No video

UKU NDIYE YALAKWA, ANTHU AKUCHILIMBA BLANTYRE ZOMWE ACHITA🙌🙌🙌

  Рет қаралды 197,478

HOT 265

HOT 265

Күн бұрын

Пікірлер: 563
@chrisboyce2
@chrisboyce2 Ай бұрын
Mfiti zopemphera Chakwera ndi mbale wake Usi ndipo anthu inuyo Mulungu akuyendelereni mwapadera ( SKC FOREVER IN OUR HEARTS 💔)
@timothynjakwa3913
@timothynjakwa3913 Ай бұрын
ayambe ayendera amayako
@JessicaManda-zm1ug
@JessicaManda-zm1ug 28 күн бұрын
Amen
@AchinaKellz
@AchinaKellz Ай бұрын
Inu agaru yehova wake uti,kupusa ziwanda yehova wamoyo sakhala ndimbava akuba akumpha, mulungu azakulangani osapota zopusa ukule garu iwe chairman
@EscoChingayipe99
@EscoChingayipe99 Ай бұрын
Don't judge anyone only god can judge
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Ай бұрын
Kodi ngongole imasitha dziko poti mukufuna mwaonjezere anthu mamvuto musise katundu osati ngongole
@ManganiStanley
@ManganiStanley Ай бұрын
Ndipo live atsitse katundu
@CatherineDesire
@CatherineDesire Ай бұрын
Ngongole pa campaign aoneke abwino
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Ай бұрын
God bless this thinking, ineso wad like why keeping poor malawians in a bandage yangongole mmalo mokaika mankhwala mzipatara, kutsitsa katundu, kuwaonjezera aziphuzitsi ma salaries kuti aliyese azifikira zinthu mosavuta. Izi zikungoperekaso mwayi kwa mbava za m,bomazo kuti ziziba ndalama in the name of kupereka ngongole kwa amalawi mxiiiii
@CatherineDesire
@CatherineDesire Ай бұрын
@@user-hl3st3cc4v maona Ngati ndi thandidzo angobitsa Chichewa kodi NDI ngongore yangati ya fincca adzaole tidziwiya ,adzatenge timinda NDI tinyumba akalephera kubwedza
@Gautengstanzo
@Gautengstanzo Ай бұрын
Zimayamba wez wez, sungapangile zinthu pakamodzi
@JasonMailos
@JasonMailos Ай бұрын
Mwamchitq bwino munthu wakupha ameneyo angampeleke chilima zoona
@Henry-vw2cz
@Henry-vw2cz Ай бұрын
Midzimu yakwiya😂😂😂😂😂😂
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd Ай бұрын
Anthu siyani kaduka.. mulungu simunthu.. Mulungu anaziwa kale kuti Usi azakhalapo vice president wa dziko la Malawi. Tivomereze chifunilo cha yehova pa dziko lathu la Malawi.
@tingamasi106
@tingamasi106 Ай бұрын
Chifuniro cha mulungu kuti chilima aphedwe?
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@tingamasi106 eya
@SylvesterMoyowinah
@SylvesterMoyowinah Ай бұрын
Mulungu okupha ameneyo siwakumwambayu ai
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
Awus mulibe nselu misimu yah andu 8 yinkukusatilani nkomaso awusseni amalawi ndege yinangwa bwanji osat samanyi munkunenaso mulungu ankuphasani matenda onyassa phamodsi ndi ashankwela mulungu anankuwonani 👌👌👌👌🙏
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@esaMoha-dm4kj inu mulungu????
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
@@esaMoha-dm4kj pelepa kuwecheta iseseni. Ambuje Mlungu akunde yakuti uchimbichimbi uyiche kwa mmwejo. Ajaliwe wakulungwa.
@user-qw3hj1hc7s
@user-qw3hj1hc7s Ай бұрын
Mcp chipan chonunkha kwambiri 😢😢
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@user-qw3hj1hc7s chonunkhila ndichiti???
@JamesNgwaya-vz1ox
@JamesNgwaya-vz1ox Ай бұрын
Kupha
@patassonelucaszovuta3431
@patassonelucaszovuta3431 Ай бұрын
Sewelo leni leni tikufelanji apapa pangosowa mulelemba
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage Ай бұрын
😂😂
@alicehananiya
@alicehananiya Ай бұрын
Eya pakusowatso make sikono ndi winiko
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Dramatising politics .this guy is useless
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 Ай бұрын
Nde mwati ndinu a UTM? Muzivere chisoni bwana😢😢
@WitnessPhiri-zr9uf
@WitnessPhiri-zr9uf Ай бұрын
Nde anthu mukuwona akakupasani ngongolezo mulemela mumene Zinthu zikudulilamu tsiku ndi tsiku ndalama ya ngongole siyingakupindulileni asise zinthu pandalama yanu yochepayo ikupindulilani 😢
@JenniferFyson
@JenniferFyson Ай бұрын
Powerful prayer 🙏
@user-nr4mi7pt8g
@user-nr4mi7pt8g Ай бұрын
Anthu owopa mulungu ngati abusa a chakwera
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 Ай бұрын
Amalawi tichenjere😢 kwambiri. Timva zinthu.lets think and work together.Tiwunikilane. and love each other ❤
@trymhango1509
@trymhango1509 Ай бұрын
Abale mundiuzireko a vp nzeru alibe chifukwa iwo amayenera asanayambe kulankhura kunkhalakaye cohete ose pasonkhanowo popereka ulemu kwa skc ndikunena zimu wawo uutse mtentere kenako kuwapepesa a malawi zaifa ya chilima kwinako mkumakamba mbwerera zakezo
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn Ай бұрын
Amalawi chonde osayelekeza kuvotela izi
@spargomw
@spargomw Ай бұрын
Ndani angavotere Manga? 😂😂😂
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Ай бұрын
Musova
@footballhighlightsofficial7248
@footballhighlightsofficial7248 Ай бұрын
😅😅😅
@fumbomumba5016
@fumbomumba5016 Ай бұрын
Palibeletu Fundo apa koma A vp awa he's only proud kuti ndi vice president
@madakabichi2251
@madakabichi2251 Ай бұрын
Kape uyu
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Ай бұрын
​@@madakabichi2251kape umamudziwa koma 😂😂😂😂 mesa kape amakhala osauka ngat iweyo
@lameckmajiga5426
@lameckmajiga5426 Ай бұрын
Bwana micle usi athu amakukondani kwambili!! Koma pa game yomwe mukusewela ndichakwelayi athu akutulukani chifukwa azindikila kuti inu muli under M.C.P mukanakhala kuti mukutengapo gawo muma program ama candle 🕯 komanso kuchita zomwe anthu ena a UTM akuchita mukanayenda moyela kwambili komanso zikuwoneka kuti mukufuna kuzutsa chipani chanu cho odya zake alibe mulandu!!! Ife tikanakuvotelani chifukwa cha chilima koma mwaluza basi!!! Pepani bwana usi!!!
@KizitoChikuni-dy9us
@KizitoChikuni-dy9us Ай бұрын
Akuwa patipo anthuwo yogulisira kut tionere imeneyo? Zopoila
@user-pb7mn1kx4t
@user-pb7mn1kx4t Ай бұрын
Blantyre inachulukadi mbuzi,am from by city koma delali ndi la nkhumba basi
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Ай бұрын
Munachuluka amoya 😂😂😂😂
@YatoRoy-kt4lh
@YatoRoy-kt4lh Ай бұрын
The guy has a good heart
@JamesIngeni-ku3qj
@JamesIngeni-ku3qj Ай бұрын
Which good heart ndi oipa uyu trust me
@WedsonZuzewatayamakina-rn8yp
@WedsonZuzewatayamakina-rn8yp Ай бұрын
Ndiye mwati chani😂😂😂😂 ine sindinatolepo mfundo atah olo pang'ono
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Ай бұрын
❤❤
@geokah78
@geokah78 Ай бұрын
We need a system that everyone fine support without being influenced by any political figure. Dr Usi reflect on this.
@user-qt7hx7hq4f
@user-qt7hx7hq4f Ай бұрын
Nde munayenda basi nkumawauza anthu zoti ndinkavala ma kabudula awiri ..zitithandiza chani ngt a Malawi
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 Ай бұрын
A chairman wo akalamba😂😂😂
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd Ай бұрын
Ndiye kukuwa mwalemba pa munthu wa nkhanipo akuwa pati reporter wa bodza iwe
@GeraldChisamba
@GeraldChisamba Ай бұрын
😂😂😂😂 😂😂😂 always cadet amatero mix mizimu yama albino
@EmmanuelstoneyJere
@EmmanuelstoneyJere Ай бұрын
Olo opepherayo akuona ngati akupanga sewero ndi manganya
@LawrenceBelson
@LawrenceBelson Ай бұрын
Mizimu ya anthu 13 yayamba kuonesa unya nawo ayise kufupika ngt mchimba
@MillyKachepa
@MillyKachepa Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Apa ndiye ndikufuna nyimbo ija anayimba Joseph mkasa anasankha olakwika
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
Ndipo zoona
@user-qo3kg6rv9f
@user-qo3kg6rv9f Ай бұрын
Komanso zokamba zake ndi zabwata bwata phuuu
@randettaclaan
@randettaclaan Ай бұрын
Kodi Dr. Micheal Usi ndiu wa DPP kapena wa UTM///////////////// Nanga slogun ya woyeee ndi ya UTM
@juntoiman
@juntoiman Ай бұрын
100 percent walankhula zondigwira ntima bale
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Kkk
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Zaziii
@NenaniMwamadi
@NenaniMwamadi Ай бұрын
Zasewerooo bas usiì
@RachelKamanga-vt3fp
@RachelKamanga-vt3fp Ай бұрын
Ambuye akupaseni moyo wautali me utsi muzina loti musinthe malawi wathu Ufumu unasata Daved kuubus chifukwa choti mulungu sakuva zaanthu
@user-vw7tj2ss3l
@user-vw7tj2ss3l Ай бұрын
Fundo pa line katundu anali azanu anja inu ndi achimulilenji sakusiyan
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Mbuzi iyi ya MCP. Usi usanamize anthu ndiwe wa MCP. Wavala za MCP osati UTM. Ukunamiza ndani nyani iwe. Pamtumbo pako Usiku.
@ManganiStanley
@ManganiStanley Ай бұрын
Galu kwambiri ndipo akundinyansa kwambiri
@omardyman8083
@omardyman8083 Ай бұрын
Osaiwalatu ndimazimbabwe awaa​@@ManganiStanley
@user-zl9vj6hc6y
@user-zl9vj6hc6y Ай бұрын
*wayankhulapotu .. Koma ndege inagwa chifukwa chani bwana*??
@LovenessShugar
@LovenessShugar 2 күн бұрын
Ine ndikufuna Dr usi ife tikufuna thandizo lawo ngongole atipase
@JohnKanjete
@JohnKanjete Ай бұрын
🤗🤗🤗🤗anthu sakukufunani bamboo asikono mwakhalila mpando wamagazi 😊
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
Inuso ndinu a boza pena nanga akuwa pati apa chimutima cha nyawu icho
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
Ngongole muyambe mwaona tikuyandikila mavoti 4 years munalikuti kuti muwapase ngongole mwabwera nthawi yochedwa inu mwapha chilima nde mukuona kumene ali chilima akusangalala muvutikapo apa panya panu ana anjoka inu
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Ай бұрын
Ngongole ilibe nthawi , utha kutenga olo tsiku lovota
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Ай бұрын
You can say this again, anthu tavutika all these years iwowa qnali pheee ,kumangokweza zinthu ndalama akusungira campaign? Rubbish
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
@@prettytambala5687 eti nde panopa akimalubwa zausilu aba ndalama za amalawi ena agwidwa nazo zana
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
@@user-hr6dj4xc8l khalani ndi umunthu inu nde ubwino wakuba ndalama ndi uti? Mesa kumangophelatu dziko chithyola anamupeza nazo zana president nkumati musiyeni azipita what doesn't mean you're rubbish
@patesnkajenda4258
@patesnkajenda4258 Ай бұрын
Fundo palibe bwana ingodyelanitu basssssss😂😂😂😂😂😂
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Ай бұрын
Uyudi ndi manganya srs ,masewero paliponse
@RatifMakiyi
@RatifMakiyi 6 күн бұрын
Usi Khala serious ukulongosola zithu zisamveka kutundu wa malawi
@HarrisMathew-ve5ib
@HarrisMathew-ve5ib Ай бұрын
Akuti kukhalatu ma Team ampira uku 😂 😂
@alfredbamusi1093
@alfredbamusi1093 Ай бұрын
Ndi ntchito yabwino kuti akuzipanga available to the public anthu apempha ngongole kuti upange boost capital chomwe ndi chabwino koma zimafunika kuti ayambile kukonza moyo wa ma customer amene ali anthu ogwila ntchito m'boma ndinso ma labour onse azipasidwa ma salaries omwe atazipanga match kukwera kwa mitengo ya zinthu omwe ndi ma buyer ama businesses amene akuvuta kupita pa tsogolo
@CathrineBizza
@CathrineBizza Ай бұрын
Mfundolesi usawi kkkk
@ShepherdChisale
@ShepherdChisale Ай бұрын
Musamatichotse feel nanu......penapake muzingodula pofunikila pokhapo. Ma Bandle akuvuta kale awa😢😢😢😢
@JumaGadaff
@JumaGadaff Ай бұрын
Mwayankhula bwana koma ndege inagwa bwanji boss 😂inuyo bwana ndinu opanda mnzelu mulungu akukantheni chisanathe chaka muyankha mulandu
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
Umayankhula bho heavy
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@JumaGadaff kafuseni mulungu kuti ndege inagwa bwanji chifukwa ndamene amadziwa chilichose
@IanChidothe
@IanChidothe Ай бұрын
Ndipo akudziwapo kanthu uyu
@rasnocuss4183
@rasnocuss4183 Ай бұрын
Chirimba one love!!!!!🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤🎉 mwana wapaden Manganya
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 28 күн бұрын
Zopepela zakozo osamantchula mulungu ukuwona ngati mulungu ndiwosewela naye
@UsenLashid
@UsenLashid Ай бұрын
Tengani ndalamazo or musazabweze Ayi ndi misonkho anu atuzuza thawi yayitali tengani zaulere
@lawrencekayona9247
@lawrencekayona9247 Ай бұрын
Ndinaonela atapanga comedy as a president of the republic of Malawi lelo izo
@LucyTatianahChikwekwe
@LucyTatianahChikwekwe Ай бұрын
Usi mu ma speech akewa mmmm chikondi chikupelewera bwenzi ali mu chisoni 🙏
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Ай бұрын
Bambo asikono woyeeee😅😅😅
@DevisonHala
@DevisonHala Ай бұрын
Monga muja mudamukondera chilima kuchikangawa pomupereka kuti aphedwe koma inuso mudzafa kulibe wa mbewu
@wotchidawood
@wotchidawood Ай бұрын
😂😂😂😂 yakwiya ndi midzimu bambo uwona wamphesa chilima garu iwe
@FrankMasamba-uk6mc
@FrankMasamba-uk6mc Ай бұрын
Iweyo Usi ukamalankhula kumatchula dzina la chakwela , panyapako kwambir
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂akutopetsadi bwanji ameneyu
@AlexZanda-e5i
@AlexZanda-e5i Ай бұрын
Ndakunyadilaniii amalawi welocom to Tanzania
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Ай бұрын
Apapa yalakwa , Mr Usi mwakwiyisa anthu kwabasi shaaa
@johnmpatama1461
@johnmpatama1461 Ай бұрын
Mzimu wa Chilima waononga microphone 😂😂😂
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage Ай бұрын
😂
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
😂😂😂
@user-nz7oz7lx5f
@user-nz7oz7lx5f Ай бұрын
😂😂😂
@user-bp6cq5pe3c
@user-bp6cq5pe3c Ай бұрын
Za ndale doest require presence of God. Ndale nzasatana who rules
@arthurkayuza
@arthurkayuza Ай бұрын
Is that soccer player from chirimba?
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Ай бұрын
My vote only for USI, I president of my heart
@user-oc6xd4tv9l
@user-oc6xd4tv9l Ай бұрын
,😂,😂😂 akuti lathulija manganya woyeeee
@user-px9gd6fc6w
@user-px9gd6fc6w Ай бұрын
😮e paka manganya oweeeee mmmmmmhhhhhhh
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Mpaka bambo asikono woyeee😂😂😂😂
@IssahAluba
@IssahAluba Ай бұрын
Zomwe akulimbana nazo athu awa zaziiii, noe mukuyenera kutsitsa zithu mtego komaso mudziwe kt kugwa kwandarama yathu yakwacha mukuyenera kuganiza kwambili mukapanda kutelo zithu zizativuta mpakana kale
@JaneMhango-zl6pt
@JaneMhango-zl6pt Ай бұрын
Kujaila kungongola ndiye mulephere kubweza ndalamazo. Dziko la malawi latha ili. Ma president ake ndi akuba onse.
@user-lk8kj9zv6x
@user-lk8kj9zv6x Ай бұрын
Komano za ndege ya kuchikangawa zinayenda bwanji
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Ай бұрын
Sangayankhe ..ndi yudasi iscariot
@tamalangoma2765
@tamalangoma2765 Ай бұрын
I thought kafukufuku adakali kuchitikabe?
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Ай бұрын
@@tamalangoma2765 look sharp..use common sense. Pakamwa pa usi sipanalankhule zachilima mpaka lero
@elbeys783
@elbeys783 Ай бұрын
Awaso nde ayi, athu akuvutika osamuuza za umphawi wanu muli ndalama osamatipusitsa
@RhodaBandah-sh1ir
@RhodaBandah-sh1ir Ай бұрын
Chakwela satipasaso nsimayo Ukuyakhulabwanji iwe manganya
@JackNagoli
@JackNagoli Ай бұрын
Koma ma comment wa abwana mukuwaona? 😂😂 timaganiza kaye zokalakhula sitikufelanjitu iyi iya
@Gautengstanzo
@Gautengstanzo Ай бұрын
Zimayamba wez wez am sure manganya akonza zinthu, very soon katundu atsikaso
@RhodaBandah-sh1ir
@RhodaBandah-sh1ir Ай бұрын
Ngongole sisitha zithu bwana ..mungowawonjezela mavuto Kasiseni zithu kuma shop full stop
@REXCHARLESKAJAWO
@REXCHARLESKAJAWO Ай бұрын
Bambo asikono ife sitikufuna ngongole ai, coz ngongole yo ndiye mavuto oooopsa Kwa ana anthu. Koma pangani zoti zinthu zisike pansinka kuti aliyese athe kufikira mtengo wakatundu osiyana siyana emwe mtengo wake wachita kuopsa ngati muja uchitila mkango
@GIFTEDWARDCHIGUMULA
@GIFTEDWARDCHIGUMULA Ай бұрын
MP wachinyamata and chi player mbambande🤜🤜🤜, msikawo akonzedi eee
@user-mf5ce9wj4m
@user-mf5ce9wj4m Ай бұрын
It's so sad to see Malawian are still fooled by MCP.what a hell
@EdwinHowardmkandawire
@EdwinHowardmkandawire Ай бұрын
Bola Ali vice president basi olo anthu atakuwa
@user-kr1tf2tu7s
@user-kr1tf2tu7s Ай бұрын
Iweyo ukati kumdula kwa zithu,,Ausi amapanga zithu usakafunsa ama factotry bwanji za umburi
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya Ай бұрын
Musanayambe kukamba zasewerozo mutatiyankhako kaye funso likumatisowesa mtendereri, Kodi ndege inayenda bwanji ku chikangawa? Zangongole zanuzo ifeyo ayi, munali kuti ndi chakwera wanuyo? Nkhani ndikusisa katundu, zinazo mukakambirane ku state house
@AbdulhameedWyson
@AbdulhameedWyson Ай бұрын
Chisilu iwe
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya Ай бұрын
@@AbdulhameedWyson tangopita ukalandire nawo ngongoleyo munthu iwe
@manfredzalirabetha2440
@manfredzalirabetha2440 Ай бұрын
Galu wamuthu uyu yudas scariot wamuphetsa chilima iwe sizikupindulira zimenezo mzimu wa chilima ukuzunzani nonse ku chikangawako
@SurprisedFlamingoBirds-ko1dw
@SurprisedFlamingoBirds-ko1dw Ай бұрын
Uyu SI wa UTM ayi,asagawanise chipani,ingoimilani indipendent yo basi
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Ай бұрын
Musapusitsike Chakwera anabweranso modzichepetsa
@EnockMaluwa
@EnockMaluwa Ай бұрын
Wise words Dr utsi
@user-vq5fe6mo6o
@user-vq5fe6mo6o Ай бұрын
Koma abale osapha wanthu mlungu azakulangan inu ife kumuz timavutika timasowa chakudya kamba inu atsogoleri kukweza katundu tikhulupilirapo chan apa
@AnitaChakwana
@AnitaChakwana Ай бұрын
Ati olo magalimoto apange ng'wing'wing'wii uyu anazolowela sewelo 😂😂😂
@kelvindickson
@kelvindickson Ай бұрын
Kkkkkkk munafulumila kumusogoza nzanu ndichifukwa zambili zikungooneka zopelewela
@earnestchapita2194
@earnestchapita2194 Ай бұрын
Nanga bwanji asilikari sadaseke maso popemphera bwanji
@MeshackLondwa
@MeshackLondwa Ай бұрын
I don't think bodyguards closed their eyes 😂😂😂😂😂 , Amen.
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Ай бұрын
Ife àngon tikulira mwana wakwathu kuntcheu kapolo iwe galu iwe olo mcp sitikuifuna ukulankhura zapambolo pako
@KestenMukhwapa-qp2gj
@KestenMukhwapa-qp2gj Ай бұрын
Za ziii zeni zeni zopanda ndi Schererville womwe
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Ай бұрын
Iwe ukati kaduka ukutanthauza chani nawe zausiru , MULUNGU wake utiyo amene anaziwakuti mfiti usi adzakhala vp, u vp ochita kupherau ndiye ukamutchule MULUNGU usatchule dzina la MULUNGU pachabe akukwapula , us si MULUNGU koma anapangana ndi chakwera kuti aphe chirima kenako ampase u vp ngati akutuma kuti uziwaikirakumbuyo agalu amenewa ndiye wauponda awa palibe chao afiti opemphera
@user-qh4dd6nq3k
@user-qh4dd6nq3k Ай бұрын
Kma chilimba 😂😂 zoti anthu aliokwiya ndi ifa yachilima ndiye aziti ndiambuye
@EscoChingayipe99
@EscoChingayipe99 Ай бұрын
Amen powerful player
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du Ай бұрын
Koma manganya ndi udindo wa VP sidzikugwilidzana guy's 😂😂 iyi ndi minyama
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Ай бұрын
Zamakabudula akowo anthu apindula nazo chani pomwe anthu akugona ndinjala. Dzuno pamenepo panali ena lelo ndiwe ndipo mawa ndi ena samala osatenga Malawi kusowa zochita.
@PetrosGere
@PetrosGere Ай бұрын
Kķkķkkk Koma nde kunabebatu
@DarlingtonChinyamunyamu
@DarlingtonChinyamunyamu 3 күн бұрын
Chinyamu50
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Ай бұрын
Ndikuon ngat Anthu anu okuthandiziran sadakuthandizen Kungokhal ngat sewer sinthan okuthandiziranio
@user-xr9mc5hg5t
@user-xr9mc5hg5t Ай бұрын
Munthu ukamangitse okusakira mtchele
@SylvesterMoyowinah
@SylvesterMoyowinah Ай бұрын
Kodi muli pa campaign 😢😢 kodi
@umboneyusufu4499
@umboneyusufu4499 Ай бұрын
Aka manganya ngati adalephela mayeso awumphunzitsa nde lelo angatukule Malawi
@IbrahimkDyman
@IbrahimkDyman Ай бұрын
Kodi uyuyo akuona ngati ndioziwa tchito 4year yathayi anali kuti (manganya ayenera kubwerera ku tikuferanji)
@vincentkhunsanama584
@vincentkhunsanama584 Ай бұрын
Ngongole mumupatse munthu ogulitsa zitumbuwa mwati
@IdahCharles
@IdahCharles Ай бұрын
Ukudabwa mmesa uli pamenepo kamba ka imfa😢
@CharlesChagudubuka-rm6bh
@CharlesChagudubuka-rm6bh Ай бұрын
Tamangodyani ndalamazo bas,uku tikudikira report la kuchikangawa,koyenda ndege ma hours 3800, ngati imayenda wapansi
@HappyBirchForest-zy8nq
@HappyBirchForest-zy8nq Ай бұрын
Ndipo inu
@user-su2dq5lr1h
@user-su2dq5lr1h Ай бұрын
Amalawi azanga Pena mukamalakhula muziganiza osamangokamba zithu zopanda umboni musiyeni usi ndi thawi Yake iyi yakwana
@FrankHaruni
@FrankHaruni Ай бұрын
Akuluwa alindifundo dxopusa kobasi adximuudxa Chakwela dxoti mulungu simuthu amasithadi kom osati kwaife ndiwe galu kobasi
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 86 М.
Violet Beauregarde Doll🫐
00:58
PIRANKA
Рет қаралды 47 МЛН
АЗАРТНИК 4 |СЕЗОН 2 Серия
31:45
Inter Production
Рет қаралды 489 М.
Nurse's Mission: Bringing Joy to Young Lives #shorts
00:17
Fabiosa Stories
Рет қаралды 13 МЛН
Фейковый воришка 😂
00:51
КАРЕНА МАКАРЕНА
Рет қаралды 4,9 МЛН
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 53 М.
BON KALINDO KUNG'ALULA MWA NYOO!! 5 September 2024
43:54
HOT 265
Рет қаралды 7 М.
KWAGWANJI- PP CONVENTION 6 September 2024
19:26
HOT 265
Рет қаралды 190
NDUGU YANGU AMOS MAKALA NAOMBA UNIPOKEE CCM MIMI NA MLINZI WA TUNDU LISSU
5:11
CCM TEMEKE MEDIA ( CTM )
Рет қаралды 908
Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera
21:04
Malawi Page
Рет қаралды 140 М.
KOMA ASENA AMATHA MAWU.....TAMVANI KUYANKHULA UKU KU MCP
14:57
Strong Malawi
Рет қаралды 15 М.
HOT CURRENT KUNG'ALULA MOSAONA NKHOPE 1 September 2024
55:12
TIKUFERANJI 01 JULY 2017
29:45
Edson Gunsalu
Рет қаралды 627 М.
TIKUFERANJI 25 MAY 2019
29:39
Edson Gunsalu
Рет қаралды 530 М.
Violet Beauregarde Doll🫐
00:58
PIRANKA
Рет қаралды 47 МЛН