Zimene analankhulapo a Nkuche ndi a Bamusi ine sindikugwirizana nazo. A purezidenti ndi munthu ngati ife tomwe , tikuwanena kuti ali involved mungoziyi ndiye tiyembekezera bwanji iwowo kuti aulutse report imeneyi? Nawonso zikuwawa m'mtima zowanena kuti ali involved. Akawulutsa iwo automatically mnenanso kuti ndi abodza. Ine ndikuganizira kuti ndibwino a MDF ndi amene awulure report limeneli kuti pasakhalenso chikayiko chinachilichonse pa a purezidenti.
@DevisonHalaАй бұрын
Muja adanenera kuti ose anali mundegemo aferatu afunikaso kunena kuti lipoti ndi ili mwachangu moyo sagula ngati ndiye adapha chilima iyeso aphedwe asachite chinkhope kule ngati chikumwa supu
@swinibanda5412Ай бұрын
Muankhula mutopa koma osati kupangitsa phuma President kodi mukumuona ngati opusa amakhala ndizambiri zochita motion simudziwa ndinu mbulidi