of ruring udf ,dpp ,he said mcp will not enter into government,now ge has come to the same mcp very sharm.
@KapepuzaFernandos-bd6nv
@KapepuzaFernandos-bd6nv 8 ай бұрын
MCP sikulamulila ikulamulila ndi tonse alliance Kofi a MCP mukuiwala zimenezi chifukwa choti mwamuimisa chilima kumudekhesa NDE mukuona ngati mukulamulila ndi inu a MCP mukunamatu
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 8 ай бұрын
Chakwera Ali busy kugwesa anthu ose oziwika chakwera amapanga ndale zodanisa
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 8 ай бұрын
Uladi Musa, Dausi, Patricia kaliati and Ken Msonda are the most useless politicians Malawi has ever had.You cannot show to anyone what they did to Malawians except jumping from one party to the other for their financial gains
@PatrickNampota
@PatrickNampota 8 ай бұрын
Ndipo ulad musayo sazimvera chisoni ndithu eeesh manyaka a munthu
@binalidjeyshabahzombamalawi
@binalidjeyshabahzombamalawi 8 ай бұрын
Powerful words big boss
@ConfusedAtv-bs4gc
@ConfusedAtv-bs4gc 8 ай бұрын
Munasowa munthu wankulu izi ndizowowa Kuno kudowa tikudandaula kwambiri pakuona zimene zikuvhitikazi enafe takhala tikudzola mpaka matope timati kuifela mwina Kuti nafenso tizagwileko ntchito Koma lelo tikuona abwana akutenga anthu oti anaola kale kale pankhani zandale nkumati uladi tikumudziwa Kodi ndichani chimene anachita mudziko lino chooneka manga ndizaka zingati wakhala akugwila ntchito ndiboma manga wakhala maboma angati pempho Kuno kudowa abwana tisafele malebo owola kale ifenso tikudikila ntchito tachokela patali Mene tinkapha gwapeyi uladi Musa kudalibeko asamakonde nyama yoti azake APHA kale ayi
@faithkamlongera5128
@faithkamlongera5128 8 ай бұрын
Big up brother, titsukeni mitu
@OsmanMailosi
@OsmanMailosi 8 ай бұрын
Msilamu ameneyu ndiwadyera, ulendo uno saputsitsa a mmalawi, wakuba, mbuzi yamunthu, mcp ndiye yolowa munthu msilamu weniweni chitsiru Cha munthu
@HildatoweraMhango-et4mz
@HildatoweraMhango-et4mz 8 ай бұрын
Nkhalamba zonse pano osazivotelaso ngati iwowo akuti peter saima nawonso saimaso
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 8 ай бұрын
Uladi Mussa he's a betrayer 😂
@PatrickNamakhoma-zm6kq
@PatrickNamakhoma-zm6kq 8 ай бұрын
mwayankhula bwino. mfundo zothyakuka. koma ka chingereziko komzani. kakamavuta kasiyeni. si mlandu
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 8 ай бұрын
Zoonadi
@BenardBanda-d1f
@BenardBanda-d1f 8 ай бұрын
Ukunena zoona kwambiri
@LembeniMtenje
@LembeniMtenje 8 ай бұрын
Ulemu wanu munthu wamkulu
@cjaylucky
@cjaylucky 8 ай бұрын
Kuyakul koveka kwambil
@kondwanimunthali7401
@kondwanimunthali7401 8 ай бұрын
Uladi is an empty tin making alot of noise
@richardbanda9997
@richardbanda9997 8 ай бұрын
A Uladi, kumeneko kuthokoza chifukwa akutulutsani kundende? Shame. Remember what you were saying about MCP? MCP, samala nayeni uyu.
@alexsumani6823
@alexsumani6823 8 ай бұрын
Change golo yu useless pa ndale
Mr Jokes Performing live at Mzuzu University, (Full Video)
33:43
Osman Kalyoncu Sonu Üzücü Saddest Videos Dream Engine 269 #shorts
00:26
Это было очень близко...
00:10
Аришнев
Рет қаралды 6 МЛН
A Kaliati Amangidwa Chifukwa Akuganizilidwa Kuti Amakonza Chiwembu
2:39
Senzo Meyiwa Murder Trial | 28 October 2024
Newslive SA
Рет қаралды 190
Anthu Awa Ayenela Ku Khala M'Boma 2025   Jaffa Mussa
7:38
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 2,1 М.
What If Russia and NATO Went to War Tomorrow?
24:05
THEE ALFA HOUSE
Рет қаралды 30 М.
Chikangawa Commission of Enquiry yotsogozedwa ndi anyamata a Chakwera.
11:36
За Трампом и Путиным стоят кукловоды “Голдфингеры” / №841 -Швец
52:03
Юрий Швец -- официальный канал
Рет қаралды 501 М.