Timakudyadirani DC osamanyengerela amenewa, anthu oipa a kumkuyu musaiwale witika mulungu akukuonani
@VictorPhiri-vo4qj3 ай бұрын
Oh the blood of Abel cried to God and God heard the voice of Abel's blood,surely the blood of nine innocent lives,can not speak to the same God who does not change,surely the same God will hear them.
@doreenkaliati31663 ай бұрын
Amen
@RashidSaid-lk6bb3 ай бұрын
Ur a real man DC .B. kalindo and GOD must give long life and protection and don't stop am from south Africa port Elizabeth
@NastonVickta3 ай бұрын
Komano pempho langa kwa Inu a president a anthu osauka a BON KALINDO, musazamalize ngati agalatia opusa, tiimilireni nyengo zonse,
A Bon Kalindo mwalankhula za mphanvu kwambiri, George Kasakula akupanga campaign ya chakwera, zomwe akupanga akulakwa.
@MuhammadSauzand3 ай бұрын
Nyengo ino ndiyoyikano m'manda mcp. This is the fall of mcp.
@GeorgeMuserima3 ай бұрын
Bon pankhani ya ku MBC yo I support you 100 percent ndipo anandinyasa kwambiri moti ndinakalipira GOtv ndisakufuna chifukwa cha program achibwana ngati imene ija
@judithmichael-h9u3 ай бұрын
God protect you Mr president Bon kalindo
@WezzieChimuzi-ek7bk3 ай бұрын
Eti ayamba kuopa Ndege kkkkkk asaope naonso awachotsele zipangizo zina mu Ndegemo ikagwe iwo akaphyere momo akuopa Im'fa??? Anzao anaifuna?? Ameneyu ndi galu kwabasi ..azipita kolumbilitsako mbuzi yamunthu
@SimeonSanex-vw4py3 ай бұрын
Bon kalindo umayankhulira bwino kwambiri mopanda mantha,coz polakwika sumasekelerapo,always we proud of you BON
@HamilBilly3 ай бұрын
Keep standing for malawian mr kalindo,big up
@TatendaBanda-ef4mp3 ай бұрын
The DC, inuyo simusekelera zopusa.
@doreenkaliati31663 ай бұрын
Iwe ndi kuktunda iyaaaaaa mumatiimira ndinu zonse mu zonse ❤❤❤❤
awa ndachotsiru ngati kuli kufuna kuti apange mbiri mudziko yankhanani zina ndikuchokela ku south Africa Port Elizabeth p e
@aggiemlotha12083 ай бұрын
Manganya maguy .... dzina liziyamba ndi title Dr, professor etc ... ine i choose to listen from people whose their name starts with Dr, or Prof 🎉..... enawa mbola
@BeatriceRobert-jq6ci3 ай бұрын
Koma anawaputsitsa ndani koma nde asewera yachabe aaaa mpaka zawo moyo kupita ndinthu mmmmm Mr DC mwayakhula chilungamo
@AlliUsuman-mj1mr3 ай бұрын
Nanga ndichifukwa chani mu ndege muja munalibe aliyense wa MCP
@DjFiquickTech3 ай бұрын
If have knowledge Mr . Bon come with the trueth. Zongosokosa mwayamba kale , we had people like Kamulepo, Chekufwa Chihana, .Koma inuyo mungosokosa apa .come to International court of of justice to assist Malawians. You are now coming up with confusion and you are not president of Malawians.
@FortunePhiri-kl7oe3 ай бұрын
Fuseck wena
@sopaniisrael52403 ай бұрын
Kalindo wakhuta thelele
@CatherineDesire3 ай бұрын
Mnalibeso wa MCP mu ndege muja why?
@yalinhlema3 ай бұрын
Akudziwana
@moseskavalo33043 ай бұрын
Choyamba amange aja anaphwanya magalimoto aanthu a DPP aja , bwanji anthu ameneaja sanamangidwe mpakana pano, koma anthu aku Ntcheu anamangidwa same day, zompusa ,dzikoli silawo lokhatu
@OrtoniMware3 ай бұрын
Mumakwana boss
@DarwinBobot3 ай бұрын
OSAOPA OSAFOOKA DZIKO NDI LATHU .MCP MA CRIMINALS
@MosesKalenge2 ай бұрын
Good news Dc🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@BlessingMkonda3 ай бұрын
Ambuye azikudaritsani mumatirimirira
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb3 ай бұрын
Iwe mesa ukumenyera nkhondo DPP ukanalila 2025 ulila kachikena
@QueenMsowoya3 ай бұрын
Dangerous child has spoken 😂😂😂😂
@JacobBanda-s1f3 ай бұрын
Mukufuna maudindo chabe inu,tiyeni uko.
@BlessingsKandulu3 ай бұрын
tamudulani mutu chakwera kumeneko amalawi plz
@Patricenkhoma09Tricia3 ай бұрын
Step down babylon your old by evison matafale
@RACHEALKanyenda-b8f3 ай бұрын
Ulemu kwa DC
@Grevulo3 ай бұрын
Kumwamba kukhale Nanu a kalindo keep on speake the truth
@GraceLimani-zw7dx3 ай бұрын
Manyazi akuwagwira mene anachitira anthu aku ntcheu anawakhaulitsa a masewera ndi angoni awaliza tu koma angoni
@JamesStanford-my1zj3 ай бұрын
😅
@HuaweiIdentity-kt2kd3 ай бұрын
Auzeni osawabisila
@IssahTchakato3 ай бұрын
Perfect boss
@MbalasoJustin3 ай бұрын
Ndiye kuyankhulatu kumeneko mwauze
@CarolynMtegha3 ай бұрын
I concur with you Bon,I was bored with kasakura and Mvula since they are the same people who were doing cheap propaganda on times TV.... Please citizens of Malawi what kalindo has said is very right be neutral coz it will follow u
@paulinekayuni16213 ай бұрын
Zoona akumalankhula ngati a Malawi ndi mbuli saganiza. Ayenera kuziwa kuti anapangitsa okha a Malawi kukwiya mene anapangira handle
@franciskapakasa363 ай бұрын
KALINDO IS JUST ANOTHER OPPORTUNISTIC
@frankjolijo3 ай бұрын
Kwa inutu😅😃😃😃😃😃
@AlinafeMaunda3 ай бұрын
Tapitan uko inu
@FortunePhiri-kl7oe3 ай бұрын
Mfundoless
@jamesgama54893 ай бұрын
Or mabanjatu akutha chifukwa cha imfa ya chilima
@SimeonNkhata-gc8bf3 ай бұрын
Niuzeniko bro
@jamesgama54893 ай бұрын
@@SimeonNkhata-gc8bf bro umaziwa kungoyipasa motto basi
Ndipo zinthu zake sindikuzimvesa kut boma ra mcp limaganiza bwanji panthawiyo osapanga zinthu mwachangu ndizoonad kut inar taget
@SamsonChavula3 ай бұрын
Tilibe lawyer ife
@dondamissonchdziwe39583 ай бұрын
Koma ndiye takwiya kukwiya,moti Wanthu sakukwanisa kugona Ndipo kunkuyuu Lero akuyankhula,koma zikaza mufikira azalira ngati Nkhumba, Chakwera ndi gulu láke azaona tsiku Lina apha Wanthu, koma nthawi ina Yehova mwini azati pasira ngati m'mene adamu perekera Goliath m'manja mwa David.amenewo akuti agula zida zankhondo koma tsiku Lina tizazi tenga ndifenso Ana obadwira komweko
@MasterBlack-r2n3 ай бұрын
inu ndi amfumu. kunkuyu akulankhula Mo pusa kwambili. anthu amenewa atikwana
@jonas-xh4hz3 ай бұрын
mumakwanira atsogo
@samdiverson97333 ай бұрын
Dccccc machine our president wa amphawi
@PatrickMailos3 ай бұрын
Pheeeee kumastand kumvera bon kalindo 💪 the DC
@josephlukhele-v5c3 ай бұрын
We are Desperate country indeed , anthu ngati DC can not unit Malawians. Supporting you is wasting time. Surely there is no sense padzimene mukukamba. Back to DPP IYAAAA
@MaureenMollen3 ай бұрын
The great man Bon kalindo❤❤
@EstherBonga3 ай бұрын
Umatiimiliza DC
@NescotNyamwela3 ай бұрын
Boma lose la mcp nkhuku za anthu.
@innocentsathasteven40933 ай бұрын
THE DC TELL DEM THE TRUTH MAYBE THEY'RE DON'T KNOW ENETHING AT ALL APHUZITSENI CHILUNGAMO NDI MWANOTU PAJA
@George-e6h3 ай бұрын
Inu nzeru mulibemo even kuti iwine DPP akakumanani udindo mutukwanaso. UTM munainyozaso. Bwererani ku uphunzitsi.
@ElizahMadi3 ай бұрын
Salute Mr DC
@MarthaMartha-rw4zz3 ай бұрын
Akatero nde kuti mbc wo apasidwa ndalama koma ayaruka nawoso amenewa akuona ngt athu akugona et😢
Wakhuta thelere ndiwe wakumudziwe iwe ife sitimalidziwa kkkk kwerani ndege mupite ku south osatuma munthu isaaaa
@CollenChapenda3 ай бұрын
Nthawi yong'aluradi eeee kkkkk
@japhetbanda-b4i3 ай бұрын
May the Lord guide during this difficult time
@McDonaldNtchirah-bz6do3 ай бұрын
We follow you King big up
@FrankJumah-jc8mf3 ай бұрын
God blesss u born k
@williamalvis60283 ай бұрын
The DC
@AlexMduladulaMafuleka3 ай бұрын
Tamanenaniso za anzanu a Manganya kaya nanga daily MCP koma simukunenapo bwanji za m'bale wanuyi
@innobashirbernard78533 ай бұрын
Big up our brother Bon kalindo
@wishesnsunza38233 ай бұрын
Wise and courageous words
@LeadChanza3 ай бұрын
Amalavi ndiwokhwiya zedi kwambiri ndi inu aBon kalindo chifukwa ndinu wodziwika kuti ndi wodzindikira koma mukungoyankhulira kwanu,mukutipusisa kasumen/panseu basi osatikutipasa zochita ife amafoni basi
@LeonardEnock-e1t3 ай бұрын
Akut tiku user bundle yontchipa mmmm ndinazimvera chisoni 2000 bundle yikuntchipa munthu wopusa kwambiri moses kunkuyu shame on
@jameschimbe20593 ай бұрын
DC has spoken 😂
@HalisonSolomon3 ай бұрын
MBAMBANDE DC ASUKULUZE AGALU AWA SAMAMVA IYAAAA NDIPO 21 DAYS IKATHA TIKUFUNA MA DEMO MCP ICHOKE
@JamesChipande3 ай бұрын
Kod ifeyo tiziopa kulolibe kuopa tose nda Malawi nde atimage tose ndiyeka