Zomwe ayankhura Mai Joyce Banda zokhunza Tonse Alliance kucha kwa Lero

  Рет қаралды 17,114

Makosana

Makosana

Ай бұрын

Пікірлер: 52
@PreciousKaliati-l6u
@PreciousKaliati-l6u Ай бұрын
Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you
@MphatsoMhoney-xn2ft
@MphatsoMhoney-xn2ft Ай бұрын
Malawi leaders are always talk wisely when they are out of gavervent,give them charnceand see there performance
@mwale86
@mwale86 Ай бұрын
This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 Ай бұрын
Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r Ай бұрын
@@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 Ай бұрын
Alipo women & girls oti anapindula ndi izi akamba awa?? Atchuleni. She could've mentored a girl or girls for presidency if she was sincere😢😢
@SanidaChirwa
@SanidaChirwa Ай бұрын
Our excellent ngat mfuna mbiri yanu izakhale yabwino mkamwalira ,tulukani mu Tonse Alliance,mpakidwa magazi oyipa kwabas
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Ай бұрын
The best leader
@GilbetaMasamba-te8kp
@GilbetaMasamba-te8kp Ай бұрын
God continue bless you your excellency ma, your such a blessing to malawi
@NatashaMakay-k5e
@NatashaMakay-k5e Ай бұрын
Anthu omwe munapanga ngwilizano, mumafunika kutuluka kalekale. Mwaona zisankho zayandikila muzioneka ngati okonda anthu..antku munawatengela kumavuto.
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Ай бұрын
Aaaa awa amayi adyela adzuzitsa malawi kutipatsa MCP yokupha komatsa yankhaza iiiiii tsitidzayiwala mayi banda anatipanga nkhadza dzedi chifukwa chofuna moyo wawo kukhale pabwino otsati amalawi akhala pabwini ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii mulape mulungu akhululukileni mwanatiyika pa dzuwa
@mkajikosya-uq5hs
@mkajikosya-uq5hs Ай бұрын
Nanga malemu SKC apepesenso?
@FosterChakanga
@FosterChakanga Ай бұрын
​@@mkajikosya-uq5hskumakhala ndi umunthu sometimes
@chikondichanza9772
@chikondichanza9772 Ай бұрын
Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame
@juntoiman
@juntoiman Ай бұрын
Mmmmm Iwe wachibwana Eti Ameney Mesa ndimunthu Modzi adapusisa malawi
@user-ry9ql9jv3y
@user-ry9ql9jv3y Ай бұрын
This woman is our Gem. Very good and we love you
@MaryMlomba
@MaryMlomba Ай бұрын
Repent before it is late
@RuthChilobwe
@RuthChilobwe Ай бұрын
Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged
@mkajikosya-uq5hs
@mkajikosya-uq5hs Ай бұрын
God bless her excellence Dr Joyce Banda
@dianachabs
@dianachabs Ай бұрын
Ambuye adzikudalitsani masten ntchito zachifundo ndiye mukuzichita
@AlexBand-f4p
@AlexBand-f4p Ай бұрын
Mwaganiza bwino kwambirimbiri tulukakoni kumeneko mwaganiza bwino kwambiri mayi zikomo zikomo
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Chipanda Dr Joyce Banda sitikanadziwa kuti mu Boma mukunedwa ndalama
@mwale86
@mwale86 Ай бұрын
Ndipo zowona no president has allowed an audit while in office it's only HE Dr Joyce Banda mayi awawa ndikatundu
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Unakasiya Chilima mkamwa mwa Ng'ona.
@BenardPhili-wp5jt
@BenardPhili-wp5jt Ай бұрын
Amayi anthu timakukondani komanso Inu Mai mumatikonda amalawi munawamangira yumba anthu osauka ambirimbiri kuno kunkhamenya, anthu atavutika ndi ngozi za madzi munawathandiza powamangiranso nyumba kumwera
@FosterChakanga
@FosterChakanga Ай бұрын
Tulukakoni masten,,asakupakeni nawo manyiwa pliz.Inu ndi mbambande
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 Ай бұрын
Makhuluku akumalawi
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Ukhuluku wakuti anasintha dzikoli with 100 days ukhuluku anapangila kuti
@PreciousJames-fh1xs
@PreciousJames-fh1xs Ай бұрын
Amai mumakwanila palipose zitukuko muno mudziko lamalawi mwapanga m, boma ririrose Tikanena zothandiza osowa nde ndikudya kwanu ndipo simuona khope kana mtundu Amai Banda Mulungu azikudaritsan thawi zonseeee eee
@DevisonHala
@DevisonHala Ай бұрын
Inu mayi chilima mumanena kuti ndi mwana wanu ndiye munachilandila bwanji chipongwe chimenechi
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District.. Chilumba and Khwawa in Karonga Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation
@BlessingsBanda-nh7ur
@BlessingsBanda-nh7ur Ай бұрын
Zilibwino koma zomayika background music instrumental ndizopoyila pama serious massages
@isaihmagani5697
@isaihmagani5697 Ай бұрын
Lankhurani chabe chichewa
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Anthu amalandila nkhuku kumaweta mabanja kumapeza ndalama ndikumadya bwino panyumba pawo.. Mbuzi, N'gombe
@SaeedHurzrut
@SaeedHurzrut Ай бұрын
hule wachabe chabe
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Nthawi yawo mankhwala mzipatala samasowa..kunalibe basi kaguleni ku pharmacy
@mwale86
@mwale86 Ай бұрын
Ndipo zowona
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Ай бұрын
Mmmmmm m'mai otapa tapa uyu uliboh mudzapita ndindalama amzathu
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Nzeru zawo ndizopititsa patsogolo dziko maka maka anthu ovutika ammamidzi
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Ambuye azikudalitsani ndikukupatsani moyo wautali
@rightlombe380
@rightlombe380 Ай бұрын
Which youths do you assist?
@mwale86
@mwale86 Ай бұрын
Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??
@mkajikosya-uq5hs
@mkajikosya-uq5hs Ай бұрын
Ambiri anapindula anagawa njinga zamoto pano akulipilira ana ma school fees through Joyce Banda foundation
@mwale86
@mwale86 Ай бұрын
Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo​@@mkajikosya-uq5hs
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Kodi kabaza ku Malawi kuno anabwera ndindani
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Tapitani ku ma secondary a Boma mdziko muno atsikana akupelekedwa ma fees..
@vitujames53
@vitujames53 Ай бұрын
Mzimayi wachikondi uyu
@JusticeMpondaphili
@JusticeMpondaphili Ай бұрын
Awa ndi mai amzelu sangakakamile ku mcp acokako
@user-px6kt8rx2p
@user-px6kt8rx2p Ай бұрын
Nzeru sabwelekana inuyo muganiza zanu
@user-px6kt8rx2p
@user-px6kt8rx2p Ай бұрын
Inuyo mukati achokako ku mcp inu mudakhalapo wa mcp?
@user-px6kt8rx2p
@user-px6kt8rx2p Ай бұрын
Sitikufunaso makadeti muno mmmalawi
小丑把天使丢游泳池里#short #angel #clown
00:15
Super Beauty team
Рет қаралды 37 МЛН
SPILLED CHOCKY MILK PRANK ON BROTHER 😂 #shorts
00:12
Savage Vlogs
Рет қаралды 45 МЛН
Вы чего бл….🤣🤣🙏🏽🙏🏽🙏🏽
00:18
ACHEWA AKU DOWA ASAMBWAZA EE!!🙌🙌
18:10
HOT 265
Рет қаралды 899
CRUISE 5 MAFUMU MATIKI
1:14:37
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 144 М.
小丑把天使丢游泳池里#short #angel #clown
00:15
Super Beauty team
Рет қаралды 37 МЛН