Achakwera Sakupanga Zinthu Mmene Adalonjezera | Wina Wazuzula Mmene Zinthu Zikukhalira

  Рет қаралды 14,309

Mukuziwa?

Mukuziwa?

Күн бұрын

Пікірлер: 60
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo 3 ай бұрын
Mwayakhura bwino kwambiri ❤ ndipo athu awa achoke mwankhaza mademo achitike ife tikumva kuwawa amalawi
@RoseMkandawire-e2g
@RoseMkandawire-e2g 3 ай бұрын
Chakwera sangarire ayi chifukwa iye.niamene.wapha.chirima kkkkkkkk mubusa kumuchosa ku mzuzu.kukamusiya.ku lirongwe amafuna kuti akamuphe.ndipo akamudwe ku nyanja kuribe magazi ndeno amafuna magazi kkkkkkkk koma chakwera sataniki
@DoricaGoweka
@DoricaGoweka 3 ай бұрын
Ndipo zachita kuonetseratu kuti ngozi yandege imeneyi anachita kukoza zimenezi imene taluza abale athu 9 imfa yamamgawa simasowa ayi Lazaro ndi anthu ake ndi dzigawenga
@cjaylucky
@cjaylucky 3 ай бұрын
NO PAIN NO GAIN TIYEN PASEO ON 10 JULY BASI CHAKWELA ACHOKWE BAS WALEPEL NO PAIN NO GAIN
@JustinLipipa
@JustinLipipa 3 ай бұрын
Afiti awa a Congress, Congress singasinthe ndi ng'ona zokhazokha izi aaaaaa
@HamanjaManyela
@HamanjaManyela 3 ай бұрын
Poor people feel the pain right now
@yohanezimba8329
@yohanezimba8329 3 ай бұрын
The problem is Malawians make decision during anger, and 2025 will do the same similar choice because of anger. Others they are speaking as if they are wise but the true sense these people if they happen to be chosen they will also worsen this country
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 3 ай бұрын
Exactly the point
@MisheckAselo
@MisheckAselo 3 ай бұрын
Yonseyi ndi mission ya chakwera, koma iye akutsogoza anzake iye azamka kuti sikumanda basi a chakwera be careful pple we watching you 🖕
@OmegaChingamuka
@OmegaChingamuka 3 ай бұрын
Tilankhulireni anzathu inu ife atitseka pakamwa akuti tisamalankhule Mau anphanvu amene mwanena ndithu ambuye akudalitseni Ifeyo nde tikulira misozi yathu sidzatha 😢😢😢
@zayedmitawa8345
@zayedmitawa8345 3 ай бұрын
Kulankhura mwa nzeru uku koma oipa adana nazo.Wandale amafuna atakhala zaka zochuluka paudindo yet akapeza mwai mmalo mogwira ntchito to gain trust kwa anthu onse amakhara busy ndi 'kwapsya tonola' mkumaembekezera kuti akaba ndalama ,ndalama zomwezo azapangira campaign kuti awine.Chitani zinthu zabwino kuti zabwinozo zizakupangireni campaign zokha popanda kuononga ndalama zanu Mwai munapatsidwa ,mukuutaya nokha
@ChomboNgosi
@ChomboNgosi 3 ай бұрын
Vilombo ivi
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 3 ай бұрын
Ndi agalu awa brother palibe zonse analonjeza zaboza zonkhazonkha chilibe zeru iiiiichiiiii
@TamalaSoko-vg5wq
@TamalaSoko-vg5wq 3 ай бұрын
Munena zoona brother ambuye akudalitsen
@HamidaIweni
@HamidaIweni 3 ай бұрын
Mwandiyankhula bwino kwambili❤
@SamuelMponda-y3d
@SamuelMponda-y3d 3 ай бұрын
Vc president ameneyo ngamene agulitsa Chilima amene amakonza zothetsa Tonse Aliance. Iye, pamwambo anati; Chakwera ndi wake komanso Chilima ndi wake. Kodi pamene amanena izi, Chilima ali kuti?
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 3 ай бұрын
Your speech is good bro, keep it up
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc 3 ай бұрын
Ulamuliro upusa even mwana wachichepele sangaganize mopusa ngati chakwerayu
@RoseMkandawire-e2g
@RoseMkandawire-e2g 3 ай бұрын
4:10 4:10 4:10 4:11 4:11 4:12 4:12 4:12 4:12 4:12 4:13
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc 3 ай бұрын
Chakwera achina zikhale ng'oma and other team opusa zitsiru za anthu oma ankhula America English koma athu opusa ngati nsima
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 3 ай бұрын
This guy is saying zoona, just imagine celebration ya ku sankhidwa kwa Mr Usi ngati VP? Shame shame
@leviefeston7626
@leviefeston7626 3 ай бұрын
Apolice ndi opusa kwambili Amalavula chingamu ndi mtegmdza olawa MCP ichike
@MandalaChaona
@MandalaChaona 3 ай бұрын
Evil men,Greedy, Jealousy men. Wait for your judgement day. Mulingati abwino popeza nyansi zanu zabisika
@DaveDambo
@DaveDambo 3 ай бұрын
Security departments kusanduka ya a chakwera aaaa zokhumudwitsa kwambiri 💔 God knows everything.🙏
@RoseMkandawire-e2g
@RoseMkandawire-e2g 3 ай бұрын
4:10 4:10 4:10 4:11 4:11 4:12 4:12 4:12 4:12 4:12 4:13
@Gwedeza-oz3jv
@Gwedeza-oz3jv 3 ай бұрын
Mmmh pali anthu amene anapatsidwa luso lolankhula ndithu nkulu uyu akulankhula momveka ndipo ndutha kuona kuti ndithu dzikoli panalibe chifukwa chobwezeletsa anthu opandanzeruwa , Nkulu iwe mulungu azikuteteza komanso mukhale healthy
@DavieChiwale
@DavieChiwale 3 ай бұрын
Sitikusowanso zabwino kwa afiti amenewanso atsala ndi masiku owerengeka
@OwenNyangu-nv1yt
@OwenNyangu-nv1yt 3 ай бұрын
Adafa pa mdipiti wopelekeza maliro aja samalawi? Kodi Malawi ndi anthu amayina okha?
@AllanChabwela
@AllanChabwela 3 ай бұрын
Mukuyankhuladi chilungamo zaonjeza
@MphatsoChengetani
@MphatsoChengetani 3 ай бұрын
Very good speech
@WisdomBlack-uu7zt
@WisdomBlack-uu7zt 3 ай бұрын
Za kugwa kwa ndege akudziwapo kathu awa ndichifukwa bwana aja anauzidwa kut ndege malo
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 3 ай бұрын
😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢
@EssaPindani
@EssaPindani 3 ай бұрын
Koma walephel kuyendesa malawi unku uyu achoke
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx 3 ай бұрын
A nkava kuwawa mu mtima ankangonena zimenezo koma sakugona asiyeni azuze anthu tsika mu mtengomo a tipeza a Malawi pansi pano
@PeterPhiri-nd6op
@PeterPhiri-nd6op 3 ай бұрын
Kuyakhula kwa bwino
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili 3 ай бұрын
Munthu asanafe mumayamba kugontha nimukhutu
@Malekano-k3x
@Malekano-k3x 3 ай бұрын
Good speech
@GrolyGondwe-e9s
@GrolyGondwe-e9s 3 ай бұрын
Zilombo zimenezo
@hussenadam3786
@hussenadam3786 3 ай бұрын
True Malawian
@PetroMatias
@PetroMatias 3 ай бұрын
👍👍👍👍👍👍👍gud
@TasiMunthali
@TasiMunthali 3 ай бұрын
Achakwera ndi gulu ace wakanika
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 3 ай бұрын
Zowona alimife tili mumavuto
@TadalaPaul
@TadalaPaul 3 ай бұрын
Umumu muli mfundo guyz i proud for you vp
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 3 ай бұрын
Chipani ichi 🙌🙌 ndimkangomva ine
@HamanjaManyela
@HamanjaManyela 3 ай бұрын
Ineso eeh
@JoyceBanda-k8t
@JoyceBanda-k8t 3 ай бұрын
Akulephera kumanga kumkuyu okupha Allan witika koma kulimbana ndi bon kalindo mcp ndi ya satanic
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 3 ай бұрын
Muone ma tie amene ali pakhosi atau afira magazi okhaokha. Onani chithunzi chili pa video imeneyi.
@CHIWSABINYAMBOSE
@CHIWSABINYAMBOSE 3 ай бұрын
Alibe nzeru awa
@ElizabethKoopa
@ElizabethKoopa 3 ай бұрын
Chakwera andipatse vote langa ninalakwitsa kuwavotere
@Uncle_B265
@Uncle_B265 3 ай бұрын
Malawi tinagulisa uyuu
@raphaelfanuel4608
@raphaelfanuel4608 3 ай бұрын
Inu simunalemekeze maliro asanachitike bwqnjiii
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 3 ай бұрын
Namu bwana mukuyangu rabwinino man big
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc 3 ай бұрын
Democracy will never demolishe we are in new generation
@ziyamikanmakowa5981
@ziyamikanmakowa5981 3 ай бұрын
Mfiti za anthu izi
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 3 ай бұрын
Tiyeni Amalawi tigwilizane anthu awa achoke basi
@AckimMhango-v1x
@AckimMhango-v1x 3 ай бұрын
You are talking
@AREFRIEDNELSON
@AREFRIEDNELSON 2 ай бұрын
Mpaka muyaya kuti dzikoli adza nkhare ndi family yakwawo lokha tuuuuu amenewa afika poti akhoza kuthila poison mmadzi kuti athu onse afe pamene zafikiramu chifukwa tuuuu apapa chimbare chakalika
@CleverChiumia
@CleverChiumia 3 ай бұрын
Yankhulani tikumveni
@chachaamoah3592
@chachaamoah3592 3 ай бұрын
Wa MCP sasowa uyu.mulibe nzeru MCP boma lazitsiru
@HamanjaManyela
@HamanjaManyela 3 ай бұрын
Machende ako
🔴 NTV LIVE | October 2024
NTV Kenya
Рет қаралды 1,1 М.
Bike Vs Tricycle Fast Challenge
00:43
Russo
Рет қаралды 105 МЛН
Life hack 😂 Watermelon magic box! #shorts by Leisi Crazy
00:17
Leisi Crazy
Рет қаралды 28 МЛН
Help Me Celebrate! 😍🙏
00:35
Alan Chikin Chow
Рет қаралды 58 МЛН
MCP Ikuwina Zisankho Mu 2025 - Redson Munlo
19:53
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 4 М.
Nze eyatta bbosa, bano mubaate tabuula alagidde omulamuzi
15:09
GROUND MEDIA UG
Рет қаралды 566
KUSEMPHANITSA KWA ZIZIMBA, ZOMWE ZINAPHETSA SAULOS CHILIMA 🤯😭
35:46
Bambo agwira akazi Awo pachigololo
16:28
Mukuziwa?
Рет қаралды 4,8 М.
Applying for grad schools abroad? Here’s what you need to know
1:12:46
Top 9 Ya  Anthu Olemela Kwambiri Kumalawi
8:17
Sam Malvitha
Рет қаралды 88 М.
Bike Vs Tricycle Fast Challenge
00:43
Russo
Рет қаралды 105 МЛН