Ife sizachilendo chifukwa mbiri ya mcp tikuidziwa.osadandaula alekeni abise lipotilo pano koma after voting September n next yr anthu adzadziwa choona ngati za imfa ya Gadama and company.
@samanthamuller764319 күн бұрын
Ndipo anthu ife tikudikira lipoti lilikutiko
@PreciousSteven-e5s19 күн бұрын
Mavuto dziko lokoma lija lasanduka lofera chifukwa cha and andare kufuna kupanga. Zofuna zawo osakonda anthu awo omwe anavotora zophanazo ayi zafika. Pena anakangopitiliza kulephera. Kupanga zomwe analongeza fuko lamalawi osati kuonjezera kuphaso sad for our motherland country very shameful
@GodisoneNoel19 күн бұрын
Zinali zokonza boma la emcp
@AlihIbrahim-s7v19 күн бұрын
Zaziiii mukuwona ngati chakwelayo azivela inuyo basi ndikumangobwebwetako,,,zikuthandizani chiyani izi popanda action or mademo ayi muli ziiiiii basi mufuna report😂😂😂😂koma malawi yovetsa chisoni kobasi
@HumphreysBanda-e7g19 күн бұрын
Ife timaona ngati mukubwetetsa Zend zeni mayo data yangaa ine