Times Exclusive..A Nicholas Dausi kuwakana a APM as 2025 presidential Candidate

  Рет қаралды 71,515

Malawi Lovers 🇲🇼

Malawi Lovers 🇲🇼

Күн бұрын

Пікірлер: 198
@chisomombeta6446
@chisomombeta6446 9 ай бұрын
Powerful interview.....koma nkhani ndiyakuti onse amene anasumira chipani no chance ....Ayambitse chao
@dominicmphepo-jk8lk
@dominicmphepo-jk8lk Жыл бұрын
Hie guys no politician in Malawi will come to save our interest, they will be saving their own interest with their families. Let's go out there and work hard and support our families these guys akupanga Michele yawo ife tizingovutika nazo chabe.
@Littlefair7
@Littlefair7 Жыл бұрын
Koma achinyamata ndi amene akumva kuwawa dziko, yet ndi amene Safuna kulowa ndale, dziko la malawi panopa likufunika andale atsopano.
@Asidibrahim
@Asidibrahim Жыл бұрын
U are right
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Brian akuluwotu abwera ndi nfundo zosanveka Chifuwa akugwilitsa ntchito may oti, AKUTI, zikuonesa zokha adausi ndi ndioononga, Akuluwa ndi osusuka Msonda 2, Ukufuna uwauze Anthu chani😂😂😂 akuti akuti akuti Interview yonse yathera ndi mawu oti AKUTI kkkkk koma ndiye publicity secretory abambo Inu ndi ofuntha
@patrickmubiana9505
@patrickmubiana9505 Жыл бұрын
Independence. Of Zambia. Was on 24. October. 1964. Not 1963. Thanks big Man. Following you from Zambia.
@ibrahimwezely-pn6te
@ibrahimwezely-pn6te Жыл бұрын
Komatu dpp isamale izizi sizingabweretse chipambano, chipanichi ndichamphanvu ngati onse ali limodzi united. Chiyembekezo cha amalawi chili ku dpp koma nd🎉immene zikuyenderamu kaya tiziziona. Koma asawadelere adausi ndi ena omwe akutsutsana ndi akuluakuluwa
@norabanda3891
@norabanda3891 Жыл бұрын
I think B ans D should get married..they really get along well...they understand each others political language and share a great sense of humour ...bless them 😂😂😂😂😂🎉🎉🎉uluuuuuu
@MaizeTSoccerLeague
@MaizeTSoccerLeague Жыл бұрын
I wish could understand language, but looking and listening at the clip shows that here is a serious thing going on
@evansedgarmatope2463
@evansedgarmatope2463 Жыл бұрын
I have started to love Nicolas H.Dausi, he speaks the truth now....
@chesterdiquissone6063
@chesterdiquissone6063 Жыл бұрын
He understand politics very well.
@pasterPatrickGNsulupi
@pasterPatrickGNsulupi Жыл бұрын
Ai ndiotsokonedza bwanji tsakulankhula ena onwe anali kumenekowo? Ndi wa MCP mkuluyu
@Chief-Phungwako
@Chief-Phungwako Жыл бұрын
He is grown now
@frankkuluunde
@frankkuluunde Жыл бұрын
You are doing good so not forget kuti these people read more people while Brian zidamukanika Ku State
@walusungukayange8759
@walusungukayange8759 Жыл бұрын
This is one of the best interview. I always like the interaction between Brian and Dausi.... You're really democrats. ❤❤❤❤❤
@teddienamabande671
@teddienamabande671 Жыл бұрын
Dausi ndiosokoneza.
@CardoJustin
@CardoJustin Жыл бұрын
A Brian inunso ndi munthu osokoneza adausi ku nsonkhano sadapite zimenezo azitenga kuti ? Adausi zawavuta chifukwa zofuna zawo sizidatheke akatengane ndi nankhumwa akaone kopita
@esthergweje4038
@esthergweje4038 Жыл бұрын
Munthalika akumufunatu ndi anthu mmamidzimu ndi nkona amzanu anaona kuti azangoimira Munthalika yemweyo bwanji a Dausi mungoyambitsa chipani chanu at least mukamasuke musawasokoneze anthu tikuvutika ndi ifeyo osati inu ovuta ndi ife amalawi osati inu
@TrysonChimenya4-fm8nt
@TrysonChimenya4-fm8nt Жыл бұрын
Dausi is showing signs ,of going back to MCP, Politics indeed is a dirty game, Never trust these recycled politicians.
@lastonekaponya7675
@lastonekaponya7675 Жыл бұрын
A dausi ngati mukufuna kusiya chipani dzingopitani Ku MCP komwe munaliko sitikukudandaula wava
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Nkhani koma imeneyo
@chipi892
@chipi892 Жыл бұрын
Yambani chipani chanu Mr Dausi to ease your pain
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 Жыл бұрын
😂😂😂 big up Nic , i agree with you the party doesn't belong to a person .
@victoryganizanimwale9046
@victoryganizanimwale9046 Жыл бұрын
Brian Banda you are very good in this field of interviewing people..Keep it up good work sir
@lyiemax
@lyiemax Жыл бұрын
Dausi ndiwa MCP palibe chanzeru chimene anganene chomanga chipani chathu cha DPP
@towellabanda2218
@towellabanda2218 Жыл бұрын
Dausi have learned his lessons I support him 😂😂😂😂
@violetmanasecheonga4495
@violetmanasecheonga4495 Жыл бұрын
Amen 🙏
@joyceellis9045
@joyceellis9045 Жыл бұрын
Anthu awiri awa tsiku lina adzagwirana pa manja 😂. Koma they are like Tom and Jerry. They need each other's presence 😅.
@joemlelemba6572
@joemlelemba6572 Жыл бұрын
Mr dausi we don't like you, zizungu zanuzo sizingati thandize kulibe oti tongamubvotere ku dpp apart from Peter mutharika , age is just the number , we need matured people like him , inuyo a dausi mwapanga chani ku chipani , Inu ndi wa mcp tonse tikudziwa ndipo we know you mumkayenda wapansi mukupanga driving school yanu mu Blantyre mu , kukambisana satero program siyanu , musadzawaitanenso awa , palibepo chamzeru
@StevenPongolani-pp9by
@StevenPongolani-pp9by Жыл бұрын
Brian banda continue doing your good job
@jonathanchirwa3297
@jonathanchirwa3297 Жыл бұрын
❤❤😂😂😂 Mr Banda you're super
@edwardmusamba8173
@edwardmusamba8173 Жыл бұрын
Hon Dausi were u there ? If u were not there I will appreciate u investigate properly B4 u comment. U hv a very good base for your argument but u were suppose to attend that meeting so that u tell them your opinion.
@ThokinhoLupande
@ThokinhoLupande Жыл бұрын
Akuti akuti akuti akuti akuti,akutiyo ndani
@patrickmsendema4982
@patrickmsendema4982 Жыл бұрын
The best interview
@frankkuluunde
@frankkuluunde Жыл бұрын
That's political science
@FrankMlosola
@FrankMlosola 9 ай бұрын
Politics devide and rule
@CharityJumbe-q3b
@CharityJumbe-q3b Жыл бұрын
Koma mukungoona kuwada a Dausi,Munthuyu akulankhula zoona mmene multiparty imakhalira
@patriciondadzela2869
@patriciondadzela2869 Жыл бұрын
Dausi is just ranting? He has a court case to answer so seeking sympathy of MCP .
@LawrenceBadafriday
@LawrenceBadafriday Жыл бұрын
Anthu awa ndi ma brothers😂😂😂
@greychizaka4088
@greychizaka4088 Жыл бұрын
this is again one of the best interviews. Dausi ndi Brian amayakitsa moto ahahahaha
@MitengoFrancis-sp9ox
@MitengoFrancis-sp9ox Жыл бұрын
MR DAUSI. Chimenene. Mwayankhula APA ndi zosamveka Ngati inu mukufuna kubwelera Ku. MCP tangopitani musachuluse zokamba APA
@edwardmusamba8173
@edwardmusamba8173 Жыл бұрын
Brian I love and enjoy your interview. Keep it going u are are too genius.
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Жыл бұрын
Brain mumawaitanila chiani amenewa. Nthawi Yao inatha. Tinatopa nazo nzeru zao zoononga dziko
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Жыл бұрын
Dausi wa kwathu ku Mwanza koma zochita zanu mulibe chitukuko and zokamba zanu mmmmmm manyaka
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Жыл бұрын
Nduona ngati akutumidwa ndi MCP galu uyu kuti ayipite DPP, komaso akufuna kuti milandu yake ikhululukidwe
@edsonnyirenda-uv3sb
@edsonnyirenda-uv3sb Жыл бұрын
Pena muzingokara chete basi,osamangoyankhira zili zonse
@WinnerChisambi
@WinnerChisambi 8 ай бұрын
Koma Brian ma video Anu ambiri sakutha bwino why amangoyima basi kumapitirila ndimau okha bas why
@ussimasi2458
@ussimasi2458 Жыл бұрын
Dausi ndi brian aaa anthu inu mukakumana ayi 🤣🤣🤣🤣ndimaseka
@EleneoKalemera
@EleneoKalemera Жыл бұрын
i love this dausi mpaka ndayamba chifuwa ndikuseka kkk
@LastoneBottomane
@LastoneBottomane Жыл бұрын
Daus ndiwa nankhumwa akulankhulira nankhumwa team yanankhumwa mbuzizawanthu
@patiencetebulo
@patiencetebulo Жыл бұрын
Dausi ndiwe chitsiru bas ok
@Littlefair7
@Littlefair7 Жыл бұрын
Mr. Dausi akunena zoona koma, APM should step aside and pave way for new blood. DPP ikuonetsa poyera kupusa kwa amalawi.
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Kodi adausi mukuona ngati boma liri pa Times Radio abambo inu mulibe chopanga ndithu pitani ku konko ku MCP
@ThoccoBondo-mx7vt
@ThoccoBondo-mx7vt Жыл бұрын
Dausi bwinotu osazimangilira muyankha bwanji zithu zoti inu kunalibe kkkkkkkkk
@promisemakawa1556
@promisemakawa1556 Жыл бұрын
Brian ndi Dausi😅😅 mumamvana Kwambiri, mumandiwaza😂😂
@darrenduisel3683
@darrenduisel3683 Жыл бұрын
Iwe Nicolas Dausi usatenge ngati Amalawi opepera which party you're belongs D P P kapena M C P ? Ndiwe gwape kwabasi ukuwasokoneza Amalawi maganizo ngati ulj wanzeru bwanji sunapite ku meeting??????
@RexChipolo
@RexChipolo Жыл бұрын
😅😅😅😅😅 woza nazo,bring it on
@kondwaniphiri-f2g
@kondwaniphiri-f2g Жыл бұрын
Awatu alindimbali yawo Mr Dausi mukwaziwa sanganene zabwino ku Dpp
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 Жыл бұрын
Heated interview
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Жыл бұрын
Chisiyeni Chipani cha DPP a Dausi chifukwa mukugwira ntchito ndi MCP
@MpanjeHardware
@MpanjeHardware 7 күн бұрын
Zaboza zimenezo
@CardoJustin
@CardoJustin Жыл бұрын
Inu adausi ku dpp amene asakufuna achoke zipani ndi zambili mukonza kukajoina
@merviselias6230
@merviselias6230 Жыл бұрын
190%B B Dausi ayambise chake munthu osokoneza ndi amsonda ,Malata,Mavote siinu adausi,Mavote ndiife anthu akumudzi,NGCmuli angati adausi,ukayambise chipani chako dausi nonsense
@merviselias6230
@merviselias6230 Жыл бұрын
Iwe dausi unayamba kale ndale, ngati ulindi mzeru osayambisa chipani chako bwanji,munthu osokoneza,adausi inuyo mulingati hule, kumene mungaone Kuti zikuyenda mumathamangira komweko, tikufuna APM ndiifeyo anthu akumudzi amene tiliamphawi osati inuyo Adausi
@chrispeter5256
@chrispeter5256 Жыл бұрын
and i quote "iweyo usanabadwe 1992 - 1993"......kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
@kondwanichiweza4101
@kondwanichiweza4101 Жыл бұрын
mpakana chakhumi ???
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Жыл бұрын
A Dausi ndinu a MCP tonse timadziwa kuyambira kalekale ndiye za DPP zisiyeni eni wake agwilizana
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn Жыл бұрын
Brian ndi a Daus chonde thiti zanga zikuwawa mkuseka😂😂😂
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Жыл бұрын
Ine Dausi ndi Brain mumandiwaza muzipanga izi deile kkkkk😅😅
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Жыл бұрын
Brain ndi Dausi aphana 😂😂
@rachidermak8827
@rachidermak8827 Жыл бұрын
Munagulisa buluku ia polisi pá ntengo WA 2000000
@samuelsergio5343
@samuelsergio5343 Жыл бұрын
A Dausi ali mugulu lofuna kuti amalawi adzivutika.president ndi muthalika yemweyo
@LovetoClerk
@LovetoClerk Жыл бұрын
😂😂😂😂 Braan ndi Dausi umandiwaza
@RexMysonChinaghana
@RexMysonChinaghana Жыл бұрын
Zachisoni nzeru za MP
@CardoJustin
@CardoJustin Жыл бұрын
Adausi ingochokani ku dpp mulibe phindu ku chipaniko tazingopitani ku mcp komweko
@JustinZidana-n2r
@JustinZidana-n2r 8 ай бұрын
Munthu ndi uncle ake
@biza4111
@biza4111 Жыл бұрын
kkkkkk eish ngati ndiibwereze
@DanielJuly-dj2ji
@DanielJuly-dj2ji Жыл бұрын
Brian ndi Dausi 🤣🤣🤣🙌
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Жыл бұрын
Mwayamb kunyozan nokh nokha odya mbewanu kumasulir kt odya mbewa ndi Anthu opanda nzer? Mwatimasulat yapa
@Mbwanaayami-hp3xk
@Mbwanaayami-hp3xk Жыл бұрын
Dausi libe nzeru tsogoleri ndi APM omwewo kagwere uko iwee
@chrismoffatmdhluli7010
@chrismoffatmdhluli7010 Жыл бұрын
Biggest interview ever 😂😂😂😂 akuti nkhani imeneyo tibaiyedzeka Bwanji? 😅😅😅😅
@FelixKachera-je4yk
@FelixKachera-je4yk Жыл бұрын
Mwati kubwera makadi!!! Eeeeee oooo mwati mchani Kodi??? Ohooo ahhhh mufuna makadi?? Chabwino mwakhalaso ngati kamuzu wakale uja?? Chabwino zioneka zokha...
@osmanhassan8466
@osmanhassan8466 Жыл бұрын
Interview ya Dausi ndi Brian simalongisoka,kumachuluka kucheza
@rachidermak8827
@rachidermak8827 Жыл бұрын
Mupite,kuchipani kuano. Nanga pamenepo mulankhula ni ndani inuwo kukula mtima basi
@SamsonGood-cw7pp
@SamsonGood-cw7pp Жыл бұрын
Zonse mchabe wabwino ndi yesu yekha basi
@PoulImed
@PoulImed Жыл бұрын
Daus ndikatundu mmadzi ndipo akunena zoona ndipo APM ngt sasamala chipanichi chikutha
@user-sx7fg1NEDG
@user-sx7fg1NEDG Жыл бұрын
Waku ngona uyu kkkk
@emmanuelkenneth4768
@emmanuelkenneth4768 Жыл бұрын
Akulankhulatu zomveka koma nkuluyu ngati chipani ichi sichisamala chitha ngati ma katani, Munthu wanzeru mamayenera kumva maganizo a ena ndikupereka maganizo ako then kupanga chiganizo chabwino chokomera anthu onse.
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Жыл бұрын
Don't trust Dausi, don't forget ali ndi milandu yoopsa yomwe akuyankha, nde don't expect kupanga zinthu zokomera DPP, akufuna MCP izinva zoipa za DPP kuti akhululukidwe milandu yake
@alfredbanda1693
@alfredbanda1693 Жыл бұрын
​@@robertrichman9376inuso nde abodzatu dausi akuyakha milandu iti muli mumalawi inu koma
@tracymantchichi8347
@tracymantchichi8347 Жыл бұрын
Muzaphana Inu😂😂
@funnykatchenga-uk5mf
@funnykatchenga-uk5mf Жыл бұрын
Dausi opole moto, siwe wa DPP. ukanakhala nsomba ukanakhala nkholokolo, maoazi ako.
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@dhaoudhiabedinegomaseko2363 Жыл бұрын
Dausi ngosokoneza nkale akatelo akufuna adyekonso kwinaku uyu kumusatila uchimwa naye limodzi uyu sanalape ndiye zikumuzunguza mutu
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue
@PeterKhumbilaZimba-ql9ue Жыл бұрын
Aki and popo
@siliyasevenie7052
@siliyasevenie7052 Жыл бұрын
A dausi wa ndi a MCP, osangochoka kubwerela komwe unachokela galu iwe! Ufune usafune APM ayimanso ndipo awinanso
@RobinNkosa
@RobinNkosa Жыл бұрын
awa kumvetsetsa kwangowavuta. ineyo sindikuona vuto iliyonse. komanso is this the right proceedures yonenera zinthu? bwanji iwowa a dausi sanapite kwa a president awo mkukakamba nawo? kukula mtima akuruwa. kkkk
@MaupoMakwakwa
@MaupoMakwakwa Жыл бұрын
Kkkkkkkkkkk you guys are brothers now !! Brian akuti Kodi simuyankha Kuti ndakulandilani kkkkkkkkk
@peterchilewa380
@peterchilewa380 Жыл бұрын
Asatinyase dausi wa mcp
@louisgolden
@louisgolden Жыл бұрын
Dausi akuopa mafuso😂😂😂
@Misasi19
@Misasi19 Жыл бұрын
Brian Banda walakwisa kumuitana kucheza ndi munthu oti kunalibe kunsinkhano,mukachezanso ndi wina tizamvanso zina
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Жыл бұрын
Sindikumukhulupilira Dausi zolankhula zake
@chisomockuwa6869
@chisomockuwa6869 Жыл бұрын
Adausi pangani canu nd anankhumwa
@blandinabonaventure
@blandinabonaventure Жыл бұрын
Ndipo
@jameboy3924
@jameboy3924 Жыл бұрын
Uyu ndi wa mcp
@JamesThambo
@JamesThambo Жыл бұрын
Dausi ndi publicity secretary thats why akuyankhula maganizo a anthu ndi ma shadow president. Udziganiza Brian wamva
@kamwendoderek6567
@kamwendoderek6567 Жыл бұрын
adausi ngati mufuna upuresident ingonenani
@Phaless-ur6en
@Phaless-ur6en Жыл бұрын
Dpp ithelalimodzi ndi amuthalika
@blessingskaliasi4956
@blessingskaliasi4956 Жыл бұрын
Phanani bas 🤣🤣
@crementnkhoma7735
@crementnkhoma7735 Жыл бұрын
Daus choka mchipan usatisokoneze
@AbdullahDewas-k8q
@AbdullahDewas-k8q Жыл бұрын
Adawusi ndi galu alibe fundo kodi sakupitilanji ku m c p ko bwanji kodi amasetenga ngati aliyeka
@VonexMafunsa
@VonexMafunsa Жыл бұрын
Daus ndikachan
@tronygiftmitengo
@tronygiftmitengo Жыл бұрын
Akuwatuma ndi a mcp
@Marialongwe-nzlib
@Marialongwe-nzlib Жыл бұрын
Dausi akanakhala kut sanatuluke sibwenzi atabwera pa Tv ndinkhani zakuchipinda, Apa Abwera kuzayalutsa Chipani Mcholinga choti kuseriko amutame, inshort Dausi uyende Bwino
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Kkkkk wadyera uyu
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Oononga uyu
Times Exclusive featuring Shadreck Namalomba - 22 July 2023
1:17:52
Times 360 Malawi
Рет қаралды 16 М.
Times Exclusive featuring Moses Kunkuyu - 11 November 2023
1:19:45
Times 360 Malawi
Рет қаралды 62 М.
Всё пошло не по плану 😮
00:36
Miracle
Рет қаралды 4,4 МЛН
НИКИТА ПОДСТАВИЛ ДЖОНИ 😡
01:00
HOOOTDOGS
Рет қаралды 3 МЛН
How it feels when u walk through first class
00:52
Adam W
Рет қаралды 26 МЛН
Times Exclusive featuring Hon. Nicholas Dausi - 8 July 2023
1:12:56
Times 360 Malawi
Рет қаралды 104 М.
Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera
21:04
Malawi Page
Рет қаралды 150 М.
Brian Banda full interview with politician Ken Msonda on Times Radio
24:24
Times Exclusive featuring Honourable Nicholas Dausi - 15 April 2023
1:01:50
Times 360 Malawi
Рет қаралды 259 М.
Times Exclusive featuring Prophet Shepherd Bushiri - 27 May 2023
1:05:55
Times 360 Malawi
Рет қаралды 170 М.
mfumukazi 10.01
28:17
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 13 М.
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 56 М.