Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc
@TamikaKaponya2 ай бұрын
Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni
@gracemaluwa46742 ай бұрын
Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen
@MarthaBanda-ye4pt2 ай бұрын
Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭
@AminahMussah2 ай бұрын
ndipo amphwa kwambili 😭😭😭😭
@henrychawinga46392 ай бұрын
AMEN
@mphatsomonjeza43712 ай бұрын
God is with her 🙏🏻
@LywellChilupsa2 ай бұрын
Ndipo ine ngati ndilire
@AntinHawile-rw9fj2 ай бұрын
kulira kosalekeza tikulira nanu mayi mary chilima km ambuye yekha ndiyemwe akuziwa kwezan maso kwa yehova ndpo zonse zizakhala bwino mama😢😢
@nysonchapasuka72702 ай бұрын
May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.
@CharlesChilinde2 ай бұрын
Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko. Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉
@GladysMwantenga2 ай бұрын
Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima
@Martha-m6e2 ай бұрын
Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.
@TamikaKaponya2 ай бұрын
Ndipo kwambiri
@TizifaBanda-xn5tm2 ай бұрын
Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu
@doreenkaliati31662 ай бұрын
Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed
@doreenkaliati31662 ай бұрын
Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@DavidPhiri-o6w2 ай бұрын
Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty
@ChristinaNyirenda-zb1if2 ай бұрын
Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz
@stevenkambuku2 ай бұрын
Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip
@FanscioDancun2 ай бұрын
This is like bringing tears again
@SimeonAbraham-u2j2 ай бұрын
Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu
@DolicahGift2 ай бұрын
😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢
@Lazarus-qo1sl2 ай бұрын
We need your mercy our father 😢
@JaneMoyo-ws2di2 ай бұрын
Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC
@Melinavituhs-tc8ys2 ай бұрын
Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭
@eliaskachali-xn2ve2 ай бұрын
Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose
@rhodahjere87472 ай бұрын
Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭
@JoyceChawawa-og1cj2 ай бұрын
Only Almighty God knows
@Adamuson2 ай бұрын
Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.
anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo
@Geraldmkwewu2 ай бұрын
Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere
@TwalikiWisiki2 ай бұрын
Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face
@mcsellahntv68962 ай бұрын
Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.
@AustinBanda-ee6sb2 ай бұрын
A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka
Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.
@cmsanyama2002 ай бұрын
Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?
@ziwani36822 ай бұрын
Rest in peace skc 😭😭
@EllenNgoon-nc8vg2 ай бұрын
😢😢 koma dziko iri
@TrizaGeorge-q8w2 ай бұрын
Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja
@mphatsosadiki49832 ай бұрын
Only God knows😢
@NoelBurton-x1z2 ай бұрын
SKC forever ❤
@vitumbikomateche2 ай бұрын
Skc for life
@Biath-m4b2 ай бұрын
Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife
@JaneMasikini2 ай бұрын
Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh
Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC
@GiftKumbweza2 ай бұрын
Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene
@WorriedNdhlovu2 ай бұрын
Mapwala ambuyako iwe
@temwekamlenje43582 ай бұрын
Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.
@vukanifracksonchinkonde73242 ай бұрын
If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi? Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad. Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal. It's primitive life to fuel enemity for your personal gain. Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse Be civilized guys!!!
@johnkatapeh71822 ай бұрын
RIP SKC
@georgeraphael81982 ай бұрын
Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅
@AgathaJerard2 ай бұрын
Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂
@lindaphiri35432 ай бұрын
😂😂😂 ndipo zosawakhala
@AustinBanda-ee6sb2 ай бұрын
@ Jane ❤❤ ndaikonda comment yako
@SalaJawali2 ай бұрын
Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo
@nishanchiwaya45612 ай бұрын
Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅
@JaneMoyo-ws2di2 ай бұрын
Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC
@RichardKuden2 ай бұрын
Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂
@GeoLikwanya-cb9gn2 ай бұрын
Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼
@Nunalinn2 ай бұрын
Kodi iyeyo akazake sanapite nao
@CamlonLogistics-ju6mb2 ай бұрын
Mary chilima akufunika mapemphelo
@BlessingsTembenu2 ай бұрын
Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy
@EsetaGerate2 ай бұрын
😭😭😭
@JamesChiphwanya-m4v2 ай бұрын
Mery chilima usamale ndizopasana moni wamanja zanuzo kuli ma poison kumalawi kaya ayudasiwo musamale nawo