This country need serious demonstrations. We don't need to beg or ask anyone to demonstration because it's our rights.
@MathewKalinkhu13 сағат бұрын
Ndigwirizane ndi Bayana Chunga, dziko la Malawi ndilomvetsa chisoni, makamaka boma ili la MCP. Kaya ndichifukwa choti anakhalitsa kunja kwa boma kaya. Zamanyazi.
@LeyvanSamuel-pe5tc15 сағат бұрын
Tiyeni kuma demo guys tikayipase 🔥🔥💪💪
@bettieulaya5702Сағат бұрын
Kuli madhemo achani
@StewartKalipinde-g2j15 сағат бұрын
True
@HarryMkango11 сағат бұрын
More fire guys
@RobertLuka-wy9cl11 сағат бұрын
Wayana chunga God bless you ❤❤❤❤
@MisheckMwale-v8q13 сағат бұрын
Thank you wayana
@issahmaloto914111 сағат бұрын
MCP yationongera dziko😢
@RodgerChaula-r5z2 сағат бұрын
More 🔥🔥🔥🔥
@RodgerChaula-r5zСағат бұрын
Bayana you are the best
@MzadziWanga14 сағат бұрын
Ma demo awa mwapangira malo olakwika coz ku Lilongwe anthu ambiri analembetsa ma id nde anthu sangazatuluke ambiri , mukanapanga ma district atatu awa, zomba Blantyre n mzuzu kma Lilongwe nde aaa
@YohaneChinthomba13 сағат бұрын
😂😂😂 Is Mzuzu district?? Kapena ndikhalepo mbuli?
@MzadziWanga12 сағат бұрын
@@YohaneChinthomba whatsoever as far as I know, mzuzu is also involved in government activities , whether is city or district I don't care bola ndapereka maganizo anga kt ma demo akanachitira Madera ameneo, nde bweran mudzachonge aphuzitsi
@Jacksonmuhackeya14 сағат бұрын
Mukusokoneza dzikoli ndi inu olemba za unzika amene mukufuna kuti kusogoloku Amalawi azavutike awine amene mukufuna
@robertmkandawire989813 сағат бұрын
We need audit of NRB, cause they are not serious!!😢😢😢😢
@JamiesonKaunda12 сағат бұрын
Nsambo ndiwe mbuzi ya munthu ukulephela kuyankha momveka
@LilianKachala-yz2xf12 сағат бұрын
A Parliamentnso Sakutithandizanso.A Speaker Sadaipange Table mpaka parliament kutsekedwa Abale tithandizeni Amalawi pakupanga Zinthu Zanu Parliament.Okusankhanitu ndife mukutipondelezafe.
@nellietchuwa991312 сағат бұрын
Bwanji ma concern s anu mkatenge injunction yoyamba kalembrera than kuupita nndi mademo
@Tophillpvtsecondary-x7l13 сағат бұрын
Malawi need God intervention , truth shall be seen when God will say its enough
@MosesDicostar3 сағат бұрын
Ife tikuyenda wapasi kuchoka ku zambia kubwera kumalawi kuzapanga ma demo
Agalu awa achoke basi....zisilu za anthu ....chakwera waononga ziko
@nellietchuwa991312 сағат бұрын
Even nthawi amapanga lamulo poyamba amavomera to suit their narrative by then now is haunting them (dpp)
@StevenFombe6 сағат бұрын
Kodi Gregory gondwe angayankhure PA radio exclusive interview with Briana banda
@isaaczuze3 сағат бұрын
Moses kunkuyu anapha Allan Witika .....munthu woyipa iwe
@FrankKasiya10 сағат бұрын
Koma jakama mukumuziwa berani muone ndimupanga hare
@Kamwachale15 сағат бұрын
Please whose is near chimwendo Banda that magetsi kunsanje NDI Madera ena a Ku BT magetsi akuthimathima paene akumawanamiza wanthu Kuti magetsi ansiya kutima.
@DanielNandajester12 сағат бұрын
Paja afumu anafera PA wire amagets cholinga escom ioneke yolephera
@HarryMkango11 сағат бұрын
A mcp akuchoka basi olo.atani ndimenyela ufulu basi osalola zopusa kuyambila kale timavota opanda id
@jacquelinChitsulo4 сағат бұрын
Oh oh anthu amalandira ndalama kuti azipondereza ufulu wa a Malawi?, this is very pathetic kutichotsera ufulu wathu, Ndakhumudwa now i can understand why ku Kenya kuja anthu anakalowa ndi ma Demontrations ku Parliament.1
@LilianKachala-yz2xf12 сағат бұрын
It's. true kunonso ku CK Zimatero ndipo anthu amangibwelera ngakhale kwa a DC anthu akubwelera Ziphasonso OSapatsidwa ndiyeno mzikazi zikalembetsa bwanji anthu alibe Ziphasozo
@DavidJabesi-r1h4 сағат бұрын
Akulu akulu a NRB pogwila ntchito yanu lekani ku masewela ndi nzelu za amalawi inuyo chifukwa muli m'mipando musaganize kuti kunja kuno kulibe anthu anzelu mukanakhala enamukanagwila ntchito yanu mokomela amalawi onse osati kugwilisidwa ntchito ndi anthu a ndale,
@GRIGORYLASTON13 сағат бұрын
I CAN'T HEAR THIS BUT I THIS WEDDING WILL BE THE BEST
@LovemoreCathy12 сағат бұрын
Wochunga inu ndi 1..Ulemu wanu 💪🔥
@aubreymagombo590713 сағат бұрын
Capacity alibe ine ndina lembesa 2022 mpaka pano card sinatuluke ndilibe ID pano
@JulieNdekha13 сағат бұрын
Peaceful much kulibeko unless ngati ndiza church... Izizi musanamepo apa
@EllenGomani-i4f11 сағат бұрын
Nsambo ndiwe chitsiru kwambiri
@peterchikwakwa84762 сағат бұрын
Sambo sounds sketchy 😢😢😢
@PeterRabson-z3w13 сағат бұрын
Nawe Patrick kankwatira sukumva kuti nkhani n ma numbers mu parliament mo iwe chibanzi chinakudya moyo cha mcp mafuso opoira ukumufunsa nthendayo
Iwe usamapusise Amalawi munthu ngati ak usowa chimanga chokuti adye pakhomo pache ndiye achoke ku mulanje akalembese ku thyolo ukuganiza bwanji
@SteveKaphamtengo-gf2mp14 сағат бұрын
Dziko silawo dziko ndi la amalawi Ife zachibwana ai ngat NRB sinapeleke chauzika ndiye kt at adzavote ndi NRB Ife ai
@AdamJames-x7x14 сағат бұрын
kumkuyu ndiwe wabodza kwambiri, mutu ngati choswera malambe galu iwe
@DalitsoPhiri-sq5nl15 сағат бұрын
Me demo will show omwe Ali ku parliament kuti azixitengera serious akapasidwa nkhani ndikunena izi cz ku parliament pakakhala nkhani yoti ndiyokhudzana ndi boma zimangofafanizidwa
@AcksensioChikondi14 сағат бұрын
Eeeeh kunkuyu 🔥
@MartinMartin-d3g13 сағат бұрын
Apa pakufunika amalawi onse akalembetse ku lilongwe