Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera

  Рет қаралды 127,517

Malawi Page

Malawi Page

4 ай бұрын

Honourable Nicholas Dausi speaking at the Mwanza development rally where the president of Malawi, Dr Lazarus Chakwera was present

Пікірлер: 358
@innocentissah2636
@innocentissah2636 4 ай бұрын
Anthu adyera amakhala ndi mbalume ndikuonera chitsiru chimenechi chotchedwa Nicholas Dausi
@innocentchapotera7416
@innocentchapotera7416 4 ай бұрын
adzafa imfa yowawa kwambiri
@petereliezer3795
@petereliezer3795 4 ай бұрын
Osapsa mtima ndale za ku malawi ndi part of entertainment 😂
@patrickmasa7145
@patrickmasa7145 4 ай бұрын
Uziwa et zongovela izi dausi macheza awa ahaaa kuwatengela upusa adha​@@petereliezer3795
@KennedyTchauya-fl5yk
@KennedyTchauya-fl5yk 4 ай бұрын
The king is back🌋🌋 welcome Mr Dausi , home is best
@jeffchikwapata6933
@jeffchikwapata6933 4 ай бұрын
Anthu akuononga malawi ndi amenewa
@user-kp6ng8bc2f
@user-kp6ng8bc2f 4 ай бұрын
Day wa one kuzachimanga Kaye chikachapike mutu ku maulako
@DokotalaPhungu-lk4kn
@DokotalaPhungu-lk4kn 4 ай бұрын
Dausi kujiya kumeneko. Limbikira akupasa u minister. Udyeretu. This is your last term.
@user-oh5vs1gl4n
@user-oh5vs1gl4n 4 ай бұрын
chisilu chimenechi ife pambuyo pa adadi
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 4 ай бұрын
Ako nde wasiya kut nawe bwampini
@EmmanuelMbilu
@EmmanuelMbilu 4 ай бұрын
Ill never stop following him or atasitha chipani🔥💯...... He's just a vibe person 😂
@jacobjerome6538
@jacobjerome6538 4 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂 munthu osokoneza ngati uyu ine sindimamuonepo ayi,kuchenjela kwake koopya heavy
@MacDonaldkachala-cm5gc
@MacDonaldkachala-cm5gc 4 ай бұрын
Dausi greatest of all times, good vibes😁😁😁
@towerankhoma1380
@towerankhoma1380 4 ай бұрын
Ndipo inenso sindidzasiya kumukonda 😂😂😂
@user-jq1gy5ds9n
@user-jq1gy5ds9n 4 ай бұрын
Kwambiri kumalowa chipani chabwino osati chipani chamunthu
@DickLinje
@DickLinje 4 ай бұрын
❤😮 of😢😢 ​@@jacobjerome6538😅😅🎉😢😅😅🎉
@InnocentKapesi-gx7yf
@InnocentKapesi-gx7yf 4 ай бұрын
Awa ndi achitsiru kwabasi
@carlossadimba595
@carlossadimba595 4 ай бұрын
That's great move Mr president and braval to Mr Dausi you are taking a good choice .....
@user-qh5jo5qh3b
@user-qh5jo5qh3b 4 ай бұрын
Apm my vote
@HarveyMhango
@HarveyMhango 4 ай бұрын
❤❤❤❤ Ambwana umatha
@joeljere4385
@joeljere4385 4 ай бұрын
Chakwera ❤ Dausi❤
@smokeestery1101
@smokeestery1101 4 ай бұрын
Ukalande mcp,, DDp waikanika, sungaithe dpp ase wachepa
@patrickmpinganjira3099
@patrickmpinganjira3099 4 ай бұрын
My man Hon. Nicholas Harry Dausi
@WilfredMathews-yl6ij
@WilfredMathews-yl6ij 4 ай бұрын
Politics is the game of Numbers 😂😂❤
@GeorgeFwanthaphiri-ov4bt
@GeorgeFwanthaphiri-ov4bt 4 ай бұрын
❤❤❤❤❤
@DanielJuly-dj2ji
@DanielJuly-dj2ji 4 ай бұрын
Dausi is too clever. Eish ! 🤐🙌
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 4 ай бұрын
Mbalame yokuba iyi achita Manyazi APM akulowa boma❤❤❤
@ulemubanda3934
@ulemubanda3934 4 ай бұрын
Boma lake liti?😂😂
@websterkausiwa8919
@websterkausiwa8919 4 ай бұрын
Zokaikisaa kwambri ku dpp kukuchitika za nsete kwambri zikundikhumudwisaa kwambri
@georgemmeto9722
@georgemmeto9722 4 ай бұрын
Osakaika....DPP ikulowanso boma...khulupiliran anthunu
@user-fh3dn8kt2j
@user-fh3dn8kt2j 4 ай бұрын
Never
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 4 ай бұрын
Ndipo kwambiri 😮
@StevenPongolani-pp9by
@StevenPongolani-pp9by 4 ай бұрын
Politics is the game of thrones
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 4 ай бұрын
Ndipo kwambiri
@rodglae6657
@rodglae6657 4 ай бұрын
@evancenasoro922
@evancenasoro922 4 ай бұрын
Ukatelo afuna malo ukoooo😂😂😂😂 ichiiiiii
@mcbethmbewe5421
@mcbethmbewe5421 4 ай бұрын
A rolling stone gathers no moss...
@noelcheonga8247
@noelcheonga8247 4 ай бұрын
Dausi I like this politician whether he changes side to MCP I like his character
@baziliobwanali4753
@baziliobwanali4753 4 ай бұрын
Keep going Dausi
@Johnfrank-gi5uc
@Johnfrank-gi5uc 4 ай бұрын
Imeneyo ndiyo Democracy aliyense ali ndi ufulu wopita komwe akufuna ineso ndiponso ku UDF don't blame it's my rights to do so, thanks
@khaleedsaidi6232
@khaleedsaidi6232 4 ай бұрын
Democracytu taionatu ife ndipo ndakulupilila kuti anthu a dpp analidi ademocracy ndipo anthu aja asakhala ademocracy. Nthawi ya dpp akaitana amcp kuti akhale pamonsi amakana lelo Iwo aliboma akawaitana a dpp akumabwela semene zikuoneselatu kuti dpp ndi imene imaziwa democracy ndiime phopo bwanji
@user-hm1bf6cw8t
@user-hm1bf6cw8t 4 ай бұрын
Dausi ndi machine ayiseye 🔥
@josephngoliwa
@josephngoliwa 4 ай бұрын
Hon. Dausi thank you simunanyoze Dpp and APM.. Zikomo.
@MatthewsPhiri-jh7zl
@MatthewsPhiri-jh7zl 4 ай бұрын
Welcome back
@IbrahimWezely-qd4vj
@IbrahimWezely-qd4vj 4 ай бұрын
Feel free this is your original party, takulanfirani madala
@GladysGwaza
@GladysGwaza 4 ай бұрын
The servant of the people ( do service to the people)
@user-nj3pv2wc1n
@user-nj3pv2wc1n 4 ай бұрын
Zoona boss
@user-qq3ip1od6i
@user-qq3ip1od6i 4 ай бұрын
Munthu oipaaaaa,, wadyela.. Osakonda dziko
@luciuschigoga2607
@luciuschigoga2607 4 ай бұрын
And when he left MCP for dpp he did well neh? Wise up
@lazaruschitsamba8394
@lazaruschitsamba8394 4 ай бұрын
no this is politics
@issahabdullah7186
@issahabdullah7186 4 ай бұрын
These Greedy politicians doesn't care for the Needy
@kha6068
@kha6068 4 ай бұрын
Abambowa ndi achitsilu chonchi kani
@HenzelPat-vd8cz
@HenzelPat-vd8cz 4 ай бұрын
🔥🔥🔥🔥
@MaryTchapo-py4hh
@MaryTchapo-py4hh 4 ай бұрын
Atha bac
@franciscazuwawo3426
@franciscazuwawo3426 4 ай бұрын
Dausi ndikatundu 😂😂😂🙌🙌🙌
@user-ir5xk2sw3k
@user-ir5xk2sw3k 4 ай бұрын
Uyu ndi swiswili uyu Dausi!
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g 4 ай бұрын
🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️
@user-dv7ht6vn9s
@user-dv7ht6vn9s 4 ай бұрын
Ku Mwanza samufuna uyu.... Kubisa mawanga mbuzi iyi... Fisi wachabechabe.... Sadzawinanso ku Mwanza
@TamandaniMwale-sr8vd
@TamandaniMwale-sr8vd 4 ай бұрын
Shaaaaa Kalulu
@InnocentNkhonyo-rs9lq
@InnocentNkhonyo-rs9lq 4 ай бұрын
Malawian politics
@mijerimasiye7310
@mijerimasiye7310 4 ай бұрын
Malawi walero womvetsa chisoni zedi nkhalamba zingotipusitsa zili pheeeee
@stevegowa7940
@stevegowa7940 3 ай бұрын
😂
@TrimaMpima
@TrimaMpima 4 ай бұрын
Yee
@YusuffuDaud-cs7yu
@YusuffuDaud-cs7yu 4 ай бұрын
Monica ndiye watchena ndipatse number yako
@timothylipenga8413
@timothylipenga8413 4 ай бұрын
Chi Vibe 🎉🎉
@user-oo5bx1rl3j
@user-oo5bx1rl3j 4 ай бұрын
Iweyo Dausi ukuganiza kuti anthu angadye stadium. Ndikupempha inuyo a MCP don't trust Dausi olo anthu akwào samàmukonda ai monga ndanenela kale kuti he is a sweet talker
@luciuschigoga2607
@luciuschigoga2607 4 ай бұрын
Inu mmafuna anene kuti chani chomwe bomali siikudziwacho?
@robertrichman9376
@robertrichman9376 4 ай бұрын
Mbuzi iyi
@user-ie5pc4ox8i
@user-ie5pc4ox8i 4 ай бұрын
Olo chakwera sakumutorela kuyankhula ichichi aaaaahhh
@chifundokumbali-nv7fz
@chifundokumbali-nv7fz 4 ай бұрын
Awa ngadyera
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 4 ай бұрын
Dausi, Dausi, Dausi..........ayi zikomo Ambuye akuone ndithuuu.
@user-fh3dn8kt2j
@user-fh3dn8kt2j 4 ай бұрын
😂😂😂
@user-kz3ps1je1n
@user-kz3ps1je1n 4 ай бұрын
Sadziwa chomwe amafuna uyu
@yamikanijames6915
@yamikanijames6915 4 ай бұрын
Mwamuchosa ndiye umafuna azifinyika
@BlessingsButao-cm8sx
@BlessingsButao-cm8sx 4 ай бұрын
All the best
@MacDonaldkachala-cm5gc
@MacDonaldkachala-cm5gc 4 ай бұрын
Dausi , leaving DPP, knowing that it's worn out and no direction, it just moving like a dragon fly, Martha😂😂😂😂
@AnnoyedCaptainHat-ol4dj
@AnnoyedCaptainHat-ol4dj 4 ай бұрын
Koma Dausi ndi mbuzz eti
@backfordrowanlwazi7892
@backfordrowanlwazi7892 3 ай бұрын
Mukunama mufunseni Dr Joyce Banda mpaka kuthawa mudziko muno
@backfordrowanlwazi7892
@backfordrowanlwazi7892 3 ай бұрын
Late Nelson Chikalamba Khonje anali waku Khondowe Nkhata-Bay north anakana mai ake omubereka
@MacDonaldkachala-cm5gc
@MacDonaldkachala-cm5gc 3 ай бұрын
You can't join your mother, it's not a choice It's by nature, you can join the party 'coz it's a choice, just because DPP it's not a party, it's Mutharikas family business that's why things are going this way, I understand it's not a problem for jobseekers, the yes bwanas 😂😂😂
@user-bg3rt8dy8u
@user-bg3rt8dy8u 3 ай бұрын
Nice
@JamesSaidi
@JamesSaidi 4 ай бұрын
ineso ndikumva sugar ndima comment dpp is winning this game
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 4 ай бұрын
Kkkkk tizilpa koma, we are sinners, too much lies and hypocrisy
@RonaldFunsani-ik1us
@RonaldFunsani-ik1us 4 ай бұрын
Chisilu ichi chokuba chifuna chikwama ichi
@merviselias6230
@merviselias6230 4 ай бұрын
Tinakutulukani adausi ahule pa ndale,,😂😂😂😂
@HelvBen-sc1zu
@HelvBen-sc1zu 3 ай бұрын
Ichi nd chitsiruuuuu
@yamikanijames6915
@yamikanijames6915 4 ай бұрын
Welcome to MCP Mr dausi
@prestonkasito1815
@prestonkasito1815 4 ай бұрын
Akuluwa
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 4 ай бұрын
Ndausi ndi opusa kwambili
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 4 ай бұрын
Why???
@StiveriaChikonga-rh3fi
@StiveriaChikonga-rh3fi 3 ай бұрын
Ndipo ndi mbuzi yachabe chabe
@user-iu7fj4vl8v
@user-iu7fj4vl8v 4 ай бұрын
Nkhope kunyasa ngati manyi
@user-oe5vb2in3e
@user-oe5vb2in3e 4 ай бұрын
Dausi abambo oputsa heavy
@ChikondiChikwakwa-if7du
@ChikondiChikwakwa-if7du 4 ай бұрын
Kkkkkk ndale zimampangisa munthu kukhala chitsiru ndithu
@user-kp6ng8bc2f
@user-kp6ng8bc2f 4 ай бұрын
Ichi ndi chisilu ndithu.
@user-cb2cv9fz7m
@user-cb2cv9fz7m 4 ай бұрын
Awa kkkkkkk maliro wo mulira ambili
@SACHAMAGIC
@SACHAMAGIC 4 ай бұрын
Politricking at crimax
@kubengovender6996
@kubengovender6996 4 ай бұрын
Nonsense!!
@petermsamariamapira8933
@petermsamariamapira8933 4 ай бұрын
be careful Mr President anthu wa amayimbila ng,oma komwe kuli mpunga, cholinga azidyabe ,ovutika kumangofutuka ,Mulungu akuona
@user-rk3kq9fn6p
@user-rk3kq9fn6p 4 ай бұрын
Only zitsiru,nzomwe zimaombera m'manja kape ameneyu..
@user-st4nz7th6i
@user-st4nz7th6i 4 ай бұрын
Kazitape
@Yamikie-yamikie
@Yamikie-yamikie 4 ай бұрын
Ngamisala awa
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 4 ай бұрын
Dousi Dousi Dousi, umafuna chani kwenikweni?
@AkiduMustapha-vq2nt
@AkiduMustapha-vq2nt 4 ай бұрын
Iziiii ndichifukwa dziko silikupita pasogolo Kuba omwewo amabawo akungodzungula ndimaudindo kumangosintha zipani
@madalitsoonale5338
@madalitsoonale5338 4 ай бұрын
Ndipo kwambir awa akubwezeletsa chitukuko pambuyo
@user-nm8gp1du2m
@user-nm8gp1du2m 4 ай бұрын
Awa ndiwosokonekera awa,,, zakuziwa chimene akufuna panoyo pa moyo wawo.. Akungosokoneza Malawi
@dicksoncassim1954
@dicksoncassim1954 4 ай бұрын
Iwe ndi wa congress iwe wachita bwino kukuthothora ku mcp
@user-dl8ng2zn1r
@user-dl8ng2zn1r 4 ай бұрын
Daus
@user-xd2uz1bh3l
@user-xd2uz1bh3l 4 ай бұрын
Dausi watha bas. Ndipo saoloka pa ndale ai😂😂😂😂
@evancenasoro922
@evancenasoro922 4 ай бұрын
Iyeyo anali kut osabweletsa chitukuko kwawoko, akumupopa chakwela chomcho, kuba bas
@user-wi9hz8fk8i
@user-wi9hz8fk8i 4 ай бұрын
Wakulizani Dausi makape
@simonpaul6567
@simonpaul6567 4 ай бұрын
Mbuzi yamunthu iyi
@user-cm5pv8dn7k
@user-cm5pv8dn7k 4 ай бұрын
Machende ako chi nicholasi dausi omafuna udindo ku dpp mukuziwa kuti APM sakucheza ndi ana
@user-vp8mr5ot7q
@user-vp8mr5ot7q 4 ай бұрын
Mbava is shame to my motherland country, Guys we must know that we gonah be same like zim
@juniortsegula3847
@juniortsegula3847 4 ай бұрын
Mboliyako dausi
@wilsonali7890
@wilsonali7890 4 ай бұрын
Zitsiru za anthu izi
@user-zs2cg7xl8w
@user-zs2cg7xl8w 4 ай бұрын
Wabweraso uku iwe eeee😮
@user-ln5hw7dn9g
@user-ln5hw7dn9g 4 ай бұрын
Za ziiiiii
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 4 ай бұрын
😂😂😂😂.....my question is where is chilima since I don't see him wht going on 😅
@DanielNkhata-ip7ds
@DanielNkhata-ip7ds 4 ай бұрын
Akusapa poloeera sopano dausi
@AllanMwakalenga-wn5ib
@AllanMwakalenga-wn5ib 4 ай бұрын
Samalani naye Dausi... Akuwonongerani MCP yanuyo....
@user-ir5xk2sw3k
@user-ir5xk2sw3k 4 ай бұрын
Machende ako dausi!
@StiveriaChikonga-rh3fi
@StiveriaChikonga-rh3fi 3 ай бұрын
A chitsiru awah 😎 ndiye ukuwona ngati mene wa choka ku dpp ife tikukusowa umatipasa bzy saname buzi iwe
@LeoC-in6um
@LeoC-in6um 4 ай бұрын
Sitinga bleme daus nduufulu wake nice posatilowa APM is one kuntha kwako uko
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 4 ай бұрын
😂Ineyo sakomenteso 😂 ndikugonva kukoma ndi makoment ndawaonawa 😂😂😂zadziwika kut dpp ndi boma basi ❤ Apm woyeeeeeeeeeee❤❤
@user-ee6be5kl5o
@user-ee6be5kl5o 4 ай бұрын
wapanga bwino dausi kuchitaedwa ku chipani Cha dpp , akunama uyo afuna kukudyelani ndalama chenjerani nayeni ameneyo akukupusitsani ndinthila kuwili mumasokoneza kwambiri
@LenzoChilek
@LenzoChilek 4 ай бұрын
Oyee!!!!!!!!
@user-ft9ex5gy5c
@user-ft9ex5gy5c 4 ай бұрын
Even president akuziwa Kuti ndi tambwali uyu.kuthwa pakamwa zaziiiiiii
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 4 ай бұрын
Iyi ndembuzi yeni yeni ndithu machende ako galu
@victorbanda9039
@victorbanda9039 4 ай бұрын
Mpaka kutukwanatu wasiya machende abambo ako kutchula aazako
@user-cm7zw6pk6d
@user-cm7zw6pk6d 4 ай бұрын
Amadyera mphotho bambo Nicolas Dausi .Amakometsa kumene kuli madyo .
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 4 ай бұрын
Kkklkk Dausi
@user-gq6nj6yo6f
@user-gq6nj6yo6f 4 ай бұрын
Ukupepha kumanga manda osamanga iweyo
KWAGWANJI KUMALAWI
1:43:49
Jimmy
Рет қаралды 35 М.
Times Exclusive featuring Honourable Nicholas Dausi - 15 April 2023
1:01:50
Times 360 Malawi
Рет қаралды 230 М.
Китайка и Пчелка 4 серия😂😆
00:19
KITAYKA
Рет қаралды 2,8 МЛН
Why You Should Always Help Others ❤️
00:40
Alan Chikin Chow
Рет қаралды 42 МЛН
MPHEPO ZINAYI: CHAKWERA AYIMANSO
48:18
Zodiak Malawi
Рет қаралды 28 М.
A Nicholas dausi alowa mcp
2:51
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 25 М.
MALAWI MILITARY PARADE, January 2024
31:53
Malawi Page
Рет қаралды 21 М.
Brian Banda Interviews Ken Msonda
8:37
Mzimba District, Malawi
Рет қаралды 36 М.
TIMOTHY MTAMBO KUTHAMBITSIDWA NDIMAFUNSO UKU...
59:42
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 59 М.
MOSES KUNKUYU EXCLUSIVE INTERVIEW
56:13
Zodiak Malawi
Рет қаралды 25 М.
Uladi Mussa at MCP, Kumachenjera pa town
12:45
Malawi Page
Рет қаралды 52 М.
Gule wamkulu wa kwa Njombwa
23:44
John Kadzandira
Рет қаралды 855 М.