Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana
@PaulokossimasiPaulo7 ай бұрын
😂 hulem nkayo
@ernestbwanalisauteni34832 жыл бұрын
Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk
@confidencebanda1092 жыл бұрын
Mayi uyo ndiwolakwa bola akanathesa banja za uhule wake akanapangila pa nkhomo pa makolo ake fro malawi
@chippiephiri45052 жыл бұрын
Mamunayi ndiwopoyila
@HIM_GG18 ай бұрын
Za ziii kusowa zotola nkhani Chan
@LimitedMolotali9 ай бұрын
Nkaziyo ndihule aphesa amuna
@josuahkachali14892 жыл бұрын
From Malawi but am stay in Kuwait
@jamesselemani10032 жыл бұрын
Oky
@WarriorKB-l3i2 ай бұрын
Ndimanena mobweleza bweleza kuti masiku ano kulibe mabanja,mabanja anali a kale lero zasala ndi zibwana azimai angonyengesa popanda cifukwa ceni ceni.Bola osakwatila
@victorsmbewe48162 жыл бұрын
Emotional damage 🤕🥴😜
@grantmachira96682 жыл бұрын
Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha
@promise36932 жыл бұрын
Kulakwa🤔
@bosconthandala99052 жыл бұрын
👀 from malawi
@zecamariosandifolo85352 жыл бұрын
Malowo ngakhale atakhala kuti nyumbayo anagula ndi iwowo komabe ali pa banja nyumbayo ndiyawose basi
@luciajames6042 жыл бұрын
It's Mozambique
@balancosemanalckgovate84642 жыл бұрын
Yes
@ngendahayososthene13982 жыл бұрын
bambo inu ndi inu opoyira zedi.
@zakeyophiri43082 жыл бұрын
Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba
@peterbanda70032 жыл бұрын
Osamusiya bwanji
@lamackbanda68692 жыл бұрын
Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨
@lamackbanda68692 жыл бұрын
Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa
@chembachilemba76232 жыл бұрын
Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
@DelcidioDiogoPedro-ir9ni Жыл бұрын
Nkazio ntanbuali
@ndazionaanastasiaannaphiri48432 жыл бұрын
Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen
@chancyutekakayala2445 Жыл бұрын
May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji
@Envanceabwinobamusieli-sf9tt Жыл бұрын
It's chichewa in Mozambique 🙄
@zaithwachiwaya2 жыл бұрын
Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed
@zaithwachiwaya2 жыл бұрын
Kom saname nkhaniyi kadakonda mukanamuonesa mzimai wa chigololo yo timuone kkkkkkk
@simangodickson17942 жыл бұрын
Mahule , Mabanja oyambila mvitsamba
@shariffalick7962 жыл бұрын
Kodi mayina akuchulidawa ndi ku malawi ?
@balancosemanalckgovate84642 жыл бұрын
ayi, koma kalipentalayo
@chifundoalfred142 жыл бұрын
Mozambique
@chifundoalfred142 жыл бұрын
Mozambique
@joebrown11582 жыл бұрын
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
@balancosemanalckgovate84642 жыл бұрын
of cause
@chifundoalfred142 жыл бұрын
Mozambique
@jessienkhoma24922 жыл бұрын
Koma ndi ku Malawi kapena Mozambique?
@kalimawandale71612 жыл бұрын
Mozambique
@paulmgombebanda-mr19sate2 жыл бұрын
Zovuta izi
@floramtiwa2112 жыл бұрын
Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja
@tadalaimwa3942 жыл бұрын
Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
@joegibsonzulu25992 жыл бұрын
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.