Abusa akuti vote yao atengapo anapanga mistake❎ 😂😂😂

  Рет қаралды 30,397

Malawian Cameras

Malawian Cameras

Ай бұрын

Пікірлер: 177
@augustMag
@augustMag 21 күн бұрын
Powerful words may God continue bless you Fr Mnthalika 🔥
@MorrisMapiri-d6z
@MorrisMapiri-d6z 21 күн бұрын
Mlungu anamufunsa KAINI nati: alikuti m'bale wako Abele? Nde anati, taona mwazi wake ukundililira ine kunthaka. Zotsatira anali matembelero pa KAINI. Kukhetsa mwazi kumadzetsa tsoka.
@user-sv2vc7ie2m
@user-sv2vc7ie2m 28 күн бұрын
Anthu atengapotu phunzilo ndizovuta zomwe tikuziona chifukwa anthu amati akufuna kuona kusintha ndiye aonatu nyekhweeeeee
@GiftPhiri-tt7nn
@GiftPhiri-tt7nn 28 күн бұрын
Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani
@marryphili5419
@marryphili5419 21 күн бұрын
Amen abishop ndipo talira mokwana koma mulungu simunthu safulumira ndipo sachedwa one day is one day mulungu ayakha
@CathreenKadwala
@CathreenKadwala 21 күн бұрын
Father Inu Ambuye azikupasani moyo wautali simuwopa kuyankhula chilungamo
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 21 күн бұрын
What a teaching ❤❤❤ impressed me so much waooooo❤❤❤
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o 28 күн бұрын
you have spoken man of. God we. are listing God is God. does not. fail
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
@JustinChinombo-dy6tp
@JustinChinombo-dy6tp 28 күн бұрын
Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 4 сағат бұрын
Eeee eeee Bon Kalindo siwamisalatu... Adanena kuti anthu akadzatopa adzalankhura m'modzi modz....
@user-ir1lj8ir5t
@user-ir1lj8ir5t 14 күн бұрын
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
@bysongeorge3243
@bysongeorge3243
Chilungamo chokhachoka. Zokhumudwitsa wina tinamusankha anali M'busa..koma lero anasanduka ..
@ReginaKasambiza-ie2rp
@ReginaKasambiza-ie2rp 28 күн бұрын
Kumwamba kulande vote yanga
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632
Father mumakwanisa ulaliki wanu wabwino kwambiri
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
@marthansaliwa7732
@marthansaliwa7732
Amen! Father Ambuye azikutetezani.
@EvelynLungu-lj8tp
@EvelynLungu-lj8tp 28 күн бұрын
Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p
True talking man of God
@user-wr1km2gh4g
@user-wr1km2gh4g 21 күн бұрын
Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 24 М.
Schoolboy - Часть 2
00:12
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 3,2 МЛН
Sigma Kid Hair #funny #sigma #comedy
00:33
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 40 МЛН
Top Hamas leader Ismail Haniyeh killed in Iran | BBC News
11:10
A Born Kalindo akuti Khulupilirani wa Bakili Muluzi Tv 😂😂 Enao ai
15:02
Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera
21:04
Malawi Page
Рет қаралды 135 М.
Mr khad kuzangobwera ndi yao ija
9:40
Malawian Cameras
Рет қаралды 8 М.
6 às 9 |EDIÇÃO DE SEGUNDA-FEIRA |05|08|2024
TV Sucessomoz
Рет қаралды 192
Schoolboy - Часть 2
00:12
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 3,2 МЛН